SAMEER SULEMAN WAULURA PA INTERVIEW KUTI MCP IKUTUMIZA ZIGAWEGA KUTI AMUPHE MPAKA ANAPANGA IZI

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 18 січ 2025

КОМЕНТАРІ • 157

  • @HamzahTwaib
    @HamzahTwaib 18 днів тому +16

    Suleman ndiwe dolo serious,,, ndiye wat big boys ili kt 😂😂😂 I like you

  • @EvanceSungani-cv9jk
    @EvanceSungani-cv9jk 18 днів тому +6

    Uyuyu timusalile kudya akhale VP adzachigwira bwino chipanichi who's agreed with me

  • @abgi.doctor.august
    @abgi.doctor.august 17 днів тому +4

    Only GOD knows what is happening MULUNGU wazatheka bwanji apitilize kukutetezani ndikukudalisani Mr Suleman 🥳🥳🥳🥳🥳🥳

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson 18 днів тому +22

    Koma ineyo kukamba zoona athu amene akumasapota mcp ali ngati mbuli kwaine 😂😂😂

    • @Franklifo2217
      @Franklifo2217 17 днів тому +2

      Sukunama aise.. kuona munthu wankulu ukumangonvela chisoni.. kut koma nzelu zilimo.?

    • @veronicagullo9373
      @veronicagullo9373 12 днів тому

      ​@@Franklifo2217xokonda kusiyana

  • @TechZaketa
    @TechZaketa 18 днів тому +7

    I like this guy ali ndi utsogoleri uyu 💪💪💪 ndithu

    • @bennkamkota8524
      @bennkamkota8524 10 днів тому

      Uyu or u president akhoza kulamula ndi mutu

  • @Japlennthondowa
    @Japlennthondowa 16 днів тому +2

    This is not interviewing but kukambilana anthu a side imodzi ,,coz chimene ndimadziwa ine akamati interview.. interviewer amafusa mafuso not taking a side
    And we are following ❤
    Just wait en see 😂

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 17 днів тому +1

    Tazaimileni upresident bwana❤❤❤❤❤😢😢😢😢😢😢😢

  • @JamesSuman-if2xo
    @JamesSuman-if2xo 15 днів тому +1

    Mtolankhani do not explain amaganizo ako. You are the interviewer. 😂😂😂😂

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 18 днів тому +7

    Ndege yasilikali imakhala ndi parachute. Anyamula bwanji vice president opanda zozitetezera mundegemo

    • @joshuaagabu3032
      @joshuaagabu3032 13 днів тому

      Akulu zimenezo ndizammafilimu. Inu ndi ine kutipatsa parachute kuti eni duphani tikafika pansi ndikuvulala modetsa nkhawa kapena kufa kumene as if we didn’t use a parachute. Vice president and his close protection team are not paratroopers trained to jump out of an airplane with or without a parachute.

    • @henryphiri6100
      @henryphiri6100 13 днів тому

      @joshuaagabu3032 4.5m high ndege ingaphanyike chonchi

    • @joshuaagabu3032
      @joshuaagabu3032 13 днів тому

      @@henryphiri6100 Ndizotheka musiyawale pali component ya speed, ku korea ndege yayaka itafika kale pansi chifukwa cha speed inalephela kuyima msanga inakamenya chikupa ndikuphulika. Pali zinthu zambiri za technical zimene anthu ngati ineyo tikuwona kuti inali ngozi yachilungamo koma poti anafa ndi munthu wamkulu wa ndale zokambakamba sizimalephela. Ngati panali chiwembu zimenezo ineyo ndilibe umboni oti ndidziloza anthu chala zimenzo timusiyile Mulungu.

    • @henryphiri6100
      @henryphiri6100 13 днів тому

      @joshuaagabu3032 magazi anapita kuti, nanga bwanji panalibe mafuta pogwera ndegepo. Mkulu dikirani mudzaziona. Inu kunalibe 1983

    • @joshuaagabu3032
      @joshuaagabu3032 12 днів тому

      @@henryphiri6100 Ndichifukwa pamapeto a comment yanga ndinati ngati panali chiwembu mulungu adzatiwonetsa tonse nthawiyo ikadzafika.

  • @joshuaagabu3032
    @joshuaagabu3032 13 днів тому +1

    Iyi inali podcast to puch DPP agenda osati interview. Mtolankhani akuchita kufunsa mafuso kuli nkhani ikomele DPP and pena akumayika ka opinion kake kokometsela chipani. 😃It is ok zipani zimakhala ndi ma podcast.

  • @HawaHussein-o5k
    @HawaHussein-o5k 18 днів тому +1

    My comrade sure man you r the best politician we love you may our lord bless you with long life health life protection n guidance more faya my bro sureman

  • @BenjaYagolo
    @BenjaYagolo 16 днів тому +1

    Uyu ndi katundu ndipo kulimba mtima kwake kumandi limbitsa mtima kwambiri long live fada

  • @matildachikhoswe
    @matildachikhoswe 13 днів тому

    Brother suleman you deserve to be a leader

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 18 днів тому +3

    Dpp my vote mcp out soon

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 17 днів тому +2

    Mr suleman ndikuziwa kt Apure azasila in udindo ,hope ya amalawi ili pain

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому +1

    Za a mtali manja, zisiyeni, kodi munthu waku mec alipo amene bambo or mai ake sadachitepo ndale. Umbuli mukuchitau, kodi iweyo suleman mwana wako sakuyenera kutenga any position m'boma la DPP simply because you were there before. Ndi umbili ukuchititsani izi, bwanji last time DPP IG sanali a northern person for example.

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому +1

    How would you feel Suleman, if someone addressed the president as "you"

  • @EliyassYusufu
    @EliyassYusufu 18 днів тому +1

    Suleman we love you so much musasiye osawopa akuchepa mcp abwelele kudabwe

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому +1

    Zamabodza izo Suleman, sete zako, have you forgotten munagula ma tractor ku India and you declared them zachabe chabe kenako munagulitsana nokha nokha a DPP, pano matractor mulinawo m'makomo, munagula pa auction ma 50 pin per tractor, lero mukunya mwano oterewo, anthu oipa inu?

  • @Sumaili-rs2we
    @Sumaili-rs2we 18 днів тому

    Zikunika president wa experience well educated and wa integrity with good strategies.

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 18 днів тому +3

    Suleman number one ❤

  • @AmosNyirenda-c4c
    @AmosNyirenda-c4c 13 днів тому

    Let Kabambe team up ndi Sulemani

  • @zebronchipate7297
    @zebronchipate7297 15 днів тому

    People with vision like you are highly wanted to run this nation

  • @wideafire9784
    @wideafire9784 16 днів тому

    wamalapu Lapu bwino, ulemu wanu my uncle Suleman..

  • @PiliranKaunda
    @PiliranKaunda 17 днів тому

    Ur strong leader mr Suleman

  • @Vincent-ce9cf
    @Vincent-ce9cf 11 днів тому

    Interviewer wake wamolare😂😂😂 Odi ndizingoonera

  • @MarryMartin-z6u
    @MarryMartin-z6u 18 днів тому +1

    Big up mr❤❤❤❤❤

  • @CharityChirwa-v8v
    @CharityChirwa-v8v 17 днів тому

    Sukunama iwedi ndimpulusi wathu ndawonela mwanawanga snamphuzila papole ndintolakhani koma zakq 5 akusaka chito osayipeza pano mozikakamoza analowa chito ya police zosezi chikangawa i love you big boss sulemani

  • @wezimwalebanda-ux4sm
    @wezimwalebanda-ux4sm 18 днів тому +5

    Sulemani sindidamuone koma amandiatsa chikoka sir i love you

  • @lameckmajiga5426
    @lameckmajiga5426 18 днів тому +2

    Ndikamuwona Samia Suleman ndimawona ngati ndawona SKC chilima!! I don't know why!! Muthu olimba ntima kwambili!!

  • @Chrisy-n1o
    @Chrisy-n1o 17 днів тому +1

    Big up sir

  • @OwenMindozo
    @OwenMindozo 18 днів тому

    This is Bishop Owen M.Tembo, let me encourage you, the Bible says do not afraid God is with you, justice is justice.

  • @matildachikhoswe
    @matildachikhoswe 13 днів тому

    Dpp will come back into power

  • @innocentnamondwe9650
    @innocentnamondwe9650 16 днів тому

    man of courage Sammeer

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumani 18 днів тому +2

    Sulemani mukunena chilungamo, momuopa mulungu koma mulungu apange zoteka kuti bomali lichoke chilungamo chioneke

  • @DominiqueChitimbe
    @DominiqueChitimbe 17 днів тому

    Good boy big man 💪💪❤

  • @FunaniChagwira-ue5pl
    @FunaniChagwira-ue5pl 17 днів тому

    Mighty DPP my Vote

  • @TameeraInglis
    @TameeraInglis 12 днів тому

    MCP musamasewele ndi katundu waboma pangolini musiye sameer Suleman simungamake pa iyeyu.

  • @AbdullahSaeed-e7z
    @AbdullahSaeed-e7z 17 днів тому +1

    May Allah bless u Mr suleiman ❤❤

  • @YasinMmadi
    @YasinMmadi 17 днів тому

    Mr sulemani pliz dzusaninso anzanu ku parliament mukhaleko kagulu anthu olimba mtima ngati Inu pliz mwina nkuliphula dzikoli pa moto

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela 18 днів тому +1

    I like this boss

  • @jackalview7491
    @jackalview7491 17 днів тому +2

    Kunkuyu peleka black box

  • @MaqsoodJailos-c6v
    @MaqsoodJailos-c6v 18 днів тому

    Following keep it up

  • @GraceShaibu-i9d
    @GraceShaibu-i9d 18 днів тому +2

    sulemani big up osatopa osafoka🔥🔥🔥

  • @CharlesChimera-l3j
    @CharlesChimera-l3j 18 днів тому

    Bwana sulemani chonde maganizo abwino musazasinthe

  • @AlainTembo
    @AlainTembo 17 днів тому

    Bwana bigup inu mumakwana

  • @JamesZanelo-iv1wb
    @JamesZanelo-iv1wb 18 днів тому

    DPP nayo analindizofooka zake and some of the challenges we're currently facing ......akungopitilra kuchokera ku ulamuliro wa Dpp. MCP ndiye ikungotimaliza basi.Mcp and Dpp nonse ndiamodzi.

  • @tiwongeluhana9272
    @tiwongeluhana9272 18 днів тому

    NTSB imangofufuza za ndege zomwe zinapangidwa ku USA koma zopangidwa ku Germany ali ndi bungwe lawolawo lotchedwa Bundesamt für Verkehrswesen (BAV), which is responsible for investigating transportation accidents in Germany.

  • @HamuzahBamusi
    @HamuzahBamusi 17 днів тому

    Koma mcp ambuye please kumene kuliko please please please ife akapolo anu simungaawatenge agaru amenewa

  • @blessjare
    @blessjare 18 днів тому

    Suleman tizikupemphererani mufike mu September mulungu akudalitseni

  • @nokosemakolija-xe9do
    @nokosemakolija-xe9do 18 днів тому +1

    Am not a journalist koma i think the interviewer needs not to take sides. Let him ask questions oyankhayo aziyankha not being directive

  • @MaryPhoya
    @MaryPhoya 17 днів тому

    ❤❤❤❤❤you are blessed sir

  • @MarryMartin-z6u
    @MarryMartin-z6u 18 днів тому

    Zoona ine pay slip yanga yochititsa manyazi😂😂😂 mdulidwe too much. Koma nthawi ya APM ndinalibe ngongore ine😢😢

  • @patriciajangaza675
    @patriciajangaza675 18 днів тому +1

    A MCP akudana ndi makaladi , amiya anali nkaladi chilima komaso akuluwa awawa akufuna atsale okuda ngati makarawa

  • @JimmyRajab-o7n
    @JimmyRajab-o7n 16 днів тому

    Mwazi onela Nokia mupange chothekela mutengenso Boma kuti muzawamange anthu amenewa

  • @MagieJames
    @MagieJames 17 днів тому

    Mcp ikuyenenayo singafane nd DPP wava awa ationesa zosaona chikangawa party iweyo ngt ukufuna mcp uziikonda

  • @ChibakuliAlia
    @ChibakuliAlia 17 днів тому

    ❤❤

  • @Andy20247
    @Andy20247 18 днів тому

    Anakwilira pa malopo inquiry ilimkati bwanji komatu MCP guyz Chaka chino chilungamo tichipeza ndithuuuuhh

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 18 днів тому

    ❤❤❤Sureman

  • @AskMeDalitso
    @AskMeDalitso 18 днів тому

    Big brain

  • @ashingsmvula3357
    @ashingsmvula3357 12 днів тому

    Suleiman stop saying you can die for Malawians...this is an insult

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p 18 днів тому

    Under APM the headlines were the same. Mr. Suleman corruption was just as bad, tizi pewa bwanji?

  • @RabeccaMkandawire-i9j
    @RabeccaMkandawire-i9j 17 днів тому

    Ambuye mutetezeni Suleiman

  • @MdalaBonomali
    @MdalaBonomali 18 днів тому

    I love this my brother Allah bless him ❤❤❤

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 18 днів тому

    Komanso 4.5m high ndege kuphwanyika chonchija. Atenga nzeru zaku Zimbabwe. Nthawi yachisankho zinali choncho ku Zimbabwe. Amagwiritsa ntchito a intelligence kuti adziopseza anthu.

    • @JJ-in-the-hut
      @JJ-in-the-hut 18 днів тому

      😂😂😂 Chakwera Ndi Mnangagwa kale

  • @amosphakira7936
    @amosphakira7936 17 днів тому

    Suleman tsogolo lako likuonekera ,si iwe Nankhumwa ai .iwe udxathandixa anthu Dxiko la Malawi tikudxiwa.

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому

    DPP inalibe transparency, zinthu mumafufuta ndi tipex, tipex adakuyalutsani agalu inu

  • @EndaleAbebaAlemu
    @EndaleAbebaAlemu 17 днів тому

    Pangolin wathu

  • @MusaJali-bu3cl
    @MusaJali-bu3cl 16 днів тому

    Chakwela ndi mbuli yophudzira yosaziwa mayendesedwe adziko

  • @edsonkamba3170
    @edsonkamba3170 15 днів тому

    Malawi is going back to the dark 🌑 days

  • @HildaLimbusha
    @HildaLimbusha 18 днів тому

    Forward with Dpp

  • @MustapherLino
    @MustapherLino 18 днів тому

    Tikamupatsa 5 years dzina tonse titha 😂😂😂 chikangawa achoke

  • @jomochirwa
    @jomochirwa 18 днів тому

    Kumalawi kwadzala zitsilu zokhazokha pa ndale.mumangokhala ndi ma propaganda auchitsilu.inutu simudzalowaso m'boma.dpp idawononga dziko lelo mudati mukoza dziko ,zitsilu inu .😅

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому

    Bomali Lili ndi mavuto oti likonze koma bomali silikadakwanitsa kuchita control shock yomwe malemu Chilima adachita go through, when the plane was out of control. Akulu akulu tisamalankhule za maganizo chabe, it doesn't matter how young and energetic we are, akulu akulu ngozi ya ndege simasewera, chinthu chija chimathamanga, imagine accident ya galimoto pa top speed ya convoy ya president, how much possible damage. Ndiye ndegetu imathamanga speed yoposa 400 to 600 km/ h, imagine At 400, and fall down from air,

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому

    Suleman ulibe umunthu, alubino wasowa kotenga, nthawi imene ija alubino mumachita kusaka in various homes, nanga anjinga za moto mumaundila kwa biwi, ziwalo mumapita nazo kuti?

  • @JamilaJafali
    @JamilaJafali 18 днів тому

    Pangolin umakwana samil

  • @JuniorSaine-d6r
    @JuniorSaine-d6r 14 днів тому

    I just luv the program but am finding some difficulties with person wearing a shirt.Am failing to call him a journalist because he is lacking journalism skills, otherwise he can do better.
    Talking about Sameer,he is a man of integrity and I do respect him alot. Viva Malawi 🔥🔥

  • @ShareefKalima
    @ShareefKalima 18 днів тому

    Ndine ntchewa koma ngoz za kuchikangawa Aliyese sakusangalala nayo mpaka panopa. Ndine wakulilongwe koma ndikuopa mulungu tabwelesan black box anthu akukhulupililan koma apart from that aaaaq M.C.P wakupha

  • @HamuzahBamusi
    @HamuzahBamusi 17 днів тому

    Nde kupanda nzeru kumeneko anyamatawa nde mesa akukunyeressni manyi thumba lachimanga pano 60 nde pamtumbo pamenepo

  • @RabeccaMkandawire-i9j
    @RabeccaMkandawire-i9j 17 днів тому

    Suleiman ndi Chilima 2

  • @AmosShadreck
    @AmosShadreck 18 днів тому

    Ee zafika pamenepa mpakana 😢

  • @yamikanijoseph9381
    @yamikanijoseph9381 16 днів тому

    Nice you are recognizing munthu amakhala mu shock muchitsanzo chanu chomwe, nanga munthu wakuti ndege ikugwa, angakhale ndishock yanji?

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 16 днів тому

    Suleman wants to seek punlic sympathy. Za ziiiiiii

  • @ekranmulepa4548
    @ekranmulepa4548 17 днів тому

    Akulu awawa ndi Dolo hv amaziwa zochita pathawi yake

  • @henryhenry6632
    @henryhenry6632 18 днів тому

    Aportuguese aku Mozambique othawa nkhondo panyelo pamanu, & peter mathanyula mboli yamake muiwale zodzaphaso ma albino mmalawi muno dzimachende dzanu

    • @HamuzahRoben
      @HamuzahRoben 18 днів тому

      😂😂😂 ma phuzo amenewa bwanji malume

    • @henryhenry6632
      @henryhenry6632 18 днів тому

      @ amalawi ndife anthu opusa kwambiri kumalola anthu awa othawa nkhondo ku Mozambique adzitiyambanitsa tidzimenyana ngati mmene kulili kwawo panopa

    • @WedsonVinkhumbo-q9l
      @WedsonVinkhumbo-q9l 18 днів тому

      Suziwa chomene ukunena

    • @EdwardPatel-f1g
      @EdwardPatel-f1g 17 днів тому

      ​@@HamuzahRoben pakamwa pozolowera kutukwana, sangathe kuyankhula mopanda kutukwana 😂🤣

    • @HamuzahRoben
      @HamuzahRoben 16 днів тому

      @@EdwardPatel-f1g eeee muli kutukwana kuposa zimayitu🤣🤣

  • @RonnexPhiri-w4o
    @RonnexPhiri-w4o 18 днів тому

    My hon Mp

  • @PatumaSelemani
    @PatumaSelemani 18 днів тому +1

    Tikufuna athu ngat inu

  • @GiftBello-v1i
    @GiftBello-v1i 18 днів тому

    You are out hope Mr Soleman

  • @BacksonLevi
    @BacksonLevi 18 днів тому

    Aaaaa Inu musakhale gt abwino apa inu kupha mwapha anthu agt zaxzzzzz alibino anja amaphedwa daire zopusa eti

    • @PatriciaBanda-e3v
      @PatriciaBanda-e3v 17 днів тому

      Munkapha ndinu musanamepo why simunamangeko muthu after mutawina😢😅😂😂😂Bakha

  • @ChristopherMwase-n7n
    @ChristopherMwase-n7n 18 днів тому +1

    Ana ake atiwo

  • @IsmailTambula-g1k
    @IsmailTambula-g1k 18 днів тому

    Mulungu akutetezan mwin kulenga ozaopa komaso palibe wamuyaya ukamafunila zako zaifa ndipamene amamuonjezela mansiku amoyo

  • @BacksonLevi
    @BacksonLevi 18 днів тому

    Ka midiya aka chazeru palibe ofusa manyaka

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 18 днів тому

    Wopembeza mafuno wopembeza pitala not mulungu

  • @WedsonVinkhumbo-q9l
    @WedsonVinkhumbo-q9l 18 днів тому

    Malawi athu ngati awa sachedwa kuphedwa

  • @PatriciaBanda-e3v
    @PatriciaBanda-e3v 17 днів тому

    Sule iweeee

  • @EdwinZiwa-x2g
    @EdwinZiwa-x2g 18 днів тому

    Walowa mumalo mwa chilima iwe basi

  • @GraceWiskes
    @GraceWiskes 18 днів тому

    DPP wa m'boma chaka chake ndi chino akane akane alole alole

  • @ZephMbeleswa-n8m
    @ZephMbeleswa-n8m 18 днів тому

    Awawa mzeru alibe malo mowawuza anthu zoti muzapange

    • @EdwardPatel-f1g
      @EdwardPatel-f1g 17 днів тому

      Iyi si program ya kampeni,. Anu nde mukufuna akambe zomwe apange bwanji.. tazingogwirani maganyuwo

    • @ZephMbeleswa-n8m
      @ZephMbeleswa-n8m 17 днів тому

      @EdwardPatel-f1g iweyo nde upanga chani chifukwa ifeyo ndi dairy ku ganyu kupanga mchele awawaso akupanga mchele wawo chifukwa chake akukamba za anthu ena kkkkk

  • @stanleymagombo-ds6to
    @stanleymagombo-ds6to 15 днів тому

    mbambande

  • @NicksonKotokwa
    @NicksonKotokwa 18 днів тому

    Eeeee guys mumakwana