NKHANGA ZAONA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 14 жов 2023
  • tidziwe tv

КОМЕНТАРІ • 87

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 6 місяців тому +6

    Mwaswela bwanji nonse amene mumamvela pa nkhanga zaona.ngati mulibwino dzikomo

  • @Bowa-c7g
    @Bowa-c7g 6 годин тому

    Ndipo musasiye mukutisegula maso❤

  • @user-xi2jz8ru1w
    @user-xi2jz8ru1w 6 днів тому +2

    Antanyiwa ndakusowani

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 2 дні тому

    Yomweyo galu iwe Nankhumwa😅😅😅😂😂😂😂😂😅😅😅😅😅

  • @gracemnenula2518
    @gracemnenula2518 3 дні тому

    More fire kt Buuuuuuu!!!

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci 7 днів тому +2

    Osafoka osatopa osawopa

  • @SalimMeer-fk9do
    @SalimMeer-fk9do 7 днів тому +1

    Zana amayi asanka chifanti malunga ngati vice koma pano ndi opposite ndi zambiri zomwe amalankhula za boza

  • @JOHNDIMA
    @JOHNDIMA 4 дні тому +1

    Keep giving us updates

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 3 дні тому +1

    Limpopo fm moto buuuuuu

  • @PreciousLewis-su2pl
    @PreciousLewis-su2pl 18 днів тому +1

    timakunyadilila big man .mtiuzilekoso wa bakili Muluzi tv tawasowa mau ake😢😢😢 guys timakunyadilan

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 8 місяців тому +1

    Mwaswela bwanji abale anga pa nkhanga zaona,ineyo kuno ndilibwino

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 2 дні тому

    😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅kwagwanji bambo

  • @GraceLobart
    @GraceLobart 3 дні тому

    Osaopa mulipa bill yanga 😂😂😂

  • @TravelodgeMalawi
    @TravelodgeMalawi 8 місяців тому +1

    Tiyenazoni ,ife tilipambuyopa tidziwe

  • @josephcalisto
    @josephcalisto 8 днів тому +1

    Limpopo moto kuti buuu

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 7 днів тому +1

    Timanyadila Limpopo fm

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 5 днів тому

    Akut anapengapo Misara kkkkkk amawona ngt amalawi angagwrinse ntchito Misara yakeyo

  • @MorganBanda-oc2jx
    @MorganBanda-oc2jx 3 дні тому

    kunoku moyo wake ndi osiphina omwewu basi. Malawi zikuoneka kut m'manja mwa atsamunda sitinachokemo ayi

  • @MarthaJafali
    @MarthaJafali 6 днів тому

    Auzeni apite kumangochi aone

  • @KenedyJolamu-rs9xx
    @KenedyJolamu-rs9xx 4 місяці тому

    Mbambande nkhanga zaona❤️🔥

  • @SalimMeer-fk9do
    @SalimMeer-fk9do 7 днів тому

    Uyu ngwa maboza saziwa kufufuza nkhani zoona

    • @robenallie6985
      @robenallie6985 6 днів тому

      Ndizzkho zimenezo ife tikumudalira anatiuza kuti onse amu ndege amwalira zinali zoona

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 2 дні тому

    Mundifunsilenso chipatala chakumangochi chimawotchedwa chakandichaka zikukhalabwanji?

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u 17 днів тому

    Live from south Africa
    Muyaluka chaka chake ndi chino

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 8 місяців тому

    More fire broo osaopaaaa kunena chilungamo.

  • @khalifacalvinajass9998
    @khalifacalvinajass9998 8 місяців тому +2

    Limpopo FM more fire

  • @user-py4nr7yz4x
    @user-py4nr7yz4x 8 місяців тому

    Mukutiyimirira kumred go go go km ndikufuna nyimboyi yoti chakwera watipweteka anayimba ND ndan

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 8 днів тому

    Koma ambuye kumwambako musatipitirire ku Malawi 😢😢😢

  • @user-kw7hv5kg7z
    @user-kw7hv5kg7z 8 місяців тому

    More fire no fear comrade go go go!!!!!!

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 5 днів тому

    Opusa iwee ukusochelesa amalawi koma amalawi anapenya zidya drama za muthalikazo ife tikupitax chisogolo ndi mcp bas

  • @AnishaMoosa-ej7yr
    @AnishaMoosa-ej7yr 6 місяців тому

    Online from Pretoria

  • @MarthaJafali
    @MarthaJafali 6 днів тому

    Koma comrede indipha ndi phwete😂😂😂😂😂😂😂

  • @user-yk5xv4dt7v
    @user-yk5xv4dt7v 11 днів тому

    Lipopo fm Palibeso ai

  • @MagretMvula
    @MagretMvula 8 місяців тому

    Tikuthokozeni ntciito ndi yayikulu mukugwila more fire mulungu aikepo zanja tione mphumulo mumalawi

  • @DysonFly
    @DysonFly 9 днів тому

    Mumakwana bwana

  • @williamskondowe8795
    @williamskondowe8795 8 місяців тому +1

    Wanunkha malawi

  • @peterphir2250
    @peterphir2250 8 місяців тому +1

    Atsogoleri tikuyamikireni koma nkhani zanu simukumaliza mukaziyamba ngati mukunena kuti ntchito zomwe akugwira anthuwa ndi malipiro pa zomwe achita powotcha wa police ku Nsanje kutanthauza kuti anatumidwa ndi abomawo, ndiye a bomawo akuuzani chilungamo chotani? Inu mukadaulula zifukwa zomwe adamuwotchera wa police kuti womutumawo adziwe kuti abisala mmbatata musamangochulukisa kuseka ndi kamangoyimba nyimbo ayi, ifeyo timamvetsera ndi chidwi kuti nkhanga zaonanji tidziwe koma mumango nena molumpha lumpha ngati kuti zomwe mukuwulusa ndi zongopeka so please help us we love you

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr 8 місяців тому

      Ndipo message yomwe imasowa muno ndeiyiyi kkk kumatambasula bobo ngati muja apangila DC Kalindo, otherwise zikumavuta kuzitsatatu. Love you ❤❤

    • @user-oj5ye6bj9q
      @user-oj5ye6bj9q 4 місяці тому

      That's true muzimalizisa nkhanizo kut tiziziwa zoona zenizeni wr real love you mr Comrade

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 8 місяців тому +1

    dyimboyi iilibwinowo😂😂😂😂😂

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q 3 місяці тому

    Kulonjedza nde analonjeza ndikalephela kusitha dzithu kwa dzaka wilili ndizatula pasi udndo Kodi pana pano sanavomeleza kuti alephela kukweza Malawi pano Malawi alipamoto kuposa alamulilo wa muthalika

  • @user-hl5ii9ns8b
    @user-hl5ii9ns8b 8 місяців тому

    More fire Limpopo

  • @SalimMeer-fk9do
    @SalimMeer-fk9do 7 днів тому

    Bola bon kalindo ndi bakili mukuzi tv amafufuza mokuya kwambiri

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc 9 днів тому

    Osapa todze ndi amalawi fredom c_to_

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 6 днів тому

    Awa ndaboza awa

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 8 місяців тому

    Timakudyadirani our comrade!!

  • @user-cg8vg5mr6x
    @user-cg8vg5mr6x 8 місяців тому

    Yah tamudziwa.....uja ali ndi bukula azibambo

  • @johnynamano3862
    @johnynamano3862 8 місяців тому

    Zomaotchazi zisiyike chifukwa tsiku lina mudzagwidwa ndiye tidzaona

  • @user-wq3dh1ly2o
    @user-wq3dh1ly2o 9 днів тому

    Tilinawe limodzi limpopo Fm mumatiimilila

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 8 місяців тому

    Mwadza bwanji

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah 3 дні тому

    Osafooka osatopa osagonja

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 8 місяців тому

    Zoona big man

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 8 місяців тому

    Achimwene mumanikwana

  • @DickMdala-pn4pd
    @DickMdala-pn4pd 8 місяців тому

    Kkkkkk koma nkhani zimankhala apa🤣🤣

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 8 місяців тому

    Eisj where are you brah Malawi first we're confused ryt niw so brah plz tell us the truth

  • @LyfodKesten-he3fr
    @LyfodKesten-he3fr 8 місяців тому

    Lipopo mo faya

  • @user-yz1fk1dx1m
    @user-yz1fk1dx1m 8 місяців тому

    Kkkkk koma eeeee

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m 8 місяців тому

    Never give up

  • @WincoJulias
    @WincoJulias 8 місяців тому

    Zikachitika timvera kwainu

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 8 місяців тому

    ❤ big up brother

  • @mcdonaldsitima2107
    @mcdonaldsitima2107 8 місяців тому

    Auze ngozi

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n 3 дні тому

    😂😂😂😂😂😂

  • @LimbaniRojha
    @LimbaniRojha 7 місяців тому

    avomele zavuta ayimikemaja

  • @smt7036
    @smt7036 8 місяців тому

    fire fire

  • @Yahiya-wm8nd
    @Yahiya-wm8nd 8 місяців тому

    Koma Patricia unaziyamba wenkha kkkkk

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 8 місяців тому

    😂😂 amangonyera mplastic

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w 8 місяців тому

    Kkkkkkkkkkkk Sevethday

  • @user-rk3jx3kg8i
    @user-rk3jx3kg8i 8 місяців тому

    Mulipo angt,

  • @user-xq3rt3ou7z
    @user-xq3rt3ou7z 8 місяців тому

    Morefire

  • @SameKaposa
    @SameKaposa 8 місяців тому

    😂😂😂😂😂 Limpopo fm

  • @jossynaitha6863
    @jossynaitha6863 8 місяців тому

    😊

  • @DamianoKapachika-ft1ye
    @DamianoKapachika-ft1ye 8 місяців тому

    Zamphanvu

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk 8 місяців тому +2

    Go deeper comrade, proud of you always 🔥🔥🔥🔥

  • @patriciacraiton-sf5vu
    @patriciacraiton-sf5vu 8 місяців тому

    Kkkkkkkk 😂😂😂😂😂

  • @chelseajackson3200
    @chelseajackson3200 8 днів тому

    Lovely song🎉🎉🎉

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 8 місяців тому

    😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 8 місяців тому

    😂😂😂

  • @ImraanJafali-dk7rg
    @ImraanJafali-dk7rg 8 місяців тому

    Limpopo fm ndimainyadila kwambli simabisa zigawenge 😂😂😂 more fire nkhanga zaona ife nde malawi olilawo

    • @HOMEOFTECHNOLOGY
      @HOMEOFTECHNOLOGY 8 місяців тому

      Mumakwana Limpopo mumatiimirira Ife a malawi potidziwitsa zonunkha za afisi a nkhaza awa tikudziwanao zambiri 😂😂😂

    • @GanieAlidih
      @GanieAlidih 8 місяців тому

      Kwan

  • @user-yo4fl4ps5p
    @user-yo4fl4ps5p 8 місяців тому

    Zifukule zose zidziwike❤

  • @AnishaMoosa-ej7yr
    @AnishaMoosa-ej7yr 7 місяців тому +1

    Network problem ashh

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 3 дні тому

    Limpopo fm moto buuuuuu

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 3 дні тому

    Limpopo fm moto buuuuuu

  • @YassinMoffat
    @YassinMoffat 3 дні тому

    Limpopo fm moto buuuuuu