Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

Limpopo APM akuthilidwa poizoni ku mangochi masanawa Ntanyiwa akuulura anthu omwe akukapanga izi

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 12 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 81

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo 27 днів тому +9

    Oh ALLAH tithandizeni malawi tikuvutika mutetezeni peter

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 27 днів тому +6

    Ineyo ndizakhala okondwa ikazangoluza mcp ndimafuna chakwera,,,mwana wake,,, zikhale,,kunkuyu,,mkaka,,,anthu amenewa azagwire life imprisonment osazawapasa bail

  • @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh
    @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh 27 днів тому +4

    Comrade pls muomboreni Mutharika..........muimbiren fon ya direct

  • @FireKajambe
    @FireKajambe 27 днів тому +3

    Pharaoh tried to kill Moses when he was young but later pharaoh died before Moses . Eksodus 16

  • @user-hs4bm2yj8r
    @user-hs4bm2yj8r 26 днів тому +1

    Mulungu kutetezeni akapolo Anu, amene khumbo lawo ndikuombola dziko lathu

  • @OusmanBen-f4o
    @OusmanBen-f4o 27 днів тому +4

    Utsogoleri wabwino sukhala wamphamvu ndi kukhetsela mwanzi ayi,koma kukhala ndi mphamvu kwa anthu ochuluka okondwela ndi utsogoleri wakowo.Anthu pano sakondwela ndiutsogoleri wa Chakwela ayi nde asapange 4c anthu kut amukonde akulephela zambiri pa utsogoleri wake,achoke!achoke! achoke basi anzake alamulire mpandowu

    • @user-gg2qn7zf4m
      @user-gg2qn7zf4m 27 днів тому

      Koma kodi amalawi inu chikuchitika ndi chani mungosekelela zopusa ngati zimenezo muziwe kuti mulungu akulanfani chifuka palibe wa muyaya pa zikomo pano muziwe zimenezo

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff 27 днів тому +2

    Dzanja lanu mulungu wamakamu tetezani moyo wa peter langani onse oipayo

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 25 днів тому

    Mulungu alowelerepo ndithu,,, ndikuteteza Ana a Malawi

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 27 днів тому +4

    Angoyelekezaa

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula 27 днів тому +2

    Amuthanyiwa tangowaimbilani ku dpp ko muwauze chonde ndinu akuluakulu nonkhanokha 😢

  • @LetweebZwewe
    @LetweebZwewe 26 днів тому +1

    Amuphe ife chakwelayo tizamupha ndimanja ngati galu wachiwewe

  • @TechnicalSupport-lk9im
    @TechnicalSupport-lk9im 25 днів тому

    Yomweyo galu iwe ulula Thanyuwa agalu amenewa ayaluke

  • @UssenNjirinah
    @UssenNjirinah 27 днів тому +1

    Nde manganyu akutani ku Mcp ku

  • @GiftNasila
    @GiftNasila 26 днів тому

    Limpopo FM ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 27 днів тому

    Indeeeeee Mr Nkhanga zomwezo timakunyadirani mukuyimirira Amalawi Ambiri.
    Mulungu wathu wamoyo adzikhala Ku Mbali yanu Mr NTANYIWA osayiwalanso Mchimwene uko ku Bakili Muluzi TV Dzanja la Mbuye lidzikutetezani.

  • @GiftNasila
    @GiftNasila 26 днів тому

    Mata Nkhanga Zaino ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @blacksonpeshes5057
    @blacksonpeshes5057 26 днів тому

    mwadzuka sitafu yonse kumeneko. tikudikila zarelo ka 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @CathyYassimin
    @CathyYassimin 27 днів тому

    Oh ya rabbie tilozeren Muthu wabwino okhulupilira lnu ,lnde kwainu kulibe utsogoreli umenewu

  • @LindaTebulo-k4w
    @LindaTebulo-k4w 26 днів тому

    Just pray for Malawi may God help us

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula 27 днів тому +2

    Ayelekeze aone zosaona

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w 26 днів тому

    Palibe chobitsika pansi panthaka, kwa oipa kulibe mtendere, palibe tchimo lomwe lizabweretse mtendere pa umoyo wa munthu ndiponso zilibwino poti zaululika sapanga abwelerako amenewo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 27 днів тому +4

    Eeeee koma abale Mcp eishhhhhh mukamachita zanuzo dziwani kuti kunja kuno kuli Mulungu our God in heaven may you protect Peter muntharika in Jesus name Mulungu musalore chititsani manyazi satana

  • @NizigiyimanaChantal-c2p
    @NizigiyimanaChantal-c2p 27 днів тому +2

    Kudziwike kut mumatha Ambuye

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j 27 днів тому +1

    Chikangawa chakwera koma zooona eeeeish ukalibe ukhuta nyama za malemu atisiya popano popano

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 27 днів тому +1

    Moto kut buuuu❤📺💪💪💪💪💪✊✊✊✊🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 27 днів тому

    Malawi Chikangawa Party yadya Chilope Chosavuka nacho.
    Mpaka kuzapezeka akuwayika pa list anthu omwe anawapha kale Chilope chitalowerera . Koma Mr Lazarus its too much hmmmm

  • @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh
    @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh 27 днів тому +1

    Aimbireni fon ya direct a DPP

  • @RajaboGostihno
    @RajaboGostihno 27 днів тому

    Comrade let's build up our nation...all the corners of the nation 4:44 4:44 4:44 4:44 Durban south....

  • @LuciusMakupe
    @LuciusMakupe 27 днів тому +1

    DPP guys don't take for granted Samalani bas

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 27 днів тому +1

    Komatu achakwela zomwe mukupangazi mulungu akuwona siku ndilimozi chomanphela ana ayini ndichani kapena mukupeleka sembe kwazanu akunyanjawo mukamakhala muziziwa kuti nanuso makasu akudikila kukakumba zenje lanu mizimu yaathu mukuphawa ndiamene akakulandileni pakhomo lopapatiza

    • @lillynhlema9656
      @lillynhlema9656 26 днів тому

      Ndipo uyuy he has never been a pastor.....kuubusa kuja ankangobisalako

  • @user-wp9js5vu6s
    @user-wp9js5vu6s 26 днів тому

    Kuli mulungu kumwambaku 🤝

  • @PeterThomas-o9k
    @PeterThomas-o9k 25 днів тому

    Ukhale nalo dziko uzikonda wekha satana iwe watopesa chakwera your not right stress yakoyo usawaphe azako
    Otsalakwa uzimve muntimamo koma kulibe chamuyaya

  • @HendrinaNyirenda
    @HendrinaNyirenda 27 днів тому +1

    Ndie mwati hug yaku nsepe ija inali ya Judas Iscariot? Ndile zophana ndizachikape😢

  • @DavieMoyo-pe8vn
    @DavieMoyo-pe8vn 27 днів тому +1

    Umakwana iweyo

  • @ShakilahMbwanaa
    @ShakilahMbwanaa 27 днів тому

    Please dpp be careful this is getting worse to us all malawian their crying a lot so be careful then listen to Tanyiwa what him saying please

  • @DysonNakhaphe-bo4dl
    @DysonNakhaphe-bo4dl 27 днів тому

    😢😢tiudzeni mene zathela

  • @MarthaWemba
    @MarthaWemba 27 днів тому +1

    Noted

  • @clalesschisale3792
    @clalesschisale3792 27 днів тому +1

    Ndale zomwe akupanga a Mcp zikanakhala kuti nayo DPP OR UDF kapena utm imapanga zomwezi sibwenzi MCP itabwelelaso mu Boma chomwe akulimbirana ndi anzawo ndi chani kwenikweni kodi kukhala ochokela zigawo zosiyana ndikolakwika ?😢😢😢😢😢

    • @user-gg2qn7zf4m
      @user-gg2qn7zf4m 27 днів тому

      Kodi chakwera iye akuyesa kuti ndi wa muyaya?kudya kuno kuli mulungu

  • @Amgwagwa
    @Amgwagwa 27 днів тому +1

    Sikusinja kkkk

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb 27 днів тому

    Mulungu tetezani azitsogoleri ofunila zabwino Malawi amen

  • @user-ss9bj5eh6b
    @user-ss9bj5eh6b 27 днів тому

    Angoyelekeza awone dziko liwaukile tatopanawo ife

  • @BrianJoe-z7u
    @BrianJoe-z7u 26 днів тому

    Uthenga waurere thanyiwa

  • @wisekanyinji5377
    @wisekanyinji5377 27 днів тому

    Sakunamatu, mcp njakupha kuyambila kale, ndie sitikudabwa kuti nchito zawo nzamwazi

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q 27 днів тому +1

    Imeneyo nde mcp kaya poti enanu mukuionela chilendo koma ife tachoka nayo pakatali nanu muidziwe

  • @JoyceJJames-kj7tg
    @JoyceJJames-kj7tg 27 днів тому +1

    Zovuta kwambili ambuye andithandize

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb 27 днів тому

    Zikomo Limpopo FM radio station %

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 27 днів тому

    Zigandanga zaku ruanda and Israel zizipita mmakwawo, sitikuzifunanso mmalawi muno except those innocent ruandaniz

  • @EdnaSiyan
    @EdnaSiyan 27 днів тому

    Chipani chanji chongokhalira ku khetsa mwazi. A Mbuye ayendereni onse ali ndi maganizo oipa

  • @thokogwebe2337
    @thokogwebe2337 27 днів тому

    May God protect him

  • @MaryJefry
    @MaryJefry 27 днів тому +1

    Adadi athu okhawo utisiile

  • @PhilmonBanda-dm7nj
    @PhilmonBanda-dm7nj 26 днів тому

    Zophanazo nde zachibwanatu

  • @mikesandali8425
    @mikesandali8425 27 днів тому

    Iwe opusa kwambili....

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 27 днів тому

    Ngati anthuwo ndi aku Rwanda bwanji interview monga kuyankhulana nawo m'modzi m'modzi pomwe akulowa

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly 27 днів тому

    Mcp Thambani Thambani chipani cha magazi magazi mwazi mwazi

  • @Jasper-xk9iv
    @Jasper-xk9iv 26 днів тому

    Mcp yathapo palibe angaivotere

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 27 днів тому

    Ngati Ku DPP kuli achinyamata ovuta kwambili aja amadziyakhula ma social media kuti iwowo ndi anamandwa iyi ndithawi yawo kuti athane nadzo zigewengadzo,,zikufunika kuti onsewo mawa apedzeke kuti onse ndi wankulu wawo ndi mitembo zigandanga zatchabe chabe

  • @ChikumbutsochantzMakumba
    @ChikumbutsochantzMakumba 27 днів тому

    Amanyengeza

  • @FloLuhanga
    @FloLuhanga 27 днів тому

    Please adziwitseni a DPP awo adziwe tatopa kulira

  • @user-fh5yn8xk2k
    @user-fh5yn8xk2k 27 днів тому

    Muyelekeze

  • @JozzyNthinda
    @JozzyNthinda 27 днів тому

    Limpopo imakwana

  • @MartinNyirenda-w7s
    @MartinNyirenda-w7s 27 днів тому

    Dziko likupita kuti ili?😮

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 26 днів тому

    Kodi page iyi ili pa whatsapp

  • @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh
    @ModesterKaphwitiKunkhe-yc7oh 27 днів тому

    Aimbireni a DPP

  • @swintonchirwa1897
    @swintonchirwa1897 27 днів тому

    Atinkenawo ndi amene akakamila

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 27 днів тому

    Mulungu akuyendele ndi mabodza akowo

  • @Malani41
    @Malani41 27 днів тому

    Chamba

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 27 днів тому

    Kukakhala security yokwanila

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o 27 днів тому

    Mudzakhala nkhondo ya chiweni went mtsogolo muno

  • @modestermalunga
    @modestermalunga 27 днів тому

    😢

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 27 днів тому +2

    Wabodza iwe galu

    • @mikesandali8425
      @mikesandali8425 27 днів тому

      Mbuzi iyi yaboza

    • @mashallahleonard2793
      @mashallahleonard2793 26 днів тому +1

      Galu ndiweyo wachipan chokuphacho

    • @IssacMateyo
      @IssacMateyo 26 днів тому

      Kodi mesa amay ako ndakazako aja ndamene adavota chipani chakuphacho chikhale boma kulibetu chipani chosapha usanadzinamize galu mbuzi iwe

  • @user-rx4ck9ze1j
    @user-rx4ck9ze1j 27 днів тому

    Kutelo ndiye ikhala yazikwanje sure