Inu Dan lufani pangani kapeni nick chakwera mwana president chakwera akudya ndalama uko minister ndimwana wake nick chakwera chipani cha family ichi kd nick chakwera bwanji zamabwela kuzapanga kapeni iyeyu basi asigwira ntchito mu office inu muzivutika udindo ndimwana wake wachakwera ine chipani cha mcp ndidatuluka kuyambira pomwe adakhala mwana wake nduna yoyang'anila ku immigration ndidanziwa kuti chipa cha family komatu mwanawake zabwera kukapanga kapeni ya mcp km udindo amapatsa ife mamembera amcp ndikupanga kape yopangila nick chakwera kuti zapatse udindo kachikena amamayi kuvutika kwamalawi ozasindikira kodi tikufuna atuluke mwana wa president achakwera nick chakwera yemwe Ali nduna yoyang'anila ku immigration atandize abambo ake kapeni chifukwa chipani cha mcp ndicha family mawudindo akupanzana pachi family chipani choyipa icho mpaka mwana wa president kukhala nduna km amalawi kumangoyang'anila zotero
Dan lu ndi wa ku balaka mangochi kmaso wa mcp uja ndi mwana wa kuzi osati kuti mcp izimenye pa mtima ai kwa m'baluku mcp kulibeko sumungqwineso anawina iye uja chifukwa choti ndi.mwana wa bwno muzimo tiyeni muimiseso wina muone pa central mangochi ngat mungazaphulepo kanthu muzawaziwe anyamata apa boma kuti amangomudyela munthu ndi kumusiya iwe chimwendo
Km amwene mcp yata basi inu zowoona okupangilani kapeni akhale Dan lufani km mcp nde basi yata vuto mcp palibe yemwe angakope anthu chifukwa chake akugula woyimba kusowa kwachipani inu amcp okupangilani kapeni yokopha anthu kuchipani Dan lufani
Koma ineyo olo oyimba onse atatha kufa kumalawi koma dan lu sindingamunene kt ndioyimba komaso iweyo Dan lu kuti uziwe zoti ndi ofoila umati achiyawo saluza iwe apa siunaluze bolaso Sena
Chikangawa km kugwesa ndalama azuse kwacha cnanga akugwesa ndie chitukuko chake sakumukonda kumene ndipo okupha ndi chakwera ndi iweyo galu kaye kunyasa khope iwe mapwala iwe okupha chilima mesa munapha chilima munapha sadiki Mia munapha anthu 9 pa ndege ija chamba eti
APM my vote izi mzochititsa manyazi kukakamiza zinthu
Akuchita kuoneka kut akuchita manyazi😂😂😂
Zamanyazi kwambiri
Lozani nzanu nyimbo ya bhooo
Peter oyeeeee 2025 bomaaaaaa
Manyazi adan .kusowa zochita .za ziiii .adad my vote
Apm ❤🎉❤🎉 my vote
Once upon a time, there was Chilima and Mia, komabe zabwino zonse Dan Luu ife tidakali pambuyo pa APM.
Zuchita kuoneka kuti,nyimboyo yodyera pasi pamtima ukudziwa kuti zonse nzabodza munyimboyi. Lozani zunu wooyeeeee. APM my vote❤
Ambiri akhamukila ku congeresi chifukwa nkhalamba ija ikukakamila pa mpando
Dpp my vote muona 2025 inuyo
Dpp my votes❤❤🥰😍
No vote zisiluinu a mcp
Chakwela my vote
Mbuzi yamunthu
My vote dpp 💯/
Apm my vote 2025❤❤❤❤❤
APM my vote❤️
Mzimu wa Chilima ukukwapulani ,,mukuwonekaso mwamanyazi zisiru za anthu
Komabe lozani zanu ija ndi number 1.
😂😂😂😂😂
Sine WA Dpp koma Utm
Aaaa Danlu manyi okhaokha ine Munthu uyu kt wa chiyao ndimakaikira kuchiyao kulibe chitsiru ngati ichi
Iwe ndi mbuzi sure
Dan Lu idyani ndalama yamisokho ya malawi 🇲🇼 yo ife dpp woyeee
Koma ngati nkusaka chakwaza,anthu azungulira mitu...Shaa! Akuti n'chiyani!???
Popeza ndi ndale...Zikazavutanso,tizabweleranso.....🤔🤔🤔
APM my vote
Mesa mumati mwasita kiyimba, munali kwa atelala kosokeke kasuli ka chikangawa ka etiiii !!!! Boni kalondo sananame Ku ti tiwona zithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂
Dan Lu nyimbo zako ndikuchitsa mu 🖥 yanga ndimaona ngat ndi iwe solo koma mmmm paja pamuthu
Apm my vote
Ndimakumbukila chaka China ndinalandila msalu zachipani chilichomse
Ndidzovalatu idzo sikuti akulandilawo kuti ndimavoti anu.mukunama atidye nawo amenewo
Voti ili muntima mwawo
Akuloza iwe Dan lu 😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤
Eeeh, Anthu awa ndi Amodzi Asiyeni!
Chimwendo Allah akakulange iweyo
Apm may vote
Kkkkkkkkk ife ndi mcp basi chete chete
Boma ndilomweli
Anthu akuoneka kuti sakukondwa 😂😂😂😂😂
Ndipo kwambiri
anthu akuopa chikangawa 😂😂😂😂
Akupha ndi inuyo a mcp😅
Inu Dan lufani pangani kapeni nick chakwera mwana president chakwera akudya ndalama uko minister ndimwana wake nick chakwera chipani cha family ichi kd nick chakwera bwanji zamabwela kuzapanga kapeni iyeyu basi asigwira ntchito mu office inu muzivutika udindo ndimwana wake wachakwera ine chipani cha mcp ndidatuluka kuyambira pomwe adakhala mwana wake nduna yoyang'anila ku immigration ndidanziwa kuti chipa cha family komatu mwanawake zabwera kukapanga kapeni ya mcp km udindo amapatsa ife mamembera amcp ndikupanga kape yopangila nick chakwera kuti zapatse udindo kachikena amamayi kuvutika kwamalawi ozasindikira kodi tikufuna atuluke mwana wa president achakwera nick chakwera yemwe Ali nduna yoyang'anila ku immigration atandize abambo ake kapeni chifukwa chipani cha mcp ndicha family mawudindo akupanzana pachi family chipani choyipa icho mpaka mwana wa president kukhala nduna km amalawi kumangoyang'anila zotero
History is best teacher
APM my vote 😊
Wachiyao mukutamikatu ku mcp mpaka munthu wankulu 😂😂😂😅
kuseliku akuti safuna ndalama koma kufuna kudzasintha zinthu koma ndaseka kkkkkkkkk
Adyeleni ndalamazo koma nyimbo zanu zizingabebe ngat zomwe mumaimba mmbuyomo
DPP my vote 2025❤❤❤❤
Mbuzi zekhazeka zili apo chakwera ni kawawa MCP nchipani cha ng'ona
Dan lu ndi wa ku balaka mangochi kmaso wa mcp uja ndi mwana wa kuzi osati kuti mcp izimenye pa mtima ai kwa m'baluku mcp kulibeko sumungqwineso anawina iye uja chifukwa choti ndi.mwana wa bwno muzimo tiyeni muimiseso wina muone pa central mangochi ngat mungazaphulepo kanthu muzawaziwe anyamata apa boma kuti amangomudyela munthu ndi kumusiya iwe chimwendo
Zosakoma anta, angotengana okhaokha kumalandilitsa nsalu,ati cholinga anthu aziti anthu akulowa Ku ng'ona party 😅😅😅😅 shame on you.
Nkhondo ya pansi pansi ine Chilima kulibe mwayaluka inu Adani sory 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Kamanjekete yomweyo😂😂😂 DPP my vote
Apm my vote awa alephera nduna zopanda nzeru
Mwaiwala muja tinagwetsa ndede ku chikangawa chitsekoso atseka 😢
Km amwene mcp yata basi inu zowoona okupangilani kapeni akhale Dan lufani km mcp nde basi yata vuto mcp palibe yemwe angakope anthu chifukwa chake akugula woyimba kusowa kwachipani inu amcp okupangilani kapeni yokopha anthu kuchipani Dan lufani
Inuyo Pagani zaddwanuzo dzuwa salozelana aliyese amalionakaye musiyeni dan lu
MCP si political party koma music industry.
Copy and paste 😂😂😂😂 learn to write your own comments
Olo takhala osaona singachite kuvotera MCP bola ndiwalondore agogo anga kumanda
😂😂😂😂😂 APM my vote❤❤❤❤❤❤❤❤
Mcp my vote.Boma ndilomweli.
Kumenya kugwetsa kwacha kulenphera kuidzutsa koma kudziwa kugwetsa ndege
May the best man win,next year
Manyaka dpp my vote
Kodi Dan lu sanarowetu DPP anali oyimba amalandila ndalama
DPP my vote
Chakwera my vote✓
Akufuna kudya nawo ndalama zaphweka Ku mcp zoo awo dyeraaaaaaaaaaaaa
Mulungu nde wasiya kuonatu kuti chikangawa awinesotu😤😤😤😤😤😤😤 azatikweze ndegetu tonse amalawi tikathele mnchikangawa ndipomwe azawine ameneyotu😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤
Mcp my vote
iwe Dan lu kwao ndikumozambiqe kumangochi kulibe Dan lu
Mmene mumkapha Chilima muja ,chitseko chanu chidatseguka???
A Dan Lu inu nde machende anu mwana opusa takusika basi
Kodi UA-cam sanaipange kukhala ya anyamata a DPP pitani pa ground plz kuti adad anuwo azawine otherwise MCP ilamulaso 2025
Akupha ndinu agalu munabwelera bwanji m'boma muonanso mwapha chilima inu agalu
Musamalowetse zamulungu aaaaa inuyo ndinuwabwino kodi
Umphawi ukakupana nkusapilira umapanga zozichotsa nyota ndikuyaluka ponseponse.
Mesa mumati mwasiya kuyimba achisiru DPP boma
Boma,,, Ndlomweri, kulibe kusintha!😂
Kuyamikila munthu yemwe wathenga forex yonse kumapita nayo ku American
Mmmmmm chisilu masavege onse achimwendowo dan lu palibepo chimene akupangapo iyeo sangawine dan lu ndipo inu osangonena kuti tawagula bwanji mesa mukuwapasa ndalama km tionesana 2025 muonaso inu masavege mcp
😂😂😂😂😂 a funny party
Chimwendo ndiye ayi .......ndinu okakamiza zithu ife sitikufuna chakwera
Chakwera ndiye satana, kwake nkupha, kuba ndi kuwononga, sangawine or pang'ono
Koma ineyo olo oyimba onse atatha kufa kumalawi koma dan lu sindingamunene kt ndioyimba komaso iweyo Dan lu kuti uziwe zoti ndi ofoila umati achiyawo saluza iwe apa siunaluze bolaso Sena
BOMA ndilomweli kulibe kusintha
Mmmm chipani chamangazi uchisilu Adan.asowa pogwira
Kkkkkk komandiye
Chala mmwamba Dpp yoye palibe angamake
Chikangawa km kugwesa ndalama azuse kwacha cnanga akugwesa ndie chitukuko chake sakumukonda kumene ndipo okupha ndi chakwera ndi iweyo galu kaye kunyasa khope iwe mapwala iwe okupha chilima mesa munapha chilima munapha sadiki Mia munapha anthu 9 pa ndege ija chamba eti
Potseka chitsekopo mwaiwalapo ku ekwendeni
Nkhondo yapansi pansi yogwesa ndege?😂😂😂😂😂
Dpp yokha ndimene timanena kut manja mwamba
Apm more fire😊
Dan wapisilila madzi a udhu mwe achisilu
Usiye zimenezo osamati chakwera woyee uziti kwacha
Eheeee 😂😂nyimbo yozikakamiza olo manyazi Ulibe ?
Chakweza zonse .. Dan Lu manyaka
Mcp ma kape, zamanyazi no future,
Nanga za chilima utiuza zotani sunenako
Ku show ya Mcp kkkk
Shame on you Dan mwana wa Lufani
Wayiwalatu mene amaphedwa chilima
Vote ❤
Dan laughed motu yomweyo boma ndi lomweri moto kuti buuuu
Zianthu zosaganiza bwino
Amufuna ku zomba uyu wathawa ndi ntcheni
😂😂😂😂😂sizikukoma
APM kumenya kugwetsa