BON KALINDO AMAFUNA KUPHEDWA KU PARLIAMENT

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 29 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 164

  • @yusufbakali-zm2hq
    @yusufbakali-zm2hq Рік тому +10

    Aululeni ndithu😂

  • @GeorgeTembo-v6i
    @GeorgeTembo-v6i 7 місяців тому +6

    Komatu ukatengera za kagame ukhala mmavuto anthu akulira misozi yamagazi chifukwa cha iwe mulungu alinafe AMEN

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Рік тому +4

    mulungu ndiwakulu ❤❤❤

  • @amoschataika1284
    @amoschataika1284 Рік тому +11

    If this nonsense of MCP continues i will report to the whole world blv me. Malawians let's save our Country from these Idiots. More fire Limpopo FM.

  • @ShaId-qc9bh
    @ShaId-qc9bh Рік тому +3

    Bwino angakusowese nawe .koma mosaopa bon kalindo alingat kamuzu I think zimu wakamuzu walowa mwabooooon ine ndilikumbaliya booooon mulungu azimudalisa .aboon kalindo akuyenela mubuku la history m'malaw ndimunthu oyamba kuzipeleka muno malaw ulem wanu booooon kalindo

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr Рік тому +2

    Limpopo ndikupemphelerani mwayi nzeru mphamvu kuchita bwino zisikire kwainu nonse mukufukula zonsisi za.nkhandwe chakwera

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu 3 місяці тому

    Pitilizan ntchito
    Yanu mulungu ali nanu
    Akuthandinza

  • @ChifundoBeston
    @ChifundoBeston Рік тому

    Zabodza izi amalawi musazimvere Bon Kalindo palibe zoti amafuna kuphedwa. Chonde inu abale anga akumwera ngati ndi mkwiyo tisafike nawo pomanena bodza lotere. Poliza nonse amene mukunena bodza limeneli mmalo wa m'bale wanga bon kalindo ndikuti izizi ndizabodza ndipo nonse machende anu, Nyini zanu,mitumbo yanu.

  • @SamuelMponda-y3d
    @SamuelMponda-y3d 3 місяці тому

    Kodi MCP ndi Chakwera angakhoze kutseka
    pakamwa anthu opitirira 20 000 000?

  • @yusufbakali-zm2hq
    @yusufbakali-zm2hq Рік тому +2

    Ndili nanu limodzi ine yb

  • @MaggieGondwe-vn2wx
    @MaggieGondwe-vn2wx Рік тому +1

    Mulungu adzikusogolerani nthawi zonse , timakunyadirani

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 Рік тому +1

    Zoona zokhazokha bigy🔥🔥dziko lavunda ili eesh.

  • @DAVIDOSMAN-m9n
    @DAVIDOSMAN-m9n 11 місяців тому

    Born kalindo God he protect u way you are

  • @IBRAHIMCHIPASULA
    @IBRAHIMCHIPASULA Рік тому

    Malawi is boring now. We salute you comrades freedom fighters

  • @stevenjabison7543
    @stevenjabison7543 Рік тому +1

    Bonikalindo ukangomupha iwe chakwela ine ndikukutsimikizilani kuti nkhondo yamundipondelamwana idzayambika pompo pompo kodi inu asilikali mwafikapoti mukuvomeleza kuti tchito simudziwa?mpaka achakwela ayamba kukhulupilila aitikali aku luwanda kuti adzidzatipha eeeeeeeeee amalawi tiyeni tidzuke chonde chonde dzikolali likupita ku phompho

  • @LimbikaniMakwandu
    @LimbikaniMakwandu 3 місяці тому

    Tell us true news mitima yathu imathamanga

  • @chrisscentn
    @chrisscentn Рік тому

    Ati Rimpopo fm....aaaaaaaa! Limpopo.

  • @KeniusSanderson
    @KeniusSanderson 11 місяців тому

    What a poor governance by a poor minded leader

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 Рік тому

    Muli ndi umboni wazomwe mukunenazi ?

    • @blandinabonaventure
      @blandinabonaventure Рік тому

      Alinawo munthu angayime pagulu kuti anthu amuvere

    • @Kellz-Mdoka1
      @Kellz-Mdoka1 Рік тому

      Osafuna asamavele machende anu

    • @thondoyaenterprise3795
      @thondoyaenterprise3795 Рік тому

      @@Kellz-Mdoka1
      U must be childish, this podcast is for public opinions. Why u insulting me ?
      Anyway i don't expect u to understand.
      We are on different levels of knowledge and understanding

    • @thondoyaenterprise3795
      @thondoyaenterprise3795 Рік тому

      @@Kellz-Mdoka1
      U need serious CIVIC EDUCATION

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 Рік тому

    Stop telling lies my friend.

  • @meganabigail-ye7fw
    @meganabigail-ye7fw Рік тому +6

    Iiiii asilikani ali pamoto bola kuno ku John timagwila in 8 hrs koma our salary is running to 400 pin iya ziveleni chison asilikali aku Malawi

  • @alickalick6509
    @alickalick6509 Рік тому +6

    Sindikudziwa kuti Chilima anali ndi zaka zingati nthawi imene timavutika ndi MCP ?
    Ndikutelo chifukwa chakuti ndi Chilima amene anapangitsa zonse amawona ngati kuti Chakwera ndi amalume ake lero ndi izi dziko labweleranso kumavuto akale.
    Anthutu koma timanena kuti njoka ndi joka singakhale somba zosatheka Chilima mukayakha pamaso pa Mulungu kudandawura kwa a Malawi.

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn Рік тому +11

    I like Nkhanga zapenya mumaona pataaaaaaaaaali

  • @BitilesiKathiti
    @BitilesiKathiti Рік тому +8

    Asilikali akumalawi amakanika kuuluka pa pala ndiye angakwanitse kulanda dziko mmmmmm zosatheka

  • @GEORGE-yr7nx
    @GEORGE-yr7nx Рік тому +8

    😢komatu choti mudziwe choti Boni kalindo akangofa dziko lamalawi mudzakhala magazi chifukwa ife sitidzalola

  • @Steven-hl6cb
    @Steven-hl6cb Рік тому +6

    ziko lomvesa Chisinau.mcp nonse mulungu akukatheni

  • @BitilesiKathiti
    @BitilesiKathiti Рік тому +6

    Nkhanga zaona mumakwana pitilizani kuulula zobisika osasiya ayaluke abakha amenewa

  • @RaheemNgoma-pk1ev
    @RaheemNgoma-pk1ev Рік тому +3

    Pena kumachita manyaz ukaziganizila kut ndiiwedi mmalawi dziko lomvetsa chison

  • @kassimwilson
    @kassimwilson Рік тому +5

    ama funa kumupha ngat ana muphela clement chiwaya

  • @Goliath461
    @Goliath461 Рік тому +2

    Koma tinene zoona asilikali akumalawi sangangokhala kumayang'ana kagame akutumiza asilikali kuno ,athuwa adyesedwa banzi, chifukwa sizoona asilikali athuwa kumangozisiya zikuchitika pamaso pao ayi m'malawimuno tilibe asilikali otiteteza akwera chipani

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Рік тому +6

    We don't have soldiers in malawi

  • @promixphotography8056
    @promixphotography8056 Рік тому +2

    Pitilinzani kuunza anthu choona ndipo ziko liziwe choona chifukwa moyowu ukupitilira zigawenga. Malawi wake up, wake up. Iyi si Democracy ai,

  • @rajabpetrolmakiyi
    @rajabpetrolmakiyi Рік тому +4

    Vuto ndiloti udindo waku Army amasankha ndi president kapena ndinene kuti ndiwandale chifukwa amasankha amene akufuna kuti azipanga zofuna ndikukomera iwowo.
    Tsono mkulu wa army alipoyi ndiwawo.
    Chifukwa how they bring army from Rwanda pamene ifeyo army tili nayo
    Pamenepo asilikali nonse amene muli ku army simukuwona kuti president Yu akunyozani kuwoneka kuti inuyo mulibe ntchito ndiwopanda pake komanso kukunyozesani ku dziko lonse lapansi kuphatikiza ku Rwanda ko kukhala ngati Malwi ndi Rwanda number 2.
    Ganizani bwino asilikali athu ndithu musawineke osafunika lero pomwe nthawi imene tinkapampanga ma demo kuti boma la DPP lituke mboma munagwira ntchito yayikulu kuti iyeyo Chakwera yo akhale President ndiye lero musakhale opanda pake kapena osafunika kapena ndinene kuti mukhale makape

  • @elliousBowman
    @elliousBowman Рік тому +6

    Satana ndi olephera May God protect the dc

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr Рік тому +2

    Chakwera dziko tinachita.kulipedza komanso tidzalisiya siunalikonze ndiiwe kunali kamudzu muludzi malemu bingu joice banda peter onsewo anavomeredza.ndipo anasiya .ndiye ndiiwe ndani kuti udzikatenga zigawenga kuruwanda kuti adzitiopsyedza ndizosatheka utafe ndiiwe ifeyo utisiya ndipo iweyo chakwera chaka chino chikakuthere kumanda utisiye tizikhala anthu tisakhale mwamantha mudziko lathu chifukwa cha chakwera 😂😂😂😂😂

    • @blandinabonaventure
      @blandinabonaventure Рік тому +1

      Ndipo asilikali aku Rwanda atiopseze dziko lathu lomwe Mulungu Chakwera akuoneni ndi, ng'oma ija, mulungu wathu ndiwamoyo

  • @AnusaNkhoma-t4v
    @AnusaNkhoma-t4v Рік тому +3

    Malawi wafika poipa ndipo tikapanda kusamala ana Athu azavutika

  • @AllieJamesNsekadala
    @AllieJamesNsekadala Рік тому +5

    MR ntanyiwa mumakwanira

  • @ritabani274
    @ritabani274 Рік тому +1

    Nthawi ya Mlungu ikadzakwana adzachoka pampandopo pemphero ndiye chida choti tigwilitse ntchito kuti dziko lathu liyende bwino ka M CP ndikachani Achakwera adzatha ngati Farao

  • @mathewsmbaluko8522
    @mathewsmbaluko8522 Рік тому +2

    Asilikali osalanda ziko bwanji ,Kodi mayesa job yanu ndikuteteza anthu ?

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Рік тому +3

    Tsiku lomwe adzaphedwelo, nkhondo yayamba pompo

  • @SammyChibagera
    @SammyChibagera Рік тому +2

    Mulungu amutetezera boni kalindo sangamuthe chilungamo sichifa akunama kwambili

  • @STARLIGHTGSM-cd8uv
    @STARLIGHTGSM-cd8uv 3 місяці тому +1

    Ai radio ili boh

  • @eliasmpita3916
    @eliasmpita3916 3 місяці тому

    Zikateto anthunu kumavoteranso chipani choterocho kupha kwambiri. Akufuna kupha achinyamata onse. Nkhanga Zaona pitirizani kufukula zambiri.
    Mfukuletso anthu amene abwere kuchita kafukufuku was ngozi ya ndege.

  • @BensonChilundu
    @BensonChilundu 3 місяці тому

    MCP ikatuluka m’bomamu mudzwe kuti simudzalowanso.Tinakuvoterani kuseri kwa ubusa poona kuti popeza ndinu oopa Mulungu,komatu zafikapa sindinu m’busa koma ndinu satana Ndipo ku ubusako mumangofuna ulemelero koma dziwani kuti Mulunguyo akukuonani ndipo posakhalitsa mulandila msautso oti muzazindikila kuti bolanso kumangodya therere m’midzimu.Mawu anga awa muzawakumbukila

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 3 місяці тому

    Mulungu ndiwazatheka bwanji Bone Kalindo amulephera ndi Mwana wamulungu amene akutisegula maso Ife ana ama 2000 tithokoze Mr Mtanyiwa mulungu azikutetezani Kwa adani kut tizithabe kudziwa zomwe zikuchitika mu ziko lathu

  • @cliffordmwale3167
    @cliffordmwale3167 Рік тому

    Comrade Ntanyiwa - Be a good journalist please! How did Bon know CCTV is not working? Anyamata a DPP muknigrira ntchito yoipitsa MCP but don't forget what ana a dad were doing in LL? Bangwe &
    Ntopwa 1

  • @MadaMzamu
    @MadaMzamu Рік тому +1

    Asilikili amalawi amangowatuma kokalanda Makara basi ndikumalondera khalango basi not to protect the country

  • @smt7036
    @smt7036 Рік тому +2

    amalawi vuto timadana ndimuthu osati zochitika zake athu anamuda peter muthalika kuyikapo abalewa lelo ndi izi

  • @meganabigail-ye7fw
    @meganabigail-ye7fw Рік тому +1

    A MCP ndi anthu omvetsa chison kwambiri nanga chifukwa chani sakuzifunsa kut the whole Malawi Born Kalindo kukhala patsogolo kulimbana naye sakumutha? Ndipo angozisiya

  • @PetuloMoyenda-bp3gl
    @PetuloMoyenda-bp3gl Рік тому +2

    Ambuyetu Ali naye ndipo mulungu akumugwiritsa ntchito Ali ngati mose wathu ameneyo

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 3 місяці тому

    Amalawi chonde tigwilane manja tiwomboleziko lanthuli komatu timawuzidwa kuti Mcp ndi yakhupha ife ana ama 2000 sitimaziwa

  • @SamuelMponda-y3d
    @SamuelMponda-y3d 3 місяці тому

    Ndimuuza Chakwera kuti wagwa mdzanja la Mulungu ndipo aipa kuposa Cinkhanira, Mulungu akugwetsa isanafike nthawi imene uiganizira.

  • @yusufbakali-zm2hq
    @yusufbakali-zm2hq Рік тому +5

    Nkhanga zaona mulibhooo

  • @RhulaniMukasi
    @RhulaniMukasi 3 місяці тому

    Olomwam,bera ndalama kalindo musaganize kut akusiyan choncho kuyaluka muyaruka ndithu apolice otan inu minyeromwanu nonse

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 6 місяців тому

    Achakwera ndimayesa munali busa apa mwawoneka kuti ubusa wanu unali wachinyengo bon kalindo akafa ndinu achakwera ziko lonse likuziwa ichi mulungu amuteteze amuteteze amutetezebe kalindo

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Рік тому +3

    Asilikali tilibe

  • @ChristopherKazembe-c8t
    @ChristopherKazembe-c8t 5 місяців тому

    Apolice akakhala chete kuthandidzira mcp kapena kut tonse government tidzikumenyan

  • @lyiemax
    @lyiemax Рік тому +3

    May the good Lord continue protecting our president for the poor and his family, our expectations rely on God through him

  • @MARKZAKEYU-nh1zn
    @MARKZAKEYU-nh1zn Рік тому

    Aphedwa bwanji .Kugomva kuti mcp ndi yokupha achakwela ndi boma lao ndi olephela basi guleyu wa vina watopa

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 8 місяців тому

    Mwadzuka bwanji abale azanga pa nkhanga zaona, ngati mulibwino mulungu akudalitseni nonsense, ineyo ndili bwino, nkhanga zilipo?

  • @uyosakala4880
    @uyosakala4880 Рік тому +3

    I like this kanga zaona from Zambia

  • @SamuelMponda-y3d
    @SamuelMponda-y3d 3 місяці тому

    Kodi Chakwera alibe zochita zina , angokhalira kukonza plani yopha anzake padzikopo

  • @PreciosNdlovu
    @PreciosNdlovu Рік тому +2

    Bangolini sangamuthe.Dc Dengelous child

  • @FatimaUmali-pc8sy
    @FatimaUmali-pc8sy 5 місяців тому

    Zikomo tikuziwa nawo pitilizani kutiziwitsa allah 24:48 bless you inshallah😢😢

  • @RhulaniMukasi
    @RhulaniMukasi 3 місяці тому

    Umbon otan nanyero iwe mot wekasukuona muyaluka ambilitu ndikuuzen

  • @AustinJali
    @AustinJali 19 днів тому

    I love nkhanga zaona more fire mthanyuwa!!

  • @carenchikwe268
    @carenchikwe268 Рік тому +2

    Ambuye atichitire chifundo ndithu mmh

  • @yusufbakali-zm2hq
    @yusufbakali-zm2hq Рік тому +3

    Mademo akhalaso liti I'm ready kk47

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 Рік тому +1

    In Malawi is there any real defense force? Are they real soldiers? One thing Malawian people should, know is this during Kamuzu Banda, Kamuzu Banda was trying to erase Malawi defense force to Malawi young pioneer if you can remember very well, this is signal to that direction Malawi defense force must wake up now before it's too late look what is going on in D R C( CONGO 🇨🇩) who is behind the war there, is Rwanda under Paul kagame now Chakwera and his party are doing the same to bring that war in the country ,Chakwera is busy wagging the war in the country Malawian wake up now.

  • @KingSikota-s2u
    @KingSikota-s2u Рік тому +3

    Kumalawi kulimbe asilikali guys tisadalile asilikali akumalawi 💪💪💪

  • @EdwinPhiri-k1w
    @EdwinPhiri-k1w Рік тому +2

    MCP is a killer

  • @zacariasjoselemessonelemes9562

    Kkkkkkkkkk i like this program, from Moz

  • @giftmingo9293
    @giftmingo9293 Рік тому

    Ndalama sanatenge nthawi ya DPP bwanji? Zitsiru zina inu you think Kalindo is a god. Munthu angamuphere ku parliament? So do you parliament building izingokhala opanda chitetezo? Mumupweteketsatu nzimayi wapolisi osalakwa.

  • @RashidKusum
    @RashidKusum 26 днів тому

    Phiriwake garu ngati ameneyu buzi yamwana

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Рік тому +2

    Amene zikukunyasa usamamvere palibe akukutuma kuti uzimvera

  • @duncainjimmy
    @duncainjimmy Рік тому

    Asilikali salary yake imeneyo kumangosekelera mbwelerazo

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 Рік тому +2

    Komatu zikuwonjezatu mmmmm

  • @blandinabonaventure
    @blandinabonaventure Рік тому +1

    Mulungu ndiwamoyo Palibe chida chosulidwa chomwe chizambane

  • @AgnesMatola
    @AgnesMatola Рік тому +1

    Mposo M'mene ziswera nkhangazo kuchuluka kwake amagwetu.....!

  • @MatiasPiloti
    @MatiasPiloti Рік тому +1

    Tiuzeni zowona tidziwe zambili

  • @KingSikota-s2u
    @KingSikota-s2u Рік тому +9

    ALLAH umutetesele boni kalindo

  • @MussaPanje
    @MussaPanje Рік тому +1

    Chakwela ndichilima machende anu angalu anthu woyipha kwambiri

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli 3 місяці тому

    Dziko zomvetsa chisoni very sad

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 3 місяці тому

    Mayo!!!!!zakazinanso 5 alamula?😭😭😭😭😭

  • @ErnestMussa-b6u
    @ErnestMussa-b6u Місяць тому

    yes i want to be on line with this channel

  • @PaulKwenda
    @PaulKwenda Рік тому +1

    Zabodza zokhazokha

  • @ebstonekonzani9126
    @ebstonekonzani9126 11 місяців тому

    .... what kind of government is this

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 6 місяців тому

    Amakachitako chiani ngati iye ndi MP.

  • @HendryChiwezo
    @HendryChiwezo Рік тому +2

    Mmmmmm mabodza awa

  • @LuoPhillipheprince
    @LuoPhillipheprince Рік тому +2

    Bwinotu bwino atha kuyaluka!

  • @louisemsowoya8235
    @louisemsowoya8235 2 місяці тому

    😭😭😭😭 ooooh Malawi 😭

  • @cabdinaasirxiddig2338
    @cabdinaasirxiddig2338 Рік тому

    Kod chakwera umaonangat momwe umatsogolera anthu mkachisi ndekut ukhozaso kutsogolera dziko lonse chonde bwelera kuntchito yako ya ubusa ndipo zomwe ukuchitazo mdzikomo mukhala kubu kogwiritsa dzida samala

  • @StanleyTembo-fl7cc
    @StanleyTembo-fl7cc Рік тому +1

    May Almighty God continue blessing him with more life

  • @KassimSteven-j1z
    @KassimSteven-j1z 17 днів тому

    Ndipo sizitheka

  • @Sugerman-tw4do
    @Sugerman-tw4do 3 місяці тому

    Manganya wasewelo ndi vas lelo

  • @memoryedwin
    @memoryedwin Рік тому +1

    Eeee koma mavuto

  • @aaronmbawa2884
    @aaronmbawa2884 Рік тому +1

    Maganizo amuthu sichifunilo chamulungu

  • @FloraBanda-l8u
    @FloraBanda-l8u 9 місяців тому

    Nkhanga zaona akuti aliyese atenga chikwanje chake yemwe alibe agule akakukhapa nawenso uwakhape aliyense amve kuwawa😂 like your news Nkhanga pitilizani kuwona patali, may God protect the DC president of poor people.

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 Рік тому +1

    Mavvto Malawi bon mulugu alipho

  • @SalmanjussabAzombwee
    @SalmanjussabAzombwee Рік тому +1

    Umakwana bon