Cruise 5 with Moses Mwalabu Former Street Kid Part 2
Вставка
- Опубліковано 27 вер 2024
- A continuation of a chat with Moses Mwalabu, a former street child but now Executive Director at One Step Foundation, an organisation which he founded to help street connected children. In this episode he talks about his plans to grow his organisation and expand to other cities in Malawi.
This is very inspiring.
The message will remain relevant till the end of time.
Thus very true during his time I pursued my diploma in youth development with 70 k the whole duration of 3 three years thus from 2015 to 2018 I graduated....
Thank you bwana Mwalabu mumakwana stay blessed
😅
Munthu akapempha nyimbo ziziyikidwa
Wina kumalephera zinthu with resources intact....God bless these guys.
Thank God my brother, we are proud to be Mwalabu's and zikomo pokamba chilungamo chokhachoka mulungu adzikudalitsa. Momwe ndimaidikila part 2 😂😂 make up to part 5 ❤❤
But this person is honest
Keep the good work Mr Mwalabu
When time is right indeed God will make it happen
This man wakumana nazodi yes and wapilira,koma anthu akukumana Nd zokhoma
Enafe takula momvutika koma uyuyu ndiye wakula mozuzikadi ndipo mwa munthu uyu ndaphunzira zambiri
Komaso mulungu analinaye cholinga
This man Joabu is full of wisdom 🎉🎉🎉
Live longer Brother Moses Michael Mwalabu Chimbewa
It's so emotional, I have learned a lot
Nuff respect !
Dolo kwambiri
Inspiring
God never fails
Nkhan za pat 2 zachinam'balala
Nkhaniyi ndi yayitali. Bola wamva.
Akumanga
Ndimaonela ma program onse km iyiyi ndaphuzila zambiri
Zandivuta kupanga comment 😒
Zowona zake zimachitikadi yaaa
Eya ndi yomwe timadikira
Khani yabwno ndinthu koma ine ndingakupeze bwanji.
😭
😢😢😢😢
Wow, delay is not a denial
Uyu ammanga uyu 😂😂
Akamumange chifukwa akulankhula chilungamo
Mmmmmm this guy is too much, he is doing alot
Koma mkulu uyu anava kuwawa
I will vote for you uzaimeso pa u president wa dziko la Malawi. Long live Moses!
finally here is part 2. Thanks Mr Chakhaza for implementing it.
Finally kudikila kutopa
Eeee Koma palinkhani apa😂
God bless you
Kkkkkk koma joab nde ukuyanganaakkkkkkkk
May good Lord bless you Mr Moses
This guy has really inspired me,,
Ati iwe taima kkkkkkkkk koma a Joab
i have learnt a lot in this God bless Mr Moses Mwalabu
I envy ur perseverance😢U had all the reasons to give up on education. Ur full of generational wisdom. God has a purpose for your life. God bless you.
I have liked humble beginning of this guy. I believe, God will do more for him cos of his honesty
ochenjera mkuluyu