Chakwera zimene wakwanitsa kupha chilima basi palibepo chimene akupanga komaso nanga asikali Aja Amati azapanga ma video ya momwe chilima alikuti anthu Aja chonde asawaphesotu
Let me correct you in Mzimba sugar ndi k 2495 in big mart shop ya fair price Chakwera dziko lamukanik passport anasiy kupang ndet only in lilongwe zoona zak achinyamat ntcht njee Achoke I will support that
Abwana president chakwela Ali ngati chidole kapena kuti katuni ena amagomungwila ntchito zaumunthu uyu mulibemo ndipo ndi khutukumve chakwela wa mwazi uyu
Iwe galu iwe watikwana sopano wamva tadikila next year kuti peter mthalika wakoyo azatenge boma ngati angazalongosole zithu.mesa peter yo akuzimvela ma propaganda anuwo.
Onse akumapanga ma comment opusa si dzika za ku Malawi palibe munthu amene angakondwe ndi dziko la Malawi mmene likuyendela pano tiyenela tikonze dziko osati kumangopanga ma comment opusa ayi zautsilu basi
Choka galu iwe chikukupangisa iweyo kukhala dzika kwambili ndichan? Kunziva u malawi kwambili? I will counter attack thy way i want iam also a malawian citizen stupid cadet.achipeleke chizikocho kwa mlomwe nzanuyo ngati iyeyo azakupaseni zinthu zaulele fotsek
Tikhara kuti tikungotukwana bas pa social media sizitithandiza Ife tingopanga zoti Mulungu atione ndikutivera chisoni basi Tizizivera chisoni kuti Mulungu atikhululukire
Best of the best bakili muluzi tv
Anthu Andale ndiabodza koma awawa eeeeeee awonjeza kwambiri
Watching from Zimbabwe
I like this TV keep the fire burning dude
Akutivutisadi ng'azi ameneyu 🐬🐊🐊🐊🐬
Yes mwamuza zona ZIKOMO kwambili potiziwisa chikhalidwe chake
Ine n'saname Chakwera amandinyasa
Kkkķķ😅
Chakwela ndi mfiti kwabasi
Olo chimodzi palibe chomwe wapanga iye, 30minutes olo itakhara non stop sizingatheke ayi ,
Akwanilitsa bwanji kupanga zonsezo ndalama akupatsa anthu akunja kumalemba anthu aganyu Kuti azimpha anthu ndalama zake zomphela anthu
Best TV ever..may God continue protecting you Bakili Muluzi TV
😅😅😅😅koma anthu.inu musandisekese akut akaziwo mimba nguuu ngat mbuzi yakhuta mphale yokuba
😂😂😂😂😂ati kagowero kkk km naseka bwanji
Boss mwaiwalatu chitukuko China chomwe MCP yapanga kupha Ralph ndi Chilima
Afune asafune 2025 azaluza akumkuyu akumpusitsa kape wawoyo
Onse ndi amagazi mmanja kumkuyu sakudziwa comwe akuyakhula
Ifee nga ngaa nga nga pambuyo pa ngwazi yamuyaya Dr LAZURUS CHAKWERA wathu wokendedwa 🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤❤
Galu wachabechabe iwe
Chokani apaa mwana wang'ona iwee, mwapha chilima asatana inuu 👹👺👿☻ , kunali ng'azi ina mdzaka zammbuyozo mumkaitchulanso kuti ngwazi, , lero alikuti?
Aaaaa koma kunena zowona kutengela mmene analonjezela zambiri szinatheke 😢
Best tv bakili muluzi
Best TV station in Malawi so far.
Ndaonadi nkhope yamfitidi
Akunamizana akuti awina ndipo sawina anthu ameneyo ndipo azafa ndi mtima ndithuu my vote for Dpp hoyee
Mr Kamwendonjira okudya Matako agaluwa sangawine Chisankho in the Next Polls
Kkkkkkkkkkkk koma brother mumatha Inu mudzangokhala president ndinuyo chaka chikubwerachi
kumkuyu ma chende abambo ake chakwera ndi mcp ndizigawenga za kupha anamupha chilima mcp ndi chipani chazigawenga zitsiru zokha zokha
Chakwela mumuone khope yakeyo chigawenga cheni cheni akakhaka mkaka ngati wagwa kotamba
Ali Maso rwaa! Ngati Nazikambe kkkkkkk koma Manganya😂😂😂
I trust bakili muluzi TV always because is talking true
We really appreciate for this channel
😂😂😂 bon voyage kkk da gama emweyo wa gowelo
Kunkuyu mapwala ake ndithu
Kunkuyu umve zimene ndikunenazi,, iweyo ndi amene akumuuza zabodza chakwera wakoyo. Achakwera mumve Mau angawa,, kunkuyu akukunamizan ndi mfundo zake zopeperazi. Chifukwa iyeyu akukulimbikisan kukuuzan zabodza zomwe amalawi Eni ake sakukondwera. Muzafa ifa yowawa.
Bakili TV number one ❤
Kkkk ati kamuyenda njila anadya matako agalu.nde ndi nkazake ngt otupa mutu uja😂
Kkkk 😂😂 khaniyo ndiyowona amange gowelo bs zachamba bs
Zomwe wakwanitsa ndi kupha ndikumanga osalakwa
Best TV in Malawi keep
Koma ada awa amatha kwambiri, kuwelenga mwachifase ndimodekha
Tamulimbikiseni nkhani yomanga gowelo Ku airport komwekoyo😂😂😂
Iwe ndi one❤
Ndiana sakuziwa kathu auze mwina aiwala. 😅😅😅
Chakwera chomwe wa kwanitsa ndi Mabokosi AMALIRO osati chitukuko Chitsiru cha munthu .
Chitumbili chingwile pangali mbwaa in 2025😂
Chakwera tatopa nayo bolani afe basi anthufe tatopa naye kwambiri
Mcp izalila maliro onyamula wina azathawa malawi akufuna
Chilichonse chamoyo chikàmaphedwa sichilephela kuphupha chikamafa , umu ndimomwe chikuphuphila chipani cha magazi cha mcp killing party
Chakwera waononga dziko la Malawi .angongwetsa kwacha mosanganizira anthu osauka
Koma pa udindo wa upulezidenti uja umafunika kukhala okhwima nzeru.😂😂😂akt amakajambulitsa zithunzi ku china akazawo Ali pompo ..
Kkkkk akuti umange gowero Garu iwe
Thanks brother for news
President uyu ndi pa nja penipeni munthu osadziwa chimene akuchita ndi munthu wanji
Sindikudziwanso Kuti ndiophunziladi uyuuu
Kunachita kuyiwala zomwe alankhula dzulo zimayenda Koma mkalasi munthu ameneyu
Keep it up brother man!!
They ,MCP are playing too much with lives of Malawians ,but God is watching
Chakwera Kodi sigaru ameneyu
Yakwia ndi mizimu
Zoonadi amange Gowero ku Airport komweko.
❤❤❤timakunyadila man kwambiri tione ku lsrael ndi ku Russia zikuti bwanji kumeneku
Komanso Mzuzu airport Ngati airport ya witchcraft kkkkkk
Kkkkk chitukuko chake ndi kuba 😅😂😂
Abwana bwanji mzakhale president zikuwoneka kut muli ndi nzeru zoti mngasinthire znthu
Powerful long live bakili muluzi TV
tafufuzani za ku Burkina Faso kuli president wazeru kwambili mutibweletse mbili yake bg man
Yes plz
Chakwera zimene wakwanitsa kupha chilima basi palibepo chimene akupanga komaso nanga asikali Aja Amati azapanga ma video ya momwe chilima alikuti anthu Aja chonde asawaphesotu
Akadzi Ake kamimba ngu Ngati mbudzi yakhuta mphare yakuba 🤣🤣🤣
Zoonad MCP singawineyi, thanks bro for informing us
Kumukuyu alibe ku immigration anthu akuvutika kwambiri komaso kuba passport amati yikhala k50,000,pano ndi k500,000
😅😅😅 at bola Vasco da gama 😅😅
Welcome bwana for today again
Amen ❤
Kunkuyu ndi mfiti otheratu
😂😂.😂 Chilichonse chakwera ndichakwera adatelo APM
😅
Let me correct you in Mzimba sugar ndi k 2495 in big mart shop ya fair price
Chakwera dziko lamukanik passport anasiy kupang ndet only in lilongwe zoona zak achinyamat ntcht njee
Achoke I will support that
Iwe aise video iyi ndiyakale wamva galuso iwe eti uzingoponya ma videos akale kale
Iwe osamaba za bakili muluzi tv
Abwana president chakwela Ali ngati chidole kapena kuti katuni ena amagomungwila ntchito zaumunthu uyu mulibemo ndipo ndi khutukumve chakwela wa mwazi uyu
Ķķkkk chitukuko chake ndi kuba😅😅
In fact chakwera nd mbuzi
Dziko la Malawi silidzasithaso ngt atsogoleli anthu sadzasintha
Kkk koma ndaseka yandibaya yomanga kagowero ku ku airport
Kumkuyu ndi Mr nonsense
Ndipo Mcp sizalowaso mu boma
l,m watching from .am angry with Britain .mcp never win
Ine ndikanakhala peter ndikanangozitaya kuti apume kutukwanidwa.mwina iweyo nkuzakhala minister galu iwe.
Video iyi ndiyakale tinayiwonela kale
Bakili mulizi❤❤❤❤
Amangilen pofikiladi abusawo nkhosa zikudandaula busa amanthawa😄😃😄😃😄😃
Inu ndinu heroe bwana ,MCP isazabwelere muboma kufikila titafa chifukwa muwaru,gadama,solobala ,chilima,chisiza anaphedwa ndi MCP komanso amatenje
Iwe galu iwe watikwana sopano wamva tadikila next year kuti peter mthalika wakoyo azatenge boma ngati angazalongosole zithu.mesa peter yo akuzimvela ma propaganda anuwo.
Kodi anthu ngati inu Mmakonda kulowa mma page ndikumapanga ma comment opusa fukwa chani? Za usilu basi ngati mwabwerela pano ma comment awusilu Manyi anuso
Onse akumapanga ma comment opusa si dzika za ku Malawi palibe munthu amene angakondwe ndi dziko la Malawi mmene likuyendela pano tiyenela tikonze dziko osati kumangopanga ma comment opusa ayi zautsilu basi
Choka galu iwe chikukupangisa iweyo kukhala dzika kwambili ndichan? Kunziva u malawi kwambili? I will counter attack thy way i want iam also a malawian citizen stupid cadet.achipeleke chizikocho kwa mlomwe nzanuyo ngati iyeyo azakupaseni zinthu zaulele fotsek
Good good continue
Following 😊
Nice one
He has forgotten about the boolet train your just reminding him now poor Malawi that used to be a milky and honey country shame on us 😂😂😂😂
99 percent ya anthu ma comments section atopa ndi amcp adzawina bwanji mavote
Apanga post not bakili muluzi page yake ai nokha simukuona inuyo
Kkkkkkkk koma amangedi ka gowero ku airport azigonela komweko
Akapume atisautsa mokwana agalu amenewa
Kkkkk khani ndiyomanga gowero ,
Mosses ndi mmodzi mwa afiti mmalawi muno.
Bwana kumanena kuti mwamaliza 🙄😫
Amangokhala chateee😂😂😂😂
Kkkm
Ichichi Cha bakilichi ndi amdala mitunda isanu
Kkkkk Anyamata tilipo ife timanga ka Gowero Bro 😂😂😂😂
Tikhara kuti tikungotukwana bas pa social media sizitithandiza
Ife tingopanga zoti Mulungu atione ndikutivera chisoni basi
Tizizivera chisoni kuti Mulungu atikhululukire
Palibe chimene akuchitawa awa