MAFUNSO OVUTA OMWE ATOLANKHANI ANAWAPANIKIZA NAWO A BON KALINDO LERO PAMENE AMACHITITSA CONFERENCE

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 7 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 358

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt Місяць тому +22

    Kuyankha mafunso mosanyengelela munthu the DC😂😂😂.

    • @PropeeLucious
      @PropeeLucious Місяць тому +1

      Mafunso ake ATI amalephera kuyankha o ha ha ha ha ha

  • @stevechikaonda3145
    @stevechikaonda3145 Місяць тому +6

    Tinene kuti wopaanda nzeru nduyu walemba kuti atolankhani anapanikiza Kalindo, coz he has been consistent and confident in his responses to the posed or you just wanted to lure us and watch this

    • @edsongeorge8032
      @edsongeorge8032 Місяць тому

      nkhaniyi ndiyoona malume opanda nzeru ndamene walemba izi.

  • @macrinenduna1024
    @macrinenduna1024 Місяць тому +21

    Pamenepa mukati atolonkhani anapanikiza mafinso, ndifunso liti lajejemetse Malawi Fist?

    • @user-vt4zo7eo2s
      @user-vt4zo7eo2s Місяць тому +1

      Ineso sindikupeza olo limodzi

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Місяць тому +1

      Palibe malawi first number one

    • @MarkJere-c2d
      @MarkJere-c2d Місяць тому +1

      Njila imodzi yofuna kut muonele kaaaa kkkk

    • @user-zy1eh3pt8v
      @user-zy1eh3pt8v Місяць тому

      I had the same question 😂😂😂😂

    • @edsongeorge8032
      @edsongeorge8032 Місяць тому

      @@user-zy1eh3pt8v inenso I wanted to ask kuti ndipati pomwe Bon kalindo ?

  • @danielmurichi5673
    @danielmurichi5673 Місяць тому +7

    Anyamata wa ali serious bwino kwambiri
    Keep it up osagonja ndipo boma limeneli lisamale osama one ngati malawi ndiiwowokhawo nafeso ndi malawi
    Pasafe olo mmodzi panewa kuteloko nkhondo idzayamboka chifukwa nthawi tiliyi ndiya democracy
    Tikufuna ufulu oyankhula osati kuopsezedwa

  • @user-sb2mw3xz4j
    @user-sb2mw3xz4j Місяць тому +9

    😂😂😂Koma KALINDO eish big respect,

  • @KingfrahMachado
    @KingfrahMachado Місяць тому +4

    Ndipo inu a bon mulungu aziwe pachilungamo chimene mukuonesa kwaife amalawi osauka❤

  • @TEACHTHEWORDMINISTRIESINTERNAT
    @TEACHTHEWORDMINISTRIESINTERNAT Місяць тому +12

    In fact chilungamo chake anayenera kuti adzigula sticker ndi amene wagwidwa atazemba pa boarder. Wokhulupirika apatsidwe sticker yaulele, wozemba akapezeka agule sticker ngati mbali imodzi ya chindapusa.

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 Місяць тому +6

    The DC woyeeeeee 🎉🎉🎉🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @KingfrahMachado
    @KingfrahMachado Місяць тому +4

    Akapusa mwezi sivuto end President aziter kuyakha mopanda mantha💪💪💪🔥

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z Місяць тому +6

    We love you Mr DC

  • @CharityGondwe-bw9gs
    @CharityGondwe-bw9gs Місяць тому +12

    Mumatiimilira mr kalindo ndi azanuwo murandire ulemu❤❤❤❤❤❤❤

    • @InnocentMtafya
      @InnocentMtafya Місяць тому

      Musaiwale atamupatsa u ambassador kupita kunja, anazasanduka munthu wina nkumati a Malawi sioafela koma makobidi nde dilu, mwaiwala, eti anapepesa...🤔🤔mmmhhh!(Ndalamaa eeeh!!!!)

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Місяць тому

      Kkkkk go ko nko sambe madzi achitedze basi 😂😂😂 😂😂😂 kalindo umakwana

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Місяць тому

      Osadanda tililimozi ati u ze 💪💪💪🔨🪓🗡️ bwino zatikwana

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Місяць тому +2

    Bon .you are very intelligent gentlemen. Iam behind you❤❤❤❤❤

  • @BenedictFriday-c2w
    @BenedictFriday-c2w 24 дні тому

    The DC keep it up the good work

  • @DollarChagamba
    @DollarChagamba Місяць тому +7

    Palibe fuso lomwe lawakanika kuyankha

  • @user-bi5lg8mg9y
    @user-bi5lg8mg9y Місяць тому +24

    Mr Bon kalindo z very strong weapon speech

    • @StanleyDama
      @StanleyDama Місяць тому

      Do y know the meaning of weapon ?

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Місяць тому

      ❤❤❤ 1277 kkkkkk

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Місяць тому

      Gwira chito kalindo 😂😂😂😂 kuswa kuswa kung'alura kung'alura😂😂 tiyenawo osawasiya😂😂

    • @ChipanganoPhiri
      @ChipanganoPhiri 24 дні тому

      Big boss

  • @user-rb7mp3rv7g
    @user-rb7mp3rv7g Місяць тому +5

    Pamenepa mafunso ovuta alipati please ma topic anuwa tamaonani Kaye aaaa😂😂

    • @martinndawala8125
      @martinndawala8125 Місяць тому +1

      Amangofuna anthu akhale ndi chidwi chowonera 😂😂

  • @HanishKenneth
    @HanishKenneth Місяць тому +7

    Kutchaya kugwetsa we are united

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju Місяць тому +3

    The DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥MRA sikuganizira ife ochita malonga...in add off kubweretsa sticker ndi njira imodxi yofuna kusokoneza ife a business kuti tisamapindule ...Boma lionepo bwino apa....

  • @PetroGondwe
    @PetroGondwe Місяць тому +1

    Kalindo is a true light to Malawian paths.youths wake up please,osamangovina amapiano fight for your nation and your future.

  • @daviebanda5098
    @daviebanda5098 Місяць тому +4

    Kkk akut amathamanga ndimasuti😂😂😂😂 booom the DC🔥🔥🔥

  • @AronZayaweh
    @AronZayaweh Місяць тому +8

    Masiku atha kale awaa chakwela abwelele kudambw

    • @UssenNjirinah
      @UssenNjirinah Місяць тому

      Kkkkkk mpaka pele ajawuleje kudambwe Kwene chinyago changatama ku state house chijaule kwawo kwawo kudambwe

    • @user-dl4ud7mp4n
      @user-dl4ud7mp4n Місяць тому

      😂😂😂😂😂

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Місяць тому +5

    Mr Chikangawa akutitola kwambiri

  • @PatYøna
    @PatYøna Місяць тому +2

    Yesterday I saw achinyamata akulemba anthu a kwa tongole in area24, ndinafusa modzi wa Iwo anati atumidwa kuti alembe anthu osati obwera but amagazi ... Kuti adzilandira ntukula pakhomo every month and fertilizer. But onse ogula malo ayi asamulembe. Is this fair abale inuuuu 😢😢😢

  • @PastinaHope
    @PastinaHope Місяць тому

    Tikuthoza kwambir a bon karindu pa zime mpatipangira ife osauka mulungu akhare ND Inu nose ❤❤🎉

  • @FrancisMbwana-z5l
    @FrancisMbwana-z5l 29 днів тому

    Very powerful from kalindo

  • @DysonChiumia
    @DysonChiumia Місяць тому +3

    The DC🔥

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 Місяць тому +3

    The DC🔥🔥🔥🔥

  • @EffordKapichi
    @EffordKapichi Місяць тому +1

    You are our weapon chief

  • @user-ee1ci2ku6o
    @user-ee1ci2ku6o Місяць тому +6

    We are frant of you mr kalindo DC 💪💪💪💪

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Місяць тому

    Kalindo ndinkamuna ogona kukhomo kosachinjika abro 🔥🔥🔥🔥 Yehova apilile kumusunga ndimoyo wautali

  • @YamikanipilatoPilato
    @YamikanipilatoPilato Місяць тому +2

    Number one chi dc

  • @BlessingsNyirenda-ru7ss
    @BlessingsNyirenda-ru7ss Місяць тому +2

    More fire born kalindo

  • @williammasiano1194
    @williammasiano1194 Місяць тому +2

    Viva Malawi 1st ...eish anthu amafika potopa

  • @emmanuelmuyilaa
    @emmanuelmuyilaa Місяць тому +4

    Koma kumeneko❤

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Місяць тому +5

    Kumpoto kumwera tikuoneka ngati sindife amalawi. Koma achigawo chapakati ndi a Malawian. Kumupoto kulibe chilichose i love you Mr DC and your members mademo alhalepo tikufuna chilungamo si nkhondo koma kukoza ziko lathu

  • @JonathanHeadson
    @JonathanHeadson Місяць тому +3

    Mafunso akeso ati ovutawo nanu

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Місяць тому +6

    Kuchokera 2020 mupaka pano chimene tapidula ndibomali kukumangidwa boza kulankhula mozikona kulekerera muchitidwe wa katangale kulembana pamutundu ntchito kuononga immigration kuononga ACB kuononga admac kuononga apolice kuononga nkhalango ya chikangawo po gwesako ndege kuononga nrb kuononga chipani cha utm kusunga nduna zachiwewe muchipani zopanda phindu. Ndizina zambiri zaonongeka kumalawi ndichitukuko chimene talandila kumalawi for 4years mmmm

  • @isaacthawani5442
    @isaacthawani5442 Місяць тому +2

    Ndie awa akut mafuso ovuta mene akuyakhiramo sukuona kt dola ndi kalindoyo mbuzi iwe

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek Місяць тому +4

    The DC moto wokhawokha

    • @ClementKawinga-ik7wn
      @ClementKawinga-ik7wn Місяць тому

      Chakwera bomaaaaaaaa palibenso amene ndikumuona basi ndi Lazarus

  • @DonPhiri-u2j
    @DonPhiri-u2j Місяць тому

    Ife tikungodikira mulungu atithandize coz ulosi wa malemu grace chinga unanena kale kuli kuti kukubwera chipani cholimbana ndi mwazi komaso thukuta kma mukamaliza zonsezi muziwe kuti mulungu achitapo mbali yake ife tikuyembekeza pamulungu osati munthu amen

  • @PeturosiNyirenda
    @PeturosiNyirenda Місяць тому +1

    😂 bon kalinda nd 1🎉

  • @PropeeLucious
    @PropeeLucious Місяць тому +2

    Ndati ndikuuze I kuti bon kalindo akupusisani eye ndi ganyu imeneyi please please achinyamata musamangotenga ndizina zili zonse mtambo anakunamizan pano ndi bon kalindo please changamuka achinyamata mmalo mosaka ndalama kuti moyo wanu usithe muli busy kuchemelera munthu wina mmmmmmm

    • @SalaJawali
      @SalaJawali Місяць тому

      Utiuza zopusa zo ife tilibe Maso owonela kuti dziko muno zinthu sizilibwino

    • @robenallie6985
      @robenallie6985 Місяць тому

      Iwe ndi wa mcp

    • @SharonNdadza
      @SharonNdadza Місяць тому

      Nawe akupasa a mcp ndrama? Chonsechonso azimbuyanu akuvutika mma midzi uko

    • @PropeeLucious
      @PropeeLucious Місяць тому

      @@SharonNdadza ndye zoyankhula za kalindo zipangisa kuti ambuye asavutike mmmmmmm mbuli za kalindo muzafa chifukwa chosatilq zinthu zopusa ngt zimenezo

    • @PropeeLucious
      @PropeeLucious Місяць тому

      @@SalaJawali iwe ndye kalindo ndi amene angasithe zinthu musanamizidwe kuti kape ngt amene uja palibe chimene angaphule

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Місяць тому +1

    Kalindo ndi wa DDP chonde a Malawi musapuse naye akudya ndalama za peter anapatsidwa target

  • @MadalitsoChipangula-i3z
    @MadalitsoChipangula-i3z Місяць тому

    Mwana uvuta kwambiri the Dc zimenezi ndizo zofunika kwambiri kunokwanthu kumalawi

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 Місяць тому

    More fire bon

  • @jamessingini-fh1bz
    @jamessingini-fh1bz Місяць тому

    I cant wait pa 8 August ,bravo team Dc❤

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy Місяць тому +2

    The DC ❤❤

  • @ChikondiMaguza
    @ChikondiMaguza Місяць тому

    Am coming to join u guyz❤

  • @TachikoMwanamanga
    @TachikoMwanamanga Місяць тому +1

    The DC 🔥🔥❤️

  • @OMEXTWAIBU
    @OMEXTWAIBU Місяць тому +1

    Chakwela my vote ❤

  • @HiAlvin
    @HiAlvin Місяць тому +2

    DC awavula Ngati anadya ndalama akabweze alephera kufusa

  • @RasLuntha
    @RasLuntha 28 днів тому

    We must fight for our rebarty and freedom

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb Місяць тому +2

    Mafunso onse ayankhidwa, what else do u want?

  • @TanazioUziyele
    @TanazioUziyele Місяць тому +2

    Aaa akalindo ndale

  • @Atheeeefire
    @Atheeeefire Місяць тому

    Respect the DC keep the fire burning

  • @user-eo2hl9ug1h
    @user-eo2hl9ug1h Місяць тому +1

    Muyende..bwino...Isha. Allah

  • @COSMASSDAVITY
    @COSMASSDAVITY Місяць тому

    D.C MWANA OVUTA NDIWE NYO😂❤

  • @MercyJohnsonkanchure
    @MercyJohnsonkanchure Місяць тому +2

    Mr DC ulemu wanu kuti yimilira Amalawi

  • @evalisterphiri8435
    @evalisterphiri8435 Місяць тому

    This is true, ma profit ndiochepa kale koma BOMA ili palipose utulutse ndalama and now this mmm.... Mademo akufunikadi

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Місяць тому

    Komano bon kalindo wawayankha bwino.Lopanda nzeru ndiboma ndiutsogoleri omwe ulipoli.Pa 8 go konko

  • @user-sm4vo2uo7g
    @user-sm4vo2uo7g Місяць тому +3

    The dc mwana wachabe

  • @DanJohn-ws5gl
    @DanJohn-ws5gl Місяць тому +2

    Mbambande the DC

  • @user-oe3dz7dy4j
    @user-oe3dz7dy4j Місяць тому

    Zoona amacharger ndarama popereka chidindo,,, your true fighter kalindo

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c Місяць тому

    Born kalindo respect big up

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Місяць тому

    Ife tikudikila pa 8 pano ✊💪✊

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 Місяць тому

    Born ❤❤❤ ndi one guys timakufirani abro❤❤❤

  • @MagunjeNewa
    @MagunjeNewa Місяць тому

    Mr Born kalindo hoyeee

  • @user-ri8em6my2e
    @user-ri8em6my2e Місяць тому +1

    Bon tiwomboleni asatana amenewa asatibere chonde 😭😭

  • @user-pe2tu1ip3v
    @user-pe2tu1ip3v Місяць тому

    Good news ❤good work

  • @WillmotChiuimia-vr6ou
    @WillmotChiuimia-vr6ou Місяць тому

    Yes , kuyankha kwabwino ndinthu mmm ndikanapanga nawo mademo amenewo yes yes

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m Місяць тому

    The DC ❤❤❤❤❤

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Місяць тому +1

    Mulungu akusungeni ndi moyo gays wina aliyese ukumba zenje pa inuyo agwelemo yekha mudzina la yesu

  • @RobertChisenga-ci2mq
    @RobertChisenga-ci2mq Місяць тому

    I wish bon kalindo azakhere minister of the land
    Kaya zikhare ng,oma mai yolam kukuyu
    Azakhara mwaufumu muno kaya.

  • @heartilygarven2624
    @heartilygarven2624 Місяць тому

    Ulemu wanu Mr DC kuyankha mopanda nkhawa

  • @estherkachingwe3605
    @estherkachingwe3605 Місяць тому

    God bless you Mr Bon kalindo

  • @PeterChuma-jr1vz
    @PeterChuma-jr1vz Місяць тому

    Atolankhani agonja kunooo kkkk kuyankha mosaopa

  • @AgnessKavalo
    @AgnessKavalo Місяць тому

    Kkkk komatu bon kalindo amathamanga ali mu suit 😂😂😂😂😂😂😂 koma mdaseka mokweza mau 😂😂😂

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Місяць тому

    The DC president wa anthu osawuka 💪✊ we always with you

  • @smartselemani2070
    @smartselemani2070 Місяць тому

    Sweet talk with hidden agenda.

  • @InnocentMtafya
    @InnocentMtafya Місяць тому

    Ambwiyee !!! Mafunso afunsidwa ndimayembekezela zachabe ,koma ambwiyeee!!!

  • @GiftSoko-w4h
    @GiftSoko-w4h Місяць тому

    KATUNDU BOOOOOOOOON KALIIIIIIINDOOOOOOOOO LOVE YOU MY GUY

  • @GladsonBanda-m3e
    @GladsonBanda-m3e Місяць тому +1

    Apresitent chamba chilitho nkumati tikuimira anthu kumangadi zingongo you should read as an example kalindo

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Місяць тому

    Atolankhani aku malawi ndi mbola, amafunsa zopepera kwambiri.
    Utolankhani weni weni unapita ndi achina Eunice Chipangula osati izi zathovwa.

  • @Agin2pex-ms3di
    @Agin2pex-ms3di Місяць тому +1

    Buka matevu 🎉

  • @IanAllstal
    @IanAllstal Місяць тому

    Kodi kalindo umkachedwa ndi ma drama chifukwa chani? The D C 🔥🔥🔥

  • @macksonmkandawire5718
    @macksonmkandawire5718 10 днів тому

    Bon kalindo kkkk make ndi vice president sopano

  • @user-ii6lu1wy5f
    @user-ii6lu1wy5f Місяць тому

    We are with you Mr DC

  • @GreenBadani
    @GreenBadani Місяць тому +2

    💪👍💞

  • @innocentmusuli7380
    @innocentmusuli7380 Місяць тому

    Mongo bwereza zomwe ndakhala ndikunena kuti any time, any day, any week, any month from now achinyamata azuka ndikuchosa nyasi zonse belive this

  • @MaloneBanda
    @MaloneBanda Місяць тому +4

    Good work 💥💥💥💥

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Місяць тому

    Akalindo ayaluka mademowo kumwela Koko

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z Місяць тому

    Achina kalindo ndiakamuna osati masewela.

  • @isaacharoon5652
    @isaacharoon5652 Місяць тому

    Kalindo akuchita bwino,komano kwa anthu amene amaononga zinthu za anthu,inuyo a kalindo anthuo muzawalipila,chifukwa anthu akuba amalowelela.simutisaukisaaaaaa?

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 Місяць тому

    Chokani apa inu mulibe strategy iliyonse other than mademo.
    Don’t worry tikakufinyani konko

  • @MarthaBango
    @MarthaBango Місяць тому

    😂😂😂😂😂iiIi ati masuti kothamanga😂😂

  • @DoulassSamuel
    @DoulassSamuel Місяць тому

    Iweyo born ukungofuna udindo usatinyasepoapa

  • @LucyTatianahChikwekwe
    @LucyTatianahChikwekwe Місяць тому

    More fire 🔥🔥🔥 the DC

  • @TANMBWANA
    @TANMBWANA Місяць тому +1

    Mr chikangawa zawavuta

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Місяць тому +1

    Dc 🔥🔥🔥

  • @MarthaMalopa-kw9xw
    @MarthaMalopa-kw9xw Місяць тому +1

    Pali funso lomwe lalepheredwa kuyankhidwa apa?