MCP yatengesedwa ndi nyamata wa ku Ntheu. Chakwera alibe mtendere wamtima

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 5 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 146

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana Місяць тому +18

    Zoona zake Zenizeni koma osadera nkhawa chaka chamawa kuvuta am from Ntcheu kwataine village koma mlungu adzatiyakha osaopa osafooka osatopa❤

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Місяць тому

      @@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba

    • @FrankSimfukwe-w1s
      @FrankSimfukwe-w1s Місяць тому

      Ndipo sitikuopa izisitikungokamba chabe km sitikuopa ife tikufuna chilima wathu chomuphela ndichani atiuze chomwe anawalakwila iwowo

  • @austenbushiri-cx1kh
    @austenbushiri-cx1kh Місяць тому +14

    Mawu! mawu! 🎉 big man

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Місяць тому +21

    Amalawi tonse timadziwa kut Chakwera anapha chilima mosogozedwa ndi Michael usi

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Місяць тому +2

      @@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Місяць тому

      @@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe
      Chikhulupiliro sagula
      Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu
      Mark 14:48
      (Yesu sanamugwire )
      Mark 15:21
      (Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo)
      Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka

    • @EdwinHowardmkandawire
      @EdwinHowardmkandawire Місяць тому

      Iweso kapolo ndege ija ankayendesa ndi chakwera?

    • @EdwinHowardmkandawire
      @EdwinHowardmkandawire Місяць тому

      ​@@yowasschitsosa5348kuswa zonene anthuwa

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Місяць тому

      @@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 Місяць тому +10

    Komanso kufatsakwina ndikopweteketsa ,
    Kufatsakwina ndikopusanako ,
    Amalawi ndife anthu ofatsa mopusa

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os Місяць тому

      Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Місяць тому +4

    100%facts brother mcp ndi zigawenga mbiri safuta lero taziona yalembedwaso ina apa.

  • @PIYASSFKGCHIWAYA
    @PIYASSFKGCHIWAYA Місяць тому +11

    Ulemu wanu brother

  • @MeriaMasinga
    @MeriaMasinga Місяць тому +4

    Olo Monica akuziwa kt amunanga apha chilima

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc Місяць тому +9

    Mukunena dzona brather m c p kwake kuba ndi kupha

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu Місяць тому +8

    Mmmm man mwalankhura zoona ok

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 Місяць тому +12

    Iye uja mpaka azafa akuzuzika

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Місяць тому

      @@bamusmajawa1619 munamatu simulungu ameneo and palibe munthu ali ndi mphavu yotembelera mzake,

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Місяць тому +6

    Bg ulemu wanuw mulungu adalise inuyyo nkwamasinku osse tiutseni soona sandege bg mn ashankwela angompedwa nawosso sikut wawaw kobas skc anashita nkumupha ndi ashankwela yemwyyo mfiti yyamundu😮😢

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Місяць тому +6

    Ndipo zowonadi zake. Ulemu umasowa.

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona Місяць тому +4

    Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 Місяць тому +1

    Brother More Fire 🔥....Auza Amenewo....Nthawi zonse chilungamo chimamphweteka muona mufa nd ma BP. MCP yakumpha

  • @user-yv3jp3it2t
    @user-yv3jp3it2t Місяць тому +4

    Osaopa man chakwela anapha chilima sibodzatso ayi

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Місяць тому +6

    Mau amenewo mulungu akudalisa mcp ndi yakupha auzeni ndi mbusi za anthu awa

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Місяць тому +2

    Komaso kuyakhula chilungamo MCP sikanawina kapanda chilima olo akamayakhula mwamatama akhala dzaka zingati osawina

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwana Місяць тому +5

    Inuyo mwalankhuladiii boss ulemu wanu

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 Місяць тому +1

    Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo Місяць тому

    Osatopa osafooka osawopa 💪💪💪 chakwera machende Ako aise

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e Місяць тому +3

    Kuyakhula kwachilungamo chakwera anapha chilima

  • @StevoZimba
    @StevoZimba Місяць тому +1

    Wa Bakili Muluzi VT amanena zoona😊

  • @WilliamLimwalwo
    @WilliamLimwalwo Місяць тому +3

    Zoonadi dzake, more fire,the truth will prevail 😂😂😂😂😂😂.

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji Місяць тому +2

    Ndi chipani chakupha chimenecho Cha MCP ndikukuba ndiye chitukuko chawo cha MCP basi

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z Місяць тому

    To stand on the bright side with truth and faith for all Malawian ❤

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 Місяць тому +4

    Malawi ife ndife amantha ausilu , big mwalankhula ngamo Amen

  • @KaungaYawaka
    @KaungaYawaka Місяць тому +3

    Chakwera ndiwakupha vuto anzathu achewa kuberekana nde chimene chikumlimbisani mtima mumadya naye

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz Місяць тому +2

    mcp tidakwilira limodzi ndi chilima zimu uwakwatha Wina ayelekeze kuyimila ku ntcheu mcp timpha timuyatsira nyumba osatiseweletsa😢

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Місяць тому +2

    Zoona mcpbinapha chilima zoona chakwera akuziwa ndipo ife ku mwera tizailowerela amaona ngati amalawi ndiopusa

  • @ChisomoMsiska-oi2vg
    @ChisomoMsiska-oi2vg Місяць тому +2

    Koma nkulu uyu wayankhula za nzeru kwambiri

  • @user-cn3gi2vf5n
    @user-cn3gi2vf5n Місяць тому +1

    Catholic bishops are very sharp amaima pa chilungamo Mcp ndi yokupha

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Місяць тому +3

    Auze aise,

  • @ElphinaChirwa-qk3cy
    @ElphinaChirwa-qk3cy Місяць тому

    Straight talk eeeee anthu munatipweteka kwabasi imfa iyiyiyi
    Ndipo mabala akupweteka

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Місяць тому

    Chilungamo aise Chakwera ndiyemwe anapha Chilima chifukwa cha udindo

  • @MrBone-zj1wq
    @MrBone-zj1wq Місяць тому +2

    Zitsiru zimenezo zimene zikuti zalowawa ndale,mbole zawo kwambiri

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 Місяць тому +2

    Walankhula bwino brother

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s Місяць тому +1

    Kwambliii Mr your talking the truethhh

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Місяць тому +2

    Zoona chakwera anamupha chilima

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 Місяць тому +3

    Zoona zokhazoka ndithu. Mulungu Ali pampando

  • @JumaJuma-i9t
    @JumaJuma-i9t Місяць тому +3

    Ndipo kumeneko ndiye kuyankhula

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Місяць тому

    Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f Місяць тому +1

    Chakwera wakupha tonse tikuzwa

  • @lysonkaselema7321
    @lysonkaselema7321 Місяць тому +1

    Ntcheu ndimaiziwa ndiimeneyi

  • @SandlessWakhuluma-ns1io
    @SandlessWakhuluma-ns1io Місяць тому +1

    Mau ndiwo mweo ayakhula munthu.

  • @LouisAndrew-jr1yj
    @LouisAndrew-jr1yj Місяць тому

    Ukavomereza kuti Yesu ndi Ambuye, udzapulumuka🙏🙏

  • @user-my4gr1pv8h
    @user-my4gr1pv8h Місяць тому +4

    Tizamusinja amweneo big ngamo

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Місяць тому

    Chakwela achoke and ngati Pali munthu woti akuyenela kumangidwa ndi chakwela ndi nduna zake

  • @user-gr5zt6kw3s
    @user-gr5zt6kw3s Місяць тому

    Well said bro

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Місяць тому +3

    Chakwera Mutu Ngati machende amkango

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu Місяць тому

    Zoona bro,ndipo anthu awawa ndi oyipa ndiposo ineyo amandinyasa heavy ndipo moyo wanga sindifuna kumawona,ndimava kuphweteka ndipo ineyo ndikanakha nfiti tikanaphweteka ndithu

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Місяць тому

    😂😂😂😂 amati wina ludo kkkkkkk😅😅😅😅

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm Місяць тому +2

    Mau amphavu bro MCP ndiyakupha idapha anthu ambiri

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q Місяць тому

    Mawu oveka chakwela dzelu alive mamuna ndi wabakili muluzi tv ameneuja amaganiza hsve

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE Місяць тому +1

    Kunoso ku mzimba ndife okwiya kwambiri

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Місяць тому +1

    Sindinu nokha akuntchewu ai even boma lakhotakota ndife okwita big pafupi ziko lose nyani chakwela mbuzi akupha

  • @misoMoyo
    @misoMoyo Місяць тому

    Sindikuona chifukwa chopangidwira remove nkhani aliense akuona yekha Mene zinaendera Kodi chilungamo mukufuna chotani kuchita kuoneka zokha kuti anamupha mukufunanso chani Chakwera ngoipa anatiphera mngoni wathu Rip skc

  • @Patricklichakala
    @Patricklichakala Місяць тому +3

    Thanksyou big

  • @MarcosDjussa
    @MarcosDjussa Місяць тому

    Zoonad brother umakwana

  • @JosephChikabadwa
    @JosephChikabadwa Місяць тому +1

    Ngakhale Mulungu Kumwambako akuwona Lingatalike bwanji Tsiku Lina Oyipayo Adzagonja Ndithu Mulungu Wathu Ndiwam'kulu Ali ndi NTHAWI YAKEEE AYANKHA M'mapemphero Athu

  • @LinesiKanzota-fw7sj
    @LinesiKanzota-fw7sj Місяць тому +1

    Zowonadi ndi zowawadi chakwera ndi Muthu oyipa

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Місяць тому

    Well spoken my brother ❤❤❤

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb Місяць тому +1

    Chilungamo chimawawa

  • @ElizabethMajiga
    @ElizabethMajiga Місяць тому

    Ndimwana yemwe akuziwa kuti chakwela anampha VP wake basi

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Місяць тому

    Zoona big palibenso munthu oganiza bwino angazavotere Chikangawa mcp anthu panopa ndiokwiya

  • @EdwinHowardmkandawire
    @EdwinHowardmkandawire Місяць тому

    Inuyo chikhala mmaziwa kusaka ndege munkalekelanji kupita kusaka ndege a kapolo a anthu

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 Місяць тому +1

    Ukuteta yayi àuze zowona

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Місяць тому +1

    Ndipo live zoona zake tikuziwa bwino lomwe

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Місяць тому +1

    Zowona sikunama ai mcp ndi akupha anthu zisiru za mcp mafiti

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 Місяць тому +1

    Usawope muphwanga chilungamo chake nchakuti chilima anachita kupha a mcp ndichakwera

  • @EdwinHowardmkandawire
    @EdwinHowardmkandawire Місяць тому

    Fotseki chikwera sangasowe ntendele ndipo mutaya nthawi

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Місяць тому

    Tiphe zinyau zinayi kuti tibwenze zomwe chipani cha nyau chimachita.

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i Місяць тому +4

    Mwakhwana brother uko ndiko kukamba

  • @LilianMbaisa
    @LilianMbaisa Місяць тому +1

    Ndipo asabweredi

  • @TimexKaufa
    @TimexKaufa 27 днів тому

    Chilima adakwera mundenge ndi dzigawenga ndi chifukwa a mcp adakana kukweranao

  • @FrankSimfukwe-w1s
    @FrankSimfukwe-w1s Місяць тому

    Ife tikudziwa bwino kt anapha chilima

  • @FrankAdonis-zl6qc
    @FrankAdonis-zl6qc Місяць тому +1

    Ndukugwirizana nazo mbale zoonadi zimenezo mcp chipani chongokhalira kupha

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Місяць тому +2

    Fire

  • @user-ld8gb9xm7v
    @user-ld8gb9xm7v Місяць тому +1

    Thanks brother

  • @MaritaBanda-p4z
    @MaritaBanda-p4z Місяць тому

    amenewa akufunika azasinjidwe kumene komas kunena zona palibe wa mcp angapite ku ntcheu azikalakhula mbwelera

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe Місяць тому +1

    Palibe zandale apa Koma choonadi

  • @isaaczuze
    @isaaczuze Місяць тому

    Chakwera ndi munthu yemwe anapha chilima ....kuyipa mtima

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt Місяць тому

    Ulemu waanu brother. Osawanyengelela a MCP ndi makape opanda ntchito.

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Місяць тому +1

    Lero mutenthedwa ndi message yoti inaperekedwa kale kale mukanakhala ozindikila a MCP bwenzi siku lomwe uthengawu inaperekedwa mutaumva

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 Місяць тому

    Koma olo zitalowa ndale palibe vuto chifukwa anthu adafawa ndi andale ndie sindikuona vuto

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Місяць тому

    Komanso ndege inagwera poyeratu eehh

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Місяць тому

    Zaphabvu brother

  • @Marymahendra
    @Marymahendra Місяць тому

    That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .

  • @chipiesato-ut7hx
    @chipiesato-ut7hx Місяць тому

    Osaopa osatopa osafooka mcp yakupha ndizoona

  • @user-ec4jo9cu4d
    @user-ec4jo9cu4d Місяць тому +1

    Izi nde zoona ine okhara mchewa km imfa iyi yokha idandipweteka😭😭😭😭💔💔💔

    • @spargomw
      @spargomw Місяць тому

      😭😭😭😭😭😭😭

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d Місяць тому +1

    Zowonadi brother

  • @AndrewMagombo
    @AndrewMagombo Місяць тому +1

    Zoona anthu a mcp okumpha

  • @AlexPhiri-in1re
    @AlexPhiri-in1re Місяць тому

    Zoona bro

  • @moseskapelekeza8849
    @moseskapelekeza8849 Місяць тому +2

    Kodi muli joz

  • @ELLENKANJERE
    @ELLENKANJERE Місяць тому

    Zimawawa kwambiri ighowa ngati anali amai ake or achimwene mhu akhoza kumva motani akaona muthu akangwa pamseu anthu mosachendwa akufika pamalo ngati anali pafupi koma mmmm za chisoni

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko Місяць тому

    Mudzayese ngat inuso elazi mudzayipomde

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 Місяць тому

    This is the truth

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому

    Auzeni chilungamo afitiwo

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Місяць тому +1

    Asakuopyeze mchimwene auzeni chilungamo

  • @CorneliusSande
    @CorneliusSande Місяць тому

    Eeeee koma Mulungu yekha adzamenya nkhondo

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Місяць тому

    Chizaone chipande powomola