Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 9 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b 20 днів тому +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 20 днів тому +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane 13 днів тому

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @EversDman
    @EversDman 19 днів тому

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya 19 днів тому

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 20 днів тому +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 20 днів тому

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j 20 днів тому

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 19 днів тому

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 20 днів тому

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri 19 днів тому

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g 19 днів тому

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael 20 днів тому

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq 20 днів тому

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w 20 днів тому +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy 19 днів тому

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula 19 днів тому

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 19 днів тому

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t 20 днів тому

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 20 днів тому

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 20 днів тому

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 19 днів тому

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x 20 днів тому +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @SmartMoles
    @SmartMoles 19 днів тому

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x 19 днів тому

    Zoona amwene

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg 20 днів тому +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l 20 днів тому

    Awa ndie mawu

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton 20 днів тому

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu 20 днів тому

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 20 днів тому

    Big up bro

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f 20 днів тому

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m 20 днів тому

    Ai zikomo 🥱

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 19 днів тому

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @AffickChaona
    @AffickChaona 17 днів тому

    ❤❤❤❤❤

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 20 днів тому +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 20 днів тому

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 20 днів тому

    Ambuye akudalitsen

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd 20 днів тому

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d 20 днів тому

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 20 днів тому

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu 20 днів тому

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js 20 днів тому

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 20 днів тому

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie 20 днів тому

    Motor 💥 kalindoooo

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr 20 днів тому

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg 20 днів тому

    The DC 🔥

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l 19 днів тому

    Mumatiyimilila

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 17 днів тому

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v 20 днів тому

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 20 днів тому

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q 20 днів тому

    Dc

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 20 днів тому

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi 20 днів тому

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 20 днів тому

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa 20 днів тому

    Dzelu zachepa kkkk

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k 20 днів тому

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 20 днів тому

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 20 днів тому

    Ati kutitola kapena chani

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f 20 днів тому

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j 20 днів тому

    Awuzeni

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 20 днів тому

    Kalindo samaopa😂😂

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do 20 днів тому

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 20 днів тому

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 19 днів тому

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 20 днів тому

    😂😂 kung'alulatu

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera 19 днів тому

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 20 днів тому

    Bigiliman naweni

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b 20 днів тому

    😅😅😅😅

  • @AaronLitete
    @AaronLitete 20 днів тому

    Kkkkk boma lopusa

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro 19 днів тому

    😂🤣😂🤣

  • @GiftKulture
    @GiftKulture 20 днів тому

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k 20 днів тому

    😂😂😂😂

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i 20 днів тому

    K.K😂

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o 20 днів тому

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j 20 днів тому +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri 20 днів тому

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 20 днів тому

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 20 днів тому

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n 20 днів тому +1

    😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 20 днів тому

    😂😂😂😂😂