Koma Chakwera ndi achina Chimwendo Banda akuti boma likuyenda bwino kwambiri. Eeeeeeeee! Anthu awa sadabwere kuthandiza dziko, koma kudzadya. It's a shame. Achoke basi
Bwezi akulandidwa katundu ndi ndalama zomwe akubawa bwezi kubaku kutatha koma from 1964 up to now palibe ndi modzi yemwe adalandidwapo katundu ndiye chifukwa chake kubaku zikukutha kumawalanda katundu ndi ndalama zomwe basi
kumudzi kwathu kuno ku Malawi ndimadabwa kuti kodi bungwe limeneli la ACB likutani komanso why do we say that we have ACB yet corruption instead of coming down komano ili pa makwerelo kupita mmmwamba. mwachitsanzo passport ya MK50,000 kuti ifike mmanja mwa M'Malawi nde kuti akhala atagwiritsa ntchito makobiri opyola mk200,000. ngati otsogolera ali serious to deal with this nde kuti all juniors will be afraid. ndizovuta kuti katangale athe ngati otsogolera akupanga nawo.
Ndimbamva zokha zokha zimenezo mcp anthu onse anali alimi ndie atani anthuwo akhala ali pa ulimi kwa zaka za mbili ndie asabe Mesa khotse mu mteza simukuona pamenepo kuti mbuzi aimangilila pa mbale ndie mumati ingatani Mesa kungodya mbaleyo mowonongaso ka kuti mwai umenewu suuzapezekaso ka 😂😂😂😂
Katangale kuthi athe ndi mopweka vuto mukumasakaniza ndi school opezeka wapanga katangale asamangidwe koma amenyedwe paulu kumumangilila pa bwalo athu akuona athu atha kusiya
Katenga okhoza kutha ndinthu komano anthu akupanga dala chifukwa choti malamulo anthu Ali so week let's we say titati tipange lamulo loti aliyense ogwira ntchito m,boma akapezeka ndi mulandu wakatangale azipatsidwa ban kuti sazagwiranso ntchito m,boma mpaka kalekale. Ndithu vuto limeneli likhoza kutha ndithu
Vuto la boma ili ndiloti, onse, maka MCP representatives, anali amphawi okha okha.
Nkani pano Ali pa phwando la a kakowa
Kodi Ku Malawi kuli Anthu oona patali ngat inuuuu...for sure its true
Corruption can say goodbye if only the Anti corruption bureau becomes non governmental organization
Our Gorverment is lotain Asogoleli .anthu awa alibe umunthu othandiza ziko lawo
Ine ndikugwirizana zawo abambo ayambawo kuti bungweli lithe basi, likungowononga ndalama za boma.
Koma Chakwera ndi achina Chimwendo Banda akuti boma likuyenda bwino kwambiri. Eeeeeeeee! Anthu awa sadabwere kuthandiza dziko, koma kudzadya. It's a shame. Achoke basi
Bakili mluzi TV adanena kale kuti MPC yasakaza koposa😂
Inu ana amahule adana naye bwanji katangale mesa bambo ao analowa kwa mao mwachinyengo😂
Katangale atha kuthesedwa ngati atsogoleri ndioopa Mulungu moonadi munthu wopana kuopa Mulungu angapange bwanji chilungamo.ziko la Malawi likusowekera atsogoleri achilungamo. Chawiri ACB isakhale yisalamulidwa ndi boma. Chachitatu kumalawi tinakula kuti ukalemera anthu azikupasa ulemu ndichimene atsogoleri akuba ndalama akufuna ulemu
Bwezi akulandidwa katundu ndi ndalama zomwe akubawa bwezi kubaku kutatha koma from 1964 up to now palibe ndi modzi yemwe adalandidwapo katundu ndiye chifukwa chake kubaku zikukutha kumawalanda katundu ndi ndalama zomwe basi
Anthu onsewa adali osauka that's why
kumudzi kwathu kuno ku Malawi ndimadabwa kuti kodi bungwe limeneli la ACB likutani komanso why do we say that we have ACB yet corruption instead of coming down komano ili pa makwerelo kupita mmmwamba. mwachitsanzo passport ya MK50,000 kuti ifike mmanja mwa M'Malawi nde kuti akhala atagwiritsa ntchito makobiri opyola mk200,000. ngati otsogolera ali serious to deal with this nde kuti all juniors will be afraid.
ndizovuta kuti katangale athe ngati otsogolera akupanga nawo.
ndi boma la mbava zokha zokha zakatangale ndi kupha chakwera ndi chigawenga cha kuba ndi kupha
ACB yili ngati nthambi yoyima payonkha koma boma Lili NDI mphamvu kuwophyeza kuti milandu yisapite KU court.
Waste of money KU ACB
Kodi kumalawi kuliso boma inesindikuona boma soapa ndikuona mbava
Ayi osati osaukafe koma umakhala munthu utatopa ndikuyemdera that is why umangopeleka ka deal kkkkkk koma zoona chakwera mmmm
Moti kuti munthu awadzudzule akum'manga, what type of government is this.
Evil government full of intimidation and hypocrisy
Mtsogoleri sayenera kuyang'ana nkhani yakatangale ndi nkhope yachisomo ayi. Apa pokha akuyenera atchedwe kuti dictator pofuna kupereka mantha kwa onse oganizira zokachita mnchitidweu. ACB payokha singakwanitse. Komanso katundu ndi ndalama zidzibwezedwa ku thumba la boma, kuti zitumikire moyenera.
Mmmm mm koma kumalawimu
I wish it's high time boma limayenera kuganizira zosintha malamulo athu okhuzana ndizakatangale ndikuika zilango zokhwima osakhala izi zomangoti basi abwenza ndalama ndiye takhululikira kapena akamangidwa kungokakhala Chaka chimodzi kenako aziti amachita behave bwino ndiye boma lawakhululukira, mmene tikupangira ndimilandu yogwililira kapena murder zomwe zomwezo zitabwera kukatangaleku, munthu azikakhala even 9 years alipa alimand anthu tiziopa kugwira chaboma,panopo chinthu chomwe chikutisaukitsa amalawi ochuluka ndikatqngaleyu,ine ndimaona kuti mmene tinathana ndiulamuliro wankhanza wachipani chimodzi wa MCP ndimaona ngati pamafunika pabwere Chihana kapena Muluzi wina yemwe angatimasule kusinga zomwe zatimanga kukatangale
Nthata za njala izi ndipo mistake yomwe tinapanga a malawi mulungu atikhululukire ndithu...
Ngati anabisa black box kulibwanji report ya Chilima?
Ndimbamva zokha zokha zimenezo mcp anthu onse anali alimi ndie atani anthuwo akhala ali pa ulimi kwa zaka za mbili ndie asabe Mesa khotse mu mteza simukuona pamenepo kuti mbuzi aimangilila pa mbale ndie mumati ingatani Mesa kungodya mbaleyo mowonongaso ka kuti mwai umenewu suuzapezekaso ka 😂😂😂😂
Katangale sangathe chifukwa ose ali m'boma akuba
Kupeza apeza nanga akupangapo chiyani pofuna kuthana ndi katangale?
Katangale kuthi athe ndi mopweka vuto mukumasakaniza ndi school opezeka wapanga katangale asamangidwe koma amenyedwe paulu kumumangilila pa bwalo athu akuona athu atha kusiya
Chakwela you mast go
Katenga okhoza kutha ndinthu komano anthu akupanga dala chifukwa choti malamulo anthu Ali so week let's we say titati tipange lamulo loti aliyense ogwira ntchito m,boma akapezeka ndi mulandu wakatangale azipatsidwa ban kuti sazagwiranso ntchito m,boma mpaka kalekale. Ndithu vuto limeneli likhoza kutha ndithu
Pakufunika kusintha malamuro ena ya dziko lino, munthu akapezeka ndkatangale anyongedwe bas mzaona kuti katangale wayamba kusika chifukwa anthu azawopa kufa, komaso acb ithesedwe chifukwa palibe chimene ikuchita.
Basi tu kusazikana kumeneku achakwera muusiya mpando bola tiwone amanganya wo
ACB is useless
Atsogoleri kuyambira 1994 akhala akuba ndalama koma milandu yawo siyithera Kuma khoti.
Ndiye justice system NDI useless chifukwa amavomera kutseka milandu popanda chigamu
Cover the boss
Chakwera must go
Ife izizi tatopa nazo ameyo achoke basi. Chifukwa mmutu mwake mwadzadza mamina.
So sad💔💔
Mabodza okhaokha
Achoke
katangale m'malawi mkovuta kutha chifukwa president ndi nduna amapatsidwa mphavu zambiri so mkovuta kut zinthu zina zikomzeke m'malawi muno
Pali boma limene lingabwere lopanda katangale palibe chachilendo zidalipo kaleso
Bwana apa zawonjedza koma inu muli dziko liti....tatiyeni. Tizimvako chisoni plz plz
@@GospelSoldiers-sr7np mpata ulipo ositha boma koma musaganize kuti mavuto amene alipowo angathe
Tingovomela mavuto kumalawi