Manganya ndi wa MCP ndipo ndi mzake wa Chakwera. Komanso mukaona chiyambiyeni ma cabinet Onse apitawo , Manganya sanachotsedwepo mu cabineti.Komanso iye uja magazi ake ndi a MCP, Thanks
Nthiko watenga kumakaphikira nsima nyumba mwa eni wake kusiya kumaphikira nyumba mwako ndi ana Ako,,,,manganya asatibowe! And manganya adaikapo nkono pa imfa ya chilima 😊
Inetu brother ndine malawi Koma ndilibe ID Koma ndili ndi passport ndipo 2014 ndinaka vota komandinagwirisa ntchito ndi pepala lochokera kwa amfumu akwathu nde zama ID ifeyo zimenezo sitikupanganao
Ken msonda za ma candles chikumuza ndi chani anthu tiyasa ma candles Malinga ndi chikulupilo chathu komaso Ausi ndi a MCP not UTM.nkhani yo vota pa libe ku gwilisa ntchito chitupa Cha udzika anthu akavote mwa chisawawa ngati momwe timachitila kale pofuna ku vota komaso anthu omwe tingakhale ma centres muzawonesese nkhope za chilendo zisazapezeke
Manganya akutinamiza ife a amalawi. Ndalama akulandira kuchoka ku Boma kuti adzigawa. Ken akudwara koma sakudziwa ayi. Ayi sitikugwirizana nazo kuti anthu akagwilitse ntchito chophaso cha unzika ayi. Aliyese akavote basi. Manganya ndiwa MCP ankangobisara kumbuyo kwa UTM. Manga anali kumthira kuwiri. Taphunzira kuti Manga ndi Yudas. Anagulitsa moyo wa Chilima. Za imfa ya Chilima zikuonetsa kuti sixikumukhudza za imfayo. Akushashalika kwambiri ndi ndalama za Chakwera. Ndalama zinari za ifeyo a Malawi anaba pogwilizana ndi Pulezident Chakweraa.
Ken msonda ali mgulu la n, gonna uja palibe chamzeru chimene akupanga kuletsa ma candle cho zikuchita kuwonetseratu kuti akusowa mtendere moto ukwawotcha sakugona tulo mzimu wa Chilima ndi anthu 8 aja uli pamitu pawo mtendere adzawusowa moyo wawo wonse
Ngati akunena kuti opanda cha uzika asakabvote pamenepo pokha nde akunama chifukwa anthu ena chauzika chawo anayamba kuyendera kale kale mpaka pano sanapatsidwe zonsezo akupangila dala ndicholinga choti adzabere zisankho Bola kumbvota opanda chauzika chifukwa kale timambvota opanda chauzika
Brother manganyatu ndi wa MCP kuyambira kale akupanga masewelo ake nde Ku UTM kujatu anangopitilatu ndiukazitape umtila kuwili. Nde zonse akupanga manganya ndi kampeni ya MCP
Manganya ndi wa MCP ndipo ndi mzake wa Chakwera. Komanso mukaona chiyambiyeni ma cabinet Onse apitawo , Manganya sanachotsedwepo mu cabineti.Komanso iye uja magazi ake ndi a MCP, Thanks
Zoonadi zake ndizimenezo
Ndipo kuvota kovotera ID pakufunika kwiyo wawukulu kt chakwera asakhaleso ndi mpavu komaso akuna kwambiliiiiiiii
Manganya ndi udasi anapeleka Yesu uja, naye adzafa ngat chilima musiyeni,
Manganya akupanga ija ndi campaign motumidwa ndi chakwera ndipo anthu tisamukhulupilire
Makandulo apitilre
Ovota adzakhale mmalawi aliyense
Manganya ndi WA mcp
Manganyatu akudziwadi kanthu za SKC. Ndipo ameneyu akuyenera achotsedwe ku UTM. Nzoonadi, m candli akamayaka tu anthu wa mtendere sakuupeza choncho anthuwa asasiye kuyatsa kuti anthuwa amve mtedza.
Mayi amaphikira ana ake chakudya kunyumba kwake, osati kunyumba ya munthu wina
Wachamba ken msonda kauzuzu kowonda kamja ngamti kali ndimatenda mwina matena
Manga ya akumupangila campaign a Chakwera
Amalawi anasukusula ndalamazoo alandire ndi zawo koma asazabvotere ankhanzawo opanda chifundowo
Mpaka lelo manganya sadayankhulepo za imfa ya chilima
MANGANYA NDIOSOKONEZA KWAMBIL NO PAIN NO GAIN
Thawi yawo yantha amenewo zaka zonsezi Malawi akhala akukanda ndiye lero adziti ngongole ? Samapanga zimenezo skc asanamwalile bwanji?
Chakwera zake zada ndiye akuyesa yesa kugwilitsa ntchito zitsilu zinazake kuti mwina kapena ziwale zupusa zakezo naye maganya chikagawayo tamutulukira kale kuti ndiwagulu la chikagawa ndipotu chomwe adziwe chakuti chilichose akupanga Malawi yadanawo kunkhosi mcp panu ikuveka mwachifungo chonunkha ndipo Kubota tivota momwe zimayendera mbuyomu zuyenda chimodzimodzi gati akuwona kuti Kubota kulibe ok ubwinoso wanthawi timamupatsa chakwerawo ukuntha timuyendera ndimapazi kukamusuntha gati sitipatsidwa mwayi olembetsa ndi zintupa zosiyana siyana ifetu sitipanha nawo zakudabwe
Palibe kuthetsa kuyatsa candle lo sitilolo
Zoona a malawi sitichedwa kuyiwala akatipasa chibanzi
Manganya ndi Yudas. Pano akuchita kusangalala busy kupereka umboni wa umphawi wake wa kale
Athu avutika vutika wina azibwela apatsa ndalama fukwa yovota ikubwela...Ajaso ngoouma mutu ndi mpala uja et awagwiritsa ntchito chakwera aja km akunama ife kupoila kwao tadziwa kale
Manganya galu wamunthu wamchira weni weni komanso fiti yamalaza.
Msonda machende ake pamodzi nd banja lakelo
Nthiko watenga kumakaphikira nsima nyumba mwa eni wake kusiya kumaphikira nyumba mwako ndi ana Ako,,,,manganya asatibowe!
And manganya adaikapo nkono pa imfa ya chilima 😊
Zoona,,koma anthu amuzindikile manga ya alandile ndrama koma osawavotela
I think this government has lost its target bcz there's no need of giving Money to the Malawians
Shina shillishosnse soshitka nkwa anduamenewa ashankwela ndiomwe ankutumaso ngani yyonse amanganya ndi waw mcp ngani yyankusa abanda amangidwe ngati ashankwela ankufunna kt mulungu awatetese. Live in the sauth ✌️✌️👈👈✌️👌
Kumbukirani Michael usi simumalawi ameneyo ndiwakuzimbabwe
As long as uli mzika ya Malawi you are ligible to vote even though popanda Cha unzika
Iyeyo awasiye anthuwo ndi ufulu wao bs ngat iyeyo ngat sakusangalatsidwa nazo asiye cipanico ena apitilize
Akupanga kampeni ya mcp
Don't trust manganya he is on MCP ticket
Manganya akupanga kampeni wa Mcp not kuthandiza Malawi, komaso Ken Nsonda ndi manyi amunthu Ma ARV apeweteka!
Manganya akupanga campaign Chakwera akuziwa kuti akuwowozedwa ndichifukwa wagwirisa kamanganya. utm imuwu manganya kuti akamapanga musonkhano azipanga za mcp osati za chilima. Manganya better udasi ata zindikira kuti walakwa anabweza ndalama ndikukazikweza mumtengo koma manganya akudya ndalama ndikupangira campaign. Musonda zeru alibe. Kuvota aliyese amene ndizika yamalawi yiyenera kuvoto ukhale ndi ID or ulebe ali ndiufulo kuvota.1994 timavota without ID pano zavuta pati
Inetu brother ndine malawi Koma ndilibe ID Koma ndili ndi passport ndipo 2014 ndinaka vota komandinagwirisa ntchito ndi pepala lochokera kwa amfumu akwathu nde zama ID ifeyo zimenezo sitikupanganao
Ndalama yilibe Neef ,akungonama sanatinamize
Ndiyekuti ngati aside akuvomereza kuti anaphadi bwanji akulesa okuphawo
Sitikugwilizana nazo onse ndi amalawi
This government is worse in the history of Malawi
Ken msonda za ma candles chikumuza ndi chani anthu tiyasa ma candles Malinga ndi chikulupilo chathu komaso Ausi ndi a MCP not UTM.nkhani yo vota pa libe ku gwilisa ntchito chitupa Cha udzika anthu akavote mwa chisawawa ngati momwe timachitila kale pofuna ku vota komaso anthu omwe tingakhale ma centres muzawonesese nkhope za chilendo zisazapezeke
You are welcome
Manganya Palibe angachite chothandiza Amalawi,,,
Mwambi umenewo WA kunyumba kwake ndi amake ndi wa MCP athu AMene atsalila kugwilizano ndi amene anampeleka chilima
Kodi police yikugwira ntchito ndi mcp or dziko la Malawi
Ndim'mene manganya akupangila zikusonyezetatu kuti chipani cha mcp analowa kale kale, komanso za kuphedwa kwa Chilima amadziwa po kanthu
Komanso zimene akupanga panozi ndi compain nthawi yonseyi anali kuti anthu m'mene amvutikira muja m'malo moti ndalama zomwe akugawazo zithandizire zosowekera mdziko, palibe chanzeru chimene akuchita amalawi pano tinachenjera tiyeni tilandire ndlamazo tidye ndi misonkho yathu imeneyo mbvoti ili mumtima
Ali part of campaign koma ya MCP
Ndalamazo akupatsidwa ndi Boma.
Manganya akanakhala kuti ndi wa utm bwenzi nsimayo akuphikila kunyumba kwakeko
Manga siwa utm ayi uyu ndi wa mcp ndipo chakwela ndinzake kmso akuziwapo kanthu
Manganya ndiyemwe anaperekera zida kt skc afe pano tinamutuluka
Magenta anachoka kale muutim ali ndi chipanichake choir odyazake alibemuladu kuchiliba
Ndizonvesa chisoni kwa ansonda chilima sanali munthu wamba kuntundu WA AMalawi ife ngati AMalawi chilima tizamukumbukira komanso tizimukumbukirabe
A miko usi tsi a. U. T. M ndi a. M. C. P. Chipani chakupa anthu cha magazi
Manganya ndi poison
Akufuna kupusitsa anthu komanso part of cumpian
Kampeni , ndipo ndalama zikuchoka kwa Chakwera
Chintchora pakuti wosewa ndi akuba that's why Ali ndi fulu ndipo Amalawi tisadzayelekezeso kuvotela mbava izi
Analowa kale MCP amangokuputsisani ziwani kuti
Udindo omwe alinawo siwamuyaya
A ussi ali ndalama ndakalazo akutekutenga kwa anthu okuba a MCP omwe amatibela misonkho yathu
Ndekuti Ali mwa modzi amene anapha chilima. Koma a UTM sasiya kuyatsa makendule mpaka chiilungamo chioneke
Manganya akutinamiza ife a amalawi. Ndalama akulandira kuchoka ku Boma kuti adzigawa. Ken akudwara koma sakudziwa ayi. Ayi sitikugwirizana nazo kuti anthu akagwilitse ntchito chophaso cha unzika ayi. Aliyese akavote basi. Manganya ndiwa MCP ankangobisara kumbuyo kwa UTM. Manga anali kumthira kuwiri. Taphunzira kuti Manga ndi Yudas. Anagulitsa moyo wa Chilima. Za imfa ya Chilima zikuonetsa kuti sixikumukhudza za imfayo. Akushashalika kwambiri ndi ndalama za Chakwera. Ndalama zinari za ifeyo a Malawi anaba pogwilizana ndi Pulezident Chakweraa.
Manganya sakuchita bwino chifukwa anthu avutika ovutika Lero nthawi yawathera akufuna kunyengera anthu ndi sweet cholinga azingomva kusekemera mmilomo pomwe m'mimba mulibe kanthu (2)Keni msonda ndi atimke nawo alibe mphavu ku MCP ndi chifukwa akumalolera ku mwayankhura cholinga azipedza ndalama yogura matemba (3)pa chiyambileni cha ifa ija ine ndapbudzira za kuti MCP ndi chipani chamagadzi
Ken msonda ali mgulu la n, gonna uja palibe chamzeru chimene akupanga kuletsa ma candle cho zikuchita kuwonetseratu kuti akusowa mtendere moto ukwawotcha sakugona tulo mzimu wa Chilima ndi anthu 8 aja uli pamitu pawo mtendere adzawusowa moyo wawo wonse
Sakuunthandiza manganya akuononga kwambiri
Choyambilila manganya ndiwadyela khalidwelake ndiosiyanila ndi winiko chachiwili mtiko omwe alinaowo aphikile msima yodya mkaziwake ndi ana ake.
Manganya si WA UTM koma WA MCP
Manganya ndi wa Mcp musapusitsike and iyeyu ndi modzi yemwe akudziona kuti akhoza kupanga anthu kukonda so Mcp
Ulutsani kuti asapusisike amalawi Manganya munthu oyipa kwambiri
Manganya akupanga ndale kumene
akugwilitsidwa ntchito manganya aona kuti nthawi yatha 4years yose palibe chomwe achita kukweza zinthu basi anthu kumudzi akuvutika
Ken Nsonda kukula naye galu ameneyu akathetsere kwa Make
Kulira maliro kulibe malire
Oyipa ameneyo msondayo afuna pongopezeeapo ndalama kuchoka kuboma akagwere uku
Aliyense akavoti zoyiika malirezo ayi
Akhale iwowo ndi manganya wawoyo yamakabduulo yatenga mavote ose
Manganya anapeleka chilima komanso ndi wa map
Manganya ndi tikufelanji weniweni.
Ngongole it's just the waste of money palibe amene angabwenze
Manganyayo ndiwa chipani Chang'ona
Zovotera cimpaso cokha sitikugwirizana nazo ife aliyese akufunika kuti apange njira zoti aliyese azavote mwaufulu wake
Ngati akunena kuti opanda cha uzika asakabvote pamenepo pokha nde akunama chifukwa anthu ena chauzika chawo anayamba kuyendera kale kale mpaka pano sanapatsidwe zonsezo akupangila dala ndicholinga choti adzabere zisankho
Bola kumbvota opanda chauzika chifukwa kale timambvota opanda chauzika
Part of campaign akufuna kugula anthu aziwasatira akubiasalira kumbuyo kwa boma ndi wa MCP ameneyo
Ken Msonda alowelera bwanj za nyumba ya mwini ?alibe mphamvu yolesa candle lighting
Pepani tiyakha. Lelo. Manga. Alingati. Khoswe. Amati akakuluma. Iyeyo amapepeze. Cholinga. Chakuti. Tisamuve.kulumako. Ndimene Alili manganga. Muthu oyipa
Mannganya ndi udasi akupanga kampeni manganya
Ndipo zenizeni zunenedwa apapa ziii
Manganya ndi wa mcp osati utm ndipo imfa ya chilima manganya akudziwapo kanthu
Brother manganyatu ndi wa MCP kuyambira kale akupanga masewelo ake nde Ku UTM kujatu anangopitilatu ndiukazitape umtila kuwili. Nde zonse akupanga manganya ndi kampeni ya MCP
Manganya ndi wa mcp aliyense akudziwa amalawi musapusitsidwe
Manganya akuyenela kukuthidwa, this is just kampeni
Adaniathu ndiomwe timakhalanawo pafupi
Bwana trust mwasowatu
Sitikuvomerezana nazo zimezo
Ndalamazo tizitenge ndizathu
Ayi Mesa chipani chake ndixhomwechi cha MCP
Imene ija ndi ndale komanso campaign in other way,nde akanawalolanso ena achite nawo campaign yawo coz it's part malamulo
Manganya ndiwa MCP
Ndinu aboza inu ma properganda anuwo si azakupindulirani muzalira mukhaula mcp yiwinaso tikuziwa munatumidwa inu nd dpp mukufuna abale anthu abwelereso mumavuto azilowa munyumba 6 oclock zako izo
Part of campaign
Mukunena zowona manganya ndi wa mcp komaso akupanga kampen
Kanpeni. 2ndlama .za .chakwela. .3ndale
Phala akunenalo athu omwalila menemo fiti ameneyo
Akupanga kampeni ndipo ndi wa mcp
Ali part of kampeni
Aleselanji makandulo wachabe
Zovotela lb tisazalole chonde amalaw
Nsonda alibe mzelu ndipo alekeletu
Ken msonda asatiuze zo chita
Ken nsonda adatha
Ndikampeni ndithu