COMRADE LWARA - KUMANGA ANTHU NGATI ACHINA KALIAT NDICHINTHU CHOWAWA KWAMBIRI.

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 23 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 17

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 3 години тому +2

    Am waiting Bakili Muluzi TV atiuza znsezi madzulo pano dikirani

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 3 години тому +3

    Team yodziwa mpira siopa finalz Manganya akuopa finalz

  • @BensonChilundu
    @BensonChilundu 4 години тому +2

    Chipani chomwe chili m’boma chikamamanga anthu chotero dziwani kuti chipanicho ndi cholephera ndipo chituluka m’boma.Dziwani ichi,munthu ngati wapanga cholakwa m’nyumba ya munthu kenako mwini mkukupeza ndipo mwamwayi wapeza mpata wothawa ndipo kuti uli mkati mothawa kenako mkumva zoti akukutukwana yamba kuyenda.Mayi Kaliati tili nanu limodzi ndipo Mulungu yakha ndi yemwe akudziwa chilungamo chake.

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses 3 години тому +2

    Chisiru manganya ndiyemwe akuyenda pasi pasi, chilungamo chikubwera palibe chisisi pansi pano.

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb 8 хвилин тому

    Next year, enanu muzidzati kumangidwa, kungolandila bail kenako rearrest pompo... Am seeing enanu mutalandidwa chuma chanu, kwangokhala ndi mira wanuyo basi...
    Am seeing enanu mukudzipha...

  • @InnocentNitamanMilanzi
    @InnocentNitamanMilanzi 23 хвилини тому

    Judge ameneyo akati asanene bwino
    Timuombera asamale

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 4 години тому +2

    Manganya ponyelera pako Kumene Uli plus yr boss

  • @MalvinMakolija
    @MalvinMakolija 35 хвилин тому

    Dziko lomvetsa chisoni kwambiri mmalo momathetsa mavuto okhuza mafuta bzy kumamanga Anthu zamanyazi😢😢 kwambiri mukuononga mbiri ya boma lanu inu a MCP samalani people they're very tired with you samalani samalani

  • @KalongaWhy
    @KalongaWhy 2 години тому

    Mukuyankhura zachibwana pamenepo ndipamene mukana lusa kupita konko chimenecho chikanakhara choyamba kuyambisa mademo kupita kupolisi konko koma amalawi kaya zopusa zokhazokha

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam 4 години тому +1

    Komano boma lamalawi lowola ndithu zimenezi nde tiziti chiyani

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 4 години тому +1

    Mupite pa police po mukaotchepo, apólice wonso mupite mmanyumba mwawo muotche nyumba zawo ndikuphanso wana wao Ngati m'mene achitira Wanthu aku Maputo Moçambique apólice amocambique Ali Ndi Mantha panopa anayesesa kuitanisa herocopita Ku south Africa kuombera Wanthu Koma apólice amocambique agonja, Ndiye popeza Amalawi Ndi opusa Mantha,muzipenya Wanthu amocambique Ndi owopsya sangafane Ndi A Malawi ndinu ogona

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 3 години тому

    Ma Corwards amcp ndimanganya apanga propaganda akuwonga ngati manganya angawine amfiti.

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses 3 години тому

    Inu chakwera anangopezeka mwangozi kukhala president, munthu ngati amakanika kutsogolera m'pingo kuli bwanji kutsogolera dziko. Awa akanika angopakira azipita asadikile kuchoka mwa uyo uyo.

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 4 години тому +1

    They won't win Mcp, they are waiting time

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 3 години тому

    Apa tiwona ngati ma court aku malawi ndi a corruption dii.
    Gwirani amene anapha Chilima
    Leave this nonsense

  • @marthaphiri3600
    @marthaphiri3600 4 години тому

    Usi mu coward kuopa mzimai kkkkk

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 3 години тому

    Atimange osusa tonse asale MCP yokha yokha kulibe malo kupolisiko kodi sitikwanako