Very nice and colourful dance from chichiri prison.We celebrate you president Nyusi and Lazarus maccarthy chakwera as you are presiding the official opening of Malawian trade fair.Achakwera palipose mungayende timakukondani kwambiri ndinu mtsogoleri wamaso mphenya aakuru kukonzanso ziko la malawi kuti libwelere mwakale ndipo zaysmba kale kuchitika.Osusa ali mmazi.
Now it makes sense, kani ndi a kaidi eti. Nde kuwaveka uniform ya mabwana awo kuti chani. Mabwana mwawavula kaye uniform kuti a kaidi a kavinile. Koma uchitsirunso
Ngati asilikali ake a 1949 tu, uniform ikuchita kukana thupi. Kaya anadya liti kaya.
Tawatulusani akaone ana ndende imaphweka muli mwana wanzako kma siziziwika m'mawa ndiwako
I'm one of moz which agriculture is in Mozambique? Akunena kafarm kalipaVuanduzi , ndikaAzungu wosati Nyusi
Koma ubale ulipati pachikwera ndiNyusi ulipatiko, fit yazuza athu kuMozambique ibwere kuno ngati zanzeru 😢
Very nice and colourful dance from chichiri prison.We celebrate you president Nyusi and Lazarus maccarthy chakwera as you are presiding the official opening of Malawian trade fair.Achakwera palipose mungayende timakukondani kwambiri ndinu mtsogoleri wamaso mphenya aakuru kukonzanso ziko la malawi kuti libwelere mwakale ndipo zaysmba kale kuchitika.Osusa ali mmazi.
Better these days timavutika mages,mafuta ndiye polankhula kumafunika kuganiza komwe mwachokera kaye
Zaziiiiii chiwongolelo chophela anthu paseu mukudya kumeneko kunkhuta et kuli njala simudziwa
Shikangawa nayeso kusatizila kuvina kkkkk😂😅😅
Aaa nawo akaidi akufuna adye nao za cikangawao
Akuti mwatenge bwino akumalizani chikangawa akwezaso mitengo
Angowakhululukira ma inmates wa
Akayidi akufuna mutuluka kikkkkk
Zazii zeni zeni
Kkkk manyasa sitizatheka basi busy basi ndi chikangawa kkk
Mbuzi zokha zokha zakuman
😢😢😢😢😢 chose so mukugona NDI njara amalawi😢😢😢😢
Now it makes sense, kani ndi a kaidi eti. Nde kuwaveka uniform ya mabwana awo kuti chani. Mabwana mwawavula kaye uniform kuti a kaidi a kavinile. Koma uchitsirunso
Makape ndarama samalandila zooneka
Iye nkumasekera izi
Rlp 😢😢😢 The white chewa
Catholic priest
You preserved our culture well 😢😢😢😢
Osauka akati avine
NOSE INU MAVINALA CHAKWERA NOSE NDINU ZITSILU
Chodzivutitsila kuvinila anthu okuzunzani ndichani? Amvekele mwetu ngati zeni zeni mxwiiiii
Ngati zikukuvuta kwa mako ukuganiza kuti aliyese zikumuvuta zeru muzikhala nazo polakhura
Mmm
Comment reserved kudzazionesera kuti ndife asilikali titumizeni kuja mumanena
Koma😂😂😂 level yachina las dema
Akayidi koma
Nice
Awa sabwerako
Camera mbora
Awawa zifukwa zowankhululukira mzokwana anyamata avina bwino kobasi kkkk
Zobheba
Kkkkkkkk anthuwo kuwonda kumeneko iiiii
Dziko lokongora koma mwaliononga agalu no makape
A prison nda security amphawi awa onvesa chisoni
Koma zikoli momwelikuyendela paliso chifukwa chomakavinila pamaso pa chakwela
asilikali wiosaziwa chimene ali mmalo mongopempha ndipakamwa koma kumaziyalusa choncho zomvesa chisoni kwambili zaziiiiiiii
Ndye akaware akufana nda Anyusi
Ok
Nthawi yomweeyo ndikulamula Kuti amasuleni milandu yawo yathetsedwa, nkhothi liyime
Ndalamah anakonza anthu akuvutika awah....,,
Za chibwana kufuna ndalama basi maluzi wa
Takatungeni magazi ku mozambikiko mubwezele Bushiri magazi ake mutenge ena a abale anu ife ayi mutisiye tokha.
Kufuna ndalama uku koma kulikufa chakachino inu chomavinira ndichani inu
Koma eee anthu akuwondako ku ndende uku
Kaye kunvesa chisoni
Malawi
Osangothawa pamenepo bwanji
Km guys umbawi sizindu guys kumavina motero kufuna ndalama
Achokela limodzi asiyen
Kufuna ndalama tawonani wapolice kuwonda
Za ziiiii ku prisonikonso kulibe ufa
Akaidiwa aimba nyimboyi akuopa kt awaphera komko chikangawayo ndi mfiti inzakeyo
😂😂😂 zaugaru basi
Koma anthu muli ndi mphanvu zobvinira eti
😂😂😂😂Koma
😂😂😂
😂😂😂😂😂😂
Koma zikoli momwelikuyendela paliso chifukwa chomakavinila pamaso pa chakwela
Koma zikoli momwelikuyendela paliso chifukwa chomakavinila pamaso pa chakwela
Koma zikoli momwelikuyendela paliso chifukwa chomakavinila pamaso pa chakwela
Koma zikoli momwelikuyendela paliso chifukwa chomakavinila pamaso pa chakwela