@@Kellz-Mdoka1 U must be childish, this podcast is for public opinions. Why u insulting me ? Anyway i don't expect u to understand. We are on different levels of knowledge and understanding
Sindikudziwa kuti Chilima anali ndi zaka zingati nthawi imene timavutika ndi MCP ? Ndikutelo chifukwa chakuti ndi Chilima amene anapangitsa zonse amawona ngati kuti Chakwera ndi amalume ake lero ndi izi dziko labweleranso kumavuto akale. Anthutu koma timanena kuti njoka ndi joka singakhale somba zosatheka Chilima mukayakha pamaso pa Mulungu kudandawura kwa a Malawi.
Mulungu ndiwazatheka bwanji Bone Kalindo amulephera ndi Mwana wamulungu amene akutisegula maso Ife ana ama 2000 tithokoze Mr Mtanyiwa mulungu azikutetezani Kwa adani kut tizithabe kudziwa zomwe zikuchitika mu ziko lathu
Comrade Ntanyiwa - Be a good journalist please! How did Bon know CCTV is not working? Anyamata a DPP muknigrira ntchito yoipitsa MCP but don't forget what ana a dad were doing in LL? Bangwe & Ntopwa 1
In Malawi is there any real defense force? Are they real soldiers? One thing Malawian people should, know is this during Kamuzu Banda, Kamuzu Banda was trying to erase Malawi defense force to Malawi young pioneer if you can remember very well, this is signal to that direction Malawi defense force must wake up now before it's too late look what is going on in D R C( CONGO 🇨🇩) who is behind the war there, is Rwanda under Paul kagame now Chakwera and his party are doing the same to bring that war in the country ,Chakwera is busy wagging the war in the country Malawian wake up now.
Ndalama sanatenge nthawi ya DPP bwanji? Zitsiru zina inu you think Kalindo is a god. Munthu angamuphere ku parliament? So do you parliament building izingokhala opanda chitetezo? Mumupweteketsatu nzimayi wapolisi osalakwa.
Nkhanga zaona akuti aliyese atenga chikwanje chake yemwe alibe agule akakukhapa nawenso uwakhape aliyense amve kuwawa😂 like your news Nkhanga pitilizani kuwona patali, may God protect the DC president of poor people.
Aululeni ndithu😂
Komatu ukatengera za kagame ukhala mmavuto anthu akulira misozi yamagazi chifukwa cha iwe mulungu alinafe AMEN
mulungu ndiwakulu ❤❤❤
If this nonsense of MCP continues i will report to the whole world blv me. Malawians let's save our Country from these Idiots. More fire Limpopo FM.
Which world 😂😂😂
U will be reporting as who ???
Bwino angakusowese nawe .koma mosaopa bon kalindo alingat kamuzu I think zimu wakamuzu walowa mwabooooon ine ndilikumbaliya booooon mulungu azimudalisa .aboon kalindo akuyenela mubuku la history m'malaw ndimunthu oyamba kuzipeleka muno malaw ulem wanu booooon kalindo
Limpopo ndikupemphelerani mwayi nzeru mphamvu kuchita bwino zisikire kwainu nonse mukufukula zonsisi za.nkhandwe chakwera
Pitilizan ntchito
Yanu mulungu ali nanu
Akuthandinza
Zabodza izi amalawi musazimvere Bon Kalindo palibe zoti amafuna kuphedwa. Chonde inu abale anga akumwera ngati ndi mkwiyo tisafike nawo pomanena bodza lotere. Poliza nonse amene mukunena bodza limeneli mmalo wa m'bale wanga bon kalindo ndikuti izizi ndizabodza ndipo nonse machende anu, Nyini zanu,mitumbo yanu.
Galu panya pako mbava ya chakwera
Kodi MCP ndi Chakwera angakhoze kutseka
pakamwa anthu opitirira 20 000 000?
Ndili nanu limodzi ine yb
Mulungu adzikusogolerani nthawi zonse , timakunyadirani
Zoona zokhazokha bigy🔥🔥dziko lavunda ili eesh.
Born kalindo God he protect u way you are
Malawi is boring now. We salute you comrades freedom fighters
Bonikalindo ukangomupha iwe chakwela ine ndikukutsimikizilani kuti nkhondo yamundipondelamwana idzayambika pompo pompo kodi inu asilikali mwafikapoti mukuvomeleza kuti tchito simudziwa?mpaka achakwela ayamba kukhulupilila aitikali aku luwanda kuti adzidzatipha eeeeeeeeee amalawi tiyeni tidzuke chonde chonde dzikolali likupita ku phompho
Tell us true news mitima yathu imathamanga
Ati Rimpopo fm....aaaaaaaa! Limpopo.
What a poor governance by a poor minded leader
Muli ndi umboni wazomwe mukunenazi ?
Alinawo munthu angayime pagulu kuti anthu amuvere
Osafuna asamavele machende anu
@@Kellz-Mdoka1
U must be childish, this podcast is for public opinions. Why u insulting me ?
Anyway i don't expect u to understand.
We are on different levels of knowledge and understanding
@@Kellz-Mdoka1
U need serious CIVIC EDUCATION
Stop telling lies my friend.
Paja inu zonse ndizonama
@@blandinabonaventure
Evidence brother
Malawi cannot be fixed like this.
Lets engage positively
Iiiii asilikani ali pamoto bola kuno ku John timagwila in 8 hrs koma our salary is running to 400 pin iya ziveleni chison asilikali aku Malawi
Sindikudziwa kuti Chilima anali ndi zaka zingati nthawi imene timavutika ndi MCP ?
Ndikutelo chifukwa chakuti ndi Chilima amene anapangitsa zonse amawona ngati kuti Chakwera ndi amalume ake lero ndi izi dziko labweleranso kumavuto akale.
Anthutu koma timanena kuti njoka ndi joka singakhale somba zosatheka Chilima mukayakha pamaso pa Mulungu kudandawura kwa a Malawi.
I like Nkhanga zapenya mumaona pataaaaaaaaaali
Asilikali akumalawi amakanika kuuluka pa pala ndiye angakwanitse kulanda dziko mmmmmm zosatheka
😢komatu choti mudziwe choti Boni kalindo akangofa dziko lamalawi mudzakhala magazi chifukwa ife sitidzalola
Ndipo
ziko lomvesa Chisinau.mcp nonse mulungu akukatheni
Nkhanga zaona mumakwana pitilizani kuulula zobisika osasiya ayaluke abakha amenewa
Pena kumachita manyaz ukaziganizila kut ndiiwedi mmalawi dziko lomvetsa chison
ama funa kumupha ngat ana muphela clement chiwaya
Koma tinene zoona asilikali akumalawi sangangokhala kumayang'ana kagame akutumiza asilikali kuno ,athuwa adyesedwa banzi, chifukwa sizoona asilikali athuwa kumangozisiya zikuchitika pamaso pao ayi m'malawimuno tilibe asilikali otiteteza akwera chipani
We don't have soldiers in malawi
Pitilinzani kuunza anthu choona ndipo ziko liziwe choona chifukwa moyowu ukupitilira zigawenga. Malawi wake up, wake up. Iyi si Democracy ai,
Vuto ndiloti udindo waku Army amasankha ndi president kapena ndinene kuti ndiwandale chifukwa amasankha amene akufuna kuti azipanga zofuna ndikukomera iwowo.
Tsono mkulu wa army alipoyi ndiwawo.
Chifukwa how they bring army from Rwanda pamene ifeyo army tili nayo
Pamenepo asilikali nonse amene muli ku army simukuwona kuti president Yu akunyozani kuwoneka kuti inuyo mulibe ntchito ndiwopanda pake komanso kukunyozesani ku dziko lonse lapansi kuphatikiza ku Rwanda ko kukhala ngati Malwi ndi Rwanda number 2.
Ganizani bwino asilikali athu ndithu musawineke osafunika lero pomwe nthawi imene tinkapampanga ma demo kuti boma la DPP lituke mboma munagwira ntchito yayikulu kuti iyeyo Chakwera yo akhale President ndiye lero musakhale opanda pake kapena osafunika kapena ndinene kuti mukhale makape
Satana ndi olephera May God protect the dc
Amen
Chakwera dziko tinachita.kulipedza komanso tidzalisiya siunalikonze ndiiwe kunali kamudzu muludzi malemu bingu joice banda peter onsewo anavomeredza.ndipo anasiya .ndiye ndiiwe ndani kuti udzikatenga zigawenga kuruwanda kuti adzitiopsyedza ndizosatheka utafe ndiiwe ifeyo utisiya ndipo iweyo chakwera chaka chino chikakuthere kumanda utisiye tizikhala anthu tisakhale mwamantha mudziko lathu chifukwa cha chakwera 😂😂😂😂😂
Ndipo asilikali aku Rwanda atiopseze dziko lathu lomwe Mulungu Chakwera akuoneni ndi, ng'oma ija, mulungu wathu ndiwamoyo
Malawi wafika poipa ndipo tikapanda kusamala ana Athu azavutika
MR ntanyiwa mumakwanira
Nthawi ya Mlungu ikadzakwana adzachoka pampandopo pemphero ndiye chida choti tigwilitse ntchito kuti dziko lathu liyende bwino ka M CP ndikachani Achakwera adzatha ngati Farao
Asilikali osalanda ziko bwanji ,Kodi mayesa job yanu ndikuteteza anthu ?
Tsiku lomwe adzaphedwelo, nkhondo yayamba pompo
Kumalawi mumadziwa nkhondo?
Mulungu amutetezera boni kalindo sangamuthe chilungamo sichifa akunama kwambili
Ai radio ili boh
Zikateto anthunu kumavoteranso chipani choterocho kupha kwambiri. Akufuna kupha achinyamata onse. Nkhanga Zaona pitirizani kufukula zambiri.
Mfukuletso anthu amene abwere kuchita kafukufuku was ngozi ya ndege.
MCP ikatuluka m’bomamu mudzwe kuti simudzalowanso.Tinakuvoterani kuseri kwa ubusa poona kuti popeza ndinu oopa Mulungu,komatu zafikapa sindinu m’busa koma ndinu satana Ndipo ku ubusako mumangofuna ulemelero koma dziwani kuti Mulunguyo akukuonani ndipo posakhalitsa mulandila msautso oti muzazindikila kuti bolanso kumangodya therere m’midzimu.Mawu anga awa muzawakumbukila
Mulungu ndiwazatheka bwanji Bone Kalindo amulephera ndi Mwana wamulungu amene akutisegula maso Ife ana ama 2000 tithokoze Mr Mtanyiwa mulungu azikutetezani Kwa adani kut tizithabe kudziwa zomwe zikuchitika mu ziko lathu
Comrade Ntanyiwa - Be a good journalist please! How did Bon know CCTV is not working? Anyamata a DPP muknigrira ntchito yoipitsa MCP but don't forget what ana a dad were doing in LL? Bangwe &
Ntopwa 1
Asilikili amalawi amangowatuma kokalanda Makara basi ndikumalondera khalango basi not to protect the country
amalawi vuto timadana ndimuthu osati zochitika zake athu anamuda peter muthalika kuyikapo abalewa lelo ndi izi
A MCP ndi anthu omvetsa chison kwambiri nanga chifukwa chani sakuzifunsa kut the whole Malawi Born Kalindo kukhala patsogolo kulimbana naye sakumutha? Ndipo angozisiya
Ambuyetu Ali naye ndipo mulungu akumugwiritsa ntchito Ali ngati mose wathu ameneyo
Amalawi chonde tigwilane manja tiwomboleziko lanthuli komatu timawuzidwa kuti Mcp ndi yakhupha ife ana ama 2000 sitimaziwa
Ndimuuza Chakwera kuti wagwa mdzanja la Mulungu ndipo aipa kuposa Cinkhanira, Mulungu akugwetsa isanafike nthawi imene uiganizira.
Nkhanga zaona mulibhooo
Ndimabva kukoma ndi nkhanga zaona
Olomwam,bera ndalama kalindo musaganize kut akusiyan choncho kuyaluka muyaruka ndithu apolice otan inu minyeromwanu nonse
Achakwera ndimayesa munali busa apa mwawoneka kuti ubusa wanu unali wachinyengo bon kalindo akafa ndinu achakwera ziko lonse likuziwa ichi mulungu amuteteze amuteteze amutetezebe kalindo
Asilikali tilibe
Apolice akakhala chete kuthandidzira mcp kapena kut tonse government tidzikumenyan
May the good Lord continue protecting our president for the poor and his family, our expectations rely on God through him
Aphedwa bwanji .Kugomva kuti mcp ndi yokupha achakwela ndi boma lao ndi olephela basi guleyu wa vina watopa
Mwadzuka bwanji abale azanga pa nkhanga zaona, ngati mulibwino mulungu akudalitseni nonsense, ineyo ndili bwino, nkhanga zilipo?
I like this kanga zaona from Zambia
Kodi Chakwera alibe zochita zina , angokhalira kukonza plani yopha anzake padzikopo
Bangolini sangamuthe.Dc Dengelous child
Zikomo tikuziwa nawo pitilizani kutiziwitsa allah 24:48 bless you inshallah😢😢
Umbon otan nanyero iwe mot wekasukuona muyaluka ambilitu ndikuuzen
I love nkhanga zaona more fire mthanyuwa!!
Ambuye atichitire chifundo ndithu mmh
Mademo akhalaso liti I'm ready kk47
In Malawi is there any real defense force? Are they real soldiers? One thing Malawian people should, know is this during Kamuzu Banda, Kamuzu Banda was trying to erase Malawi defense force to Malawi young pioneer if you can remember very well, this is signal to that direction Malawi defense force must wake up now before it's too late look what is going on in D R C( CONGO 🇨🇩) who is behind the war there, is Rwanda under Paul kagame now Chakwera and his party are doing the same to bring that war in the country ,Chakwera is busy wagging the war in the country Malawian wake up now.
Kumalawi kulimbe asilikali guys tisadalile asilikali akumalawi 💪💪💪
MCP is a killer
Kkkkkkkkkk i like this program, from Moz
Ndalama sanatenge nthawi ya DPP bwanji? Zitsiru zina inu you think Kalindo is a god. Munthu angamuphere ku parliament? So do you parliament building izingokhala opanda chitetezo? Mumupweteketsatu nzimayi wapolisi osalakwa.
Iwe zmatengq process kupusa kwakoso
Phiriwake garu ngati ameneyu buzi yamwana
Amene zikukunyasa usamamvere palibe akukutuma kuti uzimvera
Asilikali salary yake imeneyo kumangosekelera mbwelerazo
Komatu zikuwonjezatu mmmmm
Mulungu ndiwamoyo Palibe chida chosulidwa chomwe chizambane
Mposo M'mene ziswera nkhangazo kuchuluka kwake amagwetu.....!
Tiuzeni zowona tidziwe zambili
ALLAH umutetesele boni kalindo
Chakwela ndichilima machende anu angalu anthu woyipha kwambiri
Dziko zomvetsa chisoni very sad
Mayo!!!!!zakazinanso 5 alamula?😭😭😭😭😭
yes i want to be on line with this channel
Zabodza zokhazokha
.... what kind of government is this
Amakachitako chiani ngati iye ndi MP.
Mmmmmm mabodza awa
Ulape ndi ndi mtsigoleri wakuphayi
Bwinotu bwino atha kuyaluka!
😭😭😭😭 ooooh Malawi 😭
Kod chakwera umaonangat momwe umatsogolera anthu mkachisi ndekut ukhozaso kutsogolera dziko lonse chonde bwelera kuntchito yako ya ubusa ndipo zomwe ukuchitazo mdzikomo mukhala kubu kogwiritsa dzida samala
May Almighty God continue blessing him with more life
Ndipo sizitheka
Manganya wasewelo ndi vas lelo
Eeee koma mavuto
Maganizo amuthu sichifunilo chamulungu
Nkhanga zaona akuti aliyese atenga chikwanje chake yemwe alibe agule akakukhapa nawenso uwakhape aliyense amve kuwawa😂 like your news Nkhanga pitilizani kuwona patali, may God protect the DC president of poor people.
Mavvto Malawi bon mulugu alipho
Umakwana bon