Tough time do not last but tough people do last , one day we gonna be happy. We still and we will always love you Mr chilima may Allah guide you in paradise
The song is way too old but because it was a hidden to us that this song will one day be a emergency. Isn't easy to accept that the man is no more 😢😢😢😢😢😢
Mark my words...Dziko lakumidima lipanga chothekela kupha onse omwe ali ndi maso mphenya ulamulila dziko la Malawi kufikila Anyamata a illuminate mosogodzedwa ndi prophet wao atalitenga Dziko...If You know you know
I feel bad like i am the one of Malawi people but i am Zambia anyway only God knows Rip 😭😭😭😭😭😭😭😭 we are one people namvera kuyipa😭😭😭😭😭
Even here in sensheke,people are in sombre mood coz of this.Am a malawian.
Imagine am a Malawian, the way I am feeling, this is too much, Chilima has gone just like that eish😭😭😭😭😭😭
These are the times that will tell you that we are one. This is painful
Misozi sikutha mmaso mwanga😭😭😭😭😭..... tsoka iwe ozetsa chokhumudwitsa hi😭💔💔💔
this song makes multiple streams of tears
It wl take a lot of time and years to come to myself,this painful death wl be in our hearts forever,,May His Soul Rest in internal power
Imfa yowawa kwambiri misozi yosaxhoka mmaso mwanga ndamulira ngati m,bale wanga 😢😢😢😢😢
Your speach was always about wishing better for the Malawians...
Rest well our HR. Dr SKS💔💔💔🕊️🕊️🕯️🕯️🕯️
Ngati maloto kt chilima kulibe😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢
😭😭😭😭😭💔💔💔💔
Tough time do not last but tough people do last , one day we gonna be happy. We still and we will always love you Mr chilima may Allah guide you in paradise
It reminds me of Dr Kwame Mkuruma he survived four assassin's may the soul of SKC rest in peace
Mzimu waChilima ndi onse omwe adali mundege yomwe yatenga abale athu enanso- iuse mumtendere ❤
Wafa infa yowawitsa kwambiri 😭😭. Rest in peace VP, Shanil, Daniel and six others 😭😭😭😭
Ine ndudikira ya Nkasa
I love the song
Tizatonthola Koma mochedwa,,,😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
😭💔😭😭😭 dziko lodzadza ndi anthu oipa
Thanks Evance meleka and let tell all Malawians that 2025 to be united and choose the best leaders
Kma Chilima akanadziwa kut anthu ambiri timayang'anira pa iye sakanatithawa chonchi😭😭😭😭
Mhuuuuuuuuu sk puma mtendele
Mene anaimba nyimboyi Evance ngati kuti ankadziwa zizachitike💔😓
Abale this is so touching 😢😢
A very beautiful tribute ever.. Rip Dr SKC till we meet in the Glory of God 😭
Anthu talira enough is enough mulungu akadzuka papando wake wachiyerunzo iwe amene ukulilitsa anthu samala he's supreme God magastrate, superlative
Evance meleka nice voice
Indeed 😢he was the great pillar of Malawi but wicked people killed him 😢when are we going to be free sure 😢why we don't want development sure 😢
Sinaswekepo mtima ngati ifa iyi abale ndalephera kuchinga misozi yanga😢 ndamulilira chilima ndi mtima wanga onse
Imfa yawawa iyi, munthu kufa mowawa chochi😭😭😭😭 Ambuye akuona zonsezi😭😭
May God grant him internal peace in his sleep, heartbreaking 💔 😢 . Tonse tidzapita komweko ndithu
He was our hope I it wl take time to forget
I can't stop crying Lord! I have no strength anymore! Heal my country Lord 💔😭
Rest in peace Mr Chilima ndi anthu onse mwamwalilira limodzi 😢
No more chilima ngt boza😢
😭😭😭😭😭💔💔💔💔
😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔 my president,I feel like am in a continuous dream eish, we live in a wicked world.
SKC you will always be remembered
Tizazindikira bwino pasogolo
RIP SKC🙏🙏😭😭😭😭💔💔💔
Ambuye mudziwa ndinu😭😭😭😭😭
Kodi oimbawa osang{sonkhana pamodzi ndikuimbila limodzi bwanji zikhale ya 2 hours timvela
koma mesa nyimboi ndiyakale
For sure tizazindikiladi bwino pa tsogolo 😭😭😭😭
Km2 meleka nyimboyi waimba bho penaso amwene mumatiimilira ulemu wani😮😮😮😮
Zomvesa chisoni
If am dreaming, please wake me up from this terrible dream😢💔😭
The song is way too old but because it was a hidden to us that this song will one day be a emergency. Isn't easy to accept that the man is no more 😢😢😢😢😢😢
Ambuye akuona zonse😭😭
Big up Evance Meleka....RIP Bwana Chilima
Rest in Peace Dr Chilima.. The Catholic Church will forever miss you.. Kumwamba ko Mulungu akuona zonse.
Amen mzimu wanu uusa mtendele achilima ndi onse amene anatisiya
Big up mwana wa meleka
Only God knows 💔
Mulungu mudzilemekeze nokha paifa ya klaus saulos chilima amene waika maganizo ndikuthandizira kuti lero vice president amwalire mulungu muwakathe ndikhwiyo wanu zimu wake uuse mumtendere zoona wafera mbendera yadziko lanthanu kutimenyera mtendere koma osaupeza❤ chauta achita koposa
Amen😭😭😭
Very sorry Malawi anzathu mulibemwai chilima anali kufuna kupulumusa ziko 😭😭💔💔
Wafera chilungamo ndikunvesesa ndikufewa ntimawa kwake ndpo masiku ano chilungamo tizichiwopa ndithu
Wachilungamo sakondedwa
@@user-fq7gb8gm3qeeh izo nde ndi zoona
Ndimaona ngati mudzandiuza kuti boza ali moyo😢😢😢
😭😭😭😭😭 Zoonadi wafera mbendera ya Malawi chilima eish
Ya apa wayifera
I had,we had the hope........Chilima you have left us in DESPAIR....R.I.P
Be comforted. Have Faith in God! He never fails 😮
😭😭😭😭😭
Pita mukapume mumtendele
This death has dealt us a heavy blow
I love you saulos clous chilima
😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 kufela dziko ndipo wandiwawa ngati ndiwe mubale wanga chilima mayo mayo ine imfa kuwawa mweee
Nyimboyi ndiyakaletu
Ndizoonadi tidzanena nthano
I still remember this political rally, It was very emotional. The man is no more 😭😭😭💔 life is unpredictable
Nyimbo iyiy ndinaivelako pena ikumakhala ngat ikalotedzela ifa ya Tate wathu wa utm 😭😭😭😭😭😭😭
Mwapha chiyembekezo cha AMALAWI 😭😭😭😭😭😭😭😭
Mulungu akudziwa zonse
Ngati ndikulota, ndizidzimuseni Ambuye💔😭
Ndipo sitikuopa😢
Amen RIP Chilima will never forget only God knows
INNA LILLAH WAINA ILAIHI RAJIUNA 😢😢😢😢😢
Eish chilima wapitadi osadwa koma ndipemphero langa kwa mulungu kuti achitepo kanthu kwa onse okhudzidwa za imfai
U had version words... Rest well Dr SKC 😭 the president
Tidzakhalabe pambuyo pa utm osafooka
😭😭😭😭😭 koma imfaa iyii yopweteka
Misodzi mumaso mwanga to my president😢😢😭😭
Mr Meleka mwandiimilira ndithu
Inna lillah waina ilayih rajiuna
Eish mr chakwera muliko mulungu akuzindikilitseni mwina muli mu nyengo ya marko 8 ves 32 muzazindikira choonadi ndipo choonadi chizakumasulani
Ndilire bwanji ine 😢😢
Only God knows muwuse mutendele Dr chilima
So sad 😭rest well our vice president Mr Chilima, oh my God 😭😭😭😭😭😭😭
This song make cry again
🙏 may God continue be with Chilima🙏😭😭
Big up bro 💪
Ndipondi mafelandi ndembela Dr Chilima
Hallelujah God pls may these people rest in peace 😭😭😭😭
😢😢 rest well my vice president ndale sizikomanso
Am real African and I love all African s people sorry for all people.
Nice song, poor vedio camera
ndi ya Shammah vocals nyimboyi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Chifunga a day will come for you
Tikusowani achilima
nice song kutidekhetsa
Wandilitsa Evence😭😭😭😭
Oyenda ndi lupanga azaphedwanso ndi lupanga muyeso omwe umuyesa nawo nzako omwewo uzayesedwa nawo galu wankota sakandira pachabe
Mmmmm koma oyipayo anakamvera nyimboyi 😢,😭
I wish there was a second chance for him to leave
Leave ????? ?
Live
Zengerezu anayenda kwawu kwawuu
Oimba akumalawi kumagoimba ma tribute mmalo mothandidza amalawi Kut tinkhale pa mtendere ayi mmmmm
Ambuye amsunge iye ndi onse Ali mmanda
😂😂😂😂 tidzalila mpaka kale Dr chilima munali mdalitso ku dziko la malawi
Zosayenda 😢😢😢
Inu nyimbo ya kale iyi
Chakwera afune asafune 2025 ma vote sazawina ndipo ngati azawina akanifunse or pompano anifunse
Mark my words...Dziko lakumidima lipanga chothekela kupha onse omwe ali ndi maso mphenya ulamulila dziko la Malawi kufikila Anyamata a illuminate mosogodzedwa ndi prophet wao atalitenga Dziko...If You know you know