Zomwe wayankhula Waxy Kay pa Maliro a Bambo ake a Bishop Kapenga ku Robins Park in Blantyre

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 1 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 74

  • @JOHNOlesmasCosmas
    @JOHNOlesmasCosmas 2 дні тому +20

    imfa ya munthu olungama pamaso pa Yehova pamakhara chimwemwe zilibwino indeed
    waxy mzimu wa Yehova ukuyankhura iye wangokhara chotengera chake
    may His soul rest in internal peace 😭😭😭

  • @ListerMunthali
    @ListerMunthali День тому +9

    Ndikukumbuka mu ulaliki wina wake bishop kapenga ananena kuti ngati situation ndiyoti sungayisithe no matter what, osalira just say zikomo ambuye.
    Pachifukwa ichi nane ndikuti zili bwino ndi mzimu wawo for God has relieved him from all his pains🙏

  • @user-pn7cj9hb3t
    @user-pn7cj9hb3t День тому +8

    Chomwe walakwitsa Waxy Kay ndi chani anthu inu? Kapena simudziwa mau simudawelenge?

  • @WellosMphonde-wd2cx
    @WellosMphonde-wd2cx День тому +3

    Munthu akamwalira kulira kumatanthauza kusowa chiyembekezo pamene mau ake a Mulengi amati tisalire pakuti mu zonse tidziti zilibwino nde mukati speech yolakwika nde kuti chani. Lolani akulimbika mtima akhale akulimbika mtima pakuti ndi mawu ndipo mwa mawu tidzachuta mwa mawu. Say Amen/Ameen

  • @user-uo3lm5wl5j
    @user-uo3lm5wl5j День тому +5

    Ifa ya wamuthu olungama kumwamba kuli chimwemwe mwAna wazelu kwabassi ndiwochepa agazindikile mawu wayakhula mwanayu Kwa amene amakhululupila mulungu wava tathsuzo lake amen

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub День тому

      Ndipo imfa ya munthu oyera mtima imakhala yokoma chifukwa amakhala akudziwa za komwe akupita

  • @AnthonyChibwe-bf4de
    @AnthonyChibwe-bf4de День тому +4

    He has to say so,, there is no way kut azikhala akudandaula yet zinthunzo zachitika kale komaso sangathe kuzibweza pat. Mmalo moti azingodandaula wasankha kusangalala that's a good choice or adakayankhula zodandaula zidakasintha chan? Umenewo nde umunawo mesa,

  • @ALINAFEMKOMERA-cm1md
    @ALINAFEMKOMERA-cm1md День тому +2

    He got broken... He wrote a status he was comforted that he should be strong since the father is in a better place
    Now he is strong anthu muyakhulisaso
    Mumtima akuliratu munthuyu

  • @FlorahBanda-fl4vf
    @FlorahBanda-fl4vf 2 дні тому +7

    Speech iyi ndiyofunika azungu koma ife tiziti mwatilawula😢

  • @samuelkapasula-mn6es
    @samuelkapasula-mn6es День тому

    Zoonadi.....Zili bwino mwa Yesu khristu.....

  • @RedKoffii-gl2vx
    @RedKoffii-gl2vx 2 дні тому +6

    Mwana ulimba mtima

  • @thokozanisukah6448
    @thokozanisukah6448 2 дні тому

    Indeed zili bwino aliyese azafa komano kuluza munthu sichithu chophweka nde kumankhala makolo ako

  • @WakisaPhiri-e1e
    @WakisaPhiri-e1e 2 дні тому

    RIP Pastor 😭 Anthu awa amkavana

  • @ZaffboyYellows
    @ZaffboyYellows День тому

    I'm very sorry 😢Your highness young king. If you want to talk ' I'm here at any time

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 21 годину тому

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤

  • @Choicemlw
    @Choicemlw День тому

    Yesu analira pa maliro a Lazaro

  • @user-wz1jy3uj8p
    @user-wz1jy3uj8p День тому

    ❤❤❤❤❤❤

  • @POker_On1.
    @POker_On1. День тому +1

    Zibwíno 🙏🏾

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e 2 дні тому

    Owooo chabwino

  • @chemapa
    @chemapa 14 годин тому

    zabodzazo zosamvekazo Mulunguyo anamuuzira kuti? pamaliro sitchukira. tisamaseweretse dzina la Mulungu. kulowetsa chibwana pamaliro a mtumiki wamulungu.

  • @nkosikhonasiphiwemdlalose227
    @nkosikhonasiphiwemdlalose227 2 дні тому +1

    Some of the tribes in Zim they celebrate when they lose someone zili bwino akapumule ali ndi Yesu wao

  • @SinyoroMoyo
    @SinyoroMoyo День тому

    Chitsiru chamwana ,nde chojowera-jowera ndichani .ngati zili bwino osangoyankhula bwino bwino kupereka ulemu kwa anthu ena bwanji.kufuna kutchuka ndi uchitsiru udzazindikira bwino patsogolo

  • @CatherineKumwendaCatherine
    @CatherineKumwendaCatherine День тому

    Kwa munthu oti amaziwa za kumwamba mwana wayakhura zomwe Mulungu amatilimbikisa pamavuto or pa Mtender tiziti zili bwno

  • @unarinematshomo2841
    @unarinematshomo2841 День тому

    Muthu akamwarila, timarila pa nthawi imeneyoyo, ndee waxy kay sanalakwitse moti speech yake ili bho ndithu.

  • @OwenTembo-xq6ug
    @OwenTembo-xq6ug 2 дні тому

    Sizilibwino ndizolilitsa kwambili 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @MDAmir-ku4lf
    @MDAmir-ku4lf 13 годин тому

    Waxy akunena zoona, mau a munthu okhulupilira ndi oti zilibwino. Abale amzanga munthu akamwalira sinthawi yoti ife tizilira ndi nthawi yosangalala chifukwa chani ndikuyankhula choncho, chisanzo munthu akamagwira ntchito kaya ndi pa company kaya m'boma amayembekezera kuti mwezi ukatha akuyenera kukalandira salary, ndiye funso nali, ndindani amene amapita kokalandira salary akulira tipeza kuti palibe wina aliyense amakhala osangalara kuti lero tikadyera nyama, ndi chimozimozi inu ndi ine mulungu anatisankha ndikutisiya pano pa dziko lampasi cholinga chimene anatisiila pa dziko la pansi ndi chani tizimugwadira nthawi ndi nthawi, ndiye tamugwadira mulungu, mwini wake emweyo yemwe timamutumikira uja watiitana tamwalira ndicholinga choti akatipase malipiro pa ntchito yomwe iye anatipasa takhala tikumugwilira tidakali ndi moyo abale amzanga sinthawi yomalira imene ija ayi ndinthawi yotchulusa kupempha kwa mulungu kumupemphelera m'bale wathu kuti ngati anali ochita ntchito zabwino mulungu amuonjezere zabwino zochuluka pa ntchito yomwe iye anali kugwira adakali ndi moyo komanso ngati anali ochita ntchito pena zoipa mulungu asachulukise kuyang'ana zoipa zake Ameen

  • @kondwanibuleya-br9gr
    @kondwanibuleya-br9gr 2 дні тому

    😢 what a man up

  • @jamesbowman-cw8ts
    @jamesbowman-cw8ts День тому

    Koma ndiye Kuli mixed bag of comments,... Waxy this Waxy that,... aMalawi musiyeni mwana, walimba mtima ndi chiyembekezo kuti bambo ake ali malo abwino opumula ndi Yesu wawo ndipo palibe chodandaula,... Ndiye mukuti chani anthu "abwino" komanso osunga "chikhalidwe" chachiMalawi inu??
    Pena ngati ndinene kuti dikirani abambo anu akazamwalira muzayankhule speech yanu yabwinoyo,....koma poti imfa si yabwinonso. So whatever,
    Rest well Bishop Kapenga. We knew as man of God and we're sure to God your soul has returned. Rest Bishop rest🕊️🕊️

  • @Mphatsolikotima
    @Mphatsolikotima 2 дні тому

    Rip bishop kapenga 😢

  • @GetrudeGama-gu5rb
    @GetrudeGama-gu5rb 2 дні тому +1

    Zowonadi ziribwino kwaiwo kwantha kwatsara kwaife

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu День тому +1

    Osamamuchemerera mfanayu ndikape chisiru paumunthu speech umatulusa malingana ndimaro ache awa anali bambo ake osati ngt kanali kushow koziwonesera kt kaya akazi akafire zachamba

  • @BestMtawali
    @BestMtawali День тому

    Ndalama unadya zacosoma zja nyimbo zake ndizit unaimba?????😩😩😩😩

  • @jelblinds2017
    @jelblinds2017 15 годин тому

    There is nothing wrong jst that we as malawians have poor and shallow minds

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 21 годину тому

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤
    0:11

  • @Tryness-wb6dj
    @Tryness-wb6dj День тому

    Rest well Bishop Kapenga

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 2 дні тому

    Wavala mzimuwamji mwanau

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3q День тому

    Km ine kaya ndi chimodzichi km speech yi sinandivekere mwaumunthu

  • @AneesaMoosa-nv6bq
    @AneesaMoosa-nv6bq День тому

    Rest in peace bishop kapenga

  • @JosephJosab
    @JosephJosab День тому

    Ku show kapena maliro

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa 2 дні тому

    Sitinazolowele spech ngati izi kuno kwathu

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm День тому

    Mwana wamuna azikhara olimba mtima choncho waxy mbiri yako yabwno umakhara bwno ndi bambo ako ambuye akuze malire amoyo wako ndi abale ako😢

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 21 годину тому

    Mau abwino kwa munthu olungam

  • @maxyfreeman9691
    @maxyfreeman9691 9 годин тому

    Kaya mwanayu sanasute koma

  • @eltonnankhwere3284
    @eltonnankhwere3284 День тому

    Of course am satisfied with the speech it seems unakonzeka ngati ukupita
    ku show.i remember you wrote kuti tiyeni mawa tikakumane pa Robins Park ndikaimba nyimbo in other way its not fitting

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 День тому

    Wakhutu la uximu wanva

  • @ShyreenKwisongole
    @ShyreenKwisongole 5 годин тому

    Emen

  • @billykamwendo6517
    @billykamwendo6517 2 дні тому +1

    Ife ndi a Malawi, izi nzachizungu ndipo naaa ine sindingayankhule chonchi ali oti ndi bambo anga.

    • @TadalaChithope-yg9fo
      @TadalaChithope-yg9fo День тому

      Azibambo nthawi zambili amakhala olimba mtim and uyuso panja mean oyamba ayenela kukhala strong komas tiyamike kut bambo ake amwalila waxy atatembenuka mtima komas kwaimayife zovuta kom kwa mamun ngt uyu akudziwa chomwe akuchita komas mwa okhulipilila izi zosavuta ngt munawon live yadzulo mayi ake okhala akaz awo anayimba nyimbo xa phamvuso coz ndi anthu okhulupilila and akudziwa kut akuyakhula mulungu wawo

  • @HussainGaffarOlaiza-hy9sg
    @HussainGaffarOlaiza-hy9sg День тому

    💔🕊

  • @DJcliffBandakhudzanga
    @DJcliffBandakhudzanga 2 дні тому

    Waxy ndi nfana olimba mwana wamamuna adzitelo

  • @mikemakamo7360
    @mikemakamo7360 День тому

    Koma mwana wakondwelatu 😂😂😂
    Zotindipamalilo wayiwala yoh mphamvu ziko likulowa bola

  • @marryrobert7092
    @marryrobert7092 День тому

    A malawi uziwa kurangiza mwana warakwa chani kod simuziwa kuti muthu akafa sibwino kurira mokweza ndemumatu iyi azirira

  • @FranckieDambah
    @FranckieDambah День тому

    Eeeeee waxy umatha kuyankhura

  • @MarthaMfulusa-vj3xe
    @MarthaMfulusa-vj3xe 9 годин тому

    Strange

  • @daziana2023
    @daziana2023 2 дні тому

    Zilibwino

  • @TadalaChithope-yg9fo
    @TadalaChithope-yg9fo День тому

    😭

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 День тому

    Muzidyatu bwino ganjayo

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu День тому +1

    Iyi ndi lmfa osapanga zibwana kawonesa picture yanji kwa azukulu amipingo pamwambo wamaliro kakuti sharp wachani zachamba

  • @EmmanuelNgamuti
    @EmmanuelNgamuti День тому

    Young man where hv u taken the energy to make this non African speech on a day like this?

  • @DavieChangoima
    @DavieChangoima День тому

    Sorry rnp

  • @Ampambachulu
    @Ampambachulu День тому

    Bro thought he killed

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 День тому

    Waxy akanakhala ngati chija chinthubidwa cha chilima chija akanag'alura

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 2 дні тому +1

    Guys mwanai watani kodi
    Paribe muthu amasangalala pa ifa ai .
    Uyu wandikaikisa chabwino R.I.P pastor kapenga

    • @HannahChingwalu
      @HannahChingwalu 2 дні тому +1

      Chakaikitsa pamenepo ndichani?? Akuyenera kutero kumene chifukwaso zili mmalemba Mulungu ananena kuti kwaikika kwamunthu kufa,,chamoyo chilichonse chikuyembekeza imfa Ambuye alemekezeke chifukwa wakwanilitsa mau ake,,osati zanuzo apa

  • @SamsonChiwera
    @SamsonChiwera День тому

    Mmmm waxy Kay Kuno ndi kumalawi ndye yaaa kumbali Ina it's ok kuti zilibwino koma another side this speech is useless to me when you grow up that's when you will realize that l made silly speech RIP Mr kapenga

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o День тому

    Kuyankhula kotani uku, mwana wachibwana

  • @BlessingsMangwaya-mk4fi
    @BlessingsMangwaya-mk4fi 2 дні тому +9

    This is not a fitting speech for the day your father passed away 😪😪

    • @lindamyaba
      @lindamyaba День тому

      Be serious man, waxy mwaonetsa maturity, zili bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 День тому

      Sonotu anthu odziwa mawu zimaaiyana ndi osadziwa mau zili bwino basi ambuye walora

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys 2 дні тому

    Komatu for sure now irealize rhst crying during someone's daeth is for us poor imagine what is this speech 😭😭😭😭😭💔💔end with sure
    Anyway rest well pastor kapenga