Chibade my man, my mucian much love on you my bro, iweyo sunatheyi and I sked God to provide you with more blessings to career of music and give you more healthy life forever my brother
Chibade just advice please you born to be musician.... don't allow your career to be destroyed before you reach where God prepared for you to reach. Pitilizani apa zilibwino kwambri
Nyimbo yabwino, Chibade koma tikonze history apa. Bakili Muluzi si amene anabweretsa multi party ku Malawi. Kunali ndipo kuli anthu ambiri omwe anapangitsa kuti ndale za zipani zambiri ziyambikenso ku Malawi. Ma Bishop a Katolika, ndi mabungwe oyima pawokha monga PAC, Women Voice, Civil Liberties komanso a Malawi onse amene anavotera zipani zambiri mu Referendum ya mchaka cha 1993. Ine ndivota nawo.
munthu oziwa kuimba ,nzika ya Malawi yokonda ziko lake , mulungu akupase Moyo wautali chibade ...✊
thank you for entertaining us and keep resting in peace legend
Monga ife apadzana umatidalitsa kwambiri, may God be with you mene ukulangiza mkulankhulira a Malawi
Big up Chenkhumba umatiimilira.. welcome back on the ground....uona mbuzi Zina zizikusaka saka koma osabwelera mbuyo ayi keep it up.
I like so much thomasi Chibade,my brother God bless you...I'm Mario from Moatize- Mozambique.
You have been quite chibade miss your music Foster Lungu Katete Zambia.
The way I love his music God please give another chance much love from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Chibade my man, my mucian much love on you my bro, iweyo sunatheyi and I sked God to provide you with more blessings to career of music and give you more healthy life forever my brother
Thanks very much for your love to the Malawi 🇲🇼 artists, we love you our neighbors from Zambia 🇿🇲we are the ones
@@blessingskaseka,❤
You left us with tears 😭😭😭 why so soon chibade😭😭😭😭😭
Pure talent without illuminati condition. We will miss you bro 😭😭😭😭😭
Nice song coming up from chekhumba chibade
U such talented gy bro... all de best i wish u to came back to ur tune again. Your song got a message to many people
This song is not new but it's Msg still is worth today
Awawaaaaaa ndi wakulu km lest in peace
this guy was very very talent your massage well never you never die Rlp chibade
We started loving him even before his popularity
Focus Tomas chibande is very..very talented you please god help tomas chibande & give onether chance chibande tomas for his music pls.
This guy is very very talented please God help him and give another chance for his music career
Amen
Amen
True....!!!
He will be ok on Jesus name
His new album is gonna revive him, all the best Chenkhumba….
Chibade you know what you are doing keep it up koma Jada imwani pang'ono
Wow this is 🔥🔥🔥 track ,chibade sanatheyi big up
Chibade just advice please you born to be musician.... don't allow your career to be destroyed before you reach where God prepared for you to reach. Pitilizani apa zilibwino kwambri
My favorite singing 4ver amandyimbila bwn kwambiri long leave God bless you all time 🇲🇼🇲🇼
He's really deserve another chance God bless this Man for giving him another chance
Thomas chide youtube
Very sad to hear stories of his death.From USA
An old song that talks about the current situation
Sounds great and blessed talented.....
Waphatu apa chibade, Osama Ibiza unangoti ziii bwanji
This guy knows alot about historical background of multiparty
Favorite
Man Thom amatha nyimbo yakalekale ngat yangptuka kumene
Ndimamuvulira chipewa tomas chibade nthawi zonse. Mulangizi che nkhumba
Keep on trying broo ....u wl get back
Nimamkonda Chibade
King of Malawian local music 🎶
Come again Chibade please God help him
Nyimbo yabwino, Chibade koma tikonze history apa. Bakili Muluzi si amene anabweretsa multi party ku Malawi. Kunali ndipo kuli anthu ambiri omwe anapangitsa kuti ndale za zipani zambiri ziyambikenso ku Malawi. Ma Bishop a Katolika, ndi mabungwe oyima pawokha monga PAC, Women Voice, Civil Liberties komanso a Malawi onse amene anavotera zipani zambiri mu Referendum ya mchaka cha 1993. Ine ndivota nawo.
Zoonadi
Talented guy come back God is calling you to sing for the people
Man chibade zimangovuta koma luso ilili ndilobadwanalo ulemu wanu
Satan wants to ruin this talent ... please God save him with your Grace
My best artist Thomas, talented man
Theirs strong message in this song❤
tilisowa luso lako. R I P CHIBADE
Mr chibade i wish all the best kut ubwerereso pa graund
Thomas chibade malawi good pavamene uyimba
Mulungu akudalisen chibade
Nice truck from chibade big up
We miss you Thomas Chibade 😊 very happy to hear this new song ❤😊
I can see you back my boy more fair
I always follow this guy and was disturbed to learn about his behaviour of being a beer guzzler but still I love your music from Zimbabwe
😅😅
Wafikaso iwe wakachaso 😂😂
nyimbo ilu bwino kwambili ndiposo yolilisa !!!!!!!!
boma Malawi ndili masiye lopanda ayine ake .zomwe akupanga atsogolile zomvesa ,chitisa manyazi .chibade tayesesa kuwunikila amalawi
Chibade ndi legent
Morefire
Keep it up my home boy
Nice
Ur still best
Salute 🔥
More fire
Uthenga ulimo ndithu...Malawi wanyanya kuthyolera...
Palibeso angafikilepo ndani Koma pa 2345 palibeso
❤
😍😍😍😘😘😘
@Besten Selemani let me know how I can buy and support his album
Kapena adalakwa Nd chilima kutuluka DPP? Ife sitiziwa pano kulila kosatha😢😢
+265 999 40 60 09 chibade number mukhoza kuyakhula naye ya soap yokha ponyeleni Zikomo
Kkkkkk
😂😂😂😂
Ct
Kodi its a new song ?
Ayii
Yeah imeneyo inatuluka last year.
Kodi muluzi ndiamene anabwelesa multiparty kumalawi?🤔🤔 koma nice song ndipo yabwera mnthawi yake
Eya anali Muluzi
Ndingayipeze bwanji number ya chibade?
search artist of the week with Thomas chibade,watch it at the end of the program he gave out his phone number.
@@mosesphiri457 oky thanks
May your soul rest in peace brother
Nice