Dalitso Kabambe watuluka monyanyala ku DPP ndipo statement yasonyeza kale ku Chipani chomwe akupita

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 20 сер 2024

КОМЕНТАРІ • 68

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4w Місяць тому +6

    Akuzakhala running met wa APM MUZANDISIMIKIZA IYI N MISSION mark my wards

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Місяць тому +2

    He is our president at UTM. Wachoka kuchipinda kupita pa seating room. UTM and DPP we are one.

  • @hamischikalimba6626
    @hamischikalimba6626 Місяць тому +2

    Welcome to our beloved party UTM osaopa, osafooka osatopa SKC ndi ineyo ndi iweyo ndi ifeyo

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Місяць тому

      Akabambe amafuna uprezdent ndiye mmene inangocitika ngodzi ya kuchikagawa achilima mkutisiya mumtima mwawo.amakondwa kuti atenga uprezdent ku utm akuluwa musavutike nawo asiyeni akaimire ku utm

  • @thokojames5231
    @thokojames5231 Місяць тому +4

    Musaiwale naenso anali gulu lofuna kuba chipani la kondwani nankumwa ,komanso after kuionera patali kuti sangamake pa adad basino kuthawira ku UTM KUMENEKO MPATA AKAUUPEZA ayende bwino usazabwerenso ku dpp

    • @jeremiahmalikebu2393
      @jeremiahmalikebu2393 Місяць тому

      Dalitso was a favourite wa adad, he is the only one amene adad amamukhulupilira kuti atha kumupanga endorse. Believe me, iyiyi ndi movie ma guys wa(adad ndi Kabambe) akudziwana.

    • @user-st6bt5vv9c
      @user-st6bt5vv9c Місяць тому

      Mwana amalira ninkodzo wake asiyeni ayende bwino both him and others are not settled kutha kwamunthu kumeneko

    • @thokojames5231
      @thokojames5231 Місяць тому

      Komano movie imenei zitengera kuti akupitako akakhaladi president

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Місяць тому

    Ngati watuluka muchipani cha dpp pali ndjira ziwiri zokha zimene ndingamuwuze 1 kuyambisa chipani chake. 2 asalowe chipani chilichose mumalawi.
    Chifukwa pali njira imozi imene ndawona kuti kumalawi kuli vuto loti anthu wosiya zipani zao ndikumalowa kwina amakhala osokoneza kwambiri komaso amakala anthu okula mutima palipose safuna kukhala opanda udindo

  • @SueWahna
    @SueWahna Місяць тому

    Akuwoneka upule akufuna ndithu maganizo anga nduwona ngat Dpp itat yapanga alliance uyuyu afuna cholinga azakhale running mate

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Місяць тому

    Kumalawi kuyenelaso kukhala lamulo loti ngati munthu ali muchipani asatuluke ndikulowa chipani China ngati watuluka basi a siye ndale.
    2025 tikupempha ku parliament kuti akachose lamulo loti 50+1 aliyese apite ndichipani chake 2025. No alliance ( mugwirizano )
    Zikupangisa phokoso ziko silikuyenda bwino

  • @chisomokawotcha1766
    @chisomokawotcha1766 Місяць тому +2

    Ndi running mate wa peter uyu from aliance ya utm ndi dpp kuti anthu aku dpp asadzayankhure zambiri iyi ndi plan

    • @bysongeorge3243
      @bysongeorge3243 Місяць тому

      Ikhoza kukhala good move , tiona zambiri sitinati. Ku DPP kuli vuto komabe izi sizintha chikoka chomwe chilipo pakati pa anthu ngati tisaonenso ena akuchoka..

  • @PharrohmagawaZimba230
    @PharrohmagawaZimba230 Місяць тому

    Guys apa pagona ndale zazikulu iye uja akatenga president ku utm azapanga alliance ndi dpp

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Місяць тому

    Ayende bwino bola ngati machoka mwamtendele

  • @user-ln7ff4su2r
    @user-ln7ff4su2r Місяць тому +1

    It is mission not kunyanyala mungopusapo

  • @TimothyPalira
    @TimothyPalira Місяць тому

    Zitseko ndi zotseku ku utm

  • @lyiemax
    @lyiemax Місяць тому

    We love DPP and we love UTM as well, the decision is very good and powerful than joining MCP ❤❤❤

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Місяць тому +1

    Bola ngati abwelera utsogoleri weniweni osati kupusisa anthu patsogolo kutembenuka hmmm

  • @jomochirwa
    @jomochirwa Місяць тому

    Musapusitsike inu izi ndiye amati ndale zenizeni akungofuna kutipusitsa awa ,iyi ndi plan yoti dpp yonse idakhalilana pansi kuti ipangidwe ndicholinga choti utm ija ijoyiniletu ku dpp ndiye kabambe watumidwa ngati nthumwi kuchokela ku dpp kulowa utm.woooo!

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Місяць тому

    Pitani ku UTM.We want energetic leaders in UTM

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 Місяць тому

    Pamene zafikapa sip

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Місяць тому +1

    Njomba zimenezo kufuna kupusitsa a Malawi 😂, adakali ku dpp komweko koma akufuna apusise wanthu apite ku utm akatero akasankhidwa kukhala president wa utm kenako azapange n'gwirizano ndi DPP ndiye ku dppko azakhala VP wa peter akatero peter azachita resign ndiyekuti kabambe azasala nkukhala president wa DPP. Izi nzomwe amadananazo achina Nankhwa aja , peter waku Thyolo, kabambe waku thyolonso.akufuna azasiilane mpando anthuwa akuziwa chomwe akuchita

    • @user-gp10.10
      @user-gp10.10 Місяць тому

      Apa mwaganizo mozama bro,zitha kukhaladi chomcho

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Місяць тому

      Aaaa palibe ubwino wake mnzeru za alliance ife a UTM tadzidziwa ndipo tikudzidziwa takula nazo mpaka taluza president wathu palibe angavotere izi mukunena iwalani

  • @JamaniNyirongo
    @JamaniNyirongo Місяць тому

    Pitani mmtendere anthu adyera inu.
    Kususukira upresident nkana mwatuluka mtawona kuti ku utm sck wamwalira

  • @user-pu1fy9rs3h
    @user-pu1fy9rs3h Місяць тому +1

    Samapita ku UTM SKC alimoyo🤣

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y Місяць тому

    Let's meet on our alliance

  • @Aminayaumi.in8tn
    @Aminayaumi.in8tn Місяць тому

    Apa nde akufunadi kuimaliza UTm cholinga akasakhidwe kudzakhala Vice president kuti UTM itheretu iyi ndi plan

  • @FarookStambuli
    @FarookStambuli Місяць тому

    Welcome Mr kabambe to utm

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 Місяць тому

      Welcome to UTM monga ngati member chabe osati President

  • @paularason
    @paularason Місяць тому

    Welcome to UTM Mr

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg Місяць тому

    Ngati akufuna kupita ku UTM apite koma tione kaye performance yake Ali ku reserve bank and also ku DPP. sometimes timakhala ndi anthu oti atha kugwila ntchito bwino dziko ndikutukuka koma amalephera chifukwa sapatsidwa mpaka bwinobwino or kuwagwiritsa ntchito mosiyana ndi mbali yomwe iwowo amayiziwa and atha kupanga deliver mosavutikira if they given the necessary resources. So I believe ngati anagwirako ntchito ngati nkulu wa reserve bank nzeru zilimo, he can be useful ku dziko lathu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Місяць тому

    Wayiwonera patali sangamake pa Apm

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 Місяць тому

      Osapusisika inu uyu ndi Cousin wa APM pachi bale chawo

  • @PatrickMtira
    @PatrickMtira Місяць тому

    Mwapusa mr mukanangokhara komweko bwezi trem inayo akanakupatsani kuti mudzaimire km apa palibe mwachita

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 Місяць тому

    wachita bwino kusiya chipani cha kubanja

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Місяць тому

    Muuzeni akalowe Ku MCP asati nyatsa

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba Місяць тому

    A UTM musanyadire,woteroyo ngwa dyera

  • @user-vx5kv8dz3d
    @user-vx5kv8dz3d Місяць тому

    Wachita bwino akalowe UTM . Vote yanga azaipeza

  • @user-ru1mm7bf4p
    @user-ru1mm7bf4p Місяць тому

    Wadabwitsa ndani munthu olo chipani alibe

  • @BrianJoe-z7u
    @BrianJoe-z7u Місяць тому

    Aaaaakabambe kabambe

  • @user-jj1zv2rs7f
    @user-jj1zv2rs7f Місяць тому

    Munalibe impact iliyonse mwainu yen Danish bwino

  • @user-kq6rp6hn7y
    @user-kq6rp6hn7y Місяць тому

    Welcome to UTM

  • @user-jj1zv2rs7f
    @user-jj1zv2rs7f Місяць тому

    Go well

  • @AndreaSignala-hk2yg
    @AndreaSignala-hk2yg Місяць тому

    DPP 2025 boma muzakumbuka

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Місяць тому

    Kabambe akuthawa chani ku DPP? Kapena Biden wa Malawi?

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Місяць тому

    Zakhara bwino chipan cha banja ichi

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Місяць тому

    Pitani ku aford basi

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Місяць тому

    Ku Dpp usogoleri kulibeko koma dyela kukakamila udindo gogo imeneija osapasako mpata achinyamata

    • @DalitsoMatope
      @DalitsoMatope Місяць тому

      Achinyamata ngati inu alepheratu

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga Місяць тому

      Chakwera wapasa ndani mpata?? Mesa nae wakakamira 😅

    • @DalitsoMatope
      @DalitsoMatope Місяць тому

      @@MzadziWangaakufuna amalizitse kudya misokho ya malawi

    • @SaidiMbawa-st6bj
      @SaidiMbawa-st6bj Місяць тому

      @@DalitsoMatope zikugwilizana bwanji usogoleri ukufunika kwa Ana chakwela so ndi wachikulire bola awa not gogo ngati Peter kabambe kuti achoke kuli vuto kumeneko uzavomereza mochedwa

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana Місяць тому

    Ali ndi tsoka ameneyo

  • @hamischikalimba6626
    @hamischikalimba6626 Місяць тому

    Peter Mutharika sangasiye mpando once voted into power unless death takes him. So l salute that decision Kabambe has made

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Місяць тому

      Ndipo zoona Peter Munthalika sangasiye mpando wa chipani cha achimwene ake zoona

  • @user-nw6ie3xx8b
    @user-nw6ie3xx8b Місяць тому

    Prophet liyabunya analankhula za utm Zana kuti ayigula, liyabunya is not just a prophet like others no he is Elijah of our generation, love u prophet, bless me my name is Paul kheche mvuma

  • @WilisonWada
    @WilisonWada Місяць тому

    😂😂😂😂

  • @LaitoneJefitala
    @LaitoneJefitala Місяць тому

    Wachita bwino alowe chipani chapamaloponse ngati catolica

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      Catholic zoonadi ndi church ya pamalo pose koma mulibemo choonadi, like praying for the dead, Christmas, forgiving sins like God himself,kubatiza ana,ubatizonso wabodza,kuletsa kukwatila,kumafuna kupanga control boma pomwe church and state siziyenera kuphatikizana, kusintha sabata from surtuday to sunday,tsiku kumayamba usiku kuthanso usiku mmalo moti tsiku liziyamba kulowa kwa dzuwa kuthanso kulowa kwadzuwa ndi zina zambili bible likuti turukanimo mmenemo anthu anga babulo wagwa wagwa amayi wa a chigololo wa zonyasitsa za dziko ndipo mpingo umenewu uli ndi ana ake omwe amaitsatira zochita zakezo monga sunday keeping and all things that are out side the bible these practices are from pagan the chief of all paganism is the enemy of God called satan thanks for understanding ❤❤❤❤