Mr.Kamulepo and this man Bon Kalindo,we don’t need Chakwera to proceed ruling this country up to November 2024.Please let’s organise tough strategies for him to step down.Bravo Kamulepo,Bravo Bon Kalindo
To be honest Malawi is going backwards people voted for Tonse alliance for hoping better life but federal system of government is the only way enough is enough.
Mr. Kamlepo Kaluwa, ndine Mponda kuno, ndidakali kuno ku Soweto, but a'm taking my pension next year, I will be meeting you next year. I think u remember, Japheth Nkhoma, Mr. Kanyongolo, Mr. Maseko all from Soweto
Take that word .they will not manage what is coming , i believe something big is coming i say it again something big is coming anyamata soon azuka ndipo it will be like Kenya 🇰🇪 anthu akatopa amatopa kuti topi kungotopa basi
Inu a Nonse Alliance ndinu mwaba cilungamo CA a Malawi . Leromukamaphedwa, nokha mukudabwa! Mumanena kuti Peter wadaba vote za Chilima ndi za Chakwera. Za Atupere ndi ena Peter sanabe. Bwanji bwalo lamirandu linalola zipani 9 zikhale pamodzi? Tsono lero mukuti mukubwerera ku Cipani cimodzi? Pamenepa opusa ndani?
Mcp yapalamula chitedze,,, when you pray for the rain deal with the mad too,, Chakwera umva madzi chaka chino ine Mulungu anandiyankhula momveka bwino kuti akuvupula kowopsya,uyaluka,, ngati ungathe umupatse makobili Mulunguyo tiwone, my God is exposing you this year you are finished,, awa ma prophet mwawapatsa ndalamawa akukunamizani ask me i will tell you what the Mighty Lord God said,, your judgement has just begun enjoy it
Once an eagle always an eagle. We believe in you the real freedom fighter legend Kamulepo Kaluwa. We're going to vote without their stupid ID'S protocol
The Dangerous Freedom Fighter of Malawi Nation, Kamulepo Kalua.. Our trust is on you Mr Kamulepo. Long live our freedom fighter
Mr.Kamulepo and this man Bon Kalindo,we don’t need Chakwera to proceed ruling this country up to November 2024.Please let’s organise tough strategies for him to step down.Bravo Kamulepo,Bravo Bon Kalindo
Ana asatana amakomenta zodana ndichilungamo ife pambuyo panu mr kamlepo ❤❤❤❤❤❤❤
Well said, Commander. People don't know that you are a Field Marshal
Bravo Mr Kaluwa . Timadziwa Mr Kaluwa simunthu wamba kuti angamayankhe mafunso opepera ndipo wamuphu nzitsa kafunsidwe mtolankhani wa DPP yu . Siungamuthe Kamulepo wachepa
Good Messnge Mr kamulepo kaluwa, Chakwela you mast go watikwana
a veteran freedom fighter,, a comrade, last man standing
Malawian majority is Malawian s not achewa, big up kamlepo no divisions in Malawi, Malawi is 1
God bless mr kamulepo ❤❤❤❤
A mr. Kamlepo Kalua munayamba kale kumenyela ufulu, ndipo sitilola a Malawi. Alephera achoke basi. A Malawi ndi okwiya kale ndi ulamuliro wa chakwera.
Mr unable kamulepo kaluwa you are a hero thanks dad for speaking the truth we know as anew generation
Munthu wankulu kuyankhula mosaopa ngat mene amayankhula nthawi ya kamuzu nde chakwera ndindaniso pano anthu anachenjera kusiyana ndi nthawi ya kamuzu
Powerful Mr kamlepo ❤❤❤
To be honest Malawi is going backwards people voted for Tonse alliance for hoping better life but federal system of government is the only way enough is enough.
Koma sitima yayamba kudutsa ku area 50 inatha njanje
A MCP aputa Munthu wolakwika.
Nzeru zikacuruka Zina zimataika Cifukwa ninji munapanga zipani 9 kukhala Nonsa Alliance mukudziwa za ufulu wa zipani zambiri?
God bless you.
A kamlepo mulungu adzikudalitsani ❤🎉🎉🎉🎉
Well spoken loud and clear 🔥🔥🔥🔥
Mukusewela ndi kamlepo munthu amene amatha kupanga mabomba wanya chakwera
Am listening ❤❤❤❤❤❤go deeper ❤❤
The message is clear
I love your speech bwana Kamlepo
Good talking mr kamlepo
More fire kamplepo❤❤
Good news Limpopo makwana💪💪
Comrate kamulepo kalua he is great man,
Atapezeka awiri atatu olimba mtima ngati Mr. Kaluwa ndithu things can change koma vuto ndi mantha amalawi😢😢😢
Federal system of government it's the best in Malawi, we wa development not to keep billions for Malawians in the pocket,
Powerful 👊
Ekwendeni to Euthini anausiyizila pa T/A Mtwalo please wativwileko msewu wajimika chomene wula tikusuzgika pakuya kukaya ku Euthini mwee😢
Powerful 👍 👍 👍
Kamlepo adang'aza uyu ha is not the one I was listening in those good old years, he is mad now, shame
Mr. Kamlepo Kaluwa, ndine Mponda kuno, ndidakali kuno ku Soweto, but a'm taking my pension next year, I will be meeting you next year. I think u remember, Japheth Nkhoma, Mr. Kanyongolo, Mr. Maseko all from Soweto
❤ the greatest chat
Kamulepo❤❤
Tose tivota kuno
Take that word .they will not manage what is coming , i believe something big is coming i say it again something big is coming anyamata soon azuka ndipo it will be like Kenya 🇰🇪 anthu akatopa amatopa kuti topi kungotopa basi
Bravo Mr Kamlepo Kaluwa
Kandeu from south africa currently za ndengezi zisatidwe bohboh China chake sichilibwino
Following
💪💪💪💪🔥🔥🔥
Fight for Malawians mr tivote tonse opanda ma ID basi fire eee
Mwatikondwesha dada kaluwa u president ukumuyanani not galu uyo walipo watikomera chilima
A MALAWI TISALOLERE CHIPANI CHIMODZI CHOKUPHA ANTHU OSALAKWA. AMALAWI DZIKO LATHU SILACHIPANI CHIMODZI. AMALAWI TIYENI TILICHOSE DZIKO LATHU PA UMPHAWI WA MCP
Tnauzidwa kt tizawuzidwa pakadutsa masiku 10, koma mpaka pano kuli ziiii!
Inu a Nonse Alliance ndinu mwaba cilungamo CA a Malawi . Leromukamaphedwa, nokha mukudabwa! Mumanena kuti Peter wadaba vote za Chilima ndi za Chakwera. Za Atupere ndi ena Peter sanabe. Bwanji bwalo lamirandu linalola zipani 9 zikhale pamodzi? Tsono lero mukuti mukubwerera ku Cipani cimodzi? Pamenepa opusa ndani?
✊✊✊✊✊l love your speech Kamulepo kaluwa
Live from south Africa
Mwayowoyako va zeruu mwahuno
Akuti ntolakhani , osadziwa kuti CENTRAL GOVERNMENT OR FEDERAL GOVERNMENT ndichyani kukhuta NAPWIRI basi
Bola MCP isamuphe kamlepo. Anthu akupha awa. Mulungu chonde apengetseni misala a MCP
Inu wakwanatu chakwela 😢😢😢
Ngt zili zomagendanazo muwaudze asayerekedze kufika ku southern region azaona nyekhwe
Program yofunikira kwambiri
Mudziko muno tikufuna anthu ngati awa oyankhula chilungamo, osaopa ife tikufuna dziko lathu aliyese asangalare osati akumipando okha ayi
Bvuto ndi mcp administration umbuli wachuluka from the president down the line mbuli zokha zokha.
Strong speech mr kamlepo ambuye akutetezen bwana
Chilungamo
Ofunika kwasumila amenewo a mcp
Let's violence now tawonelera nyasi nthawi yaitari
Mmm but this chipani mcp mmmm not good
Kamulepo munthu mulala chomene
Chakwera pa thako pako kwizako Kuno Ku muponto Yai .kutikomera mubaliwinthu Yai
Ndamene anayambisa democracy mmalawi. Simunthu wamba uyu. Ali ndi history
Zidze mzatonse
Mumanena chilungamo
Mcp yapalamula chitedze,,, when you pray for the rain deal with the mad too,, Chakwera umva madzi chaka chino ine Mulungu anandiyankhula momveka bwino kuti akuvupula kowopsya,uyaluka,, ngati ungathe umupatse makobili Mulunguyo tiwone, my God is exposing you this year you are finished,, awa ma prophet mwawapatsa ndalamawa akukunamizani ask me i will tell you what the Mighty Lord God said,, your judgement has just begun enjoy it
Achikule munthu wazeru
Koma ndiye za mowadi zaziiiiii 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Tiye uko mwana wa mcp iwe kupusa kwako
IQ zero
Pita kanyele uko mwana wa nyau iwe
Ngat manyi akugwiran kanyelereni musatinunkhise apa iya
Galu wachabe chabe
2025 tikubwera komweko ife usilu ayi
Let's learn from South Africa what H E Ramaphosa had done t o bring unity and patriotism bent on his genuine philanthropy. Long-live!
Mcp she is not going anywhere
😂😂😂😂 She is?
Chizungu cha mcp chimenecho kutathauza kuti onse ndi akazi wokhaokha Aku mcp ko 😂😂😂
Lol😂😂😂
Chizungu chaku gule😂😂😂😂
Aweeeeee 😂😂
Once an eagle always an eagle. We believe in you the real freedom fighter legend Kamulepo Kaluwa.
We're going to vote without their stupid ID'S protocol