Ndege munthu ndiyomwe inachita iziiiii Anthuwatu akuona ngati amalawi tikadali ntulo sakudziwa kuti tinachangamukaaa Muzionaa ndipo muyankha mafuso onsewa kwa amalawi and to the whole world Mfiti Chakwera
Kkkkkkkkkk koma ntanyiwa kkkkkk usandisekese apa ....redson munlo mutu wake siumagwila olo mpang,ono pomwe ......anamangisa ukwati mamawa pofika madzulo ukwati watha ..naperi seventh day kunaperi ku blantyre ......redson munlo ndi chisilu cha munthu
That’s true Vs president he was going for funeral with suit and tie now he body is nicked so how take out his clothes is look like something that does happen, am very sorry what happened to him and died like thief and Chikwara he is proud like nothing happened
Inetu ndi mathokoza kwambiri a Limpopo FM ndipo ndadziwa ndale chifukwa cha Limpopo FM pitirizani kutipatsira nkhani zonse mulungu adzikudalitsani bambo muthwanyiwa
Ndikangolowa pa UA-cam choyambilila ndi mafuna ndi mvele Limpopo fm koma ka melody mumaikaka kamatalika kwambiri musanayambe kulankhula ofcourse ndika bwino koma kasamatalike kwambiri nthawi Zina timakhala tili pachangu nde kamatipangisa kuti tisamalize kuvela
Munthu amene amadana ndilimpopo ameneyo ndifiti
Comrade Ntanyiwa .God bless you,protect you,guide you and entire family.
SKC soul im sure ukukuyanganilani Comrade ,and the entire Limpopo DJ's🙏🙏.
Nkhanga zikungoyenela ziziona👀👀👀👁️.
Uku tikusala kudya ndi kupemphela ,chilungamo chioneke ndithu.
Limpopo 🎉🎉🎉🔥🔥🔥🔥🔥 moto kuti buu !!!!, 🔥🔥🔥
Ndege munthu ndiyomwe inachita iziiiii
Anthuwatu akuona ngati amalawi tikadali ntulo sakudziwa kuti tinachangamukaaa
Muzionaa ndipo muyankha mafuso onsewa kwa amalawi and to the whole world Mfiti Chakwera
Tikusatira mwachidwi ndinthu ndipo alimpopo mukat musatumize uthenga ndinadandaula kobas andi bon kalindoso ulemu wanu pitizan kuima pachilungamo mulungu alinanu nonse mudzina layesu mulungu wamoyo
Dzoooona osamalimbana nawo inu pangani ubwedzi ndmlungu osati munthu odzuza thupi ndyesu yekha oteteza lnuyo antanyiwa❤❤❤❤
The best fm ,,, listening from Botswana I can't wait ❤❤❤❤
Ntanyiwa komaso bakili muluzi these guys i salute 💪
Mulungu akukuteni kut onyansa mtima awa osowa umunthuwa
Asamakufikireni komano big tawakumbuseni a DPP Asiya uchetewawu adzuke
Limpopo following 🙏
SKC and others who died Rest in Eternal Peace 😢😢😢
My best ❤ Limpopo FM radio
Iwe ulingati m,zimayi mabodza umangoduladula nkhani osayimaliza kuchita kudziwika kuti ndiwe wamabodza iwendiwe galu wachabechabe nakutuluka
Listening from cosmo city, just here malibongwe drive south Africa ❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉 Comrade!!! tili limodzi apa✅✅✅🇲🇼💪💯
Inuyo ndi one ndpo sindmafuna pazidusa one hour tisanakumven mau nice big man
The best Limpopo FM radio station is the one 🔥🔥🔥🔥
RIP SKC, kodi nanga anthu 8 enawo imfa zawo zinali zotani? Pamenepa sipakumalongosoredwa
Mukhale ndi moyo wautali comrade ntanyiwa anthuwo angodana nanu akusowa zochita chifukwa mumanena chilungamo
Ngati chilima anaphedwa ndiye kut onse anaphedwa , kaya ndingozi ndiye kut onse ngozi eeeeetu
The problem is that ayesetsa kuti akuchiteni chipongwe koma alephera anthuwa Comrade ndiye nzeru zatha
A Ntanyiwa chifuwa SI chipha osatekeseka..imwani madzi ochuluka
Pheee,pano pa limpopo ndi comrade mtanyiwa
limpopo fm ft bakili muluzi tv 🔥🔥🔥🔥
Congratulation Mr mtanyiwa gp🎉❤❤❤
Masowela aaah yoooo timbwela from Zambia
I can't believe it that our brother is gone just like that No No
Chairman ndinga pange bwanji ndizikutumizilani khani
Were in Zambia but our hearts our bleeding
Ndiponso chigwada chake chimakhala chosinja kale😂😂😂 Mr ntanyiwa mumayidziwanso Randburg????😂😂 I love u Mr mumakwana Enawa ndi Ana awa❤❤❤🎉🎉🎉
Thanks for your update Big Baba
Congratulation mr mtanyiwa❤❤❤
Ntanyiwa katundu owopsa zedi ❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Iweyo Ntanyiwa ndi number one ndipo ndimamva nawe kukoma zed. Ndipo timamva zenizeni
Hehehehehe yomweyo galu iwe awuzeneni amvese comred ntanyiwa
Akutimenyera nkhondo anyamata awa amphawife😭😭😭😭😭😭😭
Oyenela kupepesedwa ndi akubanja km chakwela anapepesa ndi 5milioni ndizovesa chison kt chakwela akugawa ndalama kwa anthu omwe malilo sakuwakhuza tichedwepo pamenepa
Chobisika chili chose timavera kuchokera kwa limpopo FM kuchokera kwa khomuredi Ntanyiwa mumati vesa kukoma kwambili ndpo timaku pephelerani kwambili ndpo oyipayo sangaku kwaniseni kt akupangeni chipogwe ndpo mulungu apitilize kukutetezani mix born kalindo mulungu apitilize kukusungani ndimoyo wautari pa libe radio iliyose yomwe ingatiuze zoona zokha zokha ndi limpopo yokha bas mulungu apitilize kukumenyerani khondo nose
Bwana timakukondani ndipo timakunyadirani chifukwa mumatidziwitsa chirichose
Kkkkkkkkkk koma ntanyiwa kkkkkk usandisekese apa ....redson munlo mutu wake siumagwila olo mpang,ono pomwe ......anamangisa ukwati mamawa pofika madzulo ukwati watha ..naperi seventh day kunaperi ku blantyre ......redson munlo ndi chisilu cha munthu
TAnyiwa we are defending Malawi
Listening 🎧 from springs
Kkkkkkkkkkkk yochita zonsezi ndege yomweyo? 😂😂😂😂❤❤🇲🇼🇲🇼🇲🇼
That’s true Vs president he was going for funeral with suit and tie now he body is nicked so how take out his clothes is look like something that does happen, am very sorry what happened to him and died like thief and Chikwara he is proud like nothing happened
Ma demo akanapanga pa 20 coz ana pa 10 akhalabe akulemba mayeso
Limpopo FM 💪💪
Timakunyadirani alimpopo fm
Ku Randburg ndinapezako mbewa ndi ngumbi
Limpopo ndi namber one
Akufuna ma vote a chakwela kuti mafumuwo akalimbikitse anthu awo akati tiyeni timvotele MCP
Kodi photo ya a chilima yogwira kolona alipo angandionese?
NTANYIWA MBAMBANDE , KOMA VUTO NDI ROTI MAFUMU NDI ANTHU ADYERA KOMASO MA BISHOP MITUYAO SIGWIRA NTCHITO, NDIPO MAFUMUWA AKUFUNIKA KUWAGWIRA PAKHOSI KOMASO MA BISHOP NDI ANTHU OTI SANGATHANDIZE DZIKO CHIFUKWA MWAIWO U MULUNGU MULIBE MWSIO MEADZAZA NDI DYERA MALO MIYANG'ANA DZIKO MOMWE LIKUYENDERA NAONSO.TIWAPANGIRA MADEMO NGATI SAKUDZIWA ASATIONONGERE DZIKO CHIFUKWA CHADYERS LAO IYAAAAAA
Koditu pagulupa pali zisilu zina zadya ndalama zokukuba ndiye asowa choyankhula ......mukuteteza anthu oti akukuzunzuni kodi ndalama akukupaanizo akupasani kangati .....chakwera akuchoka pavute pasavute ngati akakamire mmalawi muno mukhala nkhondo ya nyooooo .... Chakwera kumwela sazapita komanso kumpoto
Eeeeee imfa iyi ikupweteka ukailingalira, Ambuye kumwambako mumadziwa zonse😢😢
Inetu ndi mathokoza kwambiri a Limpopo FM ndipo ndadziwa ndale chifukwa cha Limpopo FM pitirizani kutipatsira nkhani zonse mulungu adzikudalitsani bambo muthwanyiwa
Yes anawavula ndani?? Poti ndege ilibe manja 😅
Hand mistake sorry I want to press like ❤😂
Nthanyiwa umakwana timakunyadila MCP ndiyamagazi mmaja kuyambira kale
I ❤ Limpompo fm
Ndikangolowa pa UA-cam choyambilila ndi mafuna ndi mvele Limpopo fm koma ka melody mumaikaka kamatalika kwambiri musanayambe kulankhula ofcourse ndika bwino koma kasamatalike kwambiri nthawi Zina timakhala tili pachangu nde kamatipangisa kuti tisamalize kuvela
Vgg🎉
We are not young GOD is watching
God pleasease,, protect ntanyiwa Abeg 🙏
Bwana Mtanyiwa gwirani ntchito Basi osalimbana ndizinazi zikuiwalitsani zochita
We salute you
Limpopo to the world 🌍
Listening from randburg..
Same to me
Mmatiimirira bwana
Koma nde Apengedi misala mwinanso anachita kuyitanidwa kuti atsekedwe pakamwa nkona adzibusa Mafumu ndi ena azipembezo zosiyana siyana akukhala phe kumangoyang, anila dziko likungowonongeka chifukwa chodya chibanzi Mulungu akulangeni nonse amene mukungolandila ndalama koma chilungamo mukuchidziwa
Koma nde okapanga kidnap wo adzafera konkotu
Mzimu wa Chilima itipatsanso hope ina mayooooooo ine A Chilimaaaaa😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Missing dear ❤
Limpopo tiziwiseni munthu ama munkhapa chilimayo timuziwe
Mbambande Limpopo
More fire
Uyu ndi machine owopsa zedi Ntanyiwa❤❤❤❤❤❤❤
Limpopo ndekuti chani
Demonstrations a kulu timbwela better there tell us🌟 the 😭 truth why there killed our brother
Khumbo la apolisi anthu komanso a army, ma doctors,amphuzitsi....its just better life not to be rich
A chair man
Nkhani zodabwitsatuu iziiii
Ntanyiwa sing'anga amuka drip yamadzi atapita kukathamangitsa mizimu mwaterooo😂😂😂😂
Mbambande mtanyiwa❤
Limpopo FM❤❤
Mmalo mokonza zinthu mudziko muno kuti zikhale bwino, akuganiza zomapanga kidnap ana athu, sizikukumvesani chisoni mukamaganiza zausatana zanuzi👺👹👿 ?, conscious guilty sikumakupezani mukamaganiza zausatana zanuzi asatana inuu👺👹👿?, pam.... panu
Tikutsatila mwachidwi
Ndipo inuyo munasowa😂😂😂😂
Ndege inatengaso ma phone
This is sad for sure
Mumakwana inuyo big
Tiuzeni inuyo munali mundegemo mukutifusaso ife
Following ine zanga phee mix lawyer ndilibe kkkkkk
We can't 10 July come one come all their see
Kkkkkkkk ndiwe galu kwambili eti
Koma ndiye anthu awa
Ndipo mulungu azikudalisani
Kkkkkkkkkkk koma zidyamula nandolo
Rip our vp
Apatsa Ambuyache mafiti opephera km mulungu awayendele
Chimene akufunira kuti apange kidnap ana athu mchiyani?, ana alakwa chiyani?, even omenyera ufulu athu a genuine mmalawi muno alakwa chiyani?, tiwonensanaa ,
Tizapindula
Limpopo mumakwana from Cape Town
Umatha ase
Ayelekeze kupanga kidnap anawo awone zomwe zichitike mmanyumba mwawo asatana amenewa 👺👹👿☻
Koma Limpopo ikubwera boh
Our last hope Limpopo fm
More Fire Limpopo FM.....More Fire ....This is very sad 😢😢😢
Ndipo tisaladi kudyako chilungamo chioneke basi
🙏🙏🙏🙏