Ndinaganidza izi tsiku limene Achilima anatisiya kuti Marry ngati amamukonda mwamuna wake kuchokera pansi pa mtima akuyenera kuimira u President now am so happy to hear that Osatopa osatopa Mary Ambuye akutsogolerani mu zonse chifukwa chipanichi mukapatsa munthu wina ndithu kutha kukhala komweko chikadzawina azatsintha zina Ndiye Ife sitikufuna kutichipani Cha UTM chinthe chonse Mah musafooke maso patsogolo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
It's not good idea at all because we all know that there is vise president of UTM, that person he is the one who suppose to be incharge despite everything.
Maganizo anga ndamenewo since day one SKC atatisiya, mmene nduonera mu UTM atsogoleri omwe angapitise UTM patsogolo ndi Mayi Chilima kapena Che Kaliati apo ayi atenga wakunja ngati achina Dalitso Mpinganjira or Kabambe ndekuti chikhara cha mphamvu nkuzawinaso
Maganizo anga ndikuona kuti asankhe wina osati Mary ndare zotani zimenedzi munthu akayambisa chipani basi akamwarila or retirement chizikhara cha family aaaa amalawi this is another generation let's change gyz
Wachiwili wa malemu a Chilima ku chipani cha UTM amene ali Manganya anatuluka kalekale mu chipani cha UTM analowa malawi congress party. ndiye nkhani ya maudindo a ku UTM Manganya zisamukhudze ai chifukwa iyeyu ndi mpeni wa nsengwa wakuthwa konse konse. Madam Mary Chilima go ahead. inuyo a UTM musanvele maganizo a wanthu amene ali kunja kwa chipani chanu
Inu Inu VC wake uti Manganya asakupusitseni si wa UTM uyu anakakhala ndi wa UTM sanakora kukhala Vice chifukwa Chilima wafa imfa yowawa inu uyu ndi MCP mkuthekanso plan yopha Chilima inachokera kwa Maiko usi cholinga akhalepo Iyeyo musamale nae maiko Usi
Noooo,leave her alone and let her grieve her husband bwino bwino. N I don't think politics is her thing. Akweni bwanji? That woman is a firecracker,she can make it.
Kodi Mayiwa atawina koma akuziwa zoti president sayenda opanda mamuna nde mufuna kunena kuti akwatira popano palibe chikondi akaimira alire bwino bwino mamuna wake apo bii anali kale ndi chibwedzi cha nseli
Even Patricia must not contest..Civil service suffered too much when Madam Joyce Banda was rolling Malawi .she hated civil servants and she grossly stole Malawi funds in her cash gate. So Malawi don't need women to be rulers OK notre women them are become so proud and pompous.. mpaka ife ma civil servants tinawapangirq mademo. Nkuwaika mbokosi ngqti amwalira.kkkk
Anthu muli ziwanda ndithu zau adakalira mamunake nde akhale busy ndi za dziko mufuna mumupheso mary.?ngati naye ali maganizo asalowe ndale ndi ufiti iya mufina muthere ndalama zake asauke basi anatitu iye siwandale iye amakonda kuimba mulekeni mwana wa eni
It's not a good idea to make Mai Chilima leader of UTM. There's time. Meanwhile let her follow her career to the top.
Ndinaganidza izi tsiku limene Achilima anatisiya kuti Marry ngati amamukonda mwamuna wake kuchokera pansi pa mtima akuyenera kuimira u President now am so happy to hear that Osatopa osatopa Mary Ambuye akutsogolerani mu zonse chifukwa chipanichi mukapatsa munthu wina ndithu kutha kukhala komweko chikadzawina azatsintha zina Ndiye Ife sitikufuna kutichipani Cha UTM chinthe chonse Mah musafooke maso patsogolo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
🙏Zoona zake ife tikufuna chipani chisathe compaign anapanga kale chilima timangiodkira tsku
Mai Mary mukane. Anthu asakuikeni Mau mkamwa
ndipo bola asamale ana awo asaluzenso Mai wawo ayii
This woman is gonna rise
Malangizo aulele,, mai chilima osayelekeza kulowa ndale,,ndale zimapha pitilizani zina zomwe mumapanga and live longer,,anthu akukukopani lerowa mawa atayiwala zonse azakutembunukilani kuti simunachitepo ndale muzaononga dzina lanu ndikuchosa ulemu onse wa inu komanso malemu,, osayesa.
Munthu analowa kale ndale nde mukuti asayerekeze kulowa bwanjiso.😅 Komaso mukati ndale zimapha kodi ose atati aziopa chonchco zingakhale bwa. Aliyese azafa even amene amapha anzawo. Ndipo zimenezo ndizomwe mwina atha kulimba nazo mtima kuti ngati mamuna wake anafa iye aoperanji
It's not good idea at all because we all know that there is vise president of UTM, that person he is the one who suppose to be incharge despite everything.
Koma anthu mumakonda kusokoneza zinthu,Marry Chilima watani? Tamusiyeni munthu musamuike maganizo opotoka, musaiwaleso Chilima munamupopaso ndinu nomwe kumuuza kuti ayambitse chipani chake
Mawu
Mary has got a capacity to govern but only if she is willing. Azibambo ena akupangaso dyera heavy atha kuphetsa chipanichitu oooooh....
Musiyeni marry alire mamuna wake
P
P
Mayi Chilima I believe she's not a politician,Kalindo bwanji?
Tiyeni uko ndi Kalindo
We need chilima legacy
And Mai Mary chilima
She was closest to skc she is only one can take utm
Alowepo Akweni
Kufuna kumuphetsanso eti,mulibe chisoni guys ee
Kufa tose tizafa we need her now to take this party
A kalindo ndi amene angatsogolele bwino UTM,, Ali ndi masomphenya ,munthu okonda dziko ndi anthu ake,,
Kalindo is illiterate
Kalindo anasiya ndale
Kalindo azitani ku UTM mumasowa zoyankhula eti??
Fredokiss president wa UTM ndipo SKC Forever in Our Hearts ❤
Live from SA cape town muzen kaliyati Mary akurila plz
Kuwafusa kaye ali ready kutero,bcz kupanga run chipani ndi ndalama
Maganizo anga ndamenewo since day one SKC atatisiya, mmene nduonera mu UTM atsogoleri omwe angapitise UTM patsogolo ndi Mayi Chilima kapena Che Kaliati apo ayi atenga wakunja ngati achina Dalitso Mpinganjira or Kabambe ndekuti chikhara cha mphamvu nkuzawinaso
Kaliat ukhale iweyo bwanji osogolera UTM mary akadali kulira mwamuna wake please napapata
Maganizo anga ndikuona kuti asankhe wina osati Mary ndare zotani zimenedzi munthu akayambisa chipani basi akamwarila or retirement chizikhara cha family aaaa amalawi this is another generation let's change gyz
Marry saphedwa mu dzina la Yesu ndipo satana achita manyanzi No matter kuti ndi banja koma tikupanga izi chifukwa mwamuna wake wamfa imfa yowawa zinakhala ali moyo Saulosi Chilima zinali zosatheka kusiilira mkazi wake mpandowu anthu inu kumaganidza pena MCP ikufuna chipanichi chithe kungoikapo munthu chisawawa akachifulitsa ku MCP aime Marry kuti chakwera achite manyanzi kuti ndinachitanji pompha Chilima uja?
Inendikuona ngati mai chilima apatsidwe mpata bwino bwino olira amunawo Chifukwa imfa Yangozi akulu akulu ndi imfa imene imakhala yomvuta kuimvetsa zimasiyana ndi munthu oti anadwala pena anthu mumavomereza kuti munthu anamvutika ndithu Chomwe chingachitike mwina mai Chilimawo nfikungowachita support anthu omwe angayendetse Chipanicho pakadalipano kutsogolo Kuno ngati atafuna athakudzaima ngati ndalezo zilimwaiwo masiku sachedwa
ndiponso chifukwa chani iwonso ndiye kuti avomeleza aaa sikaganizidwe kwabwino ayi mix ndiye kuti akuyenera akwatiwenso mmm akalora samawakonda amuna awo ndithu mmmm maliro angozi ayi kuvuta kuiwala 😢😢
We need Mai Mary Chilima must take over
This a great idea
Wachiwili wa malemu a Chilima ku chipani cha UTM amene ali Manganya anatuluka kalekale mu chipani cha UTM analowa malawi congress party. ndiye nkhani ya maudindo a ku UTM Manganya zisamukhudze ai chifukwa iyeyu ndi mpeni wa nsengwa wakuthwa konse konse. Madam Mary Chilima go ahead. inuyo a UTM musanvele maganizo a wanthu amene ali kunja kwa chipani chanu
Nde Mary president adzawina chabwino ndikhare Burundi pa zandale poti sindipanga zandale
Osaikapo Uncle ake a Chilima yo bwanji kuti zimveke bwino
Bwanji osayika mayi kaliyati
Mmmmh musiyeni Mary pls,sakhani ena
Zoona mary aimepo ena achigulitsapo Chipani pliz osagulitsa
Please osapanga zinthu mwachipwera mtima Mary chilima sangakwanitse komaso chipani chotere chikala ngati chabanja chonde ganizani modeka
Amai chonde zisakuchedwetseni izi tapangani zosamala ana anu osati iziii mama chonde ndizopanda phindu iziii
Bola Mayi Kaliat.
😢 😢😢 guy's give madam chilima chance she can make it dont choose manganya his Judah's
😢😢😢😢😢😢😢😢😢 ndalira size pangani choncho guy's sankhani mai chilima osati manganya please
It's possible to do that ,is a right person to fill the position let her to be....
Mmmmm apapa nde ayitu koma mukwafunila za bwino mayi Chilima wo? Ganizani bwino pamenepo
Yomweyo atenge chipani basi
Zoputsa zimenezo
Abale a chilima ngati angavomere ayime basi mery,koma asadzipangile mwa yekha popanda akuchimuna coz pakhoza mwina kudzabwera udani Ali wapangilanji zimenezi
Afuna amalize chuma chimene adasiya chilima timming ya azibambo adyera.
Nyimbo yake ikhale yomwe ija ya Joseph Nkasa amati mng'ono wanga
UTM give yourself enough time to work out this gigsaw puzzle otherwise enafe mutipangitsa kuti chala changa chamukomba phala chizakhale pa holiday !
Ndiitaneni mama tidzapange surpot pamosonkhano tidzasangalatse anthu mmisonkhano yanu pliz
Let's people choose their leader freely
Ndiokwanila kuima ndipo azawina
angozosiya zimenezo mamuna wake uja anali katundu olemera, mapeto ake Mary amuphanso and poti ndiwamkazi nde azamupezerera heavy
Pakabwera wina azachigulisa chipani
Ichi so mama
Mary can't allow her husband legacy to be sold so she is worthy
Inu Inu VC wake uti Manganya asakupusitseni si wa UTM uyu anakakhala ndi wa UTM sanakora kukhala Vice chifukwa Chilima wafa imfa yowawa inu uyu ndi MCP mkuthekanso plan yopha Chilima inachokera kwa Maiko usi cholinga akhalepo Iyeyo musamale nae maiko Usi
Mom Patricia kaliyati can do that
Maganizo anga ndimaona ku UTM kulibe munthu yemwe Ali ndichuma chomasuka ngati momwe analiri chilima ambili manja awo ndiouma paichi chipani sichinga ime Sono ngati Pali maganizo amarry chilima kuti asogolere tiyeni tipenphere kuti akhare iwoo pachifukwa ndipo UTM sizatha ngati zitatelo koma mukasankha mosaganiza UTM yantha basi chipanitu ndi dalama ndiye muone bwino anatisokoneza pamene paja ine ngati sapota wa UTM ndatelo
Excellent mwalankhula bwino komaso moveka kwabasi. Ine ndine wa DPP koma fundo yanuyi ndagwilizana nayo. Uku nde kuphunzisana muchowonadi. Chipanichi akachitengela mosalongosoka chatha. Chifukwa chaka adatiphela chilima cholinga chake ndikupha chipanichiso.
Amen amen Dear
Noooo,leave her alone and let her grieve her husband bwino bwino. N I don't think politics is her thing. Akweni bwanji? That woman is a firecracker,she can make it.
Kodi Mayiwa atawina koma akuziwa zoti president sayenda opanda mamuna nde mufuna kunena kuti akwatira popano palibe chikondi akaimira alire bwino bwino mamuna wake apo bii anali kale ndi chibwedzi cha nseli
Take note that UTM is not a family party like Dpp, Udf and Aford
Who are you yourself talking this nonsense
@@Eric-gb9ms I am a proud Malawian citizen exercising my right to share my views on the political landscape of my country, and you?.
Ulendodi wa chipan ndumenewu,kuganiza kwabwanji uku.?
Koma vice wake akhale Denice thandwe mufana wa nzeru ku mzuzu
ukatswiri uli pati pamenepa🤧🤧🤧
Sangakwanise
Mukapanda kuzatenga bwino utm itha
Never and never Mai Mary will carry her husband legacy
Momwemo marry chilima uyimile kumene afitiwa awone manyi
Izi ndiye za ziii malawi mwayamba kuitenga ngati dziko lotseweletsa
Kuima kwa Madam Chilima ndifundo yabwino, pali anthu ena ali ndi ma plan ogulitsa Chipani kwa Ng'ona za mabango!
Izizi ndi zomwe zikufunika Mary atenge mpando bas....❤
It's not good idea to be honest
Musiyeni zimai alire maliro amuna ake,anthu mulibe chisoni mukufuna amupheso? izitu sizamwanatu
Shaa!!
Kkkkkkkkk Koma mau a Mulungu ndiowona sure..Dziko linachita khungu anthu lelo sakudziwa chomwe akupanga
❤❤❤❤😊
Kwesi Msusa ndiye okuti atenge chipani cha Nzake Saulosi.
Yakhwesi ndaivotera,maiyu amusiye kaye
❤❤❤
It's too early give her time to mourn her husband
Musatibalalitse Mary yo ndiokwanira
Mary alire mamuna wake bwanji sankhani wina
Koma koposa akhale wina mayi chilima ayi kuganiza kwanga chifukwa panopa Ali ndimaganizo ambili
❤❤
Terrible move.UTM constitution says what?
Even Patricia must not contest..Civil service suffered too much when Madam Joyce Banda was rolling Malawi .she hated civil servants and she grossly stole Malawi funds in her cash gate. So Malawi don't need women to be rulers OK notre women them are become so proud and pompous.. mpaka ife ma civil servants tinawapangirq mademo. Nkuwaika mbokosi ngqti amwalira.kkkk
Ruling. Noy roling
Exactly. As a female I agree
Komatu ofunika amaiwa asamale.
Za family Kodi?
Iwe zibambo wandemvu zako ukuti chipani Cha banja ndekuyakhula kwabwanji kumeneko tazikhalani ndi zeru poyakhula ngati zibambo siyeni mery ayime
Aaaaaaa brother ndikuyankhani ponkhapo. Kumankhala ndikuganiza komaso muliganizile banjali. Palibe cha zelu mayi chilima kutenga mpando wa amuna awo. Mkaziyu adakali pa ululu kulila kulilila amunache. Ife athu akwathu ndikungosonkhezela. Ngati akwanisa kumupha chilima uja awawa nde chizimu. Asiyileni chuma chomwe awasiyila amuna awochi kuti chisasokonekeleyi. Samalilani moyo wa mayiwa.
Mai Chilima musiyeni alire maliro amuna so,enanu kuthamanila kulakhula zosaveka,ngati Ali ndichuma maiwa asiyeni athandize ana ao osati muwasokonekeze mdzina loti aimilre muzidzawadyera bwino,sibwino siyeni alire Kaye maliro.
Zipani za mabanja kkkkkkk koma Ku Malawi anaza tiye nazoni
😂😂😂😂 komatu ma guys mpaka UTM mukufuna apatse WINIKO
Za drama eti
Marry chikuni hi
Marry chilima hy
Chipani cha utm chatha basi😂😂😂😂
Eeee Koma A Malawi Ambuye anakonza, zimenezi zimveke moti bwanji
Eti
Mary tikufuna azawine 2025 azatifufuzile malilo a chilima
Zama banja izi asiyeni.
Bola kaliati osati marry Mmmm
Mery alibwino Kwa omwe timakonda chipanichi,komano atati wawina zizamupanga force kukwatila mwina asakufuna pomwe akulilabe mamuna wake coz sitikudziwa kuti inye mwini anayika nthawi yayitalibwanji kuti adzakhale pabanja.
Anthu muli ziwanda ndithu zau adakalira mamunake nde akhale busy ndi za dziko mufuna mumupheso mary.?ngati naye ali maganizo asalowe ndale ndi ufiti iya mufina muthere ndalama zake asauke basi anatitu iye siwandale iye amakonda kuimba mulekeni mwana wa eni
komaso mayi chilima ngati akuvomela zompusa ngati zimenezizi avekedwa dzina oyipa kwambili. Palibe chosangalasatu apa. Asakopeke ndi zithu zompusa ngati zimenezozo. Apitilize kulilila amunawo. Koma ngati akufuna kuyaluka apange nawo phada ameneyi.
mmmm sakuyima msaname
Mary akudwala
Eeee 😳
Kkkk Kom ziona izi
Vice azakhale Denice mahata
Radio yanji iyi
mufuna akwatiwexo pompano
Akungofunapo ndalama abale anga mukamatsatira anthu amenewa muchedwa nazo.. UTM yapita ndi mwini wake basi.
Hmmm inu musavutike simunalowe mmaganizo a anthu mukuchedwa
Pambuyo panu madam
Kmano mphavu zoimila chipani azitenga kut mpamene mamuna sanathe mwezi ali m'manda kaya poti wakonda
Mwinanso ndi amene amkamunyenfelera Chilima kuti tiyeni tipange gwili zako asokogore awa Inu mudzabwere pambuyo nchonsecho akudziwa chimene akuchita and Chilima chifukwa cha kudzichepetsa ndinso ulemu ndinso kukhulupira anavomera osadziwa kuti Maiko usi ndi nthera kuwiri akapita uku akukqmba zina amatenga za uku kumamuudza Chakwera Lero amusogodza Chilima iiiiih ine mtima wanga udakandipweteka mpaka Pano moti usiku ndimangotutumuka
Mufuna Ana ankhaleno onkha heti🙄
mposo
Yoooohh
Haybo she still crying his
Husband she can't be leader that is people talking lie things