We Are In The Age of Politics of Ideas - Kamlepo Kalua

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 26 сер 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Rumphi East Member of Parliament Kamlepo Kalua proclaims that Malawi has entered a new political age characterized by the Politics of Ideas, not the politics of intimidation, killings, political violence, and political arrests.
    Pa Nyasa VoiceBox, phungu wa ku Rumphi East a Kamlepo Kalua walengeza kuti dziko la Malawi lalowa munyengo yatsopano ya ndale yomwe imadziwika ndi Politics of Ideas, osati ndale zoopsezana, kuphana, ziwawa za ndale, komanso kumanga ndale.
    #malawi

КОМЕНТАРІ • 16

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Місяць тому +1

    Powerful words Veteran Kamlepo ndipo chakwera pamodzi ndi Chipani chake ca MCP akuyenera kudziwa kuti 2025 ndi Ulendo wa kundende bas coz Malawi sadzalora kuti Nyau imeneyi tidziyiwona koma iye ndi nduna zake onse waku maula..

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 Місяць тому

    Powerful message Mr kamulepo.your matured in politics and you come from far with it.and I wish all politicians must listening to this message especially oppositions,there is a sense in this massage.mr Bakili muluzi,Mr chihana of afford,peter mutharika,and other Presidents of parties come together and join your friend to take back this nation to democracy.we need piece in Malawi not what mcp need.may God Bless Malawi and rescue to evil spirits from MCP government.we are patriots.God we seek your help in Malawi.

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Місяць тому +2

    You're the icon and true meaning of democracy in our country.
    If they have ears to hearing, let them hear your message but if they choose to be stubborn, then God, will strike and plunder them.
    Mwana wa John Tembo iwe ku MEC komwe uliko, as Malawians, we all know why Chakwera elected you to be on that position with the aim to help him win the elections simply because you're both MCP fans and also that you meet underground. You've already proven it with your speech at the press briefing which you held previously that no 🆔 no voting. That's nonsense.
    Be very careful of the deeply wounded Malawians. You will run away from Malawi if you try to a messenger of Lazarus Chakwera.
    Be warned

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa Місяць тому

    Bravo Comrade Kaluwa we're with you

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Місяць тому

    Good message Mr Kamlepo

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Місяць тому

    Good Messnge Mr Kamulepo ❤

  • @Standwell78
    @Standwell78 Місяць тому

    Liabunya analandila kale zoti azibweletsa zanyoo

  • @lyiemax
    @lyiemax Місяць тому

    Powerful!!!!

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Місяць тому

    Amadana ndi inu ndi zigawenga bigman ma plan akupha otsutsana nawo ndiko kulepherako osaopa osatopa bigman.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Місяць тому

    Awa MCP tisamvele za ID iwowo akudziwa kuti ma ID alembetsa achewa okha nde pokuti adzinena kuti alipo 14 million chonde chonde chonde amalawi dziwonetselo a ma ID ayi mukalola otsusa chanu palibe ndinthu komatso muyika malawi 🇲🇼 pamoto 2025 itsaluwetso boma mcp koma zoti opanda ID ASALEMBETSE AMALAWI TISALOLE TIKUFA 2025 NDI MCP IYI

  • @braveglorymwanzagolah4899
    @braveglorymwanzagolah4899 Місяць тому

    Listen up

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope Місяць тому

    Kuyankhula kwa nzeru

  • @happychimtedza3873
    @happychimtedza3873 Місяць тому

    Tamva

  • @user-bg7ur1gw1q
    @user-bg7ur1gw1q Місяць тому

    Odana ndi kamlepo wadya banzi

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev Місяць тому +1

    Akamulepo munali kale munatha inu.panopa mungokhalira maboza

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev Місяць тому

    Nthawi ijaso unkanama kuti dpp yakupanga kidnap pomwe it was staged by yourself.panopa ukuti mcp through zikhale akufuna kukupha how special are you? Munabalalika inu thats why andale anzanu sakukufunani chifukwa they dont trust you.muja munayamba ndale ndikale kwambili bwezi simukufumabe sympathy kwa anthu.pangan retire madala fundo mulibe panopa mwatha.