Kodi nanga mesa pamatsamba a zodiak ndi enawo akuti koma zoti walandira ndalama anavomera?komanso 8million yo anaipanga transfer online pakamodzi Kodi sikhala ndi limit patsiku?
Ngati Pali umboni kuti ndalama zinalowa mu account yake iye akanawona kuti watuma ndalamayo ndindani then amufunse kuti zakhala bwanji ?,kutenga ndalama zisali zako ndi kuba kumeneko
She was supposed to return money to the owner because she became aware of who accidentally sent that amount of money. Transferring money from one account to another signalled an element of theft in her.
Kamtima kakuba Ali nako. MY OWN WXPERIENCE: I wanted her to advertize for me on an awareness campaign, and she insisted that I should just send the money without meeting or signing a thing. Ndinaona ngati ndalama zanga zipita. I withdrew
Siwakuba Tamia apopo apolice aziona Kaye information yankhani ndi mene nkhani inachitikila mtulutseni Tamia izo ndi chisomo chamulungu kuvomela anamuuza mkului kuti unditumizile ndalama wa shaut mulandi ine watson kuno Ku Durban SA
Ndiwakuba nanga anapitiranji Ku south Africa ngt ndalamayo sanatengedi ndi iyeyo
umenewo ndimoyo wakuba ndichifukwa amalawi tikuvutika ndiumphawi tidazolowela zaulele
,,,😂😂😂same Story life goes on with straggle....sapasa pamanja guys amene anyambisa mawu awo analakwisa *(SAPASA PAMANJA)*
Otumiza tiyeni tizionesesa, osamayikana mmayesero Malawi wavuta uyu tonse tikudziwa chonde!!😊
Tamia ndi wakuba kumene akufuna kukolora pamene asanalime mmmm ntsikana iwe umuziwe yesu ndi ophunzira ake 12
😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊
kkkk
Kkkkkkkkk true indeed
Waba abweze zonse .apange back to sender kwa mwini wake wa ndalama .nkhani inthepo .ngati iyeo akufuna ndalama akagwire tchito kujoni kweko it's fine.
Yakwiya ndi mizimu😂😂😂😂😂
Ndiwakuba ameneyi sanakantawa
Ameneyo sanabe cos zinagoneka iyeyo kukana
Sanarakwise
Mr. Sam Mavitha share me the underground song. Please please. " Undiphunzitse"
Oky tamia alakwitsa ku samutsa ndalama zoti sizake pa umunthu guys
Mbava imeneyo boss😂😅😂
Chimene chimamupangitsa kusintha account yake nkubwela pomamukananso nzakeyo kuti sanaziond ndalama,nde kubako kumeneko
Mwina amaona Ngat ndi mwayi wake
Kodi nanga mesa pamatsamba a zodiak ndi enawo akuti koma zoti walandira ndalama anavomera?komanso 8million yo anaipanga transfer online pakamodzi Kodi sikhala ndi limit patsiku?
Tamia ja siwakuba,ndipo sikutiso walakwitsa ai ameneo ndi manner😅😅
Siwakuba amusye
Kusamutsa ndalama kokhako ndkubakumeneko
Koma ngati police sagwira ntchito moyenerera ndie kuti ali mbali yake
SApatsa pa manja unali mwai wake
Ndikuba kumeneko amagwidwe
Yes kumeneko ndikuba. Chifukwa mwiniwake anadziwika komaso kupta ku joni kunali kusowa mtendele ndi tchimo
Akanakhala wakuba sakanabwelako ku south
Anacenjeretsa ndipo ndidolo mbava
Munthu sungatenge ndalama zoti sizako , kumeneko ndi kuba , amupani apolice kuti apereke ndalamazo.
Ndikuba kumeneko Amangidwe ameneyo
Ngati Pali umboni kuti ndalama zinalowa mu account yake iye akanawona kuti watuma ndalamayo ndindani then amufunse kuti zakhala bwanji ?,kutenga ndalama zisali zako ndi kuba kumeneko
mbuz imanya pomwe ayimanga kkkkk wakhoza
Eya analakwitsa ndi moyo wakuba
Anaba akufunika abweze ndalama zamwini
Eya Tamia analakwinsa chifukwa munthuyo anatumiza by mistake mwanchidule kumeneko ndkuba
Zalowa zokha 😅 amujata bwa
Ndiwakuba ameneyo.Akanazibweza ndalamazo
She was supposed to return money to the owner because she became aware of who accidentally sent that amount of money. Transferring money from one account to another signalled an element of theft in her.
Zinangochitika koma iyey siwachoncho mumadziwa ukaona ndalama satanas amakulo iyey ndimunthuy angokambilan zandendele
Zatendele
Kkkkkk eeee kma zavuta mayeselo awa
Koma ameneyi wayaluka chaka chino nkhani chake chachuluka uhule ulimomo apaso akuba kkkk zachisoni
Sanabe koman zangochitik alanakhal iwow akanatan😥😥😥😥
😂😂😂😂sizochtanso kufunsa ndkuba kowonekera kwaumbuliii
Amai amenewa ndi mbava yoopsya
Siwakuba wapereka yekha wachola kunyumba kwake?
Kkk
Kamtima kakuba Ali nako.
MY OWN WXPERIENCE:
I wanted her to advertize for me on an awareness campaign, and she insisted that I should just send the money without meeting or signing a thing.
Ndinaona ngati ndalama zanga zipita.
I withdrew
Tamia ndi mbava chifukwa amamufusa iye amakana
Siwakuba Tamia apopo apolice aziona Kaye information yankhani ndi mene nkhani inachitikila mtulutseni Tamia izo ndi chisomo chamulungu kuvomela anamuuza mkului kuti unditumizile ndalama wa shaut mulandi ine watson kuno Ku Durban SA
Kudziko lapansi kulibe yemwe samaba kungoti timangosiyana mabedwe.Tamia asayankhulidwe chipongwe Chifukwa cake zaoneka lero
kuba kumenekoo
uku ndi kuba basi
Eya ndiwakuba ammeneyo ndipi wazionongeka cv
Timvele nawo brother zimenezi 😂😂😂😂😂😂
Ndikuba anakana bwanj atamutumizila?
Chakuba chimenecho ayse
Ea ndiwakuba coz nga munthuyo anamuuza kt warakwisa number anayenera kuvomereza ndikubweza ndaramazo
Wakuba bas
Or ndili ine ngatenge😂😂😂😂
Ndiokuba anapitilanji kunja
Mabigi ameneyu sanabei mutakhala inu mungatani amalawiso umbuli udakula inu mungatani
Ndikumba kumeneko ikhale kuti ndiyake sakanasitha account
Sangalakwitse Mulungu sapereka pa manja aaaa
Kumeneko ndi kuba umaona ngat zalowa Za manja lende Za sefukila masikwanozi
Zaziii kungo funapo ma comment athu ku UA-cam
Kumeneko ndi kuba analakwisa
Akanakhala kt siwakuba akanabweza ndalama kwa mwini wake koma ngati sanabweze ndiwakuba
Siwakuba ai km muthuyo amamuyesa
Kkkkk zonsayenda bwanjik apa 🤔🤔
Mmmm PA easy zimachitika
Ndiwakuba
Kumeneko ndikuba abweze ndaramayo
😂😂 km yooo
Ayitu analakwisa akangovomela ndikumubwenzera mwiniwake yo if zili zoonadi
Anapanga umbav
Akanabweza ndalama zaeni ake bas
Pena chilungamo chimafunika ndithu uku ndikuyaluka choncho munthu ndiwachichepere mbiri yako yikuonongeka eish zandikhuza bwanji bola abwenze aona kuti apanga bwanji chamwini ndichamwini basi tamia uzivere chisoni
komwe uliko
Amayenela kubweza ndalamayo kwa miniwake chako ndi chako chamwini ndi chamwini basi
Chilungamo ndichakut Tamia analakwitsa kwa kukulu Mistake ngt imeneyo mix kwa munthu otiso akuchita naye malonda sanayenera kupanga zimenezo Apo nkhan ndi kubweza ndalamazo bas.
Ndiokuba ameneo
Kkkkkk km khani zake 😊
Ndi wakuba ameneyo😮😮
Mbava imeneyo
Ndiwakuba ameneyo
Ndiwakuba basi khani ikuzikamba yokha big
Kumeneko ndikuba sakazisakusa ndalamazo
Ea niwakuba iyeyo anakavomela
Ndiwakuba ndi chifukwa chan anasintha acount
Kumanena chilungamo Tamia ja ndi wakuba
Ameneyo.ndiwakuba
Kwambiri.akufuna
Nzake.angwire
Ntchito.yopanda
Malipiro
Oimba wakuba mbala?😂
Ndiwakuba kunonso zinachitika chimozimozi ndipo anagamulidwa kukaseva 2yrs chifukwa three qts yandalama anayipeza
Ndye yake Tamia mistake siyako
Mulungu amapatsa mosiyana osalora munthu kulanda zomwe Allah wapelereka mu mwezi wa Ramadan uno
Ndiwakuba basi aaaa
ngati otumiza ndalama yo inali mistake iye ndi kukana ndiwakuba
Siokuba km anachita kumungayila
Ndiwakuba ameneyo 😂😂😂
4 y
😂😂😂ndiwokubaameneyo
Ndiwokuba basi
Sanalakwitse
Mmmm ndiwakuba
Pamenepo analakwitsa anaba, chifukwa analandira ndalama yoga khala yake komanso anaziwitsidwa kuti siyake koma iye ndikupanga chitsankho choyisintha account
Sana chite bwino
akanakhara kt siwakuba akanabweza ndaramazo