Ku DPP Tikufuna Director of Youth Olimba Mtima Kuti Tikonze Chipani - DPP Cadet
Вставка
- Опубліковано 10 вер 2024
- On Nyasa VoiceBox, a member of the DPP Youth Wing, popularly known as DPP cadets, stated that the party needs a strong and confident Director of Youth to perform well in the upcoming elections. Strong parties rely on a well-organized youth wing to effectively communicate their message to voters and to protect the party.
Ku Nyasa VoiceBox, m’modzi wa nthambi ya chipani cha DPP, yemwe amadziwikanso kuti DPP cadets, wati chipanichi chikufunika mtsogoleri wa achinyamata amphamvu komanso odzidalira kuti achite bwino pa chisankho chomwe chikubwerachi. Zipani zamphamvu amadalira gulu lachinyamata lokonzekera bwino kuti lipereke uthenga wawo kwa ovota komanso kuteteza chipani.
Pakufunika dc
Pathako panu ma cadet mboli zanu
Inuyo mumamutenga ngati wa Dpp komano iyeyo ndi wa Mcp Chikangawa party
Zoona mnyamata wathu
Yeah right ndipo zimenezo zikuyenera kuchitika.
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
DPP IKUBWELAYI NDI YA NYATWA SIKUDZAKHALA ZIBWANA ZIMENEZO
Mwayankhula za phamvu.
Mtengeni DC
Akufuna wangati Fredokis zomwe sizingatheke
Musadandaule achimwe inu DOY anapezeka kale ndipo ali okonzeka kuzakhaulisa zigawenga zonse zomwe zakhala zikutibvutisa. Dolo limeneli ndila pa Ntcheu apa. Munthu wake ndiamene mwamuchulayotu. CHISALE Wohyeeeeee.
Musadandaule achimwene inu. correction not ene,,,,,,,,zikomo.
Abale anzanga uthenga ndi umenewo akulankhula mbale wathuyu. Ma delegates athu tiyeni mukasankhe CHISALE as our DOY. Dziwani kuti kungowina Chisale basi tatenga boma.
A CHISALE chonde onesani chidwi ndipo bvomerani kukhala DOY wathu.
Fundo yambo
Madala team 😂😂😂😂😂
Paja ntchito zanu ndi za zikwanje