Good on the Right Honourable the Vice President for being positive. Especially when dealing with the young nurse. Samakalipa koma kulangiza kuti mavuto akunyumba aliyapo iyi ndi ntchito anthu amakudalilani muziyesesa ku bwela ku ntchito on time. Even when dealing with the DHO the conversation sinali yoti ine ndiwonke kuti ndine VP but after reprimanding her he made her feel safe to elaborate on the challenges their hospital and district are facing. Politics aside, this guy may actually care about improving Public Service Delivery in Malawi.
Malawi needs such heart ❤,,,, continue VP
I commend this, this needs to be encouraged, please continue, with this kind of mentality Malawi will rise, God bless 🙏
❤❤❤❤❤❤ mwayamb bwino a manganya
This is good development that's the spirit that we need as malawians,,,this is exactly what Late Dr Claus Chilima wanted
Zipatala za boma mavuto aakulunso ndomweo. Ogwra ntchto amafika nthaw yomwe akufuna and sayambanso ntchto nthaw yomwe afklayo amayamba wakhala kae akut kupumula then ayambe kugwra ntchto. Imafika mpaka 9 asanayambe ai. Chomwe amadziwa nkutukwana ma patient bas
A VP ndipo muyendele ma office onse aboma,,,....amakhala pa mtambasale anthu awa..keep it up, ,,,....
Kkkkkkkkk koma vic wake kashoti
Excellent Mr VP izi nde zofunikira kwambiri
Proud of you Mr president, zikamatele dziko lathu liziyenda bwino, anthu muzipatsla amataililadi koma akamalombikitsidwa choncho ziziyenda
Ku utm''' '' mukuona koma... Mwataya gold
Big up the VP continue the good work you started when you were there long time.
Good on the Right Honourable the Vice President for being positive. Especially when dealing with the young nurse. Samakalipa koma kulangiza kuti mavuto akunyumba aliyapo iyi ndi ntchito anthu amakudalilani muziyesesa ku bwela ku ntchito on time. Even when dealing with the DHO the conversation sinali yoti ine ndiwonke kuti ndine VP but after reprimanding her he made her feel safe to elaborate on the challenges their hospital and district are facing. Politics aside, this guy may actually care about improving Public Service Delivery in Malawi.
This is great. ife ogwira ntchito mboma tikugona kwambiri. Ngati sitifuna ntchito titsanzike
Kukhala ngat madam akunyumbatu Mr Manga kkkk mukuchta kukhalana mmene mukuendamo
Mr Usi pitilizana mwina malawi akhonzaaa.......
Osafuna.asye ine ndikuva kukoma ndi vp wathu
Well done Mr president
Ma patient kumvetsa chisoni pogona pamene ndalama zaboma zikungobedwa mmm
Kkkkk kodi limeli ndi sewero lakutiferanji kodi😂😂😂😂
Iwe nde akuphela kutulo iwe za ndege wachepa nazo
Good job apule
😂😂😂😂😂 olo pa Lunch
Iyi ndi tikuferanji ya srs 😂😂
Let's continue mr vp you need to go different department of government9, we need great malawi
Keep it up our VP!
😂😂😂 It is promising slowly but let's hope greedy people won't disturb him
VP you have got my thumb
Anthu ogwila ntchito boma amatailila kwambili mwina apa atengelapo mphutzilo😊
Big up Mr vp
Mr VP Usi u did it well 👏
That's my VP ❤❤❤❤
Well done VP usi. Ntchito yofunikira
Uyu apwetekaa anthuu
Anakapangaso check ku pharmacy ngati kuli mankhwala okuti odwala alandira?
Zikachita bwno tiziyamikilako wakulu mwayamba bwno
Uyu ndiwasero basi😂😂😂
Civil servant kumakhala ngati ant civil servant.worse ku chipatala it's beyond ntchito.
Izi ndie zalowa sewelo ndithu
Good move
Sizikukhala or pangono he can't even afford chilima's footsteps
Understand that Mulungu atilenga mosiana and everybody is unique 😊
😂😂😂😂 ausi anachenjela eee
Zayambika 😂😂 big up mr usi....
Iwe ma nganya 10pn munthu apanganao cani 😂😂
Nurse kukanika kuyankha mafunso a a Usi in English Kkkķk Malawiiiii...bolakotu a DHO 🎉
Wakwanisa komanso Mbali ina anali mantha plus I think sanaganizile Kut akumana ndi VP
Yalakwa apa...mwachedwa ku vepi a nurse
Ine. Ndiye. Ndikalila. Malilo
Uyu ndiye atithandizadi zoona
😂😂😂 Km manganya
Ndawala zikuswedwa eeee
Mukawaopsezeso ku mapasport uko kuli chinyengo
Kkkkkkk kma adaa changa ndichala pakamwa
Tikuferanji 😂😂
Ndendende😂😂😂😂😂😂😂
Powerful musatsiye
New sheriff in town
Zama reform please a vice president yambsnipo before 2025
Wamisala anaona ndewuu
Koma akuoneka ngati afika movuta koma ndimunthu ochezeka
Zofunika zimenezo a VP.
Ma Civil Servants ambiri matama komanso kumalimbikira ntchito, kukula Mtima komanso kudzikonda.
Akuti ntchito ya m'boma imavuta polowa.
Achangamutseni ndithu.
Ngati azimaliza ndiyen tione
❤❤
Mu manifesto a Tonse alliance anati ankadzalowa m'boma anthu azipita ku ntchito 8:30
Aiwala nthawi yomweyi kodi?
😅😅😅😅 well planned
Nice
ndi drama kodi?
Mupitenso ku immigration mukawonekeleko bwana
Bola zipipitirire
I remember achilima anayambaso chonchi kenako nae alowa mu system...... Hope this will no stop
Zoonad chilimaso amkatero
Kkkkk ine ndimaona ngati sewelotu😂😂😂😂🎉🎉
😂
Kkk
mcp iwinaso bad
Malume mukukwana
Akuyankhula ngt akupanga tikuferanji
Mulunguakupatseni phamvu
Ngati zenizenitu, nkana unampeleka Bhiyeni umafuna zimenezi.
😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Ukuoatenga anthu ngati zitsiru USI government ukuti kulibe ndalama koma zomwe akumagawa kumusonkhano akuzitenga kuti?
Ipatseni moto a vice ama 10:41 wonjeza kubwera mochedwa kutchito ma nurse akafika ayambe kaye aseweretsa 4n then aziyamba cha ma 9 kugwira tchito
Pitilizani bwana azimayi oyembekezela timavutika zipatalamu agalu amenewa amazimva ubwana zipatalamu
ipase moto usi bola osazasitha mukazapasidwa mwayi.......try hard this year 2025 boma....
ndiye wapanga sewero lamphamvu
Zikuoneka kuti mutithandiza
mcp iwinaso
Ma nurse ku malawi osadziwa English Kkkķk km zlko. Usi wayesetsatu
Aaaa za ziii 🚮
😂😂😂😂
Ananena kuti asenda aliyense waulesi
Zandale ziduse uko nawo anthu ogwira ntchito chipatala za boma amapanga matama muzapanadi
Zapamwamba
Ubwana syndrome inavulaza a malawi ambiri