Nthawi sidikira munthu umafuna azituwa ndi maluzi mdzina loti ali loyal kwa APM? Iweyo usachedwe ndikumapanga follow moyo wa munthu wina kuti zimuthera bwanji, he is full grown man he knows what he is doing
Ndayesera kutuzura maso anga kut ndionesese ma comment a anthu amene ali mbali ya MCP, kma ndaona modz yekha bas amene wakomenta kut MCP my vote. Ma comment onsewa munthu modzi bas ndili ine mkanangokhala chete ndthu😂
Kulibe Ali ndi udindo kusankha chofuna ndi anthu angati atuluka ku DPP, kabambe, Kondwani ambiri Dan lu alakwa chani leave him I and others will love him
Ngakhale ineyo kupita kukamuchezera nzanga ndy kumupeza akumvera nyimbo ya dan lu nditha kubwerera kunyumba sindingachezenso ndioipa kwambl dan lufan crc
Inetu zinthuzi ndazikonda kwambiri achinyamata sanadane ndi Dan komano akudana ndi ulamuliro omwe Dan akusatila now pempho ndiloti tiyeni achinyamata 2025 tikapange zomwe zamuonekera Dan zikakhaleso chimodzi modzi ndi pothana ndi ulamulilowu
Dan lu machende ako ndipo ndakutuluka namapwala iwe umaimba bwino km pa zimene wapangazi tchende lako ndipo nyimbo zako zonse mdachosa muphone mapwala ako
1) Atupele Muluzi, Danu Lu akhale chitsanzo chako. Atapanga ubale ndi MCPoop(=MCManyi) anthu amutuluka. 2) Chitsanzo ikhale UDF ya abambo ako. A John Tembo ananenetsa kuti iwowo sanapangepo ubale ndi UDF polimbana ndi DPP ya Bingu👈Uzikumbukira izi. 3) Chitsanzo chowawa ndi UTM. A MCPoop anakanitsitsa kuti iwowo sanapangepo ubale osayinirana ndi UTM. Kenako anapha Chilima. Anga ndi malangizo. Ubale sitipanga ndi Nyau.
Asiyeni oyimba onse apite ku MCP we don't care about that what we need is freedom, peace in malawi,,,boma liti lomwe anagulitsapo fetereza 100,000 kufuna kupha apwawi
Palibe zimene mukukamba inu munthuyu sadya kwanu ndichisankho chake kodi wakupwetekani kwambiri inu adpp ayiayi musiyeni nzanu ndi M'malawi dan lufann pezani artist wina or Gibo piyason atha kumayimbira chipani cha dpp komanso amayimba kale mukufuna chiyani kwa dan
Olo ayimbe sangayimbe momwe anayimbila dpp akunama
Kodi Dan lu school yao anapita naye patali? Cfk munyamata ngat uja sangasapote boma ili mcp m'mene tikuvutikila Dan lu chisilu chamunthu
Am from mangochi 😢 but l will leave bro dan lu ..my vote dpp
Adan mwaganiza bwanji kufuna kutchuka kapena bwanji km ndiye muli pa topic osati patop MN Malawi wakudan🤣🤣
Ine kuchokera Ku Lilongwe Dan Lu ndikape ndipo ineso ndamutsika
Inenso ndamutuluka
Nthawi sidikira munthu umafuna azituwa ndi maluzi mdzina loti ali loyal kwa APM? Iweyo usachedwe ndikumapanga follow moyo wa munthu wina kuti zimuthera bwanji, he is full grown man he knows what he is doing
Dan lu ndamutuluka akhoza kundphesa ngat chilima
Saziziwa ndale ameneyu, komanso ndichisakho chake
Even me am from Ty ndamutuluka dan
Dan lu is full with mad and he don't know what he is doing he still young
Nde zimene mukupangazi mupindula chani😂😂😂😂 a Malawi tamaonan nkhani yojama pezan zina zochita
Dan Lu ndi kape kwambiri
Osalikonda dziko lake mwachidule kungoti ndi wa dyera
Km guys tizaname chakwera anthu atopa naye kabasi km ndikudziwa kugwa kwandalama kumalawi zamanyasi ndalama daily kugwa ai zamukanika chakwera economic yamukani dziko zithu zikufuta kumalawi ndeno wina kubwela kumayamikila za mcp zikufutani chifukwa anthu kumalawi adazindikila zoyiopa amata kuzoona zabwino amayamikila km khuluyu zamukanika chakwera
Dan lufani ndi kachisiru chakwera walephera kulamulira malawi waoneka kut ndi mburi sanalowe nkalasi zikuchita kuonetsa umbuli sizinthu
Dpp my vote, Dan Lu saganiza my boh
Wamisala ameneyo kukonda ndalama
Musiyeni Dan, iyeyo Ali ngati civil servant, amagwira ntchito ndi Boma lolamura.
I salute the Senas from. Chikwawa. they don't waste time in talking or singing they act ask chakwera nkasi for referance
Ndasiya kumupanga follow Dan Lu apite uko
Ndamu Tsika Da Lu
Dan lu sakudziwa komwe akulowera akungoyendela mwabi uja oti chagwa mumbale ndi ndiwo 😮
Chilungamo ndichimene chimavuta iyeye kumbali yake zilibho mukutaya nthawi ndinthu musiyeni Dun lu ndichisakho chake 😂😂😂
Chenjezo kwa anthu oyimba zandale muononga nazo nyimbo zanu khutilani ndi momwe mukupezera zandalezi pena zosaykisaso
Ndayesera kutuzura maso anga kut ndionesese ma comment a anthu amene ali mbali ya MCP, kma ndaona modz yekha bas amene wakomenta kut MCP my vote. Ma comment onsewa munthu modzi bas ndili ine mkanangokhala chete ndthu😂
Saziwa chomwe akuchita, akukwera chipani Cha ng'ona zoonadi😂😂😂
Mbuzi iyo amupanga follow nde abale Ake basi
Muthu akamafuna kufa amayamba kufa mmakutu kumuuza osamva, zabwino zimene akuyamikila pamenepa ndiziti? amenewa akuvuta kuwamvesesa, komano ndalama sizimatha tinazipeza ndipo tizazisiyaso zomwe tilinazo muthawiyo MULUNGU amapeleka muthawi.
Ngakhale mumusike kma ife tili nga! To follow him
Muzipanga trening Kae kuyankhula ko mukuzilumaluma bwanji apa aaaaa
Uli mbari iti nyan iweso? Ige kuno kumangochi zikutiwawa musiye sam mavita
Zafika poti aliyese emwe dzina lake likumayambira ndi dan ndikumamupanga unfollow ndikuona ngat zawo ndizimozi agalu amenewa🙄
Hustling ngati mmene iweyo ukumanenera za iye Dan Lu amene
Sindingamvelenso nyimbo zake ndi kape ameneyo
That’s the truth 😊
kod ndingampange unfollow bwanji mthila kuwili amenei 🤣🤣🤣🤣
Dan lu ndi chidzete sakudziwa pomwe Ali ai ndipo ndamutulukanso iyah
Ka mutu ka kadzungulira (mtima wake wazungulira mutu👉♥️wazungulira👉😇)tsakudziwa chimene akuchita
Kulibe Ali ndi udindo kusankha chofuna ndi anthu angati atuluka ku DPP, kabambe, Kondwani ambiri Dan lu alakwa chani leave him I and others will love him
Adani Lu akumudwisa Malawi ayenera ku sika mapoete nhamata zimamuyera ku Dpp a ayenera ku kala ku Dpp ngati zili ndalama ha mavuto wokawoka
Anali ndani wanga mkale wangowonjezera udani
Malawi yomse sindinaone munthu opusa ngati Dan lu😂😂😂
Dan lu ndayamba kukuda aise pazomwe wapang wayamba kundi nyasa ndi zikuda
Nkhani ndi malamulidwe ,achimwene, inuyo zilipo zina simukudziwa yanu ndi ya You tube yomweyo. Tisiyeni ife womwe tikuganiza mozama kwambiri. Muzakhulupirira tsiku lina maganizidwe anu akakhwima.
Angowoneka ngati nyau akavala za mcp zakezo
Waswala pangono kufa siyeni akafere komweko
Titi agone ndi njala zanuizo mumutukwana mutopa ife tetitimutsike ndithudi azichimwene anga ndi chisankho chake zikomo
Ngakhale ineyo kupita kukamuchezera nzanga ndy kumupeza akumvera nyimbo ya dan lu nditha kubwerera kunyumba sindingachezenso ndioipa kwambl dan lufan crc
Mpeni wakuthwa mbali zonse umapha atipha Dan Lu tichenjele
Pezani zina zoti muzilankhula chifukwa dan lu zake zikutheka chakwera kumenya kugwetsa
Gulu ameneyo komaso zochita zake ndichimodzi modzi ndi hule wakubala
Kape uyu Dan ndipo ndi kamwana kosakula panchombo
Koma ma representer muzipangako proved before musanabwere ndi programs
Masatanic asiyeni azipanga zawo izi ndizomwe anagwilizana kumidima kwawoko asativetse mutu ife
Iweyo sam imila mpando wa u president tiwone ngati unga kwanitse.
Uchitsiru leave Dan lu alone he has Rights
Dan lu wandinyasa ndipo ndikangokumana nawo Kwake kwatha
Iyeyo ndi mbamva
Dan Lu ndidolo 🎉 mbambande
Dan lu wapanga apa zosayenda Alibe mbali yeniyeni ali ngati lezara,amdala yatesiye wee pela ayao itunyalayisye ngawa twasisile iyayi
Ineyo ndikudziwa kuti iyeyo akungofuna ndalama, dyera yakula pa iyeyo mwina waona kuti watsala pang'ono kodi siMutharika yemwe ampulumutsa pakati pompa, ndiye bola amusunge bwino
Inetu zinthuzi ndazikonda kwambiri achinyamata sanadane ndi Dan komano akudana ndi ulamuliro omwe Dan akusatila now pempho ndiloti tiyeni achinyamata 2025 tikapange zomwe zamuonekera Dan zikakhaleso chimodzi modzi ndi pothana ndi ulamulilowu
Iam from lilongwe but Dan Lu ndimkamusata but now ndamutuluka and iwill never back gain wapanga unve
Dani lu mwangodya zimenezo voti yanga ndi apetar mutalika ❤❤❤
Akufuna kufatu uyu
So ma followers amagula Ufa kunyumba kwa dan lu ,zitsilu za mu social media 😊
Dan lu ndikape akuopa kufa
Koma ine vote yanga ili pa dpp
Mbuzi imeneyi sizaidera bas
Dan luu adzafa osauka dyera too ubwino wake amakwera zipani zakufa amagwersa zipani mwachinsinsi
Musamaneneso kuti ndi kaswili
Muzinena kuti galu alikumbuyoyu.
Dan lu machende ako ndipo ndakutuluka namapwala iwe umaimba bwino km pa zimene wapangazi tchende lako ndipo nyimbo zako zonse mdachosa muphone mapwala ako
Kuno ku nsanje dan lu ndimamukonda koma ndamutulu alibe nzelu ndi opusa
Koma muzakonzeke mukazamabweranso of course Dan Lu ndi kape kwambiri wapanga iye
Siyani ndale achimwene please
Kukana kukaimba ku conversation ya DPP kunamizira kudwala galu ameneyi
Yense akubakira dan lufani mgalu kwabasi
Nsanje ndi nkhani imodzi yomwe pa national anthem ikukambidwa momvekabwino.
Inu osapanga zanu bwannj
Mwasowa chochita eti,mmalawi analozedwa ndithu brain ndindani anazichosa kuti tizingomvera zopusa zilizonse nkumamvera umbuli Ndi nsanje.
Danlu walowa usataniki gayez chonde Dpp ndiye vot yanthu
Kodi dan lu aziendela maganizo anu alibe chisankho ngat munthu ? Kkkkkkk anthu mulibe manyazi kkkkkkkk
1) Atupele Muluzi, Danu Lu akhale chitsanzo chako. Atapanga ubale ndi MCPoop(=MCManyi) anthu amutuluka.
2) Chitsanzo ikhale UDF ya abambo ako. A John Tembo ananenetsa kuti iwowo sanapangepo ubale ndi UDF polimbana ndi DPP ya Bingu👈Uzikumbukira izi.
3) Chitsanzo chowawa ndi UTM. A MCPoop anakanitsitsa kuti iwowo sanapangepo ubale osayinirana ndi UTM. Kenako anapha Chilima.
Anga ndi malangizo. Ubale sitipanga ndi Nyau.
Asiyeni oyimba onse apite ku MCP we don't care about that what we need is freedom, peace in malawi,,,boma liti lomwe anagulitsapo fetereza 100,000 kufuna kupha apwawi
Nthata ya njala mbuzi Dan lu
Mavitha ndi wa DPP wayambaso ndale?????
Nyimbo siku koma..... Inuyo guys izi simbali yanu pangani Zina mutitaisa thawi nonse awiri😂😅😂
Tilibe naye ntchito kachitsiru gag
Dan Lu ndi Munthu woganiza kwambiri ndipo
Anthu wotengeka ndi ndarama hmmm sidzimuthandiza izi. Koma or manyazi ndithu
Tazingo jamani yanu guyz mukuchedwatu iye wavaya basi😂😂😂😂😂😂
Lebo la wachiyao wangalusya asiye asa.agwiritseso ntchito
Dun lu wawonesa kupusa kwake pa a chinyamata that's y achinyamata amutuluka am one of them
Palibe zimene mukukamba inu munthuyu sadya kwanu ndichisankho chake kodi wakupwetekani kwambiri inu adpp ayiayi musiyeni nzanu ndi M'malawi dan lufann pezani artist wina or Gibo piyason atha kumayimbira chipani cha dpp komanso amayimba kale mukufuna chiyani kwa dan
Akunama Dan _lu ndichisilu
Guys asatichedwetse D Lulu apapa waonekeratu kuti wadya ndalama ameneyo osazamuvotela ngati akufuna kuimilira U MP ndi munthu osathandiza
Ndinkayesa munthu
Dan Lu dyela basi kufuna ndalama
Dan lu samakhala ndi moyo chifukwa chama followers tisaiwaleso zimenez.
Am also muyao but this did I left him
Kodi dpp yapwetekedwa kwambiri lu ku joina mcp simunati
Mukuyesesa man
Dan Lu ndi mthira kuwili
Mbuzi yamuntu
Anatsikidwa kalekale kapeyi