ANG'ALULA MOSAIPA LERO PA 10 July 2024

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 7 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 31

  • @TisopeChagala
    @TisopeChagala 2 місяці тому +7

    Chawezi asazabwerenso

  • @kennedybanda
    @kennedybanda 2 місяці тому +2

    Mosatayitsana nthawi vision 2063 ndibodza lamkunkhuniza ndithu.
    Malawi wachulukitsa usatana.

  • @lysonmhone5425
    @lysonmhone5425 2 місяці тому +5

    Kuswa kuswa
    Kufotokoza mmene ziliri pa ground
    Mavuto anayala mphasa dzikoli
    90% ndi anthu osauka

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 2 місяці тому +1

    Yes chawezi asazabweleso apangisa kuti ine ndisamavele program iyi

  • @hopembendela
    @hopembendela 2 місяці тому +1

    Malawi we have weak politics if the politicians stop stealing the money malawi will be a better country again

  • @HamzaShaff-vo3ci
    @HamzaShaff-vo3ci 2 місяці тому +1

    Ngat mukufuna kt tizikupangan for4 mumuchose chawez

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 2 місяці тому +1

    Atsongoleri anthu onse ationongera Mother Malawi......Very sad Nation😢😢😢

  • @MarvGerald
    @MarvGerald 2 місяці тому +1

    Program imenei lelo ikumveka bwino kwambiri.
    Tikupempha chonde Chawezi uja asamapezeke kumibawako ameneuja ndiwa Mcp

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki 2 місяці тому

    Malawi is not a country it's a farm for politicians!

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI 2 місяці тому +4

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 2 місяці тому

    Kabambe anali m'boma kale bwanji sanapange zimene akunenazi

  • @ChembeWaimba
    @ChembeWaimba 2 місяці тому

    Kuyankhura it's simple kungonena mavuto sungatchule mavuto amene tadusamo, wabodza iwe kagwere uko, ine ndiye sunganinamize chilungamo ndikuchidziwa, cadet program muziwonera nokha.

  • @jimmymalanda
    @jimmymalanda 2 місяці тому

    Very good analysis the question is , what have you done at your level to help the situation apart from making this good analysis?

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 2 місяці тому

    Akalindo aja kungomangidwa ma million akumalowa ku ACC kwawo, ife kutimanga basitu tikafela konko

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 2 місяці тому

    A Victor mumalongosola bwino, vuto lakula kwambiri zaka 4 zapitazi chifukwa cha Utsogoleri wa Chakwera, sakudziwa chilichonse.

  • @YoungScott-p7e
    @YoungScott-p7e 2 місяці тому +2

    Zakhala bwino kuti munthu oipa uja chawezi Banda palibepo

  • @rexnyalugwe4910
    @rexnyalugwe4910 2 місяці тому

    Queen Elizabeth hospital mwati unamangidwa liti?

  • @JosephNgona-f9v
    @JosephNgona-f9v 2 місяці тому

    Ai dzana 60 .chomwe tapanga bro kuba kupha ndi maulendo opita ku junja pa passport kulibe kkkkk

  • @fredgabrielnyangulu
    @fredgabrielnyangulu 2 місяці тому

    Vuto lathu ife a Malawi vision yeni yeni tilibe chomwe timakhala nacho ndi kusintha zipani basi ndipo akabwera zomwe amadziwa ndi kuba . Chomwe chimandinvetsa chisoni munthu walembedwa ntchito ndi amphawi Ndalama zomwe akulandira ndi misonkho ya a Malawi more over amalandira ndalama zambiri ndie ndimadabwa kuti akamapita ku misonkhano ati akufuna allowance za chani ndalama zomwe timawalipira ndi zomwe amayenera kuti azigwiritsa ntchito ndipo ma Civol servant ndi omwe amawononga misonkho yathu chifukwa munthu akulandira ma million koma akuti misonkhano chili chonse cha ndalama za amphawi

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 2 місяці тому +1

    Kadziko kamalawika mwati kadziko or kamunda?kadziko komvesa chisoni kwambili ndiye kanakakhala kadziko kakakulu akanapanga nako bwanji ngat tikukalephera kukatukula pano?muli nsanje kwambili mujadziko kamalawi,chikondi mulibe.kadziko komvesa chisoni kakang'ono koma zochitika Eeeeh 👹👹👹.tianthu takenso timaoneka ngat tozindikila koma ziro ku 10.mumakhala ngat muli anthu anzeru koma heeee!!zero ku 10.tanzania and zambia ndikaiona kuisilira ngat ndikakhaleko ndisamuke kumalawi.nzimai akuchita kuitukula Tanzania kuona ma bridge amakono.sitima zapantunda koma kumalawi vuto kumangoyang'anana basi kuipidwa ndikuphana popanda kanthu.andale athu malo mopitisa chitukuko amalimbana ndimunthu.malo momanga misewu or ti mabridge tamitsinje tomwetu kulephera ngat boma kukonza ma bridge a standard.malawi mulibe mitsinje yaikulu ikulu yoti mutha kukhala ma bridge akulu akulu.maiko anzathu akupanga zimabilidge zazitali 20 to 50 kilometer koma ife ka bridge ka 1 kilimeter matatalazi kut kamangidwe.azitsogoleli athu ndalama amakhalangati ndizawo akuchosa thumba mwawo osati zathu.look pano misewu yambili ingoikidwa pa central region tinganene zoti zitukuko zambili zangodzadzana pakati komanso ti madevelopment akuphangilato tosekesa kwambili.ndikumanyadila tikupanga chitukuko zopusa basi.tamayendani maiko ena.bvutonso losankha azitsogoleri okut sanayendewa ndizimenezi timakangowa votera azikapeza mabusiness awo.akamadzasiya zitalemera ife kutisiya manja lende iwo ndibanja lawo atalemera.

  • @JasonMailos
    @JasonMailos 2 місяці тому +1

    😭😭😭 Malawi wanga

  • @LETUSCHIPHUPHU
    @LETUSCHIPHUPHU 2 місяці тому

    Yes vutodi ndy atsogoleli😢

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica 2 місяці тому

    Tsopano malamulo amati musanachotse logo yaeni ake anapanga video yi khaya ndi times, zodiak olo mibawa kuti musadzabvutane nawo.

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica 2 місяці тому

    60 partys shaaah?

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 2 місяці тому

    Chakwela wapha Chilima

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p 2 місяці тому +1

    Where are SKC reforms? Why is Malawi being held back?

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi 2 місяці тому

    Ufulu wotilamulira
    Osati
    Wozilamulira,
    Akulamula dziko la Malawi ndi ndani?
    Akulamula ndi America ndi Britain
    Osamanena kuti ufulu wozilamulira
    Almost more than 90% ya boma or dziko la Malawi zikuchokera
    Or kuuzidwa ndi ma west.

  • @ChisomoMandawala
    @ChisomoMandawala 2 місяці тому

    Tiyenawoni ma comrade

  • @goodwilljeza8419
    @goodwilljeza8419 2 місяці тому +1

    Man subwoofer

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 2 місяці тому

    😂😂😂 60 years for nothing shame malawi

  • @wakisawinga2744
    @wakisawinga2744 2 місяці тому +1

    Very sad nation 😭😔