Розмір відео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показувати елементи керування програвачем
Автоматичне відтворення
Автоповтор
Atimenyela nkhondo mulungu osati munthu ai
Kaya anthu achepe pa zionetselozo. Koma chachikulu ndi chakuti cholinga chaziwonetselozi chakwanilitsidwa. Madandawulo adziko apelekedwa.m'modzi Odandawula ndine.
Kodi chamupha ndi chani simukunena mwatani kodi? Kugoti atisiya basi mzimu wa chilima wayamba kwaitna aziwona zagoyamba
Anamwanso gonsolosi wina ndikukatenganso Elube ndiye mphamvu zinachuluka.
Anthu amene akuziona ngati ndi mulungu wa Malawi ayamba kufa mulungu wayamba kuyankha anthu osauka
Mawu ndi omwewo tatopa ndi chakwela Mr chilangawa 🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊
Times_so Nanu dzimene mwalemba nd izi different 😢
Nkhalamba ijatu sikufa mophweka akufa ndi mnyamata wanu wayamba kufa dziwaloyo,ngat sanafe km sagonerai
kkkkkkk kunena kwa ndithendithe. Aliyese adzafa ase usamathe mau ngati ndiwe wambewu
Anali a mcp anthu onsewa kaya adya chimbazi kuchoka ku mboma
Kod akuwerenga khanizi ndi brian Banda mulipa changutu
Boma si M C P Boma ndi Malawi
Bravo guys
Nanga thupi la Chakwera lifika liti m,dziko lathu lino? Akubanja mwawauza kale ? Nanga dziko ,mwaliuza zotani ? Auzeni anthu zoona . Maliro sabisa.
😢😢😢😢😢😢
Amutsatiratu chilima chakwera
Next year Kuli khondo osati masewera
Nkhani ndi mfundo basi osati kuchiluka
Paja zirizonse mumati anthu agulidwa. Ndiye ku ma demo kunalibe amalawi aja mumawati akutumani. Amalawi akana ma demo, kodi lero mutiuza kuti anthu anyemeredwa ma billion angati
za ziiiiii
Malamulo a mavotedwe, a dziko lathu tikuwadziwa, tisapondeleze anthu ena poti alibe chitupa cha unzika, be civil guys,
Where is brain Banda here?
Iwe uyu ndi brian Banda mboli yako osamalemba zithu zosiyana ndizomwe zili mu video ayi usiye zachikapezi
zaziii zioneserero zopanda mfundo
mutopa kkkkk mwamva kuwawa kunja kwa boma simunathe
Koma zoti ng'ona yafa nzoona?
😂😂😂😂😂😂😂 kaya
Ndemwati akwataine???
Akapanga zimenezo ndiye mavoti Azavuta kuti athu azavote mumuuze crocodile wanuyo
Timuuza iweso bilimankhwe wakoyo umuuze
@@hastingsbnyirongo athu osapota crocodile Maoneka chikangawa team imeneyo
Iii zilikotu ziliko..
Garu wafayo mukut mkulu wapolisiyo alibwino bwino ku mortuary koma unyolo unali kutiko panthawi yomwe amafayo inu
Ndiye mwati awelenga ndi Brian Banda eti
nawonso amatinamiza uyu mwina ndi brianda junior kkk
Ife sitimaziwa akadalengeza ma radio
Tikawapeza azikakodza Malo
Kupolice dothi lagwa lankhasa
Tiyenazoni
Mwanamatu boss uyu ndi E kamzikiti
Dziko lamalawi lafika paugalu tsapano
Boma ndilomweri Sitikusintha ai mpak 2030 wooooo
Makosana ma video anu amangojamajama bwanji
Timazifuna koma kuopa ku wire
kodi Brian ndiwophweka mwalemba kuti wowelenga ndi Brian banda kuwona wowelengayo ndi wina😂😂😂😂😂😂
Kodi bwanji mumakonda kudula dula nkhani .
That's true
Mau mzika iliyose ili ndiufulu ovota
Za chitipa zinayamba pa nthawi ya dpp ndipo unya uwona palibe kusintha boma boma ndilomweri
Mchiyambi chabe ichi ngati sizitheka zomwe tikufuna tizatuluka anthu ambiri
Koma Brian Banda uyu nde ndi uti?! Kkkkk
Kkkk
Nonsense
Iyambe kunfa nkhalamba yozikozera ija kaye
Koma ng ona afatu kumalawi tisangalale sopano
Ubwino wake mulungu amatenga yemwe wamufuna akule achepe,,,, osati zomwe mukufunazo
Akutelotu kuti ngona ya ngogwa itava kuti Ngona izake yafa nayoso Yangogwa tiziva
Kkkkkkkk 😂😂😂😂
😂😂😂😂
Zaziii
MuLungu ndi wachikondi ndipo sangalore kuti Ana ake akhale akulira mpaka kale 2025 MuLungu sangatisiye tokha...
Mukulira chiyani anzathu
Nde mwati thupi la malemu chikangawa tiika liti ? 😂😂
Kd afa ndi chani ameneyo
Timayesa chakwela basi kayikeni nyamayo filijimo
Atimenyela nkhondo mulungu osati munthu ai
Kaya anthu achepe pa zionetselozo. Koma chachikulu ndi chakuti cholinga chaziwonetselozi chakwanilitsidwa. Madandawulo adziko apelekedwa.m'modzi Odandawula ndine.
Kodi chamupha ndi chani simukunena mwatani kodi? Kugoti atisiya basi mzimu wa chilima wayamba kwaitna aziwona zagoyamba
Anamwanso gonsolosi wina ndikukatenganso Elube ndiye mphamvu zinachuluka.
Anthu amene akuziona ngati ndi mulungu wa Malawi ayamba kufa mulungu wayamba kuyankha anthu osauka
Mawu ndi omwewo tatopa ndi chakwela Mr chilangawa 🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊🐊
Times_so Nanu dzimene mwalemba nd izi different 😢
Nkhalamba ijatu sikufa mophweka akufa ndi mnyamata wanu wayamba kufa dziwaloyo,ngat sanafe km sagonerai
kkkkkkk kunena kwa ndithendithe. Aliyese adzafa ase usamathe mau ngati ndiwe wambewu
Anali a mcp anthu onsewa kaya adya chimbazi kuchoka ku mboma
Kod akuwerenga khanizi ndi brian Banda mulipa changutu
Boma si M C P Boma ndi Malawi
Bravo guys
Nanga thupi la Chakwera lifika liti m,dziko lathu lino? Akubanja mwawauza kale ? Nanga dziko ,mwaliuza zotani ? Auzeni anthu zoona . Maliro sabisa.
😢😢😢😢😢😢
Amutsatiratu chilima chakwera
Next year Kuli khondo osati masewera
Nkhani ndi mfundo basi osati kuchiluka
Paja zirizonse mumati anthu agulidwa. Ndiye ku ma demo kunalibe amalawi aja mumawati akutumani.
Amalawi akana ma demo, kodi lero mutiuza kuti anthu anyemeredwa ma billion angati
za ziiiiii
Malamulo a mavotedwe, a dziko lathu tikuwadziwa, tisapondeleze anthu ena poti alibe chitupa cha unzika, be civil guys,
Where is brain Banda here?
Iwe uyu ndi brian Banda mboli yako osamalemba zithu zosiyana ndizomwe zili mu video ayi usiye zachikapezi
zaziii zioneserero zopanda mfundo
mutopa kkkkk mwamva kuwawa kunja kwa boma simunathe
Koma zoti ng'ona yafa nzoona?
😂😂😂😂😂😂😂 kaya
😂😂😂😂😂😂😂 kaya
Ndemwati akwataine???
Akapanga zimenezo ndiye mavoti Azavuta kuti athu azavote mumuuze crocodile wanuyo
Timuuza iweso bilimankhwe wakoyo umuuze
@@hastingsbnyirongo athu osapota crocodile Maoneka chikangawa team imeneyo
Iii zilikotu ziliko..
Garu wafayo mukut mkulu wapolisiyo alibwino bwino ku mortuary koma unyolo unali kutiko panthawi yomwe amafayo inu
Ndiye mwati awelenga ndi Brian Banda eti
nawonso amatinamiza uyu mwina ndi brianda junior kkk
Ife sitimaziwa akadalengeza ma radio
Tikawapeza azikakodza Malo
Kupolice dothi lagwa lankhasa
Tiyenazoni
Mwanamatu boss uyu ndi E kamzikiti
Dziko lamalawi lafika paugalu tsapano
Boma ndilomweri Sitikusintha ai mpak 2030 wooooo
Makosana ma video anu amangojamajama bwanji
Timazifuna koma kuopa ku wire
kodi Brian ndiwophweka mwalemba kuti wowelenga ndi Brian banda kuwona wowelengayo ndi wina😂😂😂😂😂😂
Kodi bwanji mumakonda kudula dula nkhani .
That's true
Mau mzika iliyose ili ndiufulu ovota
Za chitipa zinayamba pa nthawi ya dpp ndipo unya uwona palibe kusintha boma boma ndilomweri
Mchiyambi chabe ichi ngati sizitheka zomwe tikufuna tizatuluka anthu ambiri
Koma Brian Banda uyu nde ndi uti?! Kkkkk
Kkkk
Nonsense
Iyambe kunfa nkhalamba yozikozera ija kaye
Koma ng ona afatu kumalawi tisangalale sopano
Ubwino wake mulungu amatenga yemwe wamufuna akule achepe,,,, osati zomwe mukufunazo
Akutelotu kuti ngona ya ngogwa itava kuti Ngona izake yafa nayoso Yangogwa tiziva
Kkkkkkkk 😂😂😂😂
😂😂😂😂
Zaziii
MuLungu ndi wachikondi ndipo sangalore kuti Ana ake akhale akulira mpaka kale 2025 MuLungu sangatisiye tokha...
Mukulira chiyani anzathu
Nde mwati thupi la malemu chikangawa tiika liti ? 😂😂
Kd afa ndi chani ameneyo
Timayesa chakwela basi kayikeni nyamayo filijimo
Anali a mcp anthu onsewa kaya adya chimbazi kuchoka ku mboma
Anali a mcp anthu onsewa kaya adya chimbazi kuchoka ku mboma