Ulemelero wa malawi unachoka basi ....Bingu was q blessing and special gift to us malawians koma tinali mu m'dima.May forgive our country and give us someone like him😮
We ll never find president like him 😭😔 abwino sakhalisa I believe when he passed away Pano asala ndi anyapapi wokha wokha bingu wamuthalika we still remember you
Good speech that people with good confidence will follow it forever, he died for body only but spirit for him still alive. Your body rest in peace almighty name of Jesus Christ Amen 🕊📖.............✍
ndine wa mcp koma pa bingu hmmm zinali nkhani zina mpaka 2009 mutu wanga unapenga bingu ngati anatumidwa ndi ambuye kudzatilamulira moti pazoipa zake zimene anthu amanena ine ndimaziika m'manja mwa mulungu coz satana anakwanitsa gawo lake kutitseka maso ndikumadana ndi utsogoleri wangilo
koma osati zinazi kungoonjezela kuipitsa mbili yake koma sindikukhulupira kudzaonaso tsogoleri ngati ameneyu ngakhale kamuzu sangafike pamzelu zake rest in piece baba
ZIMANGOONA KUVUTA BUT THIS MAN USED TO INSPIRE ME A LOT
MAY YOUR SOUL CONTINUE RESTING IN PEACE
WISE TALKING
Anthu abwino sakhalisa paxiko I remember you Bingu Mtharika I miss your voice and incouge
M'dima sumadziwa kut kuwala kuli pomwepo.
This man, anali muongoli wa dziko lino la malawi.
Koma dziko silinadziwe.
This was a real man to govern Malawi
Ulemelero wa malawi unachoka basi ....Bingu was q blessing and special gift to us malawians koma tinali mu m'dima.May forgive our country and give us someone like him😮
He was best President ever in our loved country Malawi
0
O
0
0
O
We lost such a great and visionary leader in him. May you still continue resting well Pro Bingu Wa Muthalika
I will mourn and celebrate Bingu Wa Mutharika for the rest of my life he was a good and wise president..RIP MY PRESIDENT.
Kuno chomwe amadziwa atolankhani ndikufalitsa zoipa zokhazokha osati zabwino kkkkkkk apapa am glad kuti Bingu anawatsukuluza hvy
And ichi ndichidziwitso chimodzi kuti atolankhaniso nawo ali patsogolo pakubwezeretsa chitukuko cha dziko lino pa mmbuyo.
mutha kudabwa inu kwaona atolankhani omwewo lero akumutamanda Bingu kuti anali mtsogoleri wabwino
I'm one of a Malawian who was inspired by Bingu,
May his soul continue to rest in peace
True leader we miss u
great leader ever n ever
We're still crying for you late Genius Bingu
We had genius
But God love him most
Keep on resting well our hero
God choose the best
We had a true leader. Honest and caring character.
That was the best advice from bingu
A leader with fatherly heart and love. Keep resting easy ngwazi
Ndinadziwa how great he was atamwalira. You the best president we ever had
This dude was genius indeed
The best president ever in Malawi, continue resting in peace Pro Bingu Wa Munthali. It's my prayer that God should give us a wise n strong president
We ll never find president like him 😭😔 abwino sakhalisa I believe when he passed away Pano asala ndi anyapapi wokha wokha bingu wamuthalika we still remember you
Good speech that people with good confidence will follow it forever, he died for body only but spirit for him still alive. Your body rest in peace almighty name of Jesus Christ Amen
🕊📖.............✍
We miss our best president ever In Malawi 🇲🇼
We really miss him now
He was a king
Abingu muwuse muntendele 😭😭😭😭
Awa ndiwo mawu amawi amalawi kaduka basi chomwe timadziwa😁😁👍
We lost such a great Leader
Takutoperani a MCP
Tavelani malangidzo
@@elufedavid3788 ndipo ugalu wakesotu nde winawina nanga zugwirizana bwanji ndi MCP apa? Uchimidzi
Rest well Mr bingu
Vito loti mumayamikira munthu Akachoka
He was Give the right path for development and mwadala tinampereka uyu
I miss this president and we've never had a president like Bingu wa Mutharika and we'll never have a president like Dr Bingu wa Mutharika in Malawi
Amalawi Amapangirana Nsanje Mpaka zaka Zino, Ndimaopa Kupanga Associate Ndi Amalawi Anzanga.
Amalawi Ndinu anthu oipa kwambili
Wiseman
l proud of speeches of this formar president.Rest in peace boss.
wow ine kumva kukoma
Best
Bingu genuine
Marvelous
We will never to forget sir🙏🙏🙏🙏🙏💔
RIP
❤❤❤❤❤❤
On point
Apatu nde zazerudi osati zaleroz
Only the one and the best president in our country anaphuladi dziko pamoto may continue rest in peace 😭😭😭
Munthuyu amaona kut akumutaisa nthawi 😂😂
We loss ...RIP Father Muthalika
Kodi jelouse mupita nayo kit?
❤❤❤❤❤
Inu aBakili News Channel mukuamva malangizowo?
Simuzaiwalika big munadi katundu weni weni.
Zinali Mbubzi za aKAZITAPE.
Inuyo Munali Tate weniweni, Rest in peace
Madala kuyionera patali game
Chimanyasa ulinacho😢
Only time
Lero limenero maziwa kuti anali machine kkkk panopa mavutowa tiyeni tuwaonele limodzi bola osazimangilira kkkk
Anali tate wa nfuko
ndine wa mcp koma pa bingu hmmm zinali nkhani zina mpaka 2009 mutu wanga unapenga bingu ngati anatumidwa ndi ambuye kudzatilamulira moti pazoipa zake zimene anthu amanena ine ndimaziika m'manja mwa mulungu coz satana anakwanitsa gawo lake kutitseka maso ndikumadana ndi utsogoleri wangilo
koma osati zinazi kungoonjezela kuipitsa mbili yake koma sindikukhulupira kudzaonaso tsogoleri ngati ameneyu ngakhale kamuzu sangafike pamzelu zake rest in piece baba
Tulukani Mcp man mutaya nthawi
Zooonadi zokhazokha satana ndiwochenjera koma pomaliza💔💔
Wa dpp iwe hiyaaa
Sunga yelekeze ndi manyi ali lelowa.awa anali wakulu
Awa adali am'dala bambo
Mzimu wake uziusa mumtendere osatha munthu oyipa uyu mafuta atavuta mkumati kagone pamsewu. Aaah kunapita mfiti
Am dying 😂🤣
Chimanyasa ulinacho
I like Donald Trump's stand on CNN, He calls them fake news kkkkk
🤣🤣🤣🤣
Wiseman
Nthito za manja ake ndio nkhani lero Anasiya zonse phazi ndi mulomo Mzimu wake ukuusa ndi mtendere