Eya ndiye pamene usakumvesa ndi pati? ngati akukana . Inu ndi gulu lano ndi imene mukuthandiza kuti ziko lizipita pansi, simungaziwe why satana Ali mbali yanu kwambili koma siku ndi limozi zikoli lizasintha mufune musafune .
Aaa😂😂takaesani kuimila ukhansala tidzaone performance yanu kungodzuka basi muli mufuna u President?😂😂by the way President wo mukaimila kuti zaka 35 simunakwanitse nkomwe
Iike this guy, he's very confident & he knows a lot.keep it up brother
This mn is intelligence
Keep it up
Keep it up we are behind you enough is enough
Mfundo zomveka bwino ndi zothyakuka uyu timpase u president 💪
Always behind You Braz
Keep it up my brother, following with keen interest
We support you mr
Live long broh may God protect u broh
Could like mahata to be Lider of Malawi 🇲🇼
My vote 🗳
Take my 🗳 vote
Our on Adama traole youth let's him we can have better malawi
Ibrahim not adama
Zoona uyu ndi Ibrahim Traore waku Malawi ndithu
My vote🔥
our own Ibrahim Traore❤❤❤
Good move
so wise and mature
Tili nawe aise pambuyo pako ndipo usafowoke ur my vote
God be with you always
Yes
Uyuyu ndi nkhani zina
Uyuu nde mbambande ndpo ameneyu timpange support guyz
uyu abwele pa mpando bas
Interview yakale kale iyi
Umakwana
yes I think that guy alibwino ameneyo
Amalawi ambiri akusowekera uthenga wa Denis Mahata
zoonad
Ibrahim traore wa ku malawi uyu ali ni fundo zabwino nakupanga follow lero
This guy he needs to be a President of Malawi
Ineyo ndikugwilizananawo tisithe osati peter kapena chakwera ai
Zoonad zofunika kusiya zipani zonse kupatsa Mr awawa
koma ichii chilii ndi mzeru man
Ichichi chimaganiza eish😂
Ameneyuu ndi khang'adituu mmmm
Katswiri
Ichichi mchidolo ndipo nditha kuchivotera or ka 10000000x
Comrade mahata ukuoneka kuti zelu zilimo koma wayamba mochedwa
Malamulo amakana simunafike 35years
Eya ndiye pamene usakumvesa ndi pati? ngati akukana . Inu ndi gulu lano ndi imene mukuthandiza kuti ziko lizipita pansi, simungaziwe why satana Ali mbali yanu kwambili koma siku ndi limozi zikoli lizasintha mufune musafune .
Uyu nd dolo ndthu uyu
Utsogoler obadwa nawo osat after kutopa kudambwe kumat ine mtsogoleri zachamba
Aaa😂😂takaesani kuimila ukhansala tidzaone performance yanu kungodzuka basi muli mufuna u President?😂😂by the way President wo mukaimila kuti zaka 35 simunakwanitse nkomwe
Iwe mutu wako sugwra
Lowa alliance ya Dpp bro
Denis utha kukhala utsogoleli wadzelu km vuto wadzionetsela mochedwa ku u presdentku ay asiye Bola angoyambitsa movement ya phavu
Pa mfundo zako zilibwino
Mulungu mutetezereni munthu uyu ndi ife tomwe chifukwa alindi songolo lanthu
28yrs 😂😂😂
Malawi needs wise people like you Mr Mahata
Tikufuna maganizidwe atsopano
Youth inclusion, lamulo lisinthe la dzaka za president
Denis utha kukhala utsogoleli wadzelu km vuto wadzionetsela mochedwa ku u presdentku ay asiye Bola angoyambitsa movement ya phavu
Denis utha kukhala utsogoleli wadzelu km vuto wadzionetsela mochedwa ku u presdentku ay asiye Bola angoyambitsa movement ya phavu