BON KALINDO LERO PA 03 FEBRUARY WAULURA IZI, KOMA UYU ALIBE KUSUNGA CHINSISI MPAKA APA? TAMVANI IZI

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 8 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 69

  • @tricknkhatah
    @tricknkhatah 6 днів тому +2

    Mwana woooooPsyaaaaaaa kwambiri... The DC..God bless u

  • @fumbanikumwenda9892
    @fumbanikumwenda9892 6 днів тому +5

    Let's Malawian give chance mnyamata mzathu Denis Mahata. The political philosophy

  • @alicksonsiriya8183
    @alicksonsiriya8183 4 дні тому +1

    He is telling the truth, Malawian people are suffering. I assume they are the worst in SADC

  • @ChrispineMuzungu-l8h
    @ChrispineMuzungu-l8h 6 днів тому +4

    The DC🎉🎉🎉

  • @abgi.doctor.august
    @abgi.doctor.august 5 днів тому

    The DC Boooon Kalindo president wa aphawi Malawi 🔥🔥🔥🥳🥳🥳🥳🎉🥳🎉❤❤❤❤

  • @SignalaRajabu
    @SignalaRajabu 5 днів тому

    Thanks u bon kalindo

  • @ChimwemweMathyola-q7w
    @ChimwemweMathyola-q7w 5 днів тому +1

    Kuziko lamalawi ngati kuli muthu Ozawa Maputo acanthu ndi bon kalindo bas

  • @alicksonsiriya8183
    @alicksonsiriya8183 4 дні тому +1

    Chakwera must gracefully step down he has failed the people of Malawi

  • @JunnaidahSandram
    @JunnaidahSandram 5 днів тому

    Anthu akubaa a MC P .

  • @Michaelaliemapira
    @Michaelaliemapira 6 днів тому +2

    Mutha kwakumbutsaso
    Nkhani ya resignation ljah. Kutheka aniwara

  • @ThomasMlowoka
    @ThomasMlowoka 6 днів тому +1

    The DC 🔥🔥
    More fire

  • @Michaelaliemapira
    @Michaelaliemapira 6 днів тому +2

    Azoooonad mr kalindo

  • @Sithoboy-f8y
    @Sithoboy-f8y 6 днів тому +1

    Thank mr born kalindo

  • @LysonMkomadzinja
    @LysonMkomadzinja 6 днів тому +2

    MCP olo itapanga chani ife sitikuivotela yatinyasa kwambili

  • @WhiteTenguramembeHassan
    @WhiteTenguramembeHassan 6 днів тому

    The DC Mr president for poor people l like u

  • @nkhomahhappy2826
    @nkhomahhappy2826 5 днів тому

    Very true Mr Kalindo

  • @limbanibello1985
    @limbanibello1985 5 днів тому

    Pa ground sipalibwino chilichonse Chakwera magaye.

  • @GiftBanda-s6c
    @GiftBanda-s6c 5 днів тому

    Kumawakwapula kumene The DC osawanyengerera😂😂😂

  • @BernardKalongah
    @BernardKalongah 5 днів тому

    Mr born kalindo ,awa mukut avitumbiko Mwenda akupanga izi chifukwa chot zisankho zayandikir ,paka 4yrs yapitayo ankapanga chat,

  • @BistonMacheso
    @BistonMacheso 5 днів тому +1

    😂😂😂😂😂😂😂 chalakwe zamvuta kwambiri ndipo the DC mulungu azikutetezani kwambiri ifeyo sitikhara chete pokha pokha APM alowe boma basi 1 samueli 16:1:10 yesaya 54:17

  • @miovekanola2780
    @miovekanola2780 5 днів тому

    DC we love yu

  • @SumailahWisck
    @SumailahWisck 5 днів тому

    Ipanseni moto 🔥🔥🔥

  • @ShukulaniMthipera
    @ShukulaniMthipera 5 днів тому

    The DC umatha

  • @Ayanali-cr4vy
    @Ayanali-cr4vy 6 днів тому +2

    Ummmmmmmmmmmmm page ya Bakili TV sinapangidwe hack
    UTM ndiyakubad Chilima sanali wabwino olo pang'ono. Zonsezi ndi zoonad
    Atupele Muluzi my Vote

  • @KAFEENKHATA
    @KAFEENKHATA 5 днів тому

    osaopa the Dc 🔥🔥

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni 5 днів тому

    🙏🙏🙏🙏

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c 5 днів тому

    The Dc 🎉🎉🎉🎉

  • @FundoGama-c9y
    @FundoGama-c9y 6 днів тому +2

    Unasowa kalindo ndatchera khutu kt ndinvesere zomwe wanyamuka ❤❤❤❤

  • @BrianJafali-i2j
    @BrianJafali-i2j 6 днів тому +1

    Bakili muluzi TV hacked guys

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda 5 днів тому

    Kalindo mukumenya nkhondo kwa osaukafe..No more mcp in 2025

  • @franktsoka
    @franktsoka 5 днів тому

    The DC ❤

  • @mauricesande9661
    @mauricesande9661 5 днів тому

  • @MarcusLucius-j7d
    @MarcusLucius-j7d 5 днів тому

    Kodi a DC UTM simuitchula bwanji?
    Tiziti aimuuidziwa😂😢😅

  • @alicksonsiriya8183
    @alicksonsiriya8183 4 дні тому +1

    Chakwera is the worst president Malawi has seen. Munakwera stikani

  • @AyamiMustafa
    @AyamiMustafa 5 днів тому

    DC zowona

  • @IsabelLuka-i8f
    @IsabelLuka-i8f 5 днів тому

    Tinakusowanidi bige masiku a menewa bola apa mtima wakhazikika,ofunika anduna azaumoyo ayendere kuno kunancholi Blantyre,chipatala chakwa komka chomwe anachitsekula kumene chija madotolo akumabwera mochedwa kuntchito npaka 9 o'clock asanabwere anthu kumalandira thandizo mochedwa ayi sizowona,zikumatiwawa ngati ifeyo amasikini,sizowona mutiyankhulire bwana DC kwa anduna azaumoyowo nkhaniyi

  • @LufingoMulungu-z7u
    @LufingoMulungu-z7u 2 дні тому

    Mwana wowopsa kwambiri

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 5 днів тому

    Kuno Kulilongwe kwawo kwachakwera tikumaphikila mafuta odzola akomba. Mafuta ophikila olo amukakondomu adhula.

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 5 днів тому

    Ndipo ku Tanzania nkotukukaditu

  • @fumbanikumwenda9892
    @fumbanikumwenda9892 6 днів тому

    Ine ndiye ndili pa mbuyo pa Denis mahata

  • @LenadiMthandi
    @LenadiMthandi 6 днів тому

    The DC ndinadabwa kwa two days kut simukutulusa odio takunyadiran kuti mwatifikilaso the DC mulungu akuonjezelen mphavu kwambiri

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 6 днів тому

    The DC aaa aganidza dzokhala ngati bakili muluzi TV tsonotu dzonena zake timadziziwa ndimayetsa amati wabodzo lelo nde akanena iwowo nde anthu adzikhulupila komadi chitseko chapani dzedi a MCP

  • @giftSitima
    @giftSitima 6 днів тому

    Za chimangazo olo kubalaka anthu akupulumukira ku andiamo kumene anthu akugula chimanga chamankhwala choyenera kuti chikazalidwe Malawi waola uyu ambuye atithandize

  • @LomossiSichiimbauavivafrelimo
    @LomossiSichiimbauavivafrelimo 6 днів тому

    Kodi umasintha chiyani ukamatele bwaji iwe.ossakoza😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @EnockKamoto-yu2ct
    @EnockKamoto-yu2ct 6 днів тому

    Ulemuwako the DC

  • @KelvinDickson-c1x
    @KelvinDickson-c1x 6 днів тому

    Yah ine ndi mzika ya kwa manjeko ndipo izo zikuchitika chimanga cha mbeu chapent ya green ndichomwe chikusukidwa kupangidea nsima zilikuno Kwa manje

  • @LeviChakwira
    @LeviChakwira 5 днів тому

    Ijayi si bakili muluzi TV. Fake tinayiona kale

  • @ChisomoYosefe
    @ChisomoYosefe 6 днів тому

    kaye boma la nsanje athu akuvutika kwambir chakudya kulibe anthu akusowa pogona Malawi dziko lomvetsa chisoni

  • @user-to5we9eq4z
    @user-to5we9eq4z 6 днів тому

    Tiyankhuleni boss

  • @ElizabethMulinde
    @ElizabethMulinde 6 днів тому

    Inetu ndimadziwa kut imene ija sibakili muluzi tv ayi koma alibe mtendere

  • @MussWalasi
    @MussWalasi 6 днів тому

    ❤❤❤❤❤🎉🎉🎉

  • @PiassDayit
    @PiassDayit 6 днів тому

    tiyeni tingomuza Kut achoke Mesa tikuva kuwawa ndifeyo

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 5 днів тому

    Chakwera masiku ako ndiowerengeka

  • @AlicePondani
    @AlicePondani 6 днів тому +1

    Ife timaziwa kuti wa bakili sanganyonze UTM

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu 6 днів тому

    ❤❤❤❤

  • @WarriorKB-l3i
    @WarriorKB-l3i 6 днів тому

    Dzulo ndanena kuti uyuyu si wa bakili muluzi, page iyiyi si yake chifukwa wa bakili muluzi sanganene zimene zija ai, DC ndi zache weni×2 wa bakili muluzi tv nduyu akunenanso kuti si wa bakili muluzi anthu ndi propaganda ndipo ndizoona chifukwa iwowo amalankhulana dairy ndipo awuzana kuti siye koma anyamata a mcp inenso ndinadziwa kuti ndi propaganda koma ojiya amenewo apezeka chifukwa naenso wa BM tv anafa kwambiri. Mcp kudzangobela mavoti ndidzakhala nawo mmodzi oyambitsa dziwawa mmalawi muno chifukwa ndikudziwa kuti sidzawina nde wina adzanene kuti cikangawa wawina kunena kwa DC kudzacitika zoti cikangawa sanadziwone cibadwileni yelekezani muone.

  • @austinvincent773
    @austinvincent773 6 днів тому

    Ilili ndi bodza kalindo page sinapangdwe hack ndi iyeyo osanamiza anthu apa

  • @Wordofprophets247
    @Wordofprophets247 6 днів тому

    Wanvako za Bakili TV

  • @MajiduMakiyi
    @MajiduMakiyi 6 днів тому

    Iweyo ndi azko ndi amene anapangsa

  • @BenardKasinje
    @BenardKasinje 6 днів тому

    Zaziiiiiiiiiiiii

  • @AnnesiChiwere
    @AnnesiChiwere 6 днів тому

    ❤❤❤❤❤