BRENDA KOSAMU, LOST & FEARED DEAD

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 201

  • @PeterHartzeberg
    @PeterHartzeberg 5 місяців тому +20

    Ambuye chifukwa chan ndimalephera ndikukuthokozan komwe pazochepa zomwe mwandipasa ,,,😢😢😢😢😢😢 ndisithen ambuye ndikuziwen inu muzimu ndimuchonad mayi ineee😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @ednadeliwemsungu-manyungwa1371
    @ednadeliwemsungu-manyungwa1371 5 місяців тому +8

    Surprisingly, it is the rich that go for family planning and yet those who are struggling keep on having more children without following kulera. Look now, 7 children without a father, this should change. Tisalemetse anthu oti sizikuwakhuza

    • @JaffarMongola
      @JaffarMongola 5 місяців тому

      Muziyankhula bwino plz

    • @user-jennifermisinde
      @user-jennifermisinde 4 місяці тому

      Sakunama..nanga munthu ulibe thandizo ana onseo uzitani nao.

    • @AugustineMwamadi
      @AugustineMwamadi 3 місяці тому +1

      Samazuzula munthu Ali mu coffin it's like kuyimba nthungululu pa maliro zikatere timangopepesa ndikupereka thandizo ngati lilipo kenako uphungu ine ndinu anzeru ndi ozindikira komano mudzidziwa kuti ena amaphunzira atalakwisa ofcoz am not intending to jump your point mukanalangiza izi zisanachitike osati zitachitika muzikhala ndi chisoni ndemanga mwapelekayo palibe kusiyana ndi. Kumapasa mbama munthu amene Ali pa oxygen

  • @Hannah-p7q6k
    @Hannah-p7q6k 10 днів тому

    Azlimayi timakumana ndi zinthu zowawa koma eish timapilira munyengo zowawawisa mulungu adalise azimayi onse pachisaliro chomwe amapereka kwa ana awo 😢😢

  • @kingnavitcha6243
    @kingnavitcha6243 5 місяців тому +9

    Kma Rodwell Lumbe Mulungu adzikudalitsa kwambiri 🙏

  • @BrendaDimba
    @BrendaDimba 5 місяців тому +4

    Kumalawi kuno kuli umphawi wadzaoneni,God bless you rodwell

  • @prudencebanda6516
    @prudencebanda6516 5 місяців тому +8

    Choyamba mayiwo akaseketse Kaye ana achuluka

    • @Dorah-zl9uf
      @Dorah-zl9uf 5 місяців тому

      Ndipo inu eish

    • @SinyoroMoyo
      @SinyoroMoyo 5 місяців тому

      Akatseke bwanji?sabelekanso mesa amuna anamwalira.

    • @AngellaZawanda
      @AngellaZawanda 5 місяців тому

      ​@@SinyoroMoyosakwatiwaso?

    • @AmossMwenda
      @AmossMwenda 4 місяці тому

      kkkkkkk

  • @AlinafePhili-u5t
    @AlinafePhili-u5t Місяць тому

    Zikomo ambuye chifukwa chazabwino zomwemumatipangil adalisen Bambo alordiwel

  • @MaxwellChakwela
    @MaxwellChakwela 3 місяці тому

    May God continue blessing you Mr Rodwell for reaching out and the hand given

  • @greenkosamu-uq4hg
    @greenkosamu-uq4hg 5 місяців тому +1

    Congratulations to you mr good job mulungu azikudslitsani kwambiri dziko lino munakakhala anthu ngati inu zinali bwino iwe ndithu utankhala president dziko lintha kusintha

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson 5 місяців тому +2

    Rodwell My God bless you keep it up

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 5 місяців тому +11

    Komatu mayiyu ngosamalila ana ndiovutika koma ana akuoneka osambako

    • @PeterHartzeberg
      @PeterHartzeberg 5 місяців тому

      Ndithu kukuuzan,zovalaso zowoneka 😢😢😢😢😢😢😢

    • @tadalapatrick5914
      @tadalapatrick5914 5 місяців тому

      Ndipo akuoneka ana health mulungu ndiwodabwisa samana zonse

    • @TalitaDaniels
      @TalitaDaniels 5 місяців тому +1

      Eshii ambuye sithani nyengo zamai yu ndiinu osamala ambuye

  • @MkandawileLloyd
    @MkandawileLloyd 5 місяців тому +4

    Inuyo ntchito mumaigwira mulungu azikusogolelani Lodwell❤❤❤❤

  • @GodfreyMajamanda
    @GodfreyMajamanda 5 місяців тому +1

    Linyangwa that's my home village and I was working at Linyangwa health centre from 2010 to 2014 before posted to Dedza DHO in November 20214

  • @GraceMwale-b1b
    @GraceMwale-b1b 5 місяців тому

    Uncle aRodwell Ambuye akulitse malire anu ndipo Ambuye akudalitse afikire zokhumba zanu komanso kukutetezerani pa ntchito yotamandika yomwe mukuyigwira 🙏🙏 Almighty GOD bless uncle Rodwell 🙌🙌

  • @RuthTimothyChirwa
    @RuthTimothyChirwa 5 місяців тому

    Keep it up my brother may god bless you ❤❤

  • @NaomiMoyo-x2r
    @NaomiMoyo-x2r 5 місяців тому +1

    Koma Rodwell mulungu akudalitse pofika police kutumiza anthu kwaiwe dziko likukudalira ndithu mulungu akuze malire ako❤❤❤

  • @JosephChikweni
    @JosephChikweni 5 місяців тому

    You are doing a wonderful job

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c 2 місяці тому

    Mmmm mulungu zikomo pa zinthu zomwe mmatipangera mulungu inu mkule ine ndichepe nthawi zonse😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 5 місяців тому +1

    Big Up brother ❤❤❤

  • @ChristopherKasonya
    @ChristopherKasonya 13 днів тому

    Ambuye achitilen chifundo amai awo ndi banja lawo chitilan chifundo moyo wanga ambuye ndichikhumbo khumbo changa kut mutandidalitsa kut naneso ndizadalitseso athu ena monga momwe akuchitila mr Rodwell

  • @ShakiraArridie
    @ShakiraArridie 5 місяців тому +2

    Bwana wazolengedwa zonse mudzimusamalira Rodwell mkupatsa moyo wautali

  • @ChisomoBisani
    @ChisomoBisani 5 місяців тому +1

    Kumwamba kulandile ulemu🙏🙏 mwagwira tchito yaikulu

  • @allimataka6924
    @allimataka6924 5 місяців тому +1

    Big man mulungu adzikudalitsa ndipo akupatseni moyo wautali

  • @GraceLobart
    @GraceLobart 5 місяців тому

    Zikomo ambuye 🙏 pachilichose chomwe mumandi pasa ngakhale yena amatichochepa km kwaine chokwanila kwambili ndithu 😢😢😢😢

  • @ShakirahCassim
    @ShakirahCassim 5 місяців тому

    Ngakhale sindikukuziwani koma mulungu aonjezele ppamene mwachosapo ❤🎉 achimwene

  • @ABASHACeeMW
    @ABASHACeeMW 5 місяців тому

    God 🙏 bless you bro work hard on ❤❤

  • @ObadiaMeja
    @ObadiaMeja 5 місяців тому

    Eshiiii kma ambuye😭😭😭😭😭 anthu kunjaku akuvutika ndithu! Ayendereni ndipo muwakhuze ndizanja lanu lamadalitso monga mnachitira pa tenafe posintha nyengo zathu😭😭😭😭😭

  • @Getrudegetrude-q2p
    @Getrudegetrude-q2p 4 місяці тому

    Ambuye azikudalitsani thawi zonse pa tchito yomwe mukuigwira achimwene

  • @eldabanda7453
    @eldabanda7453 5 місяців тому

    Rodwell 🙌🙌🙌 may God bless you more.

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 5 місяців тому +1

    zomvetsa chisoni anthu akwanthu ku Dedza kwa chidewere..kwa kanyenzi ku chikoma😢😢😢

    • @fannyzimba149
      @fannyzimba149 5 місяців тому +1

      Wawo kanyezi lknow the placr

  • @BrightonChimzimu
    @BrightonChimzimu 3 місяці тому

    Mul utumiki mwa inu

  • @LeonardKenneth-t9f
    @LeonardKenneth-t9f 4 місяці тому

    Tiyeni tigwirane manja powathandiza mayiwa Kuti mwina angayambeko business Kuti azipeza thandizo latsikundiku komaso tithokoze Mr Rodwell APA zaonetsad Kuti iwowa ndimzika yeniyeni yaMalawi yosadzikonda ambuye azikudalitsani malume

  • @tadalapatrick5914
    @tadalapatrick5914 5 місяців тому

    Esh god continue to bless you brother

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 5 місяців тому

    God bless you more and more blessings to you brother

  • @MiniusChiuma2
    @MiniusChiuma2 3 місяці тому

    Ndakumbukila masiku omwe ndinkadwa feya ndidabwerela kwamayi 😢😢😢

  • @RichardMolande-ri3rl
    @RichardMolande-ri3rl 5 місяців тому

    May God bless you for helping people.

  • @FrancisGomani-w5d
    @FrancisGomani-w5d 5 місяців тому

    I wish nditazakumana nawe Lodwel... May God bless you

  • @successm-vt3dx
    @successm-vt3dx 5 місяців тому

    mulungu inuyo adzikudaritsani bro

  • @BerthaNkhata-p8o
    @BerthaNkhata-p8o 4 місяці тому

    Ambuye ndikozeni ine

  • @Sofi-p1v
    @Sofi-p1v 5 місяців тому +1

    Komatu pena umphawi timachita kuusaka pa Ana 4 okhawo amenewo ndimavuta kale.ndiye nkuonjezeranso atatu ? Pena pake kungosakha kuzuzitsa Ana...

  • @AishaPanjira-od9hg
    @AishaPanjira-od9hg 4 місяці тому

    Rodwell mulungu akudalisani

  • @ShadreckKaleso
    @ShadreckKaleso 5 місяців тому

    Rodwell God bless you, all the time 🙏

  • @RaphiqueYusuf
    @RaphiqueYusuf 5 місяців тому

    Pepani kwambiri Mulungu akutsogolerenizabwino zonse,komadi anthufe tiri pamabvuto owopsya zedi.

  • @Mavitoabdulla
    @Mavitoabdulla 4 місяці тому

    Rodwell mulungu akuwonjezere masiku ambiri.usazafe

  • @JackAluya
    @JackAluya 4 місяці тому

    Only God know

  • @AngellaZawanda
    @AngellaZawanda 5 місяців тому

    Eishiiii Koma Rodwel iweyoooo???? 😢mulungu akupatse moyo ,mphavu ,zelu zochuluka .komaso akuze malile amoyo wako ngat momwe anamuchitila yabesi.chifukwa Anthu tikuthandizika .mulungu akudalitse ndithu

  • @ElizabethKazambwe
    @ElizabethKazambwe 5 місяців тому

    Imfai 🙌

  • @EricCanada-ig9xe
    @EricCanada-ig9xe 5 місяців тому

    Ambuye daritsani banja limeneri kopotsa Amen 🙏🏽

  • @PeterNsapato
    @PeterNsapato 4 місяці тому

    nde who's feared dead apapa im lost

  • @veronicachuma9313
    @veronicachuma9313 4 місяці тому

    Eish koma abale tiyen tidzilela plz izizi tu sizabwino eish mukuzutsa ana taonan iii asabelekeso yi

  • @ThinoSG
    @ThinoSG 5 місяців тому

    Gus job , be blessed

  • @MuhammadIssa-g3g
    @MuhammadIssa-g3g 4 місяці тому

    Mulungu awonjezere pomwe mukuchotsapo Mr ..

  • @sylessidrisah3032
    @sylessidrisah3032 5 місяців тому

    Komaso penapake tiziti kupolice or kuwagulilako gwaladi anthuwo inde sindikukana anawathandiza komabe

  • @mirriamwilliam-nq9wg
    @mirriamwilliam-nq9wg 5 місяців тому

    Eeeish ndalira kobas,, koma ambuye awalitse maso ake pa inu asinthe nyengo zanu kut anawa aphunzire,,,

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 4 місяці тому

    Koma pali ana mmmn, God have mercy 😢

  • @gideonnkute4820
    @gideonnkute4820 5 місяців тому

    Big up Rodwell❤❤

  • @lonnythom
    @lonnythom 4 місяці тому

    Mulungu ndiwazatheka bwanji

  • @MussahMbawalalah
    @MussahMbawalalah 5 місяців тому +1

    God bless you Rodwell

  • @FrankMsiska-i9j
    @FrankMsiska-i9j 5 місяців тому +1

    😢😢😢 chonena ndilibe

  • @sahilsenzani2307
    @sahilsenzani2307 5 місяців тому

    Mulungu akudalitsen

  • @DinaNicholas
    @DinaNicholas 5 місяців тому

    May God Bless you Rodwell

  • @Enless-n2c
    @Enless-n2c 5 місяців тому

    Ambuye mupaseni Rodwell moyo wautali

  • @FelistersBulawayo
    @FelistersBulawayo 5 місяців тому

    Rodwell Ambuye akuze malire ako

  • @justinemlongoti
    @justinemlongoti 4 місяці тому

    Ambuye azikudalitsani ndikuchulukitsa pazomwe mumachotsa pakuthandiza kwanu

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 5 місяців тому

    Nanuso my kumangobereka ana choncho lero taonani

  • @MartinChinkhuntha-e6w
    @MartinChinkhuntha-e6w 5 місяців тому

    You should be our president buddy

  • @atupelemposa4786
    @atupelemposa4786 5 місяців тому

    Mayi woziwa kusamala ana ,ana sakuwoneka kuthimbilila

  • @PaulMunukwa
    @PaulMunukwa 5 місяців тому

    Akuru Mulungu apitilize kukuza malire anu God bless you

  • @PreciousDzonzie
    @PreciousDzonzie 4 місяці тому

    Man mulungu akudalitsen mwawonetsa mtima wacikond km kwaenafe likhale phuzilo zobeleka ana ambirimbiri ndizakale ndibwin kukhalanawo awiri or modzi bas

  • @MikeMussah-w4y
    @MikeMussah-w4y 5 місяців тому

    God bless you bro and Citizen

  • @JamesMadona-s9c
    @JamesMadona-s9c 5 місяців тому

    Ambuye akuze malire anu pa ntchito yambwino yomwe mukugwira

  • @PaulKambuzi
    @PaulKambuzi 5 місяців тому

    Mayiyu ndiokonda ana ake

  • @edwardcomfort2085
    @edwardcomfort2085 5 місяців тому

    Koma Rodwell usazafe iweyo God bless you 😢

  • @ImranJuma-x9w
    @ImranJuma-x9w 4 місяці тому

    Allah bres you

  • @esternchimwala6926
    @esternchimwala6926 5 місяців тому

    Amuna anu kumwalila osawauxa akuchimuna zoona ?

  • @JanetMasache
    @JanetMasache 5 місяців тому

    Komanso mwini farm akuyenela kufikilidwa atiuze chifukwa chani sanadziwitse achibale za imfa ya tenant wawo

  • @JamesGeosterMalikebuPhiri
    @JamesGeosterMalikebuPhiri 5 місяців тому

    Koma bambo ameneyo/malemuwo amampanikiza mkaziyo samapumayi, zaka zomwe anakwatilirana nzochepa koma ana mpweche iiiìì chisoni.

  • @menkmufti6512
    @menkmufti6512 5 місяців тому

    May God bless you rodwel.

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm 5 місяців тому

    Km moyo uuu ndi ozunza mmm rodwell mulungu azikudalisa ukugwira ntchito yotamandika ambuye akuze malire amoyo wako

  • @ChifundoJeffrey
    @ChifundoJeffrey 5 місяців тому

    God bless you Rodwell❤❤

  • @JenipharBanda-e4q
    @JenipharBanda-e4q 5 місяців тому

    Mulungu azikudalitsa Rodwell Lumbe Mmmmm anthu akunvutika

  • @NaomiMoyo-x2r
    @NaomiMoyo-x2r 5 місяців тому

    Komano bwenzi akulera😢

  • @gilbertdamba7344
    @gilbertdamba7344 5 місяців тому

    Anthu akuvutika awa Koma president maulendo achuluka bwana tawathandizeni Mai awa pls kubomako

  • @joanamatiki6169
    @joanamatiki6169 5 місяців тому

    God bless you alot Mr

  • @hannockmzemanda7076
    @hannockmzemanda7076 5 місяців тому

    Mulungu tsegulani khomo la Make Ndaziona

  • @patisonlufan2823
    @patisonlufan2823 5 місяців тому

    Zosayenda

  • @edithmfunafuna
    @edithmfunafuna 5 місяців тому

    Eeeeeeeee😭😭😭😭😭😭

  • @TuwenSuman-i8h
    @TuwenSuman-i8h 5 місяців тому

    May God keep on blessing u

  • @ZaiZaituna
    @ZaiZaituna 5 місяців тому

    God bless you Mr lumbe 😢🙏🙏

  • @chissojozzacephasfrank
    @chissojozzacephasfrank 5 місяців тому

    God help people through people we thank God

  • @RehemaDaudi-ww6zd
    @RehemaDaudi-ww6zd 4 місяці тому

    Ambuye ngati sindimayamika ine muzindikhilulukira😢

  • @BridgetChaomba
    @BridgetChaomba 5 місяців тому

    May almighty God bless you rodwell

  • @CeciliaChaimabanda
    @CeciliaChaimabanda 5 місяців тому

    God bless you 🙏 mr

  • @Peterkumsanja
    @Peterkumsanja 5 місяців тому

    Komatu nkhani yokhudza kwabasi

  • @ayishaslaju6357
    @ayishaslaju6357 5 місяців тому +1

    Zoonadi Allah azikuwonjezerani

  • @JonerdandhamuzMisokwe
    @JonerdandhamuzMisokwe 4 місяці тому

    Eee zithusizilibwino

  • @MEGANABIGAILMNTHALI
    @MEGANABIGAILMNTHALI 5 місяців тому

    Ambuye azikuzabe malile anu Mr Rodwell ntchito mukuigwila kuposa apresident

  • @MalitaKapesi
    @MalitaKapesi 5 місяців тому

    Km abale dzikoli anthu akuvutika ambuye chonde tichitileni chifundo ,, ndipomwe chakwela president opanda nzeru akungoyendayenda kuononga ndalama pomwe anthu akuvutika chomchi ambuye mumuchitile chifundo chakwela sakudziwa chomwe akuchita

  • @bernarddaniel4413
    @bernarddaniel4413 5 місяців тому

    Eish koma dzikoli anthu akuzuzikatu

  • @maggiekadzombe7658
    @maggiekadzombe7658 5 місяців тому

    God bless you Rodwell eee