WADZIDZIMUSA ANTHU UKU VP NDIKA SURPRISE VISIT ku Chikhwawa District Hospital...atutumuka😂😂😂😂

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 11 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 93

  • @Vinic-f3w
    @Vinic-f3w 2 місяці тому +8

    Malawi needs such heart ❤,,,, continue VP

  • @abangaabanga4677
    @abangaabanga4677 2 місяці тому +6

    I commend this, this needs to be encouraged, please continue, with this kind of mentality Malawi will rise, God bless 🙏

  • @FloridaOssy19
    @FloridaOssy19 2 місяці тому +1

    ❤❤❤❤❤❤ mwayamb bwino a manganya

  • @DeborahHetekere
    @DeborahHetekere 2 місяці тому +2

    This is good development that's the spirit that we need as malawians,,,this is exactly what Late Dr Claus Chilima wanted

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 2 місяці тому +8

    Zipatala za boma mavuto aakulunso ndomweo. Ogwra ntchto amafika nthaw yomwe akufuna and sayambanso ntchto nthaw yomwe afklayo amayamba wakhala kae akut kupumula then ayambe kugwra ntchto. Imafika mpaka 9 asanayambe ai. Chomwe amadziwa nkutukwana ma patient bas

  • @veronicamalisero2671
    @veronicamalisero2671 2 місяці тому +1

    A VP ndipo muyendele ma office onse aboma,,,....amakhala pa mtambasale anthu awa..keep it up, ,,,....

  • @GiftNgwira-e8l
    @GiftNgwira-e8l 2 місяці тому +3

    Kkkkkkkkk koma vic wake kashoti

  • @masalinodovu1705
    @masalinodovu1705 2 місяці тому +1

    Excellent Mr VP izi nde zofunikira kwambiri

  • @DinahNantchengwa
    @DinahNantchengwa 2 місяці тому +1

    Proud of you Mr president, zikamatele dziko lathu liziyenda bwino, anthu muzipatsla amataililadi koma akamalombikitsidwa choncho ziziyenda

  • @giftsululu4274
    @giftsululu4274 2 місяці тому +4

    Ku utm''' '' mukuona koma... Mwataya gold

  • @vanalphamphaya3518
    @vanalphamphaya3518 2 місяці тому +1

    Big up the VP continue the good work you started when you were there long time.

  • @nyasavoicebox
    @nyasavoicebox 2 місяці тому

    Good on the Right Honourable the Vice President for being positive. Especially when dealing with the young nurse. Samakalipa koma kulangiza kuti mavuto akunyumba aliyapo iyi ndi ntchito anthu amakudalilani muziyesesa ku bwela ku ntchito on time. Even when dealing with the DHO the conversation sinali yoti ine ndiwonke kuti ndine VP but after reprimanding her he made her feel safe to elaborate on the challenges their hospital and district are facing. Politics aside, this guy may actually care about improving Public Service Delivery in Malawi.

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 2 місяці тому +1

    This is great. ife ogwira ntchito mboma tikugona kwambiri. Ngati sitifuna ntchito titsanzike

  • @AfickDaud
    @AfickDaud 2 місяці тому

    Kukhala ngat madam akunyumbatu Mr Manga kkkk mukuchta kukhalana mmene mukuendamo

  • @Ella13400
    @Ella13400 2 місяці тому +1

    Mr Usi pitilizana mwina malawi akhonzaaa.......

  • @omarlux3434
    @omarlux3434 2 місяці тому +2

    Osafuna.asye ine ndikuva kukoma ndi vp wathu

  • @RiaThomKata
    @RiaThomKata 2 місяці тому

    Well done Mr president

  • @elisaPhiri-k1e
    @elisaPhiri-k1e 2 місяці тому +1

    Ma patient kumvetsa chisoni pogona pamene ndalama zaboma zikungobedwa mmm

  • @HassanMaganizo-im6nk
    @HassanMaganizo-im6nk 2 місяці тому

    Kkkkk kodi limeli ndi sewero lakutiferanji kodi😂😂😂😂

  • @abbasjutasi909
    @abbasjutasi909 2 місяці тому +1

    Iwe nde akuphela kutulo iwe za ndege wachepa nazo
    Good job apule

  • @mayesouldphiri9889
    @mayesouldphiri9889 2 місяці тому

    Iyi ndi tikuferanji ya srs 😂😂

  • @RotNkhoma
    @RotNkhoma 2 місяці тому

    Let's continue mr vp you need to go different department of government9, we need great malawi

  • @brothertonekathyole7349
    @brothertonekathyole7349 2 місяці тому

    Keep it up our VP!

  • @ChifundoChikakwiya-kf1is
    @ChifundoChikakwiya-kf1is 2 місяці тому +1

    😂😂😂 It is promising slowly but let's hope greedy people won't disturb him

  • @fredbmazuwa8066
    @fredbmazuwa8066 2 місяці тому

    VP you have got my thumb

  • @GraceGonani
    @GraceGonani 2 місяці тому +1

    Anthu ogwila ntchito boma amatailila kwambili mwina apa atengelapo mphutzilo😊

  • @ChimwemweDemelo
    @ChimwemweDemelo 2 місяці тому

    Big up Mr vp

  • @KondwaniNguleti-x1q
    @KondwaniNguleti-x1q 2 місяці тому

    Mr VP Usi u did it well 👏

  • @CosmasChikwindi
    @CosmasChikwindi 2 місяці тому

    That's my VP ❤❤❤❤

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 місяці тому

    Well done VP usi. Ntchito yofunikira

  • @MacsJafali-d1m
    @MacsJafali-d1m 2 місяці тому +1

    Uyu apwetekaa anthuu

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 2 місяці тому

    Anakapangaso check ku pharmacy ngati kuli mankhwala okuti odwala alandira?

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg 2 місяці тому +1

    Zikachita bwno tiziyamikilako wakulu mwayamba bwno

  • @MenasKaliati
    @MenasKaliati 2 місяці тому

    Uyu ndiwasero basi😂😂😂

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm 2 місяці тому +1

    Civil servant kumakhala ngati ant civil servant.worse ku chipatala it's beyond ntchito.

  • @FestoniehJim
    @FestoniehJim 2 місяці тому

    Izi ndie zalowa sewelo ndithu

  • @BrendaJali
    @BrendaJali 2 місяці тому +1

    Good move

  • @GiftDaftala
    @GiftDaftala 2 місяці тому +1

    Sizikukhala or pangono he can't even afford chilima's footsteps

    • @blessingsmunthali9202
      @blessingsmunthali9202 2 місяці тому

      Understand that Mulungu atilenga mosiana and everybody is unique 😊

  • @GustoAjasi-fl9oo
    @GustoAjasi-fl9oo 2 місяці тому

    😂😂😂😂 ausi anachenjela eee

  • @MtenjeHassan
    @MtenjeHassan 2 місяці тому

    Zayambika 😂😂 big up mr usi....

  • @MoloiTeboho-x9f
    @MoloiTeboho-x9f 2 місяці тому

    Iwe ma nganya 10pn munthu apanganao cani 😂😂

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 2 місяці тому +1

    Nurse kukanika kuyankha mafunso a a Usi in English Kkkķk Malawiiiii...bolakotu a DHO 🎉

    • @chigokhalid9420
      @chigokhalid9420 2 місяці тому +2

      Wakwanisa komanso Mbali ina anali mantha plus I think sanaganizile Kut akumana ndi VP

  • @AllanMwakalenga-wn5ib
    @AllanMwakalenga-wn5ib 2 місяці тому

    Yalakwa apa...mwachedwa ku vepi a nurse

  • @tracybennie7783
    @tracybennie7783 2 місяці тому

    Ine. Ndiye. Ndikalila. Malilo

  • @janemanyamba7201
    @janemanyamba7201 2 місяці тому +1

    Uyu ndiye atithandizadi zoona

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 2 місяці тому

    😂😂😂 Km manganya

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm 2 місяці тому

    Ndawala zikuswedwa eeee

  • @MagretSaid
    @MagretSaid 2 місяці тому

    Mukawaopsezeso ku mapasport uko kuli chinyengo

  • @Marionphuxymw
    @Marionphuxymw 2 місяці тому

    Kkkkkkk kma adaa changa ndichala pakamwa

  • @AllanMwakalenga-wn5ib
    @AllanMwakalenga-wn5ib 2 місяці тому +1

    Tikuferanji 😂😂

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto 2 місяці тому

      Ndendende😂😂😂😂😂😂😂

  • @LovemoreVincent
    @LovemoreVincent 2 місяці тому

    Powerful musatsiye

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 2 місяці тому

    New sheriff in town

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 місяці тому

    Zama reform please a vice president yambsnipo before 2025

  • @osmanafadi4801
    @osmanafadi4801 2 місяці тому

    Wamisala anaona ndewuu

  • @AlinafeSolomoni
    @AlinafeSolomoni 2 місяці тому

    Koma akuoneka ngati afika movuta koma ndimunthu ochezeka

  • @clesheinvestments
    @clesheinvestments 2 місяці тому

    Zofunika zimenezo a VP.
    Ma Civil Servants ambiri matama komanso kumalimbikira ntchito, kukula Mtima komanso kudzikonda.
    Akuti ntchito ya m'boma imavuta polowa.
    Achangamutseni ndithu.

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 2 місяці тому

    Ngati azimaliza ndiyen tione

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 2 місяці тому

    ❤❤

  • @Choicemlw
    @Choicemlw 2 місяці тому

    Mu manifesto a Tonse alliance anati ankadzalowa m'boma anthu azipita ku ntchito 8:30
    Aiwala nthawi yomweyi kodi?

  • @emmanuelkenneth4768
    @emmanuelkenneth4768 2 місяці тому

    😅😅😅😅 well planned

  • @EvanceSteven-u5g
    @EvanceSteven-u5g 2 місяці тому

    Nice

  • @ruthkaoloka4772
    @ruthkaoloka4772 2 місяці тому

    ndi drama kodi?

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 2 місяці тому

    Mupitenso ku immigration mukawonekeleko bwana

  • @LemosBanda
    @LemosBanda 2 місяці тому

    Bola zipipitirire

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 2 місяці тому

    I remember achilima anayambaso chonchi kenako nae alowa mu system...... Hope this will no stop

  • @TamieMbenza
    @TamieMbenza 2 місяці тому

    Kkkkk ine ndimaona ngati sewelotu😂😂😂😂🎉🎉

  • @EmmReece
    @EmmReece 2 місяці тому

    mcp iwinaso bad

  • @ErustusPhiri
    @ErustusPhiri 2 місяці тому

    Malume mukukwana

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 2 місяці тому

    Akuyankhula ngt akupanga tikuferanji

  • @Sinya-r5q
    @Sinya-r5q 2 місяці тому

    Mulunguakupatseni phamvu

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 2 місяці тому +1

    Ngati zenizenitu, nkana unampeleka Bhiyeni umafuna zimenezi.

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto 2 місяці тому

      😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 2 місяці тому

    Ukuoatenga anthu ngati zitsiru USI government ukuti kulibe ndalama koma zomwe akumagawa kumusonkhano akuzitenga kuti?

  • @willieBillschiumbuzo
    @willieBillschiumbuzo 2 місяці тому

    Ipatseni moto a vice ama 10:41 wonjeza kubwera mochedwa kutchito ma nurse akafika ayambe kaye aseweretsa 4n then aziyamba cha ma 9 kugwira tchito

  • @StellaErias
    @StellaErias 2 місяці тому

    Pitilizani bwana azimayi oyembekezela timavutika zipatalamu agalu amenewa amazimva ubwana zipatalamu

  • @BrianBanda-j5n
    @BrianBanda-j5n 2 місяці тому

    ipase moto usi bola osazasitha mukazapasidwa mwayi.......try hard this year 2025 boma....

  • @danielkhinguirossejuliasse6106
    @danielkhinguirossejuliasse6106 2 місяці тому

    ndiye wapanga sewero lamphamvu

  • @HappinessMilanzi-b2m
    @HappinessMilanzi-b2m 2 місяці тому

    Zikuoneka kuti mutithandiza

  • @EmmReece
    @EmmReece 2 місяці тому

    mcp iwinaso

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 2 місяці тому

    Ma nurse ku malawi osadziwa English Kkkķk km zlko. Usi wayesetsatu

  • @AishaUthman-mg7db
    @AishaUthman-mg7db 2 місяці тому

    😂😂😂😂

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 2 місяці тому

    Ananena kuti asenda aliyense waulesi

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 місяці тому

    Zandale ziduse uko nawo anthu ogwira ntchito chipatala za boma amapanga matama muzapanadi

  • @MustaffMdogo-c7q
    @MustaffMdogo-c7q 2 місяці тому

    Zapamwamba

  • @FlorenceBillyGama
    @FlorenceBillyGama 2 місяці тому

    Ubwana syndrome inavulaza a malawi ambiri