Silent means (yes) wapha ? Chete, anthu akudabwa ndiye kuti wapha, key questions are, why silence? What people should expect? Do you have death results? Why did you delayed investigation of death? Why you don't know but you put inquiry for this?😢😢😢 But you, you, you, your days are numbered wallah.
Chomwe chinakupangitsani kuti muchedwe kukayamba kufufuza ndi chomwe ife sitikuvetsetsa ,komaso kuleketsa asilikali kuti basi tiyambaso mawa nchifukwa chiyani ? Keep Resting in peace Mr Saulos Chilima and all the other pipo who died in Chikangawa Continue to be Resting in peace and fight for justice for malawias so that choona chioneke
Nfiti yamunthu okupha amatelo kunamizila chilunga uzafa ukuyeda mulugu Ali nawe konse mizimu ya anthu 9 unia uwona May your soul continue resting in peace Mr saulos and eight others I'm in Mozambique
Galu iwe chakwera fiti yamunthu manyi ako ukazuse kaye anthu amene unapha aja galu iwe, okay umaganiza ngat kut amalawi saziwa kut wapha ndiwe anthu galu iwe osatchulapo mulungu apa pomwe mulungu unatikana, galu iwe chikangawa chakwera fiti zamanyi basi
Sakuziwa kod mesa anatiuza kuti ndi chifunga kmaso akawapepesa bwanji ma mfumuwo chikangawa usamawawone anthu kupusa wamva iwe upepesa bwanji ma mfumuwo ma mfumuwo ndi adyela ngati iye yemweyo 😂😂😂😂😂
Munene kuti zose akudziwa ndimulungu osati zinazo moyo wachilima unali mumanja mwa achakwera kodi or mafuso mulibe kuti mwini moyo anazilola bwaji kuti zichitike moti inuyo kwanu anthu samwalila amalawi tiyeni tikhale ndi umunthu chosecho ambiri mwainu mukutukwana pano pa social media pankhani ya achilima makolo anu ndi afiti bwanji osaweluxa makolo anu uko
The only witnesses to the tragedy r those that were in the plane & lost their lives, let's not fight over this, truth shall alwez prevail, it's just a matter of time!
Anthu Ena andiodabwitsa, are you saying kuti anthu akulowa MCP chifukwa chambiri yabwino ya Chakwera?? Mmmh kuteroku zoti kuli Mulungu mwaiwala chifukwa Cha misonkho ya Amalawi??
Kkkk koma pankhope ya apule mene akuonera pakuziwisa kuti ili ndi matha ndi china chake Munthu amaziwika pamaso kuti or uyu akukana komabe akuziziwa Maso a chakwera zikuonesa kuti mumtima akuziwapo kenakake
Palibe chamzeru pamenepo, akukapepesa Mafumu, kapena akukawapatsa ndlama? Chilima munachita kumupha musakane ndipo mzimu wa Chilima ndi anthu ena 8 anafa pa ngozi ya ndege ija plus Raff kasambala idzakhala ikufuula pa mitu panu kwa nonse munatenga nawo mbali pa kupha kumene kuja
Mbili yabwino yake yokuphayo ose akulowa chipani ichi ndiokuphaso naye kuti mufufuze uzayakha pamaso pamulungu mizimu yathu amene aja ngati ikuona ikukwapule chisilu iwe
Wuyu si president ndi chiboli boli cha president
😂😂😂😂😂😂😂
Ndipo ndi galu kwambiri
Akuyenera kufunsidwa,, coz asilikali achilendo amakatani ku Chikangawa 😢... Mudzayankha pamanso pa Mulungu
Uyu akudziwa mesa adati ndi chifunga ndiye sakudziwa so lelo wayamba kudzilumaso
Silent means (yes) wapha ? Chete, anthu akudabwa ndiye kuti wapha, key questions are, why silence? What people should expect? Do you have death results? Why did you delayed investigation of death? Why you don't know but you put inquiry for this?😢😢😢 But you, you, you, your days are numbered wallah.
Kodi lwe chikangawa umadana Naye chani kwen kwen chilima mpaka kuimisa asilikali kt asiye kumusaka chilima way way Lazaro lweyo umatha kupha galu fit
Hule iwe umapephelaso kod munthu ndiwe wa mcp kale Nde ujoyinaso bwanji hule
Ndiye ngati sakudziwa zomwe zidapha Chilima nanga akumangiranji omwe akunena za imfayi.
Chomwe chinakupangitsani kuti muchedwe kukayamba kufufuza ndi chomwe ife sitikuvetsetsa ,komaso kuleketsa asilikali kuti basi tiyambaso mawa nchifukwa chiyani ? Keep Resting in peace Mr Saulos Chilima and all the other pipo who died in Chikangawa Continue to be Resting in peace and fight for justice for malawias so that choona chioneke
Mbuziiiiiiiii,,ikudya ufa koma sikudziwa kuti ndi ufa.
Kulibe chobisika kuseli kwa thambo
Komatu chakwera mau msamatha, RIP Mr president chilima 😭😭😭😭😭
Chakwera ndi wakupha basi, bwanji amachedwa kumafufuza Za kugwa Kwa Ndege. Akudziwa kanthu
Nfiti yamunthu okupha amatelo kunamizila chilunga uzafa ukuyeda mulugu Ali nawe konse mizimu ya anthu 9 unia uwona
May your soul continue resting in peace Mr saulos and eight others
I'm in Mozambique
Kkkkkkkkk Malawi dziko lonvetsa chison kwambiri ndipo amene anatembelela dziko ili mulungu amukhululukole sure, chifukwa ndidziko lonvetsa chison kwambiri
Udzachidziwa chimenecho 😭
Mafumu anthu azamenyani musamale mukuthamangila kulandila ndalama mumalo mosova zinthu musamale.
Chakwela wakupha Mr chikangawa 😢😢😢😢
Mr chikangawa galu uyo chigawenga chamunthu kuchita kuwadula mapisimapisi azake galu iwe chakwera chikangawa chinkhope ngat chikangawa
Umbuli wanu nde mwafika nawo pa 💯 😅😅😅
Mmalo mokapepetsa ku Ntcheu kwao Kwa Chilima
Iweyo kiungu ukunam
Ngakhal kt asayankh pal chiyan chomwe awapangako zosonyez kt chifukw chakusayankh kuj wachit izii
Chakwera ndimunthu oipa kwambiri dziko lonse lapasi 💔💔💔💔💔 anapha Chilima
Ife ngati amalawi mafumu ndi atsogoleri azipani ngati simukhala ofuna kutumikira anthu simuzapatsidwa ulemu
ntchito Yake yauganayongayo mkumati MCP ntchito wabwino fodya bas
Bodza ili U TM sitikukangana Adyela ndiomwe akuchoka
U can be clever on this world but one day it's one day God is watching U baba h!
Iwe uli mbuz ukut chiuta aziwa unamukana kale chiuta poya zachipani
😂😂😂😂😂Nde mafumu ndiwoyima mituuuuu onsewa akuwabera mitsokho yawoooo nde ndikumakamupepesa mr chikangawa yooo 😂😂😂😂😂nimayikondatu
Galu iwe chakwera fiti yamunthu manyi ako ukazuse kaye anthu amene unapha aja galu iwe, okay umaganiza ngat kut amalawi saziwa kut wapha ndiwe anthu galu iwe osatchulapo mulungu apa pomwe mulungu unatikana, galu iwe chikangawa chakwera fiti zamanyi basi
Ukuziwa wekha ndi mbuli zizako 😅😅😅😅
We respected you chief alot but on this brutal murder,chakwera knows
No resignation
No cabinet reshuffle
No someone to be fired
No
Uli ndi umboni iweyo?
@@tamalangoma2765 samalatu !
Bwanji munachedwa kulengeza, munadziwa 10am kukalengeza 11pm mumadikila chai?
Sakuziwa kod mesa anatiuza kuti ndi chifunga kmaso akawapepesa bwanji ma mfumuwo chikangawa usamawawone anthu kupusa wamva iwe upepesa bwanji ma mfumuwo ma mfumuwo ndi adyela ngati iye yemweyo 😂😂😂😂😂
Evera yudasi wachikaziiii😂😂😂😂😂😂😂 eee koma kutukula dziko kuti latukukako dzikoli njara ilithoooo uphawi uli thooooo umbanva uli thooooo kupha athu nde nyanye kumanga nde akungo lakalaka kumanga dziko lonse
Simuthu wabwino chikangawa chakwera uyu
😢😢 yah akayenela kufunsidwa and uyu si president koma chilombo chowopsa
Ma mfumu maso tong'oo kulandila mr chikangawa mesa chilipo chimene akumeneko 😂😂😂😂
Ndi Mulungu wanthawi...choonadi sichipheka ...
Ulikoma iwe kupusa
Mbiri yabwino yachani nawe kachimagrass?mbiri yakuphayo kuchikangawa?
Kamtukule adakikale wa MCP
Tell us 😭😭 what is happening in chikangawa plz plz
KAMANSO CHAKWERAYO SAKUYENERA KUMAYANKHA KUMENE CHIFUKWA OLAKWA SAKHALA NDI MAU CHIRICHONSE CHIMENE ANGAYANKHULE ADZETSA NKWIYO KWA ANTHU, IWENSO NDIWE MBUZI CHAKWERA ALI NDI ULAMULIRO WABWINK KUTIKO AGALU INU
Mmene umagwetsa ndege muchikangawa mulungu analipo ndipo alipobe mulungu akuika poyera ndipo uchidziwa pompano
Munene kuti zose akudziwa ndimulungu osati zinazo moyo wachilima unali mumanja mwa achakwera kodi or mafuso mulibe kuti mwini moyo anazilola bwaji kuti zichitike moti inuyo kwanu anthu samwalila amalawi tiyeni tikhale ndi umunthu chosecho ambiri mwainu mukutukwana pano pa social media pankhani ya achilima makolo anu ndi afiti bwanji osaweluxa makolo anu uko
We have to wait from German to deliver the commission of inquiry.
Tidayika satana wakupha pampando,lero akukhuta misokho yathu chonsecho ndi chigawenga
Kamtukule wa tsata chibwenzi chake ku MCP
Anangodziwa kuitana asilikali akunja?
Chakwera akudziwa chomwe chinagwetsa ndenge ndipo tose tikudziwa zimenezo ndichifukwa achita manyazi kutulutsa report
Palibe chomwe angatiudze uyu..ngati report lama Albino mpaka pano kuli ziii 3 years atalikhalira
Wapkuphabe iwe chakwera
The only witnesses to the tragedy r those that were in the plane & lost their lives, let's not fight over this, truth shall alwez prevail, it's just a matter of time!
Ndimmene mfiti imanenela.adapha wanthu uyu
Ameneyu akuona ngat sitikudziwa kut anapangitsa ndege kut igwe ndiiyeyu.
akantukule ndi hule kupemphera iweyo hule tazingonyengsna ndi achakwera chigawenga
Iweyo Mkaka umiyedzekerense mlam wakoyo
Ngt mnene munamuyedzekera chilima
Ubwino wake ndiwanu kale simungamuyedzekere....poti ndachibwenz abwana anu..nde simuyedzeka😅😅😅😅
Akudziwa kuti ndege anagwetsa chili chonse akuchidziwa koma sangavomeke
Gwenembe kupha chilima
mulungu alipo wamoyo zizaziwika osadandaula ifa ikubwela muzaziona
UYU ANAPHA CHILIMA ASANAMEPO APA AKUDZIWAPO KANTHU CHIKANGAWA UYU GALU, KOMANSO CHODABWITSA NCHAKUTI KODI MAFUMUWA AKUMUPEPESA CHAKWERA NGATI NDANI ? KOPITA CHIPEPESO MESA NDI KU MABANJA OFEREDWA ? MAFUMU SO NDINU OPUSA KWAMBIRI ZITSIRU ZAMAFUMU AGALU
Palibepo Umboni wakut apule ndiwolakwa kungot anthufe tikuyenda okwiyakwiya pa zifukwa zanthu
Mafumu awa zikazangoziwika kuti achilima anaphedwa mafumuwanso azaweruzidwe
Mafumu Ena amaoneka ngati anzeru but ndimazoba kyungu oneka ngati wanzeru uja mpaka kupera chonchi? Eishi ndalama yavutadi
Nigalunji uyo wavala magogosi akuti chikangawa chakwera ali nd mbiri yabwino
Akuopa ma minster kuti akakhalabe ku utm akhonza kuluza mpando ndi xm mene ine ndikuonera
Which ntchito yomwe akugwila anyakwawa?? Mwalandila chi banzi vuto lake
Anthu Ena andiodabwitsa, are you saying kuti anthu akulowa MCP chifukwa chambiri yabwino ya Chakwera?? Mmmh kuteroku zoti kuli Mulungu mwaiwala chifukwa Cha misonkho ya Amalawi??
Mrs chikangalawa akufuna athandize mamuna wake kuti awine kawiri chisakho koma it won't happen in our country
Ubwino ndi otii olo chakwera atalamula bwanji koma mathero ake imfa ilipo naye azalawa imfa
Hule iwe Vera
Galu iwe chakwera unapha nzako kapolo iwe dikira siku la chiweluza ukomana ndi moto wa sufure ndpo mcp chipan chakupha sitikuchifuna ife
Amakatengako ndalama basi
Chakwerayo chikumbu mtima ngati chimapha chimuphe
The response to the incident was questionable.
KODI KYUNGU AMAFUNA CHANI KWENIKWENI? KUTEROKO WANYAMUKA KUCHOKERA KU KA ATI APULEZIDENTI AKANDIONE KUTI NDINE WABWINO?
Mulungu salakwitsa kalikose
L) l❤❤❤
In this world some people the know you than you know yourself that's he said only God knows
Chakwera akudziwa akudziwapo kanthu munthu oipa
Rest in peace Saulos Klaus Chilima 😭😭
Mudzacidziwa thawi ikubwera
Mapwala anuwo akutukulu dziko lake lithi
No nsense at all
Mkakayo maso ngati mbolo
Ana amahule inu simuziwika chipani chimenene muli
Eya akantule akuonaka kuti chakwera nzeru alive,mbiri yabwino yokupha anthuko NDE mbiri yabwino fiti ngo'ona inu
Palibepo tsogolo pamepo kungobweretsa umphawi basi ndziko mwanthu
Mkudziwapo kanthu, why delaying kufufuza
Those chiefs went to condolences to the president they are stupidly crazy mind the chiefs they could to pay their condolences to Ntcheu
Asowadi mtendele nanga report mpaka lero zithu za mu June
Who is to comfort who?
Ndipo mmmm
Kkkk koma pankhope ya apule mene akuonera pakuziwisa kuti ili ndi matha ndi china chake
Munthu amaziwika pamaso kuti or uyu akukana komabe akuziziwa
Maso a chakwera zikuonesa kuti mumtima akuziwapo kenakake
ndiye Ngati simukudziwapo Kathu apuresident ndiye mutitulusile lipoti Mesa mumanena Kuti kwabwela anthu akujelemani lipoti mpaka pano Ife chilungamo tidzachidziwa Muka Tulusa lipoti
Chakwera unapha sidiki mia saulos chilima ndi anthu ena aja
Institute an independent commission of inquiry
Ndikovuta kuti mafumu dziko lapansi akalowe UFUMU was kumwamba
Mmmmm mbiri yokupha mmmmm
Kodi maliro aChilima anachitikira ku ya boma,nanunso aKyungu mwadya banzi
Palibe zopatsana ulemu apa akudziwapo kathu pa za imfayi
Harry mkandawiri nde mpha anthu wakarekare
Palibe chamzeru pamenepo, akukapepesa Mafumu, kapena akukawapatsa ndlama? Chilima munachita kumupha musakane ndipo mzimu wa Chilima ndi anthu ena 8 anafa pa ngozi ya ndege ija plus Raff kasambala idzakhala ikufuula pa mitu panu kwa nonse munatenga nawo mbali pa kupha kumene kuja
Panyapako chakwera
Saakudziwa bwanji poti ali ndi report? Akulubwalubwa bwanji?
Mbili yabwino yake yokuphayo ose akulowa chipani ichi ndiokuphaso naye kuti mufufuze uzayakha pamaso pamulungu mizimu yathu amene aja ngati ikuona ikukwapule chisilu iwe
Ubwino wake anakuphela makolo ako
Come out with a report ya ngozi ya ndege please please please.