This is what Malawians were waiting to hear from you. You made a right decision. Thumbs up to you all. We are fully supporting you, and we shall be behind you forever.
This is practical and very positive politics. Let's follow this path. I never new that in UTM there are some pipo who think like this. There is so much unnecessary noise which pipo think is politics but nope. God bless you.
Ndinu mburi zedi mulipachangu koma choononga komaso kachipani kanu kakuntha nanga ku d p p mulibepo Udani a a a si wa UTM iwe ukufuna kuononga mpunga WA UTM
Samamva asiye adzaziona ayiwala zimene adamupangira mademo APM azabwezera zonse zija mmmn they have to learn through mistake with tose alayasi km UTM bwanji mwayamba kuti gwesa phwayi
Koma a mayi inu mutizuza kwambiri ndipo you have to learn through mistake muyambilaso tose alayasi tatopa ndi kuliratu ife Chaka chino Chigoliyati chinalephela khondo kwa David nde inu bwanji a UTM km DPP yanuyo 2020 munayipangila mademo nde mwayiwala km mukazi wa Loti adayang'ana m'mbuyo ndikusanduka chulu
Osamakakamiza aliyense ali ndi ufulu ndi chisakho chake pokavota. Panopo kuigwetsa MCP nkovuta aaaa nde gwirizanowo ndi dpp?? Mayi mukunama inu kuyakhula konseko ndi mpando musatinamizepo apa.
Inenso ndine wa pa kanthawi ndithu MCP ndayiwona ndipo ndimaidziwa. Kungoti zangovuta kt zipani zinazi ndizazing'ono nchifukwa chake people will be FORCED to make an aliance with DPP. Koma tikawunika BWINOBWINO, DPP ndi MCP palibe kusiyana. Njauju mkulu wa ACB dafa ngati simunthu mpaka pano milandu idangozizira. UTM tsaopano payokha itha/ ndi AFORD, zitha kuchita bwino ndithu chifukwa imfa ya SKC idachita CAMPAIGN YAMPHAMVU. Makamaka ku chigawo cha ku mpoto. Kubwelera ku DPP itakhala LAST OPTION, yes mwachonchi mowawidwa mtima. Mayi ndakumvani BWINO ndithu, ndipo sindikukutsutsani kwambiri, koma DPP, ikhale last option.
Paja DPP ndi kuchimake kwa Propaganda😂😂 Pepani a DPP the only new Malawi that as a nation we all expect is the coalition of UTM and AFORD period. We all all seek New parties in new Malawi to come. The MCP that Malawians have experienced this time NO majority can make such mistake to vote MCP again.
Mwaganiza mokhwima maganizo abale athu a utm kupanga mgwilizano ndi DPP komanso tili ndichikhulupiliro kuti zipani mwanenazo mosogozedwa ndi Ambuye komanso anthu kulilira dziko lamalawi pamene lafikapa liphulidwe pa moto osatira azipanizo sionse angakondwere koma ambuye achite kufuna kwake pempho a DPP zichepeseninso pa anzanuwo kondanani samaliranani khululukirananipangani umodzi ochokera pansi pa mtima may God bless you
Yes l gree with you Mai,koma ngati simungamve magnanimous a Maiyi ndiye kuti mulibe magnanimous ofuna kutumikila a Malawi koma kukhutisa mamba zanu osati kuombola aMalawi ku Bagamoyo,please paganism chtheka kugwilana manja kuombola Malawi ku mng"anjo ya moto,machine ngati achitila kuno ku south Africa kupanga boma la Malawi colution Government, osakonda anthu awo mwasiye choncho
Mai mawu anu ndi amphamvu ambuye awadalitse
Very true Madam, we need to have strong party for alliance
Zipani zonsenzi zili pansi pa DPP. so lingaliro labwino kubwerera Ku DPP
watching from Cape Town
Very true mandam ,ndazikonda kwambili bwerelani kwa amai anu basi tingwetse MCP ,
You have proven to have big brains than other men in UTM, you have our support
This is what Malawians were waiting to hear from you. You made a right decision. Thumbs up to you all. We are fully supporting you, and we shall be behind you forever.
Eishii koma apapa zikhala bwino bwanji ndipo zitero ndithu❤❤
Mau amphamvu Mai atigwira mtima Bambo wanu APM akulandilani ndi manja awiri sangalore kuti ana Ake asowe kopita iye qlipo
I totally agree with you
Komatu amai awa alankhula zomanga Malawi wasopano God bless you mama
Powerful massage madam and am looking forward for the mgwirizano that is coming viva 🇲🇼 🇲🇼 🇲🇼 viva DPP,,,, watching 👀 from Lusaka
Mau ogwila mtima kwambili 💙💙💙🔥🔥🔥
Mayi uyuyu amaganiza mwachungu ngati mwamuna 🎉❤❤❤❤❤❤❤
Mai mwayankhula za nzeru koopsya ndipo iiiiih sindikutha kukumvesesani kuti nzeru zinenezi bwanji inuyo
Good decision sitikufuna njara ku Malawi
Powerful message mama
You is best futures ❤❤ 100% that's one plan A not B ❤❤❤❤❤❤❤🎉
Good advice ,join together to remove the devil.plz.
Wake uppp UTM family, that's right decision madamm, let's forget about the past!!!
I totally agree with you madam ,,UTM must go back to its father house
Zoonadi ma tigwirizane NDI DPP,ATM,AFORD+UDF ......moto buuuuu
Ikugwetsani MCP sizamwana😂😂😂😂😂😂😂 chakwera motoooo komaso chakwera kuwina DPP yonse tidzaponyanso Yamanja alomwe kwao sitikuyesa
Dpp, UTM,Alford, and UDF chonde phalani ziko pamoto tikudalira inu
@@ivychithyoka1551 chakwera akupha Goliath ndi mwala umodzi 2025 gwirani yesu Adani muwaponde bwino achakwera ndikuthandizani kuponda achepa
Mai inuyo very true watching from LESOTHO ndipo ndi Mulungu amene wakunong'onezani kuti muyankhule mau amenewo
That's true Comrade there is no permanent political enemy in politics
UTM ndi DPP palibe udani if anything UTM yabadwa kuchokera ku DPP. Peter is cool ndiyemwe anamukonda SKC kuti ayambe ndale.
Chabwino ndakumvani nde tinene kuti UTM itsogole ngatidi Pali kumvanadi
If we want tizivutikabe let's VOTE for MCP
Mau mau,udani wampaka muyaya mundale mulibe Tiyeni kwaADad bola Ng'onazi tizitulutse 🔥🔥
MCP ndidzaida mpaka muyaya.
That's good Idea madam
Muli power speach inuyo mama🙏🙏💯💪
Powerful mama mwaganiza kuposa mwamuna ndakukondani🎉
Chakwera sakupuma bwino. Madam mumaganiza mokuya I agree and let's vote dpp utm afford udf, tigwilane manja.
Very Bravest speech Sister I salute you
Tiyeni tigwilizane ndi DPP, UDF plus Aford kungotero tagwesa
@@masterchitabwino898 ndipo chomwe chizachitike ndi zija amati 'Landslide victory', m'gwilizano omwe ungachepetsenso za kugawana mitundu. Nkhani yomwe akamba Mai wo. Atsogoleri omwe akukhuzidwa asakulirane mitima, agwilizane, azichepetse atiphule a Malawi mu nyengo yowawa ngati imeneyi..eesh!!!
Kwambili UTM mulungu akudalisen Ife tikufuna Malawi wa rendere osati Opana UTM thenks
Thenks utm popangangwilizano ndi dpp atiphera saulosi achoke fayaa
Mai kaliyati libikisani anthu ife sitifuna mcp
Good watching from Joburg
This is practical and very positive politics.
Let's follow this path. I never new that in UTM there are some pipo who think like this. There is so much unnecessary noise which pipo think is politics but nope.
God bless you.
Very amazing let's unit ❤ watching from Cape Town
Ichoke mcp please dpp my vote
That's good idea Ma, l salute you 💪💪 power to the people.
Thanks madam for the advice
❤❤❤❤ that's beautiful idea Mai kariat
We're with you madam
Well spoken madam boss 🙏🙏🙏
Patricia kaliat ndi makina paokha welcome back mom ur loved
UTM ngati ikufuna kuti omwe apha Chilima adzalipire akuyenera kupanga mgwirizano ndi chipani cha DPP kuti achotse MCP ndikufukula imfa ya Chakwera poyera koma ngati satero nkovuta DPP kudzagwira ntchitoyi pamene UTM imawanyoza pa kampeni
Chomwe wamanga Mulungu wina sangachiphwasule. M'gwilizano wa Shadow wina uliwonse omwe cholinga chake ndikugwetsa MCP, ndiri nanu pambuyo....
Bravo!!! UTM welcome to DPP
100% mai, UTM, DPP ndi AFORD gwirizanani mugwetse MCP ndi chakwera atitopetsa, mai wa nzeru kobasi.
Mphechepeche mwa njobvu sapitamo kawiri. UTM iyime paokha ili ndi tsogolo kungatalike. Sitikufuna kubwereza zomwe zachitika ku MCP.
Ndipo zoona osabwereraso mmbuyo Maso patsogolo
Koma kuima pa nonkha simungatenge boma never popanda kuphatikizana ndi chipan champhamvu 😮
Imani nokha tione dpp nde ndiyamoto ndikale
Ndinu mburi zedi mulipachangu koma choononga komaso kachipani kanu kakuntha nanga ku d p p mulibepo Udani a a a si wa UTM iwe ukufuna kuononga mpunga WA UTM
Samamva asiye adzaziona ayiwala zimene adamupangira mademo APM azabwezera zonse zija mmmn they have to learn through mistake with tose alayasi km UTM bwanji mwayamba kuti gwesa phwayi
@@PetrusTlhokwane yes edid
Dpp yikanakhara kut yimamukonda chilima sakanachokako nde musaiware kut chilima nayo anapangira kupya mtima kulowa Ku mcp kut achose dpp mu boma mukwiyo umapangisa munthu kut asapange chinthu cholondola dekani popanga zinthu
We have to join together gentlemen and ladies indeed
That is point UTM ikuyenera kupanga mgwirizano DPP
I salute you mama , good decision more 🔥🔥🔥🔥🔥
Mcp ikuchoka mudzina La Yehova usogoleli umene Mulungu sakondwera umene Mulungu sakondwera nawo amaugwetsa or patavuta bwanji
I totally agree with you Madam
Koma a mayi inu mutizuza kwambiri ndipo you have to learn through mistake muyambilaso tose alayasi tatopa ndi kuliratu ife Chaka chino Chigoliyati chinalephela khondo kwa David nde inu bwanji a UTM km DPP yanuyo 2020 munayipangila mademo nde mwayiwala km mukazi wa Loti adayang'ana m'mbuyo ndikusanduka chulu
Osamakakamiza aliyense ali ndi ufulu ndi chisakho chake pokavota. Panopo kuigwetsa MCP nkovuta aaaa nde gwirizanowo ndi dpp?? Mayi mukunama inu kuyakhula konseko ndi mpando musatinamizepo apa.
Chilima akanati sanapange alliance ndi MCP ndibwenzi Chilima alipo zedi
Inenso ndine wa pa kanthawi ndithu MCP ndayiwona ndipo ndimaidziwa. Kungoti zangovuta kt zipani zinazi ndizazing'ono nchifukwa chake people will be FORCED to make an aliance with DPP. Koma tikawunika BWINOBWINO, DPP ndi MCP palibe kusiyana. Njauju mkulu wa ACB dafa ngati simunthu mpaka pano milandu idangozizira. UTM tsaopano payokha itha/ ndi AFORD, zitha kuchita bwino ndithu chifukwa imfa ya SKC idachita CAMPAIGN YAMPHAMVU. Makamaka ku chigawo cha ku mpoto. Kubwelera ku DPP itakhala LAST OPTION, yes mwachonchi mowawidwa mtima. Mayi ndakumvani BWINO ndithu, ndipo sindikukutsutsani kwambiri, koma DPP, ikhale last option.
May God please bless Malawians, Congrats from SA😂❤🎉
I support that statement MCP should feaz out
Komanso chilimatu akanapanda kuchoka ku DPP bwenzii Ali president wathu moto kupita ku DPP palibe vuto
Omwe akusunga udaniwo tawafunsani kuti kodi wina watichosera chiyembekezo chathuyu ndi awa omwe tinasiyana nawo mwamtenderewa kwabwino kulowera nkuti? Coz pakakhala kugawanikana kwazipani MCP sichokadi u are right
Thanks Mai anthu mwayankhula bwino kwambiri thanks so much for ur spish
zoona koma tipange zimodzi chakwera achoke udani pambuyo pangani zomwezoo moto kuti bhuu!j
Amai munabadwa mwakuya more 🔥
UTM ingopanga alliance ndi DPP that's the only solution
Chipani cha MCP mchakupha komaso mayi inuyo mukunena zoona ndipo ang'onawo achoke.MCP adzayivotera ana a zikhaleng'oma 👋👋👋
Kkkkkkkkkk
😂😂😂😂😂😂
Atsogoleri a DPP, UTM, UDF & AFORD pangani smart, strong, transparent alliance kuti tisinthe dzikoli. Amayi mwalankhula mawu a mphamvu.
Bravo madam I second you❤❤
kod ndindan mai akukamba zanzeru yi
Ife tili DUU (DPP, UDF, UTM) kumastand
Well done mama nkhani.imeneo ndiyabwino tiyeni ku dpp. Amene akufuna ku mcp sianthu.amenewa
Osanena Kuti ine zinandi pweteka iyai,munene Kuti m'mene adamu phera, Chilima Aliyense M'malawi zamuwawa, ndiponso nkhani imeneyi MCP tizawona Ku sogoloku Chakwera tizawona basi
UTM yavutika mokwanira. Izi zomati Bola awa tiwachotse sizithandiza. Za alliance pamapeto. Mangani Kaye chipani UTM siyaying'ono. Ku DPP chilima anavutika. Tikufuna Chitukuko ife. Cholinga sikugwetsa MCP. Tikufuna utsogoleri wothandiza.
Mau mawa Mumakwana
Zoonadi omwe a kulankhura ndi a DPP kuti UTM ipange mgwirizano ndi DPP, ndipo akuterowoso kuwa vomereza kuwauza kuti otsogola akhale wa UTM
Ine nndinatuluka ku DPP coz of UTM apaso ndibwelela chifukwa cha UTM 🔥🔥🔥🔥 SKC
Powerful tiyeni amalawi tidzuke tigwiranane manja Mcp paulendo anthu akupha inenso I wish kuti Mcp imwalire viva UTM viva DPP Rest well our hello
Live from south Africa cape town
UTM , DPP, AFORD and AFFORD make one thing with concrete agreement we were tired please with MCP regimes
God bless you mama good decision ❤
Good solution mama !!!!!
Tilowele ku DPP komweko basi,aDadi munthu womvetsa akatilandila,adadi sadziwa kupha munthu chifukwa chophangila maudindo ndi ndalama
You r the great mama
Kwambili izodi ndizoona 1 to 1 inu nokha ndi mcp kt mungamuchose mm ayi simungathe pitan ku dpp and UDF komaso afodi basi anawa azinyera ndiiithuuu
Nice and powerful decision
UTM moto🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️
Ndipo akapanda kutuluka tiwatulutse ndiifeyo UTM,DPP, AFORD combine with UDF mcp will be defeated mai iminoyo ndi amzeru kwambiri
Very true mai
Thats good idea Mai mwaganiza bho Chakwera must go .. Alliance ya Dpp, UDF, UTM ndi Afford ilii mwala Pangan zotheka bas.
Mayi mwalankhula bwino chilima was a child of apm there is no problem to go back to DPP
Watching from Johannesburg it's good to join DPP
Eya mama joinani basi pangani zomwezobasi tibwerere ku dpp basi
Vuto lake limakhala limeneli, timakhala desperate kufuna kuchotsa chipani cholamula ndiye mapeto ake timangopanga ma plan osayang'ana kumbuyo kapena kuti kutsogoloku ziziyenda bwanji.
Paja DPP ndi kuchimake kwa Propaganda😂😂 Pepani a DPP the only new Malawi that as a nation we all expect is the coalition of UTM and AFORD period. We all all seek New parties in new Malawi to come. The MCP that Malawians have experienced this time NO majority can make such mistake to vote MCP again.
Siyani ma udani , mangani chimodzi ngati a Malawi,
MCP ichoke ndipo isazapezekenso ku Malawi.
Watching from JOHANNESBURG
Mwaganiza mokhwima maganizo abale athu a utm kupanga mgwilizano ndi DPP komanso tili ndichikhulupiliro kuti zipani mwanenazo mosogozedwa ndi Ambuye komanso anthu kulilira dziko lamalawi pamene lafikapa liphulidwe pa moto osatira azipanizo sionse angakondwere koma ambuye achite kufuna kwake pempho a DPP zichepeseninso pa anzanuwo kondanani samaliranani khululukirananipangani umodzi ochokera pansi pa mtima may God bless you
Yes l gree with you Mai,koma ngati simungamve magnanimous a Maiyi ndiye kuti mulibe magnanimous ofuna kutumikila a Malawi koma kukhutisa mamba zanu osati kuombola aMalawi ku Bagamoyo,please paganism chtheka kugwilana manja kuombola Malawi ku mng"anjo ya moto,machine ngati achitila kuno ku south Africa kupanga boma la Malawi colution Government, osakonda anthu awo mwasiye choncho
Kuyankhula kwabwino mai kumeneko ✊✊
UTM, Aford, UDF and DPP maganizo abwino
Mai MULUNGU azikudalisani chifukwa chamawu anu amphamvu ndachilimbikiso, tiyeni tigwirane manja kuti tichotse ng'onazi m"dziko muno
Brilliant idea. Ichoke MCP
Good idea
Mau mau mau pachingelezi timazati so shall it be in Jesus name