ZOMWE WAYANKHURA DAN LU ANTHU ADABWA NAZO PAMENE AMAMULANDIRA LERO KU NSONKHANO WA CHIPANI CHA MCP

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 20 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 189

  • @MarryUnyolo
    @MarryUnyolo 2 години тому +3

    APM my vote izi mzochititsa manyazi kukakamiza zinthu

  • @MarthaBango
    @MarthaBango 2 години тому +12

    Akuchita kuoneka kut akuchita manyazi😂😂😂

  • @MjombaMoosa
    @MjombaMoosa 2 години тому +4

    Lozani nzanu nyimbo ya bhooo
    Peter oyeeeee 2025 bomaaaaaa

  • @mariamwandwanga3035
    @mariamwandwanga3035 2 години тому +2

    Manyazi adan .kusowa zochita .za ziiii .adad my vote

  • @austenbushiri-cx1kh
    @austenbushiri-cx1kh 2 години тому +3

    Apm ❤🎉❤🎉 my vote

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 2 години тому +3

    Once upon a time, there was Chilima and Mia, komabe zabwino zonse Dan Luu ife tidakali pambuyo pa APM.

  • @cynthiakamwana6809
    @cynthiakamwana6809 2 години тому +1

    Zuchita kuoneka kuti,nyimboyo yodyera pasi pamtima ukudziwa kuti zonse nzabodza munyimboyi. Lozani zunu wooyeeeee. APM my vote❤

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile Годину тому +2

    Ambiri akhamukila ku congeresi chifukwa nkhalamba ija ikukakamila pa mpando

  • @DeenesNurudMeke
    @DeenesNurudMeke 41 хвилина тому +2

    Dpp my vote muona 2025 inuyo

  • @giftmakuluni
    @giftmakuluni 53 хвилини тому +2

    Dpp my votes❤❤🥰😍

  • @MlaziJames
    @MlaziJames Годину тому +2

    No vote zisiluinu a mcp

  • @hagayichiluwe
    @hagayichiluwe 2 години тому +4

    Chakwela my vote

  • @BarnetMwanyula
    @BarnetMwanyula 46 хвилин тому +1

    My vote dpp 💯/

  • @ShalomMtonda
    @ShalomMtonda 43 хвилини тому +1

    Apm my vote 2025❤❤❤❤❤

  • @PeterMsukwa-i1n
    @PeterMsukwa-i1n 32 хвилини тому +1

    APM my vote❤️

  • @kingsleydaud9094
    @kingsleydaud9094 Годину тому +1

    Mzimu wa Chilima ukukwapulani ,,mukuwonekaso mwamanyazi zisiru za anthu

  • @heavisonjames1203
    @heavisonjames1203 52 хвилини тому +1

    Komabe lozani zanu ija ndi number 1.
    😂😂😂😂😂
    Sine WA Dpp koma Utm

  • @MuhammadSamson-yz1kl
    @MuhammadSamson-yz1kl Годину тому +2

    Aaaa Danlu manyi okhaokha ine Munthu uyu kt wa chiyao ndimakaikira kuchiyao kulibe chitsiru ngati ichi

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 2 години тому +1

    Dan Lu idyani ndalama yamisokho ya malawi 🇲🇼 yo ife dpp woyeee

  • @SherifaG.Mlelemba
    @SherifaG.Mlelemba Годину тому +1

    Koma ngati nkusaka chakwaza,anthu azungulira mitu...Shaa! Akuti n'chiyani!???
    Popeza ndi ndale...Zikazavutanso,tizabweleranso.....🤔🤔🤔

  • @FebbieNjewa-g3k
    @FebbieNjewa-g3k 2 години тому +1

    APM my vote

  • @ElizabethMajiga
    @ElizabethMajiga 2 години тому +1

    Mesa mumati mwasita kiyimba, munali kwa atelala kosokeke kasuli ka chikangawa ka etiiii !!!! Boni kalondo sananame Ku ti tiwona zithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂

  • @johnjoachim3820
    @johnjoachim3820 37 хвилин тому

    Dan Lu nyimbo zako ndikuchitsa mu 🖥 yanga ndimaona ngat ndi iwe solo koma mmmm paja pamuthu

  • @YasinSabili-dj9xe
    @YasinSabili-dj9xe 2 години тому +1

    Apm my vote

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin 51 хвилина тому +1

    Ndimakumbukila chaka China ndinalandila msalu zachipani chilichomse
    Ndidzovalatu idzo sikuti akulandilawo kuti ndimavoti anu.mukunama atidye nawo amenewo
    Voti ili muntima mwawo

  • @ElizaSoko
    @ElizaSoko 2 години тому +1

    Akuloza iwe Dan lu 😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤

  • @WisdomMwale-j9h
    @WisdomMwale-j9h Годину тому +1

    Eeeh, Anthu awa ndi Amodzi Asiyeni!

  • @jamiajafali6619
    @jamiajafali6619 Годину тому +1

    Chimwendo Allah akakulange iweyo

  • @MpanjeHardware
    @MpanjeHardware 2 години тому +1

    Apm may vote

  • @JOSEPHTAPSON
    @JOSEPHTAPSON 2 години тому +2

    Kkkkkkkkk ife ndi mcp basi chete chete

  • @MaliGomani-z4k
    @MaliGomani-z4k 2 години тому +1

    Anthu akuoneka kuti sakukondwa 😂😂😂😂😂

  • @WiliWili-y2d
    @WiliWili-y2d Годину тому +1

    anthu akuopa chikangawa 😂😂😂😂

  • @mariamwandwanga3035
    @mariamwandwanga3035 2 години тому +1

    Akupha ndi inuyo a mcp😅

  • @NosiphoMazibuko-e9z
    @NosiphoMazibuko-e9z 45 хвилин тому

    Inu Dan lufani pangani kapeni nick chakwera mwana president chakwera akudya ndalama uko minister ndimwana wake nick chakwera chipani cha family ichi kd nick chakwera bwanji zamabwela kuzapanga kapeni iyeyu basi asigwira ntchito mu office inu muzivutika udindo ndimwana wake wachakwera ine chipani cha mcp ndidatuluka kuyambira pomwe adakhala mwana wake nduna yoyang'anila ku immigration ndidanziwa kuti chipa cha family komatu mwanawake zabwera kukapanga kapeni ya mcp km udindo amapatsa ife mamembera amcp ndikupanga kape yopangila nick chakwera kuti zapatse udindo kachikena amamayi kuvutika kwamalawi ozasindikira kodi tikufuna atuluke mwana wa president achakwera nick chakwera yemwe Ali nduna yoyang'anila ku immigration atandize abambo ake kapeni chifukwa chipani cha mcp ndicha family mawudindo akupanzana pachi family chipani choyipa icho mpaka mwana wa president kukhala nduna km amalawi kumangoyang'anila zotero

  • @SqueyaHosmane
    @SqueyaHosmane Годину тому

    History is best teacher

  • @FungulanReuben
    @FungulanReuben Годину тому

    APM my vote 😊

  • @bissankal774
    @bissankal774 38 хвилин тому

    Wachiyao mukutamikatu ku mcp mpaka munthu wankulu 😂😂😂😅

  • @BlazioKamagwira
    @BlazioKamagwira Годину тому

    kuseliku akuti safuna ndalama koma kufuna kudzasintha zinthu koma ndaseka kkkkkkkkk

  • @GeorgeChirwa-i8v
    @GeorgeChirwa-i8v 46 хвилин тому

    Adyeleni ndalamazo koma nyimbo zanu zizingabebe ngat zomwe mumaimba mmbuyomo

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa6267 40 секунд тому

    DPP my vote 2025❤❤❤❤

  • @thomasbotha9790
    @thomasbotha9790 3 години тому

    Mbuzi zekhazeka zili apo chakwera ni kawawa MCP nchipani cha ng'ona

  • @AndersonBishop-i2t
    @AndersonBishop-i2t 8 хвилин тому

    Dan lu ndi wa ku balaka mangochi kmaso wa mcp uja ndi mwana wa kuzi osati kuti mcp izimenye pa mtima ai kwa m'baluku mcp kulibeko sumungqwineso anawina iye uja chifukwa choti ndi.mwana wa bwno muzimo tiyeni muimiseso wina muone pa central mangochi ngat mungazaphulepo kanthu muzawaziwe anyamata apa boma kuti amangomudyela munthu ndi kumusiya iwe chimwendo

  • @FunnyKatchenga
    @FunnyKatchenga 38 хвилин тому

    Zosakoma anta, angotengana okhaokha kumalandilitsa nsalu,ati cholinga anthu aziti anthu akulowa Ku ng'ona party 😅😅😅😅 shame on you.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 55 хвилин тому

    Nkhondo ya pansi pansi ine Chilima kulibe mwayaluka inu Adani sory 🤣🤣🤣🤣🤣🤣

  • @LawrenceDickens-jk3zx
    @LawrenceDickens-jk3zx 25 хвилин тому

    Kamanjekete yomweyo😂😂😂 DPP my vote

  • @Samson-ve5rs
    @Samson-ve5rs Годину тому

    Apm my vote awa alephera nduna zopanda nzeru

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 42 хвилини тому +1

    Mwaiwala muja tinagwetsa ndede ku chikangawa chitsekoso atseka 😢

  • @NosiphoMazibuko-e9z
    @NosiphoMazibuko-e9z 55 хвилин тому

    Km amwene mcp yata basi inu zowoona okupangilani kapeni akhale Dan lufani km mcp nde basi yata vuto mcp palibe yemwe angakope anthu chifukwa chake akugula woyimba kusowa kwachipani inu amcp okupangilani kapeni yokopha anthu kuchipani Dan lufani

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 21 хвилина тому

    Inuyo Pagani zaddwanuzo dzuwa salozelana aliyese amalionakaye musiyeni dan lu

  • @PrinceThom-pe6ie
    @PrinceThom-pe6ie Годину тому

    MCP si political party koma music industry.

    • @wisdom20mkango49
      @wisdom20mkango49 Годину тому

      Copy and paste 😂😂😂😂 learn to write your own comments

  • @PatriciaAlomwe-oz8wc
    @PatriciaAlomwe-oz8wc 2 години тому

    Olo takhala osaona singachite kuvotera MCP bola ndiwalondore agogo anga kumanda

  • @ElizaSoko
    @ElizaSoko 2 години тому

    😂😂😂😂😂 APM my vote❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @NolityKondowe
    @NolityKondowe 7 хвилин тому

    Mcp my vote.Boma ndilomweli.

  • @OusieSaeed
    @OusieSaeed 24 хвилини тому

    Kumenya kugwetsa kwacha kulenphera kuidzutsa koma kudziwa kugwetsa ndege

  • @AbdulrazaqHussain
    @AbdulrazaqHussain 2 години тому

    May the best man win,next year

  • @JohnWalekana-z2f
    @JohnWalekana-z2f Годину тому

    Manyaka dpp my vote

  • @NiccoGama
    @NiccoGama 47 хвилин тому

    Kodi Dan lu sanarowetu DPP anali oyimba amalandila ndalama

  • @FlorenceDouglas-x5c
    @FlorenceDouglas-x5c Годину тому

    DPP my vote

  • @OnenessLestas
    @OnenessLestas Годину тому

    Chakwera my vote✓

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz 3 години тому

    Akufuna kudya nawo ndalama zaphweka Ku mcp zoo awo dyeraaaaaaaaaaaaa

  • @ElizaSoko
    @ElizaSoko 2 години тому

    Mulungu nde wasiya kuonatu kuti chikangawa awinesotu😤😤😤😤😤😤😤 azatikweze ndegetu tonse amalawi tikathele mnchikangawa ndipomwe azawine ameneyotu😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤

  • @veronicagullo9373
    @veronicagullo9373 Годину тому

    Mcp my vote

  • @WiliWili-y2d
    @WiliWili-y2d Годину тому

    iwe Dan lu kwao ndikumozambiqe kumangochi kulibe Dan lu

  • @AdamPetro-v2q
    @AdamPetro-v2q 11 хвилин тому

    Mmene mumkapha Chilima muja ,chitseko chanu chidatseguka???

  • @yamikanuledi1238
    @yamikanuledi1238 Годину тому

    A Dan Lu inu nde machende anu mwana opusa takusika basi

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere Годину тому

    Kodi UA-cam sanaipange kukhala ya anyamata a DPP pitani pa ground plz kuti adad anuwo azawine otherwise MCP ilamulaso 2025

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 53 хвилини тому

    Akupha ndinu agalu munabwelera bwanji m'boma muonanso mwapha chilima inu agalu

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 19 хвилин тому

    Musamalowetse zamulungu aaaaa inuyo ndinuwabwino kodi

  • @aggogokina8992
    @aggogokina8992 2 години тому

    Umphawi ukakupana nkusapilira umapanga zozichotsa nyota ndikuyaluka ponseponse.

  • @user-od5xn5iw8x
    @user-od5xn5iw8x 2 години тому

    Mesa mumati mwasiya kuyimba achisiru DPP boma

  • @WisdomMwale-j9h
    @WisdomMwale-j9h Годину тому

    Boma,,, Ndlomweri, kulibe kusintha!😂

  • @ChristopherMatemba-m4g
    @ChristopherMatemba-m4g 2 години тому

    Kuyamikila munthu yemwe wathenga forex yonse kumapita nayo ku American

  • @AndersonBishop-i2t
    @AndersonBishop-i2t 18 хвилин тому

    Mmmmmm chisilu masavege onse achimwendowo dan lu palibepo chimene akupangapo iyeo sangawine dan lu ndipo inu osangonena kuti tawagula bwanji mesa mukuwapasa ndalama km tionesana 2025 muonaso inu masavege mcp

  • @charlessulumba2521
    @charlessulumba2521 2 години тому +1

    😂😂😂😂😂 a funny party

  • @crytoniegrantliffa2431
    @crytoniegrantliffa2431 2 години тому

    Chimwendo ndiye ayi .......ndinu okakamiza zithu ife sitikufuna chakwera

  • @PatsonmahoweNyirongo
    @PatsonmahoweNyirongo 2 години тому

    Chakwera ndiye satana, kwake nkupha, kuba ndi kuwononga, sangawine or pang'ono

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 години тому

    Koma ineyo olo oyimba onse atatha kufa kumalawi koma dan lu sindingamunene kt ndioyimba komaso iweyo Dan lu kuti uziwe zoti ndi ofoila umati achiyawo saluza iwe apa siunaluze bolaso Sena

  • @ChimwemweMguntha
    @ChimwemweMguntha 52 хвилини тому

    BOMA ndilomweli kulibe kusintha

  • @ConeriasPhiri
    @ConeriasPhiri 2 години тому

    Mmmm chipani chamangazi uchisilu Adan.asowa pogwira

  • @GoefreyBanda
    @GoefreyBanda Годину тому

    Chala mmwamba Dpp yoye palibe angamake

  • @AndersonBishop-i2t
    @AndersonBishop-i2t 11 хвилин тому

    Chikangawa km kugwesa ndalama azuse kwacha cnanga akugwesa ndie chitukuko chake sakumukonda kumene ndipo okupha ndi chakwera ndi iweyo galu kaye kunyasa khope iwe mapwala iwe okupha chilima mesa munapha chilima munapha sadiki Mia munapha anthu 9 pa ndege ija chamba eti

  • @GloriaChiwanda-l6g
    @GloriaChiwanda-l6g 44 хвилини тому

    Potseka chitsekopo mwaiwalapo ku ekwendeni

  • @MadalitsoIbrahim
    @MadalitsoIbrahim Годину тому

    Nkhondo yapansi pansi yogwesa ndege?😂😂😂😂😂

  • @MpanjeHardware
    @MpanjeHardware 2 години тому

    Dpp yokha ndimene timanena kut manja mwamba

  • @SammieDickson-ln2hp
    @SammieDickson-ln2hp Годину тому

    Apm more fire😊

  • @OusieSaeed
    @OusieSaeed 24 хвилини тому

    Dan wapisilila madzi a udhu mwe achisilu

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 2 години тому

    Usiye zimenezo osamati chakwera woyee uziti kwacha

  • @FlorenceDouglas-x5c
    @FlorenceDouglas-x5c Годину тому

    Eheeee 😂😂nyimbo yozikakamiza olo manyazi Ulibe ?

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy 52 хвилини тому

    Chakweza zonse .. Dan Lu manyaka

  • @RajabLahlie
    @RajabLahlie Годину тому

    Mcp ma kape, zamanyazi no future,

  • @henryvesha4183
    @henryvesha4183 Годину тому

    Nanga za chilima utiuza zotani sunenako

  • @DeenesNurudMeke
    @DeenesNurudMeke 35 хвилин тому

    Ku show ya Mcp kkkk

  • @PhillipAcquaron
    @PhillipAcquaron 13 хвилин тому

    Shame on you Dan mwana wa Lufani

  • @EnerstManess
    @EnerstManess Годину тому

    Wayiwalatu mene amaphedwa chilima

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma Годину тому

    Vote ❤

  • @BandachisangaDoreen
    @BandachisangaDoreen Годину тому

    Dan laughed motu yomweyo boma ndi lomweri moto kuti buuuu

  • @gabrielben-vj2eb
    @gabrielben-vj2eb Годину тому

    Zianthu zosaganiza bwino

  • @Mahlodi_derickMaroala
    @Mahlodi_derickMaroala 27 хвилин тому

    Amufuna ku zomba uyu wathawa ndi ntcheni

  • @MaliGomani-z4k
    @MaliGomani-z4k 2 години тому +1

    😂😂😂😂😂sizikukoma

  • @PatsonmahoweNyirongo
    @PatsonmahoweNyirongo 2 години тому

    APM kumenya kugwetsa