Chifukwa Chimene Anthu Amamudera Miracle Chinga

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лют 2025
  • #malawimusic #scandal

КОМЕНТАРІ • 240

  • @BerthaMpeusa-m4f
    @BerthaMpeusa-m4f 5 днів тому +1

    Continue mimi God is with you😍😍😍😍

  • @CharityMbofana
    @CharityMbofana 3 місяці тому +16

    Ntengo umene ulindizipatso zabwino umakumana ndi miyala yochuluka kwabas more love miracle ♥️

  • @TelezaGapala
    @TelezaGapala 4 місяці тому +5

    You are blessed Miracle that's why people are fighting you, continue doing the work of God, i love you

  • @FigoMalosa
    @FigoMalosa 12 днів тому

    ❤❤ I love ur song. Miracle

  • @GraceBanda-t4r
    @GraceBanda-t4r 2 місяці тому +3

    The more you fight with her the more God will fight for her that's how God is GOD Bless YOU MIRACLE CHINGA FROM ZAMBIA

  • @rabeccamasebo6261
    @rabeccamasebo6261 4 місяці тому +5

    If you see people stoning the tree, it means there are fruits in that tree.Miracle is supposed to be happy because of those persecutions. Her gift attract the enemies heavy. They are stoning her to bring her down.
    What God blesses no man can put it down.
    I love you miracle.

  • @OliviaZakutha
    @OliviaZakutha 2 місяці тому

    I love this gurl 💗💖

  • @MarthaGama-q1o
    @MarthaGama-q1o 4 місяці тому +8

    Nkhani imeneyi ambiliwa ndi nsanje chabe , Miracle imabe njiiii! Ndipo Mulungu amene untumikila sadzakhala chete adzakumenyela nkhondo iwe uli chete.

  • @BlessMpoto
    @BlessMpoto 25 днів тому

    Mayi wa mulungu don't move side or take another way coz u lost live but u may continue to preach the word of God and pray in the of jesus amen

  • @RabeccaMwikho-f9h
    @RabeccaMwikho-f9h 4 місяці тому +1

    What ever koma ndi role model waine foleva😘😘😘😘😘😘 I love you miracle

  • @CharityMaudzu
    @CharityMaudzu 3 місяці тому

    I love this gal alot💓💓

  • @BeautyMwale-p6d
    @BeautyMwale-p6d 4 місяці тому +16

    The more people hates miracle,the more God blesses her I love you mimi

  • @Stargdali
    @Stargdali 3 місяці тому +1

    Go ahead mom
    God loves you more❤

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh6276 2 місяці тому

    Mimi ali cha moyooo mwanayuuy eeee more blessings mimi

  • @ShiraKondowe
    @ShiraKondowe Місяць тому

    ❤❤❤❤❤❤ love miracle

  • @IwombaaMwanza-fn3xf
    @IwombaaMwanza-fn3xf 22 дні тому

    When you are good you are good . continue with your good works forget about the failures who are rumour mongers. 🎉

  • @JimChikwasha
    @JimChikwasha 4 місяці тому +2

    The Top becomes the topic, bravo Miracle

  • @InnocentMakungwa
    @InnocentMakungwa 4 місяці тому +1

    I love u ndipo sindizasiya mama,takusowa kwa mbiza ku,muzabweretso

  • @WonganiMbuluwunde
    @WonganiMbuluwunde 4 місяці тому +1

    We really love her....kip it up miracle

  • @towerankhoma1380
    @towerankhoma1380 4 місяці тому +5

    I love her

  • @SandrahMwandira
    @SandrahMwandira 4 місяці тому +1

    When people talk much of you it means you are alive... Keep up dear don't turn back ❤❤ you

  • @AREXHarod
    @AREXHarod Місяць тому

    Endabe usatope munthu wamoyo ayenera kukumana ndimikwingwirima koma ukhurupirire murungu azakuteteza 🎉🎉❤❤🎉

  • @Anneschirwa
    @Anneschirwa 2 місяці тому +1

    mtengo omwe ulibe zipatso siugendedwa ayi,,,,,Miracle is a blessed woman

  • @GraceBanda-t4r
    @GraceBanda-t4r 2 місяці тому +1

    AFuna amugwetse mmene anagwetsela amai ake koma uyo Mulungu azamusunga azamusogolela Santana niwaboza love you change from ZAMBIA

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 4 місяці тому +1

    Beautiful girl ❤❤❤❤

  • @SeraKumwenda
    @SeraKumwenda 3 місяці тому +2

    Anthu mli nd nsanje 🎉ife timakukondabe❤❤❤

  • @LucciahDyson
    @LucciahDyson 4 місяці тому +1

    Miracle My Fav😢❤

  • @TRINTYDAFTER
    @TRINTYDAFTER 3 місяці тому

    I really love her the way she is

  • @ManessChagoga-oo3fk
    @ManessChagoga-oo3fk 2 місяці тому

    mimi you will stay my role model

  • @luciapita
    @luciapita 3 місяці тому

    Watching from Mozambique

  • @PeterMkwala
    @PeterMkwala 4 місяці тому +1

    We love your music and your representation if few hate you don't mind them just go forward

  • @VeronicaSekobi-is6dk
    @VeronicaSekobi-is6dk 4 місяці тому +6

    Nice🎉

  • @ELIZABETHTHUNYANI-un3oz
    @ELIZABETHTHUNYANI-un3oz 4 місяці тому

    Miracle you are loved ❤❤❤❤

  • @JamesWandari
    @JamesWandari 4 місяці тому +2

    Power mimi

  • @gearardphiri1506
    @gearardphiri1506 4 місяці тому +1

    I love her

  • @moreenchibade5562
    @moreenchibade5562 2 місяці тому

    Akufuna kumulanda chili mwayiyeyu Koma ndolephera ndi jelous lawo Mwanayu amalimbikira uku akuti Ambuye mundithandize❤

    • @Doreen58moyo
      @Doreen58moyo Місяць тому

      ❤ambuye adzakhara nawebe muthaw zonse
      Miracle ❤

  • @EstherSainani
    @EstherSainani Місяць тому

    I love you Mimi 💕

  • @DanielChinkwaso-xp7dv
    @DanielChinkwaso-xp7dv 4 місяці тому +3

    Miracle ndiwanzeru, osamamunena.

  • @shinekaipa6398
    @shinekaipa6398 4 місяці тому

    Miracle Chinga God is with u no matter what,thamanga mwana wankazi thamanga

  • @GidaKachitsa
    @GidaKachitsa 3 дні тому

    Nice

  • @CostasChakujumaLuhanga
    @CostasChakujumaLuhanga Місяць тому

    The more they hate the more God bless ❤

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 4 місяці тому

    Lots of lv baby girl be strong this world is 2 wicked

  • @MonicaThocco
    @MonicaThocco 3 дні тому

    Miracle sakondedwa sadekha ndi wopupuluma ,ndi mwana wolimba mtima ,ineyo sindimukondanso ndi zochitika zake ,pa maliro amai ake anayimba nawo group ya anthu woyimba nyimbo mkukhalanso yoyambitsa nyimbo, ndinamuona kuti alibe umuthu sanawonetse kumva kuwawa ndi imfa ya mai ake ,palibeponso za umzimu ngakhale amayimba nyimbo za umzimu

    • @IsabelThaundi
      @IsabelThaundi 3 години тому

      Hmmmmm mudzamvetsa nthawi inayake mayi, kulira maliro mogudubuka sikukhudzika. Nanga bwanji mumadya nyama osakhala week osadya? Muziganiza chili kwainu

  • @QueenMakamu
    @QueenMakamu 4 місяці тому

    God is with you sis

  • @ellahmaulidi2874
    @ellahmaulidi2874 3 місяці тому

    My favorite

  • @MasterMapira
    @MasterMapira 4 місяці тому +1

    Miracle, we need you here in Chiradzulu.. love you ❤ mamaa

    • @FloraNtakwile
      @FloraNtakwile 4 місяці тому

      Indeee, ku Chiradzulu kuno timamukonda, no matter what, adani osadziwa kuti Mulungu amakonda aliyense Komanso aliyense padziko pano ali ndi machimo ake zimangotengera kuti enawo timawadziwa tokha kumbali

    • @SamLangwe
      @SamLangwe 2 місяці тому

      No comment

  • @shahidahoward
    @shahidahoward 4 місяці тому +1

    Ilove you mama ❤

  • @HajiraMustapher
    @HajiraMustapher 4 місяці тому +2

    Ndipo miracle amazondedwa ngati ine iiii iwe miracle tiye tidzikhala Bola pakati pathu Pali ubale wathu ndi mulungu basi zinazo zitichedwetsa

  • @MaryChalera-t9g
    @MaryChalera-t9g 25 днів тому

    Mtengo wopanda zipatso sugendedwa miracle dont give up

  • @FotinalaKefasi-w6l
    @FotinalaKefasi-w6l 28 днів тому

    go ahead miracle to gospel

  • @lisajekiseni9162
    @lisajekiseni9162 4 місяці тому +2

    Pakurisa beans 😂😂😂 koma ndika huredi

  • @LinlyMatheweKufakwina
    @LinlyMatheweKufakwina 3 місяці тому +1

    Zabodza ibe miracle wakula ndikumuona nsanje ku Malawi 😂😂😂😂

  • @FauzaTabu
    @FauzaTabu 4 місяці тому +1

    Amalawi plz tisiyile mulungu akaweluze ekha

  • @TiwongeNgwira-jz6ge
    @TiwongeNgwira-jz6ge 2 місяці тому

    People are jealousy,,, Miracle is beautiful

  • @maggiemahewe2728
    @maggiemahewe2728 2 місяці тому

    Mwana opanda mantha God bless her

  • @FurnitureAuctions
    @FurnitureAuctions 4 місяці тому +2

    We still love her no matter what ❤❤❤ so much love miracle

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 4 місяці тому

    Mfana uja ndi walutso Komas ndi chi vibe that's why athu amamuda (ukakhala pa top umakhala topic)
    Sam mavita good explanation

  • @MercySKayange
    @MercySKayange 4 місяці тому +1

    May the Almighty God fight for you Miracle

  • @GoergeMwale
    @GoergeMwale 4 місяці тому +1

    Nice one

  • @LonelyChakula
    @LonelyChakula 2 місяці тому

    I love you miracle

  • @ZelifaMchenga-gt1yt
    @ZelifaMchenga-gt1yt 4 місяці тому +1

    Mtengo wazipatso ndio ugendedwa go.a.head mama timakukonda.ndipo umatiimira kwachinyamata

  • @ZioneKalepa
    @ZioneKalepa 4 місяці тому +3

    Olo anthu amunene koma ine nde sindingasiye kumukonda❤

  • @albertinamartins2593
    @albertinamartins2593 3 місяці тому

    Te amo

  • @JamesALLi-m8i
    @JamesALLi-m8i 4 місяці тому +4

    Yes Miracle she is beautiful 😍 🤩 girl 👧 she have powerful message to Malawi 🇲🇼 people's be strong 💪 girl 👧 we love you so much 💗 💖 💓

  • @DianaJussab
    @DianaJussab 4 місяці тому +1

    Munthu ukakhala pa top ambiri amakuda, koma ineyo ndikuona kuti zilibwino azimuda choncho chifukwa amuchulukisa matsiku amoyo wake pamene kuti aliyense aziyamikira sachedwa kumu thyola ndichoncho et more fire miracle Ife mwaiwe timapezamo mayankho asiyeni enayo ndimanong,onongo awowo akuchedwa

  • @ElizabethNgambi-e9f
    @ElizabethNgambi-e9f 2 місяці тому

    I love you miracle even if some people hate you

  • @SamuelMunthali-qt3zt
    @SamuelMunthali-qt3zt 4 місяці тому +2

    Pa zosez mboni wake ndi mlungu miracle maso patsongolo thamanga ccter

  • @ROSELIKHWAKHWA-y7e
    @ROSELIKHWAKHWA-y7e 4 місяці тому

    Nice🔥

  • @ElizabethPhiri-q3h
    @ElizabethPhiri-q3h 4 місяці тому +3

    Mtengo opanda zipatso palibe angagendemo😮

  • @sammalvitha
    @sammalvitha  4 місяці тому +1

    Subscribe

  • @MerryMusonda
    @MerryMusonda 4 місяці тому

    Khawa njeee miracle aliyese amapaga zake

  • @JaneHunga
    @JaneHunga 2 місяці тому

    Mtengo opanda zipatso sugendedwa❤

  • @Mohammed-sk1fy
    @Mohammed-sk1fy 4 місяці тому

    Kuno Kupanje,...Bola bundle ❤❤

  • @WellingtonCharumuka-p3u
    @WellingtonCharumuka-p3u 4 місяці тому

    ❤❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @GidaKachitsa
    @GidaKachitsa 3 дні тому

    Ilove u mama takusowan ife

  • @AlefaMwanyenga-b8h
    @AlefaMwanyenga-b8h Місяць тому

    Miracle amaimba bwino ndlipo nyimbo zake ndimazikonda, koma vuto amavala mabuluku zimene ndinyimbo zake sizigwilizana Komano Mai ake sitinawaonepo atavala choncho

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 4 місяці тому +1

    Mtengo umene uli ndi zipatso ndi umene umagendedwa osadanda akakhala Amalawi anazolowera kukhala pampando. Oweluza basi😮

  • @Stiv.Nkhoma-t9o
    @Stiv.Nkhoma-t9o 3 місяці тому +2

    kwa ine ndiwa sekular uyu

  • @SandrahMwandira
    @SandrahMwandira 4 місяці тому

    Be strong dear

  • @MuhaaMpate
    @MuhaaMpate 4 місяці тому +1

    Amalawi ndi choncho njiru basi muphulika amalawi thats why zimakhala zotivuta

  • @ShalifPetros-zh6gw
    @ShalifPetros-zh6gw 4 місяці тому

    Brother chilungamo choti miracle ndioslakwa khan anthufe ndi sanje lomwelo omwe amakamba zmenezow azibwera nd umbon please coz sibwino kuipisilana mbili

  • @GraceSakala-j1k
    @GraceSakala-j1k 4 місяці тому +1

    Miracle chinga amadedwa chifukwa chazochita zake uyo mwana utsilu ulimo angamukonde ndizitsilu zinzake

    • @GraceBanda-t4r
      @GraceBanda-t4r 2 місяці тому

      So tonse tikonda nyimbo zake ndife zintsilu? From Zambia

  • @Stiv.Nkhoma-t9o
    @Stiv.Nkhoma-t9o 3 місяці тому +1

    akanatchiza chimoz amaphatikiza zovula ni gospel pamene sziyendela limoz chifukwa chake amandinyasa

  • @VioletPondani
    @VioletPondani 4 місяці тому

    I love you miracle umatha iweyo

  • @julietdzikolo1060
    @julietdzikolo1060 3 місяці тому

    I pray for God's protection and blessings on her, may she be covered under His wings and abide safely.

  • @MphatsoNtaya
    @MphatsoNtaya 19 днів тому

    Yes zilibho km kuphoda too much

  • @BlessingNyirongo-u5o
    @BlessingNyirongo-u5o 4 місяці тому

    U still loved darling ❤

  • @Mafunance
    @Mafunance Місяць тому

    Miracle you are loved❤❤❤

  • @ElizabethKachina
    @ElizabethKachina Місяць тому

    Anthu nsiyeni mwana wanzanu a Malawi tiyeni tisiye mabodza kuyipitsa ana azanga Mulungu akunkhululukireni

  • @MalitaPhiri-f2u
    @MalitaPhiri-f2u 3 місяці тому

    More love Mimi❤️❤️😍

  • @Isaiahbotoman
    @Isaiahbotoman 4 місяці тому +1

    Adha awa saziwa kufufuza khani.

    • @dieternazitwere8949
      @dieternazitwere8949 2 місяці тому

      Ameneyudi ndi zoba moti video inatchuka ija yowonetsa Miracle akuba juice nkumaika mchikwama cha nzake mu shop ija sanaiwone, she was in school uniform around 2016/17

  • @TapiwaMtawali-t7e
    @TapiwaMtawali-t7e 2 місяці тому

    Keep the fire burning love

  • @EuniceGwalidi
    @EuniceGwalidi 4 місяці тому

    Kodi anthu mumasiya zanu zonyasa zija bwanji? Musiyeni mwanayu za yahwe izi ikani zanu mwabisa zija musiyeni miracle please 🙏🙏

  • @dorcaskaunda1965
    @dorcaskaunda1965 4 місяці тому

    Forward never backwards

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 4 місяці тому

    Iwe time radio inakhalako ufulu fm??

  • @evancesankhani4458
    @evancesankhani4458 3 місяці тому

    Nice narration koma use or show more pictures or references when narrating. For example, when u say page ya Mikozi inalemba so, so... put that post in your video so that people know how credible u are

  • @MaxwellChiona
    @MaxwellChiona Місяць тому

    Mavalidwe ake sabwino pogwilizana ndi za Mulungu, kudzipenta siza Mulungu

  • @GeorgeMoyo-w9m
    @GeorgeMoyo-w9m 4 місяці тому +2

    Zaziiiiii kusowa zochita basi, Even amene wabweretsa nkhaniyi apa, peza zochita zina

  • @EllahEllah-hu7hi
    @EllahEllah-hu7hi 4 місяці тому +1

    Ndipo amawaposa n keep fire burning Miracle

  • @AmosJames-iv6wz
    @AmosJames-iv6wz 2 місяці тому

    Uyuyu ndi definition yoti mulungu amatiteteza ...