Ineso so wandale komano nditha kumvomelezana ndi comrades cz Mr kabambe atalemba kalata kuwafunsa a vice president a usi kuti atenge uthenga kukapeleka kwa a presdent zokhudza commission of inquiry pa imfa yomwe inachitika ku chikangawa yet izi zinali zomwe rael utm fans komanso amalawi ambiri akufuna yet sanapangidwe support of which was very strange
This is controversial because kaliati is the one who expelled utm from tonse alliance and how come the same person kuti abwerereso😢 a mtanyiwa ndinu amisala ndye kuti mwalandila ndalama kuchokera kwa a kabambe kuti munyoze kaliati,
Zikumveka ngati zoonaditu coz zikudabwisa kuti how come mai kaliati akukamukalipira kabambe coz wafunsa za commission of inquiry yet aliyense akufuna zomwezo?
Mulungu ali mwa inu mtanyiwa long live comrade ntanyiwa zachisoni ndithu koma Mai kaliyat mzimu wa Chilima ndithu ukusowetsani mtendere, Mcp munapha Chilima ndicholinga choti mutenge chipani cha UTM koma choti mudziwe kunja kuno kuli mulungu la 40 likukwanilani
Ngati mai kaliyati zimene akuyakhula mutanyiwa ndi true story ndiye mai inu ndinu opusa kwabasi ndipo ngti mai inu muzakhale pamozi ndi mcp ndiye ndiwe mai onunkha kwasi bola musayelekeze kuchita zomenezo ndalama zimakoma bwanji kudya azanu akuvutika muziko kuzipatala mankhwala kuli anthu atundu wanji wosalhala ndi Mulungu? Musiyeni Chakwera apite ku gehena ndi nduna zake zose
Ayi Mai chilima asaimilire UTM Mcp ndiya kupha, Koma ngati za Mai kaliyat zi zili Zowona nde kuti eishhhhhh zowopsa tu akukufuna kuyitengera UTM ku chipani cha mcp mmmm, nde ngati zili choncho anthu akutulukani Mai mupita nokha ku Mcp ko
Is this mtanyiwa or chigoba? The way l know mai Kaliati sangapange chipongwe skc and Utm. If mukunenazo ndizoona ikani timvere zomwe ankakuuzanizo, akaliatiwo cz zinazi mukungopekapo and it doesn't sound real 😢
Koma Allah alipo mpaka chakwera atuluke mboma basi Allah atichosere crocodile mpaka a Malawi tiomboke mukaporo tili nawo pano ndi chakwera muthu otiyipa kwambili
Ine ndi ndikudabwa nazo u and mr DC mukuti Merry chilima apitilize pamene mamuna wake analekezela. Kodi muli ndi omboni wanji kuti mai chilima ali ndi mphaso yausogoreli? Ine ndimaona kuti mai aja amangowathandizila pena ndi pena not 100% mwachidule ndingoti chipani cha utm pin code yake inapita ndi mwini wake chilima, maiyo musieni azipanga zake musamukakamize mufune musafune utm izakhala mbili basi.
Tinalakwisa ku votera mcp .Mulungu atikhululukire ndipo tikupempha Mulungu kuti atichosele Mavuto alipowa
MULUNGU adzikudalitsani ndikukutetezelani MR, COMRADE ❤
Mulungu akati aike zobisika poyera eeeshiiiiish 🙌🙌
Ineso so wandale komano nditha kumvomelezana ndi comrades cz Mr kabambe atalemba kalata kuwafunsa a vice president a usi kuti atenge uthenga kukapeleka kwa a presdent zokhudza commission of inquiry pa imfa yomwe inachitika ku chikangawa yet izi zinali zomwe rael utm fans komanso amalawi ambiri akufuna yet sanapangidwe support of which was very strange
Release the audio please we need tangible evidence
Tikhulupirira tikamva ma Audio, Akweni omwewo 💯
Ngati honourable Kaliyati agudwa, then who is going to rescue poor Malawians, this is bad
Uyu mtanyiwa watumidzidwa ndi Mulungu kt atitsekure maso
Comrade u hv started politics now kkkk this issue seems to b personal issue wit kaliati leave our utm alone pliz
Anthu osadzindikira tayanganani dziko mmene likuyendera movuta anthu tikuva Koma sotivetsetsa tikuona Koma sitikuonetsetsa tikudzikira Koma sitikudzindirikitsitsa conco osamanyodza pamene Wina Ngati waonetsetsa chifukwa tikagwera kumphompho
U r right I feel the same❤❤❤
Hard to believe,. Mai Kaliati was one woman we trusted to stand firm for UTM party, but now tilowere kuti?
@@emmanueljelemani4203 koma zikukaikitsa izi
Ngabodza awaa, awa nga kabambe... Kaliati can't sell the party to MCP.....
Palibe chobisika pasi pa thambo Lord have mercy to Malawi
Zoona ifa ya saulosi chilima mai kaliyati mupezerepo chuma anthu opusa kwabasi anthu nose mukulandila ndalama zakuba ku choketra ku chitipa to Nsanje nose ndinu agalu ndipo kaya ndiwandale kaya ndi mubusa kaya ndiomenyera ufulu nose mukulandira ndalama kuchokera kuboma ndinu zisiru makape mbumbuzi zisetekwete anthu opanda chifundo ndipo 2025 muziwa kuti kumwamba kuli Mulungu wamoyo. Ngati mukuganiza mcp idzawine 2025 muzawona zodabwisa zimene Mulungu wamoyo azachite
Comrade we really ❤❤❤ you please keep on showing us the secret of these evils
Ndakhumudwa nawo Maiwa ndithu 😢
Koma akaliati is fit to not be president of UTM she is fit SG BASI
Atikhumudwitsa mai Patricia kaliati😢😢
Ndiye kuti Patricia ndi Manganya akudziwapo za imfa ya a Chilima! Ine ndimadabwa kuti SKCthee VP ,MW kungoti ziii bwanji
Please madam chilima tulukani UTM tengani udindo.
Eish koma guys, zina ukanva, umadwala mutu waching'alang'a, mu tea umathira sabola, mundiwo nkuthira nchenga.😢😢 akaliyati chonde Amalawi musawasakanize manyi ndi mikozo
Ife tikuvutika. Ndipo Akaliyati mukanvera oudio iyi mubwere poyera muzilongosole
Mulungu apitilize kumugwilisa ntchito Mtanyiwa
Mai kaliyati mwatinkhumudwitsa, 😢😢.
Aaaaaaa Mr Ntanyiwa musamasowetu ifetu tikudalira inuyotu kumeneko
Kaliat what's going on we had a great believe in you now you have turned the table
I love kaliyati, I think these people Ali ndi ma personal issues
Za mai kaliati nde mwapalatu abwana.
Kabambe mulendo ngati ameneyo mmm i've started luzing my trust in you comrade
Kkkkk Ntanyiwa samanama
Kwambiri ayamba bodzano ,Patricia kaliyati amaonekeratu kuti ndi mzimayi osatekeseka ,atumidwa awa
Mfiti imakusekelera masana ikuzwa kuti ikupha usiku and amakhala bale wako@@RuthKaledzera
Eish koma abale tidalile ndani pa Malawi Pano azatisogolele mamaine
Kayadi! Eeish zovuta
Malawi zoti azakhalaso wabwino ndayamba kukaika coz izii zandizizilisa khongono😢
Propaganda iyi don't be used by politicians ntanyiwa OK, muzionongera cv yanu ya bwino ija Jst bcz kaliäti wat ayima ku convention as president
Inenso ndayamba kuwakaikira a Nthanyiwa .awawa akusiyana ndi wa Bakili Muluzi tv uja...
Inu palibe chimene mukuziwa mukufuna muzitenge kuti ndinu ozindikila
But you guys Ntanyiwa is saying akhoza kutulutsa ma audio omwe amayankhulana so if he is lying can he say that??
I hope it’s not a way of ousting Mrs Kaliati from the Convention so people don’t for her. Let’s get serious. If true It’s a sad development.
This is controversial because kaliati is the one who expelled utm from tonse alliance and how come the same person kuti abwerereso😢 a mtanyiwa ndinu amisala ndye kuti mwalandila ndalama kuchokera kwa a kabambe kuti munyoze kaliati,
Ukhulupilire zomwe akunena Ntanyiwazi ndipo ndipo uzimvere chisoni kuti dziko la Malawi 🇲🇼 likurowera kutiko
Tanyuwa siwamisala ai ine ndikukhulupilila zomwe akunena tanyuwa sakunama ai anthuwa ndalama za pengesa
Zikumveka ngati zoonaditu coz zikudabwisa kuti how come mai kaliati akukamukalipira kabambe coz wafunsa za commission of inquiry yet aliyense akufuna zomwezo?
Mulungu ali mwa inu mtanyiwa long live comrade ntanyiwa zachisoni ndithu koma Mai kaliyat mzimu wa Chilima ndithu ukusowetsani mtendere, Mcp munapha Chilima ndicholinga choti mutenge chipani cha UTM koma choti mudziwe kunja kuno kuli mulungu la 40 likukwanilani
Comrade Mtanyiwa Inspiring the nations
Ngati mai kaliyati zimene akuyakhula mutanyiwa ndi true story ndiye mai inu ndinu opusa kwabasi ndipo ngti mai inu muzakhale pamozi ndi mcp ndiye ndiwe mai onunkha kwasi bola musayelekeze kuchita zomenezo ndalama zimakoma bwanji kudya azanu akuvutika muziko kuzipatala mankhwala kuli anthu atundu wanji wosalhala ndi Mulungu? Musiyeni Chakwera apite ku gehena ndi nduna zake zose
Hmm koma Pena Mtanyiwa ukamayamkhula udzidziwa kuti kulu mulungu kunja kuno umaonjeza bodza
Palibe bodza apa
Chokapa iwe utiuze zoonadi iweyo ukoo.
Inuyo onena zoona tamanenani ndipo mukhale ntanyiwayu inuyo
Inuyo onena zoona tamanenani ndipo mukhale ntanyiwayu inuyo
Kod mumanvera zitsiruzi? Awa ndi anthu oti mungamawanvere? Anayamba akambapo zinthu zabwino awawa? Zoti iwowa amakhala ndi ma person interest simudziwa? Muuze atulutse panopa ma audio-wo ngat akunena zoona? Zitsiru za anthu idzi kungofuna kugawanitsa anthu basi. Inu amalawi muli mdywooo kunvera zimenezizi zopusazi
😂😂😂😂. Kmatu naweso uli dyooooo kuvera zomwezi ngt zili zokubhowa ukanangodusa osavela olo comment kma apapa zaoneseratu kt pg iyiyi umaisata😅
You are true these people are rubbish at all
Chitsilu ndiiweyo wanvela kale bwanji ukuyika comment kkkkkkk chitsilu ndiiweyo wampatsa comlede ntanyiwa komenti 😂😂😂😂😂😂😂umbuli
Takuonani kale kuti ndinu anyamata ojiya
Chilungamo ndimwano. Iwe umavera bwaa? Museyen Ntanyiwa ndi nthawi yake
Ndiye ngati zili choncho atsogoleli nonse simakonda dziko lanu ndiye tidziti mwina dpp ndi aford bsitu
Never trust any politician.
Pali zinthu ziwili apa: mkutheka iweyo ndamene wapatsidwa ndalama from kabambe kapena amayiwa akufuna kugulitsadi chipanichi ngakhale zikukayikitsa.... kut tikukhulupilile tipatse ma audio akewo...coz wammodzi mwayinu watha apapa sazikondedwaso
ndikhani imeneyi.
Every hour ndimabwera kuyamba kutcheka ntanyiwa pa limpompo fm koma ndimapeza zakale zokhazokha ayi bwana msamasowe chonde muzibwerabwera even mtakhala ndika breaking News tatipasireni ife .ulemu wanu biggy
Thanks for telling us the truth
Oh my goodness Why Kaliyati Kaliyati Kaliyati 😮 palibedi wa straight pa ndale hey
Nice Job Bigman
Tulusani ma audios tiwanvere ndichitsiluso ameneyu panyero pakeso mai chilima limbani mtima muimile
Was wondering Kaliyati wangoti zii why eeeish koma ziliko kunjakuno abale wachilungamo palibe guys mmmmmm serious kaliyati
Samalani may Kaliati ngati nkhaniyi ndi yowona..komanso mayankhulidwe awawa comrade xikuwoneka too personal issues....
Comrade mulungu azikudalitsani mumatiimilila
Tumiza ma audios Kuti tikhulupile, mwayambana mudzifukwa zanu osatinamize apa
Ndi mayi ochenjeretsa kailati sangasiye kugulitsa chipan akuziwa kt sangawine paokha then amadana ndi Dpp paja msaiwale kt zipani zonse akalowa amamthamangitsa chifukwa Cha kuchuluka nzeru.. chilima yekha ndamene anamusunga chifukwa poti anali munthu wa chison😮😮😮😮ayisova
A Mtanyiwa ching'ambeni chinsaru c tionemo nkatimo
Marry chilima apite kuti osawuza mkazi wako bwanji leave Marry chilima alone
Kulapa pa zinthu zomwe ukuona kuti sudachite bwino ndipo ukupweteka anthu ochuluka sikulakwa, Comrade Ntanyiwa tangolapani pamodzi ndi inu UTM komanso DPP chifukwa mwayambapo kulumana nokhanokha. Lapani kuti mukhale mfulu
*Ngati zili zoona,,,,A Boni kalimdoo zinangovuta kuchoka ku UTM,,,,,Ndi munthu mmodzi akanamenyela nkhondo a malawi kuzela ku UTM kuima nao pa mphando*
Ayi Mai chilima asaimilire UTM Mcp ndiya kupha, Koma ngati za Mai kaliyat zi zili Zowona nde kuti eishhhhhh zowopsa tu akukufuna kuyitengera UTM ku chipani cha mcp mmmm, nde ngati zili choncho anthu akutulukani Mai mupita nokha ku Mcp ko
mai kaliati Malawi mukumuika pati?
Kkkkk koma ndalama anapanga kwambiri.
Munthu kulephera kulankhula chilungamo chifukwa cha ndalama.Chakwera akanakhala munthu wachilungamo sakaba ndalama komanso sakanapha vice wake.
Ayi shosha may kaliati
😭😭😭, very disappointed 💔🤦
Mwayamba bodza zinazi pitani ku box kwawo mukalalatilane komweko send vn here
Comred mwasowatu but you're welcome
Welcome ntanyiwa pamenepo ipemerere Kariati wataniso nawe Kodi ???Kariati kariatiweeee chonde Siya zimenezo mmene udamukondera chilima iweyo Kariati naweso wangokhala ngati manganya .zoonadi wokudya naye ndi amene azakupereka shit Kariatwee
koma ndarama ndiyopweteketsa kwambiri ndipo akariat mwankhumudwitsa anthu
Sizowoana izi inu...this guy might be used by someone to destroy Kaliyati's image....wayamba zaukape ntanyiwa
Bwanji tidikile mai kaliyati ngati angayankhe ndekuti ndizabodza km ngati akhale ziiii ntanyiwa moto kt buuuuuuuuuuh😂@@ChimwemweMuhelliwah
@@TemboHaswellzoona ayise let us wait and see kuti Kaliatinatichani
Mulungu alinafe ndpo tituluka mavuto osewa
Umat tivere ndani?
Komaso sakhala bwino convention isanachitike kut tidziwe mtima wa mayi ameneyu. Aaaah koma zoona mai?
Anthu andalewa guys Mmmm ayi osakhulupilra 😢 kaliati ndnapasa 100% Koma mmm ayi dzikomo
Mayi kaliyati pa chi phwi🫣🫣🫣🫣 kwinako nditukwana 😭😭😭😭😭😭😭
Chakweratu wasalapang'ono kumwalira chaka Chino sichitha mukhulupilire
Aise ukunama.Remember Chakwera is a Pastor not munthu wamba.
Ngati suzitenga bwino umwalira ndiwe
utafe ndiwe...stop trusting this pipo anthu inu
Yoooooh
Kaliati ndi hure mbuzi yamuthu crocodile nayeso ndi nzake crocodiles wakeyo onse ndi mbuzi
Inde musamasowe. We need information
Mtanyiwa machende ako nthawi yonseyi unali kuti pita uko kagone shatap zako
mtanyiwa God protect you
Kkkkkk koma Limpopo FM, nkhanga zaona ndi comrade ntanyiwa umakwana iweyo ndakufila
Koma ku Malawi ntchito ilipo komatu a Malawi tilimbe nanzo pa galaundi .
Is this mtanyiwa or chigoba? The way l know mai Kaliati sangapange chipongwe skc and Utm. If mukunenazo ndizoona ikani timvere zomwe ankakuuzanizo, akaliatiwo cz zinazi mukungopekapo and it doesn't sound real 😢
Iwe mutanyiwa uli mutesi chomene boza
GOD save Malawians please 🙏😭
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pomuyika aliyese wokhudxidwa pa ifa ya chilima
Ndipo zakhalaso bwino tadziwa convention isanachitike apa anakatidyetsa frass uyu
Koma Allah alipo mpaka chakwera atuluke mboma basi Allah atichosere crocodile mpaka a Malawi tiomboke mukaporo tili nawo pano ndi chakwera muthu otiyipa kwambili
Iwe chikukuwawa ndichani iwe ndi wa UTM tamapanga za DPP leave kaliati alone
Following up boss 🙏
Tumizani ma audio
Mr Mtanyiwa Limpopo FM 🔥🔥🔥🔥 koma sindikhulupilira kuti mama Kaliati angagulidwe ndikusiya chipani Cha UTM momwe amachikondera muja konse uko wayenda nacho chipanichi munthawi yonse yazovuta zija anaima ngati munthu wamamuna mmmmmhu zavuta ku Malawi
Ambuye Yesu anapachikidwa chifukwa cha ndlama yomweyo kkkk nde mukanene Iwo angalamdred
Ine ndi ndikudabwa nazo u and mr DC mukuti Merry chilima apitilize pamene mamuna wake analekezela. Kodi muli ndi omboni wanji kuti mai chilima ali ndi mphaso yausogoreli? Ine ndimaona kuti mai aja amangowathandizila pena ndi pena not 100% mwachidule ndingoti chipani cha utm pin code yake inapita ndi mwini wake chilima, maiyo musieni azipanga zake musamukakamize mufune musafune utm izakhala mbili basi.
Mai uyu anachenjeretsa ndipo okamuvoterawo asowa zochita
Zomvetsa chisoni bwanji😢
Antanyiwa mphindiso ya chani machende Ake kaliyati Samala wausilu iwe hule landare
Chingofa chikangawachob basi muthu oyipa kwambili ngati idya amin
A kaliati ndiye ayinsotu.
Ndizomvetsa chisoni 😢😢😢😢
MAYI KALIYATI MWAGANIZA BWANJI KOMA?? KULIRA KONSE KUJA ZOONA??? MWATIKHUMUDWITSA KWAMBIRI
Partilicia kaliyati ndi wosusuka ndi khalidwe lake sizachilendo
Koma nde za ziiiiiiiiii zeni zeni ife timawakhulupiliratu
Fire 🔥🔥
OK my god mayi kaliyati mulungu akuyendeni muzina lam ulungu yooo
Zimayi ameneyo ,,,,, asazitukwanise
Heeeeeeee😂😂😂😂😂😂😂 ndiye yayisotu
Comrade send ma vn kuti tidziwe zeni zeni koma Kaliati watikhumudwitsa
😂😂😂😂😂😂kaliyati wayaluka
Moti Mayi kaliati amakudziwa iweyoo!?
Munkati Micheal usi relo mukut Mai kaliat antanyiwa panopa nanu ndi achitsiru chothelatu ,iwe ndiwe wa dpp chomwe ukufuna ndi nkhalamba yako ija kut yilamulilenso koma mwauponda
Mmmmh Ntanyiwa ngwaboza why????