Mary Chilima akuimira President wa UTM kulowa malo mwa Malemu Amunanu awo

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 8 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 148

  • @Royhauya-uw2kr
    @Royhauya-uw2kr 16 днів тому +10

    It's not a good idea to make Mai Chilima leader of UTM. There's time. Meanwhile let her follow her career to the top.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 16 днів тому +15

    Ndinaganidza izi tsiku limene Achilima anatisiya kuti Marry ngati amamukonda mwamuna wake kuchokera pansi pa mtima akuyenera kuimira u President now am so happy to hear that Osatopa osatopa Mary Ambuye akutsogolerani mu zonse chifukwa chipanichi mukapatsa munthu wina ndithu kutha kukhala komweko chikadzawina azatsintha zina Ndiye Ife sitikufuna kutichipani Cha UTM chinthe chonse Mah musafooke maso patsogolo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o 15 днів тому +1

      🙏Zoona zake ife tikufuna chipani chisathe compaign anapanga kale chilima timangiodkira tsku

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 16 днів тому +7

    Mai Mary mukane. Anthu asakuikeni Mau mkamwa

    • @AminahMussah
      @AminahMussah 16 днів тому

      ndipo bola asamale ana awo asaluzenso Mai wawo ayii

  • @SamJalie
    @SamJalie 16 днів тому +6

    This woman is gonna rise

  • @Namphuno
    @Namphuno 14 днів тому +3

    Malangizo aulele,, mai chilima osayelekeza kulowa ndale,,ndale zimapha pitilizani zina zomwe mumapanga and live longer,,anthu akukukopani lerowa mawa atayiwala zonse azakutembunukilani kuti simunachitepo ndale muzaononga dzina lanu ndikuchosa ulemu onse wa inu komanso malemu,, osayesa.

    • @paulinekayuni1621
      @paulinekayuni1621 13 днів тому

      Munthu analowa kale ndale nde mukuti asayerekeze kulowa bwanjiso.😅 Komaso mukati ndale zimapha kodi ose atati aziopa chonchco zingakhale bwa. Aliyese azafa even amene amapha anzawo. Ndipo zimenezo ndizomwe mwina atha kulimba nazo mtima kuti ngati mamuna wake anafa iye aoperanji

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z 15 днів тому +3

    It's not good idea at all because we all know that there is vise president of UTM, that person he is the one who suppose to be incharge despite everything.

  • @ShabaniKuswere
    @ShabaniKuswere 16 днів тому +9

    Koma anthu mumakonda kusokoneza zinthu,Marry Chilima watani? Tamusiyeni munthu musamuike maganizo opotoka, musaiwaleso Chilima munamupopaso ndinu nomwe kumuuza kuti ayambitse chipani chake

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 16 днів тому +4

    Mary has got a capacity to govern but only if she is willing. Azibambo ena akupangaso dyera heavy atha kuphetsa chipanichitu oooooh....

  • @DrolieDongowa
    @DrolieDongowa 16 днів тому +9

    Musiyeni marry alire mamuna wake

  • @mayamikothomson
    @mayamikothomson 16 днів тому +6

    Mayi Chilima I believe she's not a politician,Kalindo bwanji?

    • @BillyMhone-jp3kn
      @BillyMhone-jp3kn 15 днів тому

      Tiyeni uko ndi Kalindo
      We need chilima legacy
      And Mai Mary chilima
      She was closest to skc she is only one can take utm

  • @nathannbanda3345
    @nathannbanda3345 16 днів тому +7

    Alowepo Akweni

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu 16 днів тому +6

    Kufuna kumuphetsanso eti,mulibe chisoni guys ee

    • @BillyMhone-jp3kn
      @BillyMhone-jp3kn 15 днів тому

      Kufa tose tizafa we need her now to take this party

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 16 днів тому +5

    A kalindo ndi amene angatsogolele bwino UTM,, Ali ndi masomphenya ,munthu okonda dziko ndi anthu ake,,

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 15 днів тому +1

    Fredokiss president wa UTM ndipo SKC Forever in Our Hearts ❤

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 16 днів тому +2

    Live from SA cape town muzen kaliyati Mary akurila plz

  • @MathewsNyate-y9g
    @MathewsNyate-y9g 16 днів тому +3

    Kuwafusa kaye ali ready kutero,bcz kupanga run chipani ndi ndalama

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 16 днів тому +1

    Maganizo anga ndamenewo since day one SKC atatisiya, mmene nduonera mu UTM atsogoleri omwe angapitise UTM patsogolo ndi Mayi Chilima kapena Che Kaliati apo ayi atenga wakunja ngati achina Dalitso Mpinganjira or Kabambe ndekuti chikhara cha mphamvu nkuzawinaso

  • @leahkasiwa5033
    @leahkasiwa5033 15 днів тому +1

    Kaliat ukhale iweyo bwanji osogolera UTM mary akadali kulira mwamuna wake please napapata

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 16 днів тому +1

    Maganizo anga ndikuona kuti asankhe wina osati Mary ndare zotani zimenedzi munthu akayambisa chipani basi akamwarila or retirement chizikhara cha family aaaa amalawi this is another generation let's change gyz

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 16 днів тому +2

    Marry saphedwa mu dzina la Yesu ndipo satana achita manyanzi No matter kuti ndi banja koma tikupanga izi chifukwa mwamuna wake wamfa imfa yowawa zinakhala ali moyo Saulosi Chilima zinali zosatheka kusiilira mkazi wake mpandowu anthu inu kumaganidza pena MCP ikufuna chipanichi chithe kungoikapo munthu chisawawa akachifulitsa ku MCP aime Marry kuti chakwera achite manyanzi kuti ndinachitanji pompha Chilima uja?

  • @josephinemisomali6840
    @josephinemisomali6840 16 днів тому +1

    Inendikuona ngati mai chilima apatsidwe mpata bwino bwino olira amunawo Chifukwa imfa Yangozi akulu akulu ndi imfa imene imakhala yomvuta kuimvetsa zimasiyana ndi munthu oti anadwala pena anthu mumavomereza kuti munthu anamvutika ndithu Chomwe chingachitike mwina mai Chilimawo nfikungowachita support anthu omwe angayendetse Chipanicho pakadalipano kutsogolo Kuno ngati atafuna athakudzaima ngati ndalezo zilimwaiwo masiku sachedwa

    • @priscaleofranknakari3117
      @priscaleofranknakari3117 15 днів тому

      ndiponso chifukwa chani iwonso ndiye kuti avomeleza aaa sikaganizidwe kwabwino ayi mix ndiye kuti akuyenera akwatiwenso mmm akalora samawakonda amuna awo ndithu mmmm maliro angozi ayi kuvuta kuiwala 😢😢

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn 15 днів тому

    We need Mai Mary Chilima must take over

  • @mosesnyirenda5010
    @mosesnyirenda5010 10 днів тому

    This a great idea

  • @user-yx6oo2pc3r
    @user-yx6oo2pc3r 15 днів тому

    Wachiwili wa malemu a Chilima ku chipani cha UTM amene ali Manganya anatuluka kalekale mu chipani cha UTM analowa malawi congress party. ndiye nkhani ya maudindo a ku UTM Manganya zisamukhudze ai chifukwa iyeyu ndi mpeni wa nsengwa wakuthwa konse konse. Madam Mary Chilima go ahead. inuyo a UTM musanvele maganizo a wanthu amene ali kunja kwa chipani chanu

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 14 днів тому

    Nde Mary president adzawina chabwino ndikhare Burundi pa zandale poti sindipanga zandale

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga 11 днів тому

    Osaikapo Uncle ake a Chilima yo bwanji kuti zimveke bwino

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 15 днів тому +1

    Bwanji osayika mayi kaliyati

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 13 днів тому

    Mmmmh musiyeni Mary pls,sakhani ena

  • @user-es4jt6ds8m
    @user-es4jt6ds8m 16 днів тому +1

    Zoona mary aimepo ena achigulitsapo Chipani pliz osagulitsa

  • @user-fs5gr8iv5s
    @user-fs5gr8iv5s 16 днів тому

    Please osapanga zinthu mwachipwera mtima Mary chilima sangakwanitse komaso chipani chotere chikala ngati chabanja chonde ganizani modeka

  • @user-xo8ms5wh2s
    @user-xo8ms5wh2s 13 днів тому

    Amai chonde zisakuchedwetseni izi tapangani zosamala ana anu osati iziii mama chonde ndizopanda phindu iziii

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu 15 днів тому +1

    Bola Mayi Kaliat.

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 16 днів тому

    😢 😢😢 guy's give madam chilima chance she can make it dont choose manganya his Judah's

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 16 днів тому

    😢😢😢😢😢😢😢😢😢 ndalira size pangani choncho guy's sankhani mai chilima osati manganya please

  • @LimbikaniKadzongwe
    @LimbikaniKadzongwe 15 днів тому

    It's possible to do that ,is a right person to fill the position let her to be....

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 16 днів тому

    Mmmmm apapa nde ayitu koma mukwafunila za bwino mayi Chilima wo? Ganizani bwino pamenepo

  • @tracybennie7783
    @tracybennie7783 16 днів тому +3

    Yomweyo atenge chipani basi

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu 15 днів тому

    Abale a chilima ngati angavomere ayime basi mery,koma asadzipangile mwa yekha popanda akuchimuna coz pakhoza mwina kudzabwera udani Ali wapangilanji zimenezi

  • @BennieMdezA
    @BennieMdezA 14 днів тому

    Afuna amalize chuma chimene adasiya chilima timming ya azibambo adyera.

  • @blessbless6929
    @blessbless6929 14 днів тому

    Nyimbo yake ikhale yomwe ija ya Joseph Nkasa amati mng'ono wanga

  • @StainlyMunthali
    @StainlyMunthali 15 днів тому

    UTM give yourself enough time to work out this gigsaw puzzle otherwise enafe mutipangitsa kuti chala changa chamukomba phala chizakhale pa holiday !

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin 15 днів тому

    Ndiitaneni mama tidzapange surpot pamosonkhano tidzasangalatse anthu mmisonkhano yanu pliz

  • @HellenNyambose
    @HellenNyambose 16 днів тому

    Let's people choose their leader freely

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 16 днів тому +1

    Ndiokwanila kuima ndipo azawina

  • @LottiAffati
    @LottiAffati 16 днів тому

    angozosiya zimenezo mamuna wake uja anali katundu olemera, mapeto ake Mary amuphanso and poti ndiwamkazi nde azamupezerera heavy

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn 15 днів тому

    Pakabwera wina azachigulisa chipani
    Ichi so mama
    Mary can't allow her husband legacy to be sold so she is worthy

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 15 днів тому

    Inu Inu VC wake uti Manganya asakupusitseni si wa UTM uyu anakakhala ndi wa UTM sanakora kukhala Vice chifukwa Chilima wafa imfa yowawa inu uyu ndi MCP mkuthekanso plan yopha Chilima inachokera kwa Maiko usi cholinga akhalepo Iyeyo musamale nae maiko Usi

  • @MalawiRiddles
    @MalawiRiddles 16 днів тому

    Mom Patricia kaliyati can do that

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci 16 днів тому +2

    Maganizo anga ndimaona ku UTM kulibe munthu yemwe Ali ndichuma chomasuka ngati momwe analiri chilima ambili manja awo ndiouma paichi chipani sichinga ime Sono ngati Pali maganizo amarry chilima kuti asogolere tiyeni tipenphere kuti akhare iwoo pachifukwa ndipo UTM sizatha ngati zitatelo koma mukasankha mosaganiza UTM yantha basi chipanitu ndi dalama ndiye muone bwino anatisokoneza pamene paja ine ngati sapota wa UTM ndatelo

    • @HaroonMaundala-lg5lg
      @HaroonMaundala-lg5lg 16 днів тому +1

      Excellent mwalankhula bwino komaso moveka kwabasi. Ine ndine wa DPP koma fundo yanuyi ndagwilizana nayo. Uku nde kuphunzisana muchowonadi. Chipanichi akachitengela mosalongosoka chatha. Chifukwa chaka adatiphela chilima cholinga chake ndikupha chipanichiso.

    • @doreenkaliati3166
      @doreenkaliati3166 16 днів тому

      Amen amen Dear

  • @TheLeezo
    @TheLeezo 16 днів тому

    Noooo,leave her alone and let her grieve her husband bwino bwino. N I don't think politics is her thing. Akweni bwanji? That woman is a firecracker,she can make it.

  • @Shadreckdingiswayo
    @Shadreckdingiswayo 15 днів тому

    Kodi Mayiwa atawina koma akuziwa zoti president sayenda opanda mamuna nde mufuna kunena kuti akwatira popano palibe chikondi akaimira alire bwino bwino mamuna wake apo bii anali kale ndi chibwedzi cha nseli

  • @christophermtonga8535
    @christophermtonga8535 16 днів тому +1

    Take note that UTM is not a family party like Dpp, Udf and Aford

    • @Eric-gb9ms
      @Eric-gb9ms 16 днів тому

      Who are you yourself talking this nonsense

    • @christophermtonga8535
      @christophermtonga8535 16 днів тому +1

      @@Eric-gb9ms I am a proud Malawian citizen exercising my right to share my views on the political landscape of my country, and you?.

  • @PriscahChikaonda
    @PriscahChikaonda 13 днів тому

    Ulendodi wa chipan ndumenewu,kuganiza kwabwanji uku.?

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 16 днів тому

    Koma vice wake akhale Denice thandwe mufana wa nzeru ku mzuzu

  • @greymitomoni4047
    @greymitomoni4047 12 днів тому

    ukatswiri uli pati pamenepa🤧🤧🤧

  • @NDIZOTHEKABANDA
    @NDIZOTHEKABANDA 16 днів тому +3

    Sangakwanise

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 16 днів тому +3

    Mukapanda kuzatenga bwino utm itha

    • @BillyMhone-jp3kn
      @BillyMhone-jp3kn 15 днів тому

      Never and never Mai Mary will carry her husband legacy

  • @user-pl2lj6mh1z
    @user-pl2lj6mh1z 16 днів тому

    Momwemo marry chilima uyimile kumene afitiwa awone manyi

  • @MaryMlomba
    @MaryMlomba 16 днів тому

    Izi ndiye za ziii malawi mwayamba kuitenga ngati dziko lotseweletsa

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 16 днів тому

    Kuima kwa Madam Chilima ndifundo yabwino, pali anthu ena ali ndi ma plan ogulitsa Chipani kwa Ng'ona za mabango!

  • @SeanMatora
    @SeanMatora 16 днів тому +1

    Izizi ndi zomwe zikufunika Mary atenge mpando bas....❤

  • @EmmyYafete
    @EmmyYafete 16 днів тому

    Musiyeni zimai alire maliro amuna ake,anthu mulibe chisoni mukufuna amupheso? izitu sizamwanatu

  • @KondwanKafuratira
    @KondwanKafuratira 13 днів тому

    Shaa!!

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 16 днів тому

    Kkkkkkkkk Koma mau a Mulungu ndiowona sure..Dziko linachita khungu anthu lelo sakudziwa chomwe akupanga

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 16 днів тому

    ❤❤❤❤😊

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g 16 днів тому +1

    Kwesi Msusa ndiye okuti atenge chipani cha Nzake Saulosi.

  • @andrewchiusiwa3487
    @andrewchiusiwa3487 16 днів тому

    ❤❤❤

  • @user-jl6tr9wv3h
    @user-jl6tr9wv3h 15 днів тому

    It's too early give her time to mourn her husband

  • @joanaKachiwaya
    @joanaKachiwaya 16 днів тому +1

    Musatibalalitse Mary yo ndiokwanira

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 16 днів тому

    Mary alire mamuna wake bwanji sankhani wina

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo 16 днів тому

    Koma koposa akhale wina mayi chilima ayi kuganiza kwanga chifukwa panopa Ali ndimaganizo ambili

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v 16 днів тому

    ❤❤

  • @janssenmoyo7588
    @janssenmoyo7588 16 днів тому

    Terrible move.UTM constitution says what?

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe 15 днів тому +1

    Even Patricia must not contest..Civil service suffered too much when Madam Joyce Banda was rolling Malawi .she hated civil servants and she grossly stole Malawi funds in her cash gate. So Malawi don't need women to be rulers OK notre women them are become so proud and pompous.. mpaka ife ma civil servants tinawapangirq mademo. Nkuwaika mbokosi ngqti amwalira.kkkk

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i 16 днів тому

    Komatu ofunika amaiwa asamale.

  • @user-pn6py6rf6k
    @user-pn6py6rf6k 7 днів тому

    Za family Kodi?

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v 16 днів тому +2

    Iwe zibambo wandemvu zako ukuti chipani Cha banja ndekuyakhula kwabwanji kumeneko tazikhalani ndi zeru poyakhula ngati zibambo siyeni mery ayime

    • @HaroonMaundala-lg5lg
      @HaroonMaundala-lg5lg 16 днів тому

      Aaaaaaa brother ndikuyankhani ponkhapo. Kumankhala ndikuganiza komaso muliganizile banjali. Palibe cha zelu mayi chilima kutenga mpando wa amuna awo. Mkaziyu adakali pa ululu kulila kulilila amunache. Ife athu akwathu ndikungosonkhezela. Ngati akwanisa kumupha chilima uja awawa nde chizimu. Asiyileni chuma chomwe awasiyila amuna awochi kuti chisasokonekeleyi. Samalilani moyo wa mayiwa.

    • @CyprianoSandalamu
      @CyprianoSandalamu 16 днів тому

      Mai Chilima musiyeni alire maliro amuna so,enanu kuthamanila kulakhula zosaveka,ngati Ali ndichuma maiwa asiyeni athandize ana ao osati muwasokonekeze mdzina loti aimilre muzidzawadyera bwino,sibwino siyeni alire Kaye maliro.

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 16 днів тому +1

    Zipani za mabanja kkkkkkk koma Ku Malawi anaza tiye nazoni

  • @stalickkafera3454
    @stalickkafera3454 16 днів тому

    😂😂😂😂 komatu ma guys mpaka UTM mukufuna apatse WINIKO
    Za drama eti

  • @VincentNyabanga-dw9uj
    @VincentNyabanga-dw9uj 3 дні тому

    Marry chikuni hi

  • @MustapherLino
    @MustapherLino 15 днів тому

    Chipani cha utm chatha basi😂😂😂😂

  • @patriciap.bandah3385
    @patriciap.bandah3385 16 днів тому

    Eeee Koma A Malawi Ambuye anakonza, zimenezi zimveke moti bwanji

  • @giftedmshan6779
    @giftedmshan6779 16 днів тому

    Mary tikufuna azawine 2025 azatifufuzile malilo a chilima

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 16 днів тому +1

    Zama banja izi asiyeni.

  • @user-co6sc8om5n
    @user-co6sc8om5n 15 днів тому

    Bola kaliati osati marry Mmmm

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu 15 днів тому

    Mery alibwino Kwa omwe timakonda chipanichi,komano atati wawina zizamupanga force kukwatila mwina asakufuna pomwe akulilabe mamuna wake coz sitikudziwa kuti inye mwini anayika nthawi yayitalibwanji kuti adzakhale pabanja.

  • @MaggieCement
    @MaggieCement 16 днів тому +1

    Anthu muli ziwanda ndithu zau adakalira mamunake nde akhale busy ndi za dziko mufuna mumupheso mary.?ngati naye ali maganizo asalowe ndale ndi ufiti iya mufina muthere ndalama zake asauke basi anatitu iye siwandale iye amakonda kuimba mulekeni mwana wa eni

    • @HaroonMaundala-lg5lg
      @HaroonMaundala-lg5lg 16 днів тому

      komaso mayi chilima ngati akuvomela zompusa ngati zimenezizi avekedwa dzina oyipa kwambili. Palibe chosangalasatu apa. Asakopeke ndi zithu zompusa ngati zimenezozo. Apitilize kulilila amunawo. Koma ngati akufuna kuyaluka apange nawo phada ameneyi.

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 16 днів тому

    mmmm sakuyima msaname

  • @masakaunga4099
    @masakaunga4099 16 днів тому

    Mary akudwala

  • @TaweniChavulaKamwendo
    @TaweniChavulaKamwendo 16 днів тому

    Eeee 😳

  • @imraanJafal
    @imraanJafal 16 днів тому +1

    Kkkk Kom ziona izi

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 16 днів тому

    Vice azakhale Denice mahata

  • @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy
    @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy 16 днів тому

    Radio yanji iyi

  • @GiftMwaungulu
    @GiftMwaungulu 15 днів тому

    mufuna akwatiwexo pompano

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb 16 днів тому

    Akungofunapo ndalama abale anga mukamatsatira anthu amenewa muchedwa nazo.. UTM yapita ndi mwini wake basi.

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o 15 днів тому

      Hmmm inu musavutike simunalowe mmaganizo a anthu mukuchedwa

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp 16 днів тому

    Pambuyo panu madam

  • @yowasschitsosa5348
    @yowasschitsosa5348 16 днів тому

    Kmano mphavu zoimila chipani azitenga kut mpamene mamuna sanathe mwezi ali m'manda kaya poti wakonda

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 15 днів тому

    Mwinanso ndi amene amkamunyenfelera Chilima kuti tiyeni tipange gwili zako asokogore awa Inu mudzabwere pambuyo nchonsecho akudziwa chimene akuchita and Chilima chifukwa cha kudzichepetsa ndinso ulemu ndinso kukhulupira anavomera osadziwa kuti Maiko usi ndi nthera kuwiri akapita uku akukqmba zina amatenga za uku kumamuudza Chakwera Lero amusogodza Chilima iiiiih ine mtima wanga udakandipweteka mpaka Pano moti usiku ndimangotutumuka

  • @DanielKamwendo-vs1xn
    @DanielKamwendo-vs1xn 15 днів тому

    Mufuna Ana ankhaleno onkha heti🙄

  • @PeterThomas-o9k
    @PeterThomas-o9k 9 днів тому

    Yoooohh
    Haybo she still crying his
    Husband she can't be leader that is people talking lie things