Dr Bingu Wa Mutharika best advice to malawians; Malangizo a Bingu kupita kwa amalawi.

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 7 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 82

  • @selectorbillbox3505
    @selectorbillbox3505 2 роки тому +10

    ZIMANGOONA KUVUTA BUT THIS MAN USED TO INSPIRE ME A LOT
    MAY YOUR SOUL CONTINUE RESTING IN PEACE
    WISE TALKING

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj 2 місяці тому +5

    Anthu abwino sakhalisa paxiko I remember you Bingu Mtharika I miss your voice and incouge

  • @Slyvester-zs6ww
    @Slyvester-zs6ww 2 місяці тому +5

    M'dima sumadziwa kut kuwala kuli pomwepo.
    This man, anali muongoli wa dziko lino la malawi.
    Koma dziko silinadziwe.

  • @seanmsutu6848
    @seanmsutu6848 2 роки тому +7

    This was a real man to govern Malawi

  • @chisomombeta6446
    @chisomombeta6446 8 місяців тому +3

    Ulemelero wa malawi unachoka basi ....Bingu was q blessing and special gift to us malawians koma tinali mu m'dima.May forgive our country and give us someone like him😮

  • @sakingomane5819
    @sakingomane5819 2 роки тому +18

    He was best President ever in our loved country Malawi

  • @brinokasekani7295
    @brinokasekani7295 2 роки тому +5

    We lost such a great and visionary leader in him. May you still continue resting well Pro Bingu Wa Muthalika

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 Рік тому +2

    I will mourn and celebrate Bingu Wa Mutharika for the rest of my life he was a good and wise president..RIP MY PRESIDENT.

  • @aaronkachipeso3586
    @aaronkachipeso3586 2 роки тому +5

    Kuno chomwe amadziwa atolankhani ndikufalitsa zoipa zokhazokha osati zabwino kkkkkkk apapa am glad kuti Bingu anawatsukuluza hvy
    And ichi ndichidziwitso chimodzi kuti atolankhaniso nawo ali patsogolo pakubwezeretsa chitukuko cha dziko lino pa mmbuyo.
    mutha kudabwa inu kwaona atolankhani omwewo lero akumutamanda Bingu kuti anali mtsogoleri wabwino

  • @tingo3155
    @tingo3155 Рік тому +5

    I'm one of a Malawian who was inspired by Bingu,
    May his soul continue to rest in peace

  • @ririvilla1423
    @ririvilla1423 Рік тому +3

    True leader we miss u

  • @bilali869
    @bilali869 Рік тому +2

    great leader ever n ever

  • @AlexisKantondo
    @AlexisKantondo 8 місяців тому +1

    We're still crying for you late Genius Bingu

  • @dominicmphepo-jk8lk
    @dominicmphepo-jk8lk 8 місяців тому +1

    We had genius
    But God love him most
    Keep on resting well our hero

  • @xanderotc
    @xanderotc 2 роки тому +5

    We had a true leader. Honest and caring character.

  • @imranmposa2788
    @imranmposa2788 2 роки тому +2

    That was the best advice from bingu

  • @goodwellchanunkha1971
    @goodwellchanunkha1971 2 роки тому +3

    A leader with fatherly heart and love. Keep resting easy ngwazi

  • @robertnyasulu1384
    @robertnyasulu1384 2 роки тому +1

    Ndinadziwa how great he was atamwalira. You the best president we ever had

  • @benjaminkampiyon1130
    @benjaminkampiyon1130 2 роки тому +2

    This dude was genius indeed

  • @brinobota6637
    @brinobota6637 Місяць тому

    The best president ever in Malawi, continue resting in peace Pro Bingu Wa Munthali. It's my prayer that God should give us a wise n strong president

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 22 дні тому

    We ll never find president like him 😭😔 abwino sakhalisa I believe when he passed away Pano asala ndi anyapapi wokha wokha bingu wamuthalika we still remember you

  • @williamdaisithom5913
    @williamdaisithom5913 2 роки тому +4

    Good speech that people with good confidence will follow it forever, he died for body only but spirit for him still alive. Your body rest in peace almighty name of Jesus Christ Amen
    🕊📖.............✍

  • @felixsaidi6715
    @felixsaidi6715 2 роки тому +6

    We miss our best president ever In Malawi 🇲🇼

  • @michealmussah261
    @michealmussah261 2 роки тому +2

    We really miss him now

  • @StefanoDavison-sn5rl
    @StefanoDavison-sn5rl 5 днів тому

    He was a king

  • @kassimjummah3018
    @kassimjummah3018 2 роки тому +3

    Abingu muwuse muntendele 😭😭😭😭

  • @osamabinraden9391
    @osamabinraden9391 2 роки тому +3

    Awa ndiwo mawu amawi amalawi kaduka basi chomwe timadziwa😁😁👍

  • @louisbonongwe4864
    @louisbonongwe4864 2 роки тому +2

    We lost such a great Leader

  • @anifoiuene6301
    @anifoiuene6301 2 роки тому +5

    Takutoperani a MCP

    • @elufedavid3788
      @elufedavid3788 2 роки тому +1

      Tavelani malangidzo

    • @aaronkachipeso3586
      @aaronkachipeso3586 2 роки тому

      @@elufedavid3788 ndipo ugalu wakesotu nde winawina nanga zugwirizana bwanji ndi MCP apa? Uchimidzi

  • @glorytchezan5157
    @glorytchezan5157 2 роки тому +2

    Rest well Mr bingu

  • @user-zq1oz9of7s
    @user-zq1oz9of7s Місяць тому

    Vito loti mumayamikira munthu Akachoka
    He was Give the right path for development and mwadala tinampereka uyu

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 Рік тому

    I miss this president and we've never had a president like Bingu wa Mutharika and we'll never have a president like Dr Bingu wa Mutharika in Malawi

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 Рік тому +1

    Amalawi Amapangirana Nsanje Mpaka zaka Zino, Ndimaopa Kupanga Associate Ndi Amalawi Anzanga.
    Amalawi Ndinu anthu oipa kwambili

  • @hendrixkaitano4242
    @hendrixkaitano4242 2 роки тому +1

    Wiseman

  • @RICHARDA.Y.SAKALI
    @RICHARDA.Y.SAKALI 3 місяці тому

    l proud of speeches of this formar president.Rest in peace boss.

  • @hopeskafumbiphiri6011
    @hopeskafumbiphiri6011 Рік тому +1

    wow ine kumva kukoma

  • @RobertEsinat
    @RobertEsinat 12 днів тому

    Best

  • @UZIKASI
    @UZIKASI 25 днів тому

    Bingu genuine

  • @WiseJordan-ds6km
    @WiseJordan-ds6km 2 місяці тому

    Marvelous

  • @user-ux6cw2gq2n
    @user-ux6cw2gq2n 5 місяців тому

    We will never to forget sir🙏🙏🙏🙏🙏💔

  • @levisonmthawanji4232
    @levisonmthawanji4232 2 роки тому +2

    RIP

  • @BlessingsNamilonje
    @BlessingsNamilonje 20 днів тому

    ❤❤❤❤❤❤

  • @sab311
    @sab311 Рік тому

    On point

  • @DawudiIbula
    @DawudiIbula 13 днів тому +1

    Apatu nde zazerudi osati zaleroz

  • @owenmalongo4116
    @owenmalongo4116 Рік тому

    Only the one and the best president in our country anaphuladi dziko pamoto may continue rest in peace 😭😭😭

  • @ibrahimjim281
    @ibrahimjim281 2 роки тому +3

    Munthuyu amaona kut akumutaisa nthawi 😂😂

  • @chrismakhela7133
    @chrismakhela7133 Рік тому

    We loss ...RIP Father Muthalika

  • @FatimaMwanyali
    @FatimaMwanyali 2 місяці тому

    Kodi jelouse mupita nayo kit?
    ❤❤❤❤❤

  • @allanmakwiti5145
    @allanmakwiti5145 2 роки тому +4

    Inu aBakili News Channel mukuamva malangizowo?

  • @decemberjonathan3001
    @decemberjonathan3001 7 днів тому

    Simuzaiwalika big munadi katundu weni weni.

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 2 роки тому +1

    Zinali Mbubzi za aKAZITAPE.

  • @user-ne9qn5nm9d
    @user-ne9qn5nm9d 11 місяців тому

    Inuyo Munali Tate weniweni, Rest in peace

  • @aubreychuma5449
    @aubreychuma5449 2 роки тому +1

    Madala kuyionera patali game

  • @DawudiIbula
    @DawudiIbula 13 днів тому

    Chimanyasa ulinacho😢

  • @GloryKhondiwa
    @GloryKhondiwa 12 днів тому

    Only time

  • @user-le7hd9lm8u
    @user-le7hd9lm8u День тому

    Lero limenero maziwa kuti anali machine kkkk panopa mavutowa tiyeni tuwaonele limodzi bola osazimangilira kkkk

  • @user-ig7dv8rp7r
    @user-ig7dv8rp7r 6 місяців тому +1

    Anali tate wa nfuko

  • @gastahlubi
    @gastahlubi 2 роки тому +7

    ndine wa mcp koma pa bingu hmmm zinali nkhani zina mpaka 2009 mutu wanga unapenga bingu ngati anatumidwa ndi ambuye kudzatilamulira moti pazoipa zake zimene anthu amanena ine ndimaziika m'manja mwa mulungu coz satana anakwanitsa gawo lake kutitseka maso ndikumadana ndi utsogoleri wangilo

    • @gastahlubi
      @gastahlubi 2 роки тому

      koma osati zinazi kungoonjezela kuipitsa mbili yake koma sindikukhulupira kudzaonaso tsogoleri ngati ameneyu ngakhale kamuzu sangafike pamzelu zake rest in piece baba

    • @cadohjabu5565
      @cadohjabu5565 2 роки тому +1

      Tulukani Mcp man mutaya nthawi

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 11 місяців тому

      Zooonadi zokhazokha satana ndiwochenjera koma pomaliza💔💔

  • @innocentmanyera1861
    @innocentmanyera1861 Рік тому

    Wa dpp iwe hiyaaa

  • @longimtimabii1017
    @longimtimabii1017 6 місяців тому +1

    Sunga yelekeze ndi manyi ali lelowa.awa anali wakulu

  • @leviticusbonfancio
    @leviticusbonfancio 9 місяців тому

    Awa adali am'dala bambo

  • @anoldkapolo4493
    @anoldkapolo4493 Рік тому

    Mzimu wake uziusa mumtendere osatha munthu oyipa uyu mafuta atavuta mkumati kagone pamsewu. Aaah kunapita mfiti

  • @peteruko
    @peteruko 2 роки тому

    Am dying 😂🤣

  • @DawudiIbula
    @DawudiIbula 13 днів тому

    Chimanyasa ulinacho

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 Рік тому

    I like Donald Trump's stand on CNN, He calls them fake news kkkkk

  • @enockthomasloyidi4914
    @enockthomasloyidi4914 2 роки тому

    🤣🤣🤣🤣

  • @imaanasibu7267
    @imaanasibu7267 2 роки тому +3

    Wiseman

    • @amoschilimba4377
      @amoschilimba4377 Рік тому

      Nthito za manja ake ndio nkhani lero Anasiya zonse phazi ndi mulomo Mzimu wake ukuusa ndi mtendere