Politicians In Malawi Learn to Tell the Truth Mukalephela - Samuel Lwara
Вставка
- Опубліковано 12 вер 2024
- In his latest audio Samuel Lwara pleads with Malawi politicians to learn to tell the truth when they have failed to lead the country.
M'mawu ake aposachedwa a Samuel Lwara apempha andale ku Malawi kuti aphunzire kunena zoona pomwe alephera kutsogolera dziko.
#malawi
You're a great man with an idea
Powerful Mr Lwara
Zikomo munthu wanzeruwe Samuel Lwara I salute you bwana
Eish imfa ya Dr Chilima I kupweteka tsiku ndi tsiku mutu kumachitakupweteka Rlp
Another Born Kalindo's brother from another mom
Powerful massage
Powerful talking
Ndege inali yabwino bwino koma inali plan yoti aphe Chilima thats all!
Powerful,Lwara ,you deserve respect
Powerful
Powerful indeed 💪
namuwongani dada chiuta wamutumbikani
Tikamanena wisdom ndi izi munthu uzivomereza zikavuta or uli pa position yotani accept ngati walephera
Where is osward jumani
Kweni unapamulomo😂😂
Where is Lyton Mangochi we miss him for his commitment to democracy
Don't talk about laytin men!, we don't need to hear anything about dat stupid crocodile, I'm saying dis coz dat guy is a hypocrite and he don't deserve to be a freedom fighter
Lyton mangochi zakudya Kaye ndalama ndi azikhale, chambiko nda chikuni anatelo oyimba Ena
Malawi in not a lawless country,if you break the law,u will face the music.mukati asamange anthu nde likhala dziko? mkwiyo ochotsedwa mnyumba ya housing uwu😂
Yes is not lawless country but Mcp take law in their hands ✋. This is also democratic country Mcp must respect this too and we can not accept this nonsense of arrest innocent people!
Iwe lwara wabwera tsopano tikufuna anthu ngat inu
Obwelesa mvula si azibusa ayu maan inuu, mvula amabwelesa ndi MULUNGU
Akulu inu, wat's ur point?, ngat munalibe blackbox, chimayeza temperature mumlengalenga mchiyani?, nanga mafon awanthu anafa mundege aja munalibenso?, nanga chilima anakapezeka 200 metres away from the place were the plane wer crushed y?, why chilima anapezeka alibe zovala chikhalirecho anali mu suit, and y anapezeka ndi mabala akuluakulu azikwanje mumiyendo yake😢? , eish!,
Hmmm mulungu athandize ndithu. Kuyankhula yankhulaku kukubwera chifukwa cha mabodza omwe president amatiuza zokhudza za ndegezi. He knows the truth but God will expose him
@@LeendaDeborah2005 data true , and they know wat they dd on dat day and the truth will review
Ndikudabwa adada wachitumbuka uyu akutukwana mafumu anthu komaso zimene akuyankhula onse amene akutukwana pano ali ndi zifikwa zawo iwe ukukakamila kukhala mnyumba yaboma undamange nyumba yako kumzimba uko nyumba zikuntchipa basi mpaka nalelo nyumba mlibe mkatukwane mafumu chikwa cha ndale mbusa uyu nyo ngwakutangwanika chomene ndicho chifukwa wakakangama na mamembazi ake siwosankhidwa ndi mulungu ayi .
Anthu ena owona patali akusungila serial number ya black box yomwe inali mundege yomwe inapha chilima, nde iwe ukuti munalibe black box, stop confusing the pple
Akatolika ndiwozindila not enanu
Adanena kale kuti mudalibe black box
Mtitole Makola 😂😅
Ngamo yonkha yonkha
Inuso ndiachitsilu papitapo zaka 4 chakwera akukwela yomweyo, bwanji ndege simagwa.lurwa nanuso point yanu siikuziwika mukuikila kumbuyo boma pena ayi,nde ndinu opepela kwambiri, bola kalindo amanena zomveka.