HOT CURRENT YA LERO ACHINA BRIAN BANDA ANG’ALURA AKUTI IWO SAMAOPA ALIYENSE PONENA CHILUNGAMO
1:02:24
CHAKWERA WAKAMBILANJI ZA IMFA YA CHILIMA? ~ HOT CURRENT YAPA 15 SEPT ATOKOTERA CHAKWERA NDI MCP
31:45
A Chakwera Opanda Anthu Mukhala Mfumu? - Pastor G Tembo
Вставка
- Опубліковано 15 вер 2024
- On Nyasa VoiceBox, Pastor G. Tembo reminds His Excellency the President that his presidency is based on trust. Without the people of Malawi, he cannot be President. Therefore, it is imperative that he condemns the violence being perpetuated by the MCP Youth.
Pa Nyasa VoiceBox, Pastor G. Tembo akukumbutsa a President kuti udindo wawo wa utsogoleri ndi kukhulupirirana. Popanda anthu aku Malawi sangakhale Purezidenti. Choncho, mpofunika kuti adzudzule ziwawa zomwe zikuchititsidwa ndi Achinyamata a MCP.
#malawi
Zonsezo chikangawa. yo akupangisa mesa iyetu akufuna nkhondo, ku Malawiko munthu woyipa uwu, kodi mukumusiya
be kuti azipitiza kula mula dziko la lathu la 🇲🇼 Ambuye chonde, tichoseleni chakwera chonde Ambuye munati tipempha ife, tikupempha inu. Mulungu wathu,
Anthu adzuke koma amuchotse uyu akumuti President yu.
Auze ankhutukuvewa
Tikayamba kubwezera police isazagwile munthu chifukwa tizawotcha ma offence awo
Amcp tiwabwesela ndipo Monga ine nditanawo ngakale yamifuti
Apresdent ndi munthu woyipa ,anthu akuphana iyeyo osayakhulapo osawonesa usogoreli
Zikomo abusa MCP ndi chakwela wawoyi anthu amagadzi tsadzasintha paka ndi akawina 2025 mobelamu amalawi OCHULUKA AKUFA 2025
Jezebel ndi mchewa waku mchinji
Tamufufuzeni chakwelayo kuomwe adabadwira kapena komwe kunachokela makolo ake. Nkutheka kuti simMalawi ai. Monga manganya kwa.mayake nku Zimbabwe nkuona akusineza Amalawi
Things are not going on well, sizikukhala bwino
Anthu inu please mulungu osamasewela naye please mukamapanga za ndale zanuzo wosamayikapo dzina la mulungu
Amuseweretsa patipo?
Amaudindo wonse anagulidwa, palibe chimene apolis angachite, akuwopa kuchotsedwa ntchito, boma la mcp likufuna nkhondo zikuoneka ngati choncho
Kwa iwowo ndizabwino mesa akufuna anthu azimenyana aziphana iwo azitolera magazi
Wadzetsa kale chisokonezo inu simukuona??
Alomwe kulilila ulamuliro
this is racism
Koma alomwe ndiye munatolatu
Kulankhula kopusa
Ukunena zoona..anthu awa akulira ngati achule a mu White Nile River.
Kodi ukamati Chakwera akutuma anyamata ukutanthauza chani? Iwe mbuzi kwabasi