ARINDI MWANA AGWILITSE. mpungu Joseph nkasa

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 113

  • @user-xc3fh3ej4v
    @user-xc3fh3ej4v 5 місяців тому +5

    Nkasa is the one of musician advisor in the country of malawi.....kp it up🤝

  • @anusahjenala1063
    @anusahjenala1063 6 місяців тому +5

    Mwalowa mmalo mwa soldier ndinuyo sopano😊

  • @user-cb2cv9fz7m
    @user-cb2cv9fz7m 6 місяців тому +4

    Ndipo chakwera ambuye MULUNGU akuone munthu kuipa mtima ngat imfa eee ndipo chakwera wamuonga Malawi

  • @user-tv2ic6xd4d
    @user-tv2ic6xd4d 3 місяці тому +2

    Chakwera adzivere yekha uthenga wabho Mr Nkasa

  • @KestenMukhwapa-qp2gj
    @KestenMukhwapa-qp2gj 2 місяці тому +2

    Legend we love your music

  • @YusufChipojola
    @YusufChipojola 3 місяці тому +2

    Nice mr mkasa sakumva a poster

  • @user-rc3ze2oi7u
    @user-rc3ze2oi7u 6 місяців тому +2

    WANUNKHADI MALAWI 🇲🇼 MR NKASA GOD BLESS YOU

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz 2 місяці тому

    eeeemkasa ndi katundu mumalosera zoooona

  • @JoshuaMataula
    @JoshuaMataula 5 місяців тому +1

    Phungu Mulungu apitilize kukupatsa. nzeru zochuluka kuti upitilize kutisangalatsa more fire

  • @NysonStandy
    @NysonStandy 2 місяці тому

    Mafuno abwno Apte kwa Joseph mkasa,phungu mfumu yacikhalidwe pamaimbidwe amadziko amzeru kwambiri

  • @NysonStandy
    @NysonStandy 2 місяці тому

    Mfumu kapena kt paramount ya mzeru phungu wa chilonwe ku Zomba Malawian,go ahead phungu

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 5 місяців тому

    I like this guy too much amaganiza movuta kwambili na nyimo iyi siyandale koma ngamo bsi kuswakuswa sakugawa ma sweet I like once again i like it.

  • @user-yz5yt3vj6w
    @user-yz5yt3vj6w 6 місяців тому

    Koma Nkasa umayiponyeradi kwakuya, ❤woyimba koma uyu

  • @augustMag
    @augustMag 6 місяців тому +1

    I like this song indeed Mr you are saying the truth All Malawi is Smalling

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 12 днів тому

    Nkasa koma pano ali ku Chikangawa awa dyera apa zina kuseri zina awa

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz 2 місяці тому

    keep it up mr mkasa god bless u malawi know is destroyed

  • @ungweruwinthu6907
    @ungweruwinthu6907 6 місяців тому

    What a song.. Big up Nkasa. Sugar Ali pa 3700 now.. Malawi wanukhadi

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 6 місяців тому

    Big man kuzatulukila sopano ndi waduka ndi Malawi ndizona simukunama ayiii God bless you always

  • @augustMag
    @augustMag 2 місяці тому

    Nice song keep it up good work 🔥♥️

  • @majendauzananilimitedi2049
    @majendauzananilimitedi2049 3 місяці тому

    "galimoto yomwe yaononga nsewu yomweyo singakoze, pakufunika katapila adzakonze"

  • @user-wp5rk5zk7t
    @user-wp5rk5zk7t 5 місяців тому +1

    Davide mbewe woyeeeeeeeee

  • @shamekayela5653
    @shamekayela5653 2 місяці тому

    Mr Mp indeed things are tough,covid,and Ukraine war are not a good excuse

  • @DaudJulius-hz8uy
    @DaudJulius-hz8uy 6 місяців тому +1

    Boni kalindo ndi atupele Muluzi akhonza kusintha zinthu tiese amenewa

  • @FugieKholowa
    @FugieKholowa 3 місяці тому

    This guy iiiiiiii born for his country

  • @user-ut5nx5vd6p
    @user-ut5nx5vd6p 3 місяці тому

    This man is very creative I'm telling you.mr nkasa more love to you sir

  • @user-xc1gk6bw6m
    @user-xc1gk6bw6m 3 місяці тому

    Wanukha malawi🙏🙏 may God bless you my fadah ❤❤❤❤

  • @ObreinMhone-hs4vq
    @ObreinMhone-hs4vq 4 місяці тому

    I like his music it's straight and true

  • @LovemoreKachingwe-nm8bz
    @LovemoreKachingwe-nm8bz 6 місяців тому

    Big mutchuleni munthuyo kkkkkk mumakwana ndinu prophet

  • @madalitsoyakobe2123
    @madalitsoyakobe2123 4 місяці тому +1

    🔥🔥🔥

  • @user-tr4fv6ry9q
    @user-tr4fv6ry9q 3 місяці тому +1

    Big up phungu,we like your music

  • @VernacioChintedza
    @VernacioChintedza 4 місяці тому

    Nice tune big up nkhasa

  • @grivinmaniwa166
    @grivinmaniwa166 5 місяців тому

    Ndiye kuti mavuto a dziko la malawi ndi ogonera. Chifukwatu pomwe ena akuona ngati nyimbo iyi ndi yatsopano koma ayi ndithu ndi zaka za kumbuyo

  • @CosmasJohn-zn4qd
    @CosmasJohn-zn4qd 3 місяці тому

    Umakwanira mkasa big up

  • @user-im4bs7fk9o
    @user-im4bs7fk9o 6 місяців тому

    I like this song very much the meaning is still elevant &power😂

  • @GiftMathewe-fr3kn
    @GiftMathewe-fr3kn 3 місяці тому

    Very nice song❤

  • @giftbanda4518
    @giftbanda4518 5 місяців тому

    I love this song. You've said it all Phungu

  • @regsonhara1725
    @regsonhara1725 6 місяців тому +1

    Komabe zina zikusapotabe kusangalala kuti anthu akuvutika

  • @Daniel-wk7uj
    @Daniel-wk7uj 6 місяців тому

    IZI tinasankha tokha timati tiyese achinyamata komanso opemphera lero ndi izi. APM amadziwa ndipo anatiuza kuti ngati tikufuna mavuto tivotere CHAKWERA koma ngati tikufuna zabwinobe bola DPP koma ife tinasankha kuvutika ndi anthu amulungu komanso wachinyamata oganiza bhooo.Lero mavuto okhawokha.

  • @PatsonYusufMaulana-rj9lf
    @PatsonYusufMaulana-rj9lf 3 місяці тому

    Big up my brother,that's Joseph Nkasa whom I know 100,,%

  • @ThokohKalonga-je9rx
    @ThokohKalonga-je9rx 4 місяці тому

    Big up mr Nkasa nice song

  • @daviestsamba9639
    @daviestsamba9639 2 місяці тому

    Big up Nkasa ❤ I love ur Songs but Malawi is the problem to vote MCP.Nkasa since start music 🎼 gave US message but when to to vote u do Sam mistake.
    😂😂😂😂

  • @user-uz1yp6ni8o
    @user-uz1yp6ni8o 3 місяці тому +1

    Mayo dziko langa

  • @user-pf5er7gc9s
    @user-pf5er7gc9s 3 місяці тому

    Beautiful song

  • @InnoPondani
    @InnoPondani 4 місяці тому

    Song with a massage❤

  • @JamesNgwamire
    @JamesNgwamire 4 місяці тому

    nice song tinenereni basi

  • @MaliyamualabiMaliyamualabi
    @MaliyamualabiMaliyamualabi Місяць тому

    Nice

  • @AlickMwaza
    @AlickMwaza 4 місяці тому

    Kkkkkkkkkkk kuimbatu ndikumeneku

  • @AgnesNkukumila
    @AgnesNkukumila 5 місяців тому

    Nice song keep it up

  • @MadandoChannel
    @MadandoChannel 6 місяців тому +1

    Eddie longwe Dada general 2025

  • @user-wv5hz8ce3i
    @user-wv5hz8ce3i 6 місяців тому

    Ndipo inu zachabetu kwathu komwe ngati ndife obwela mhh

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 3 місяці тому

    Mukasa umakwana❤

  • @user-et6we9mx5h
    @user-et6we9mx5h 5 місяців тому

    Mr chakwera please Malawi akuvutika kwambili tavani kulila kwa anthu

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon 2 місяці тому

    ❤❤❤

  • @KayifaSkeffa123
    @KayifaSkeffa123 3 місяці тому

    Akupaseni galimoto chondechonde😅😅😅😅

  • @LovemoreKachingwe-nm8bz
    @LovemoreKachingwe-nm8bz 6 місяців тому

    Wanunkhadi Nyasaland Maka nthawi ino eeeeeeeeeee

  • @user-cr7iy2tc6f
    @user-cr7iy2tc6f 6 місяців тому

    😢😢😢😢 nyimbo iyi inali vumbulutso

  • @mcdonaldgerard9707
    @mcdonaldgerard9707 4 місяці тому

    Nkasa nthawi zonse amalangiza, komanso kunena chilungamo angokhara osaganiza bwino ndi atsogoleli wo🤔🤔

  • @fostenkachinga9945
    @fostenkachinga9945 6 місяців тому

    Nyimbo iyii muli uthenga 😢😢😢

  • @burtonamin5913
    @burtonamin5913 2 місяці тому

    Nice keep it up

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q 3 місяці тому

    Ndithawira kuti 😢😢😢 passport ndi license atseka Malawi watha basi

  • @GenesisYafika-cs5nm
    @GenesisYafika-cs5nm 5 місяців тому

    Awuze phungu anthu opanda chfundowa,adyera

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 3 місяці тому

    Nkasa umakwana chakwera has to understand the message

  • @stevendemanje
    @stevendemanje 2 місяці тому

    Inu ndi nyatwa Mr mkasa

  • @Robert-bx8sp
    @Robert-bx8sp 5 місяців тому

    Ñice song

  • @Alomwe
    @Alomwe 6 місяців тому

    Mr Chakwera please tamvani kulira kwa Malawi

  • @AaronWiniko
    @AaronWiniko 3 місяці тому

    Legend

  • @Hobiexd-ji9kz
    @Hobiexd-ji9kz 6 місяців тому +2

    Zoo na big

    • @Henry-vw2cz
      @Henry-vw2cz 5 місяців тому

      Double salute mkasa

    • @user-bq8gb7tb1l
      @user-bq8gb7tb1l 4 місяці тому

      Tokota nkasa,koma nsaku musiye asauka yekha ndi mowa wake,zolinga ndi zofuna

  • @yamikanikhanga4527
    @yamikanikhanga4527 6 місяців тому

    Apadi ofunika D 7 ikonze Malawi

  • @user-og9fq6yu9p
    @user-og9fq6yu9p 6 місяців тому

    Auze Zions wanunkha

  • @Enockjosephy2528
    @Enockjosephy2528 6 місяців тому

    Mumakwana big

  • @user-ur6uh5nm8b
    @user-ur6uh5nm8b 5 місяців тому

    Atupele muluzi azakoza dziko❤

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d 5 місяців тому

      Eeeh this guy dyela too much like father like son, koma ngati akuganiza atupele and chilima waiphonya

  • @user-ww3fe2bz2u
    @user-ww3fe2bz2u 6 місяців тому

    Zoona big

  • @Buleyaprophet
    @Buleyaprophet 6 місяців тому

    Kkkkk mutchuleni timuziwe

  • @andrewchirwa2193
    @andrewchirwa2193 6 місяців тому

    Malawi wanukhadi mukuziwakale

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 5 місяців тому

    Welcom Nkasa kp it up chinyimbo cha heavy Malawi is on for sale koma ndiye wanunkhirathu

  • @MasterMalekwa
    @MasterMalekwa 3 місяці тому

    😢😢😢

  • @user-yk9ib1bg2b
    @user-yk9ib1bg2b 6 місяців тому

    Koma ndiye wanuknkhadi Malawi lazaro wanunkhitsa Malawi

  • @geraldlukhere1159
    @geraldlukhere1159 6 місяців тому

    Mkunena chakwela was ma trip uyu Kodi?

  • @user-ur6uh5nm8b
    @user-ur6uh5nm8b 5 місяців тому

    Phungu umakwana

  • @LazarusBwanali-qw5qc
    @LazarusBwanali-qw5qc 3 місяці тому

    Nkasa ndi akamuna

  • @user-im4bs7fk9o
    @user-im4bs7fk9o 6 місяців тому

    Usinda

  • @Cleva-dd1qd
    @Cleva-dd1qd 3 місяці тому

    Ndi choncho phungu

  • @CalmBackpacker-lw7ol
    @CalmBackpacker-lw7ol 3 місяці тому

    Nyimbo yabwera muthaw yake

  • @Cleva-dd1qd
    @Cleva-dd1qd 3 місяці тому

    Ndi mommo phungu

  • @user-pj3qi7gb3s
    @user-pj3qi7gb3s 5 місяців тому

    Amkasa 5000 ilipo gaileni number yanu ndikuthokozeni

  • @DanielMoses-yp6qc
    @DanielMoses-yp6qc 3 місяці тому

    Kkkkk

  • @user-yd7di3cf8q
    @user-yd7di3cf8q 6 місяців тому

    A malawi kuvutika chifkwa cha vote yao ai zikomo

  • @user-pj3qi7gb3s
    @user-pj3qi7gb3s 5 місяців тому

    Mkasa ndiwe mulosi ndipo ulosi wako ndiwolondola

  • @user-hp8du2lx3z
    @user-hp8du2lx3z 6 місяців тому

    Amalawi tili pamoto

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 6 місяців тому

    😂😂😂😂😂Chakwera wanunkhisadi Malawi mfiti ameneyi zedi ya MCP

    • @nkopedafter831
      @nkopedafter831 6 місяців тому

      😅😅😮😢

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 6 місяців тому

      @@nkopedafter831 😃😃😃Nthakati yoopsa zedi tiigwetsa Chaka chammawa ibwelere kumakalima maganyu😃😃

  • @dicksonmlera2777
    @dicksonmlera2777 6 місяців тому

    Malawi is on the market

  • @akimsakala327
    @akimsakala327 6 місяців тому

    Ndipo zoonaditu

  • @user-gl4wc9pq4e
    @user-gl4wc9pq4e 6 місяців тому

    Zovuta

  • @MaidakaisiNkota-oo5tz
    @MaidakaisiNkota-oo5tz 6 місяців тому

    Timadabwa kuti otiyankhulira aja alikuti

  • @user-zu4wc1kw2j
    @user-zu4wc1kw2j 3 місяці тому

    Ndeno nyimbo zako ngat menezi ungapeze 10k views...anzako akulemelelatu zomwe zija iwe busy zandale...fokol

  • @McphersonMsulira-zx2lj
    @McphersonMsulira-zx2lj 6 місяців тому

    Mapasaport ayamba kutuluka pamtengo wa 14500

  • @user-dd1qq5xq1k
    @user-dd1qq5xq1k 6 місяців тому +1

    Malawi for sale

    • @NYINBOZADZANA
      @NYINBOZADZANA  6 місяців тому

      Yamaha man please subscribe 🙏

  • @user-vq7fz5zu4d
    @user-vq7fz5zu4d 3 місяці тому

    Beautiful song ❤

  • @estonmnthali3719
    @estonmnthali3719 6 місяців тому

    Kkkkkkkk

  • @hardwickkameta1681
    @hardwickkameta1681 3 місяці тому

    Legend