Ntanyiwa sadaneneko kuti Chakwera wamwalira mukatelonso amene mukutelonu mukunama, ndatsatira bwino MA vn ake onse kuyambira dzuro atasowa kwa kanthawi koma zomwe ine ndinamva ndi zoti Ali ku chipatala cha Garden city ku south Africa, komanso musayiwale, 2018-2019-2020 mu nthawi ya Peter muthalika ambiri amakambanso nkhani ngati zomwezi president akasowa,nde monga ine sindikuwona cha chilendo choti mpaka Ena azimangidwa nazo, anthu akufuna Baba wa dziko atiwuze kuti wayenda bwanji ku UNGA koma kuli ziiiiiiiiii😢😢😢😢
Kunkuyu wachamba, panopa maiko usi akukozekela kunka ku state house, mkadakonda manganya akadantulitsa pasi udindo chimwendo kkkķkkk mimba njuu kulibe kusintha atsogoleleri kwa manu konko
Ntanyiwa umangidwatu iwe ndi bodza lako misleading Malawian ndi za bodza,ngati ulibe zolankhura kumakharako chete pena,ngati momwe amachitirako a Bon Kalindo amazakharako chete pene osati kubwetuka
Pali anthu ena amene simumusata munthu yi, please ma post ake sananene kuti president wafa koma anati Ali ku chipatala cha Garden city hospital basi
Mwat born kalindo akamamusak saoneka km ndasekatu 😂😂😂😂 man of God glory to God born kalindo pangolin my brother
COMLADE IFE SITINGATAYE NTHAWI KUPEMPHERERA CHIGAWENGA CHIMENECHI CHAZUNZA ANA A ISRAEL, CHIFE BASI TIKACHIIKE IYAAAA
Ntanyiwa sananene kuti wamwalila...Tikumutsata bhobho...osamunamizila
Kkkkk wabodza iwe umati chani uli ndi pakamwa
KAPE NDIWEYO WA CHIKANGAWA NGATI SIMUTSATA BWINO NTANYIWA UPANGE ZAKO, NTANYIWA MOOOOOOFIREEEEE , CHIKANGAWA WAFA AKAKUMANA NDI PRESIDENT WATHU SKC ,IYE AMAONA NGATI WA MUYAYA IYAAAAA
Uyu koma zokamba zake.Timva ziti.Poyamba amati president wamwalira.pano akuti president akupita ku MUST ku Thyolo?
Tidzaona mawalo kuti chakwera akusewera nawo masewero agolf
Ife sitimu pemphelera reason tili ndi njala he take our money going to Unga for shopping.
Ntanyiwa sananenepo kuti president wamwalila apo pokha musanamizle
Mmm sananenepo kuti wamwalira ayi ife tikuwasatira bwino bwino koma zikanachita bwino kuti Mr Chikamgawa akanafa iyaaa munthu wanji womva mavuto anthu ake
Ntanyiwa sadaneneko kuti Chakwera wamwalira mukatelonso amene mukutelonu mukunama, ndatsatira bwino MA vn ake onse kuyambira dzuro atasowa kwa kanthawi koma zomwe ine ndinamva ndi zoti Ali ku chipatala cha Garden city ku south Africa, komanso musayiwale, 2018-2019-2020 mu nthawi ya Peter muthalika ambiri amakambanso nkhani ngati zomwezi president akasowa,nde monga ine sindikuwona cha chilendo choti mpaka Ena azimangidwa nazo, anthu akufuna Baba wa dziko atiwuze kuti wayenda bwanji ku UNGA koma kuli ziiiiiiiiii😢😢😢😢
Mwayankhula zoona
Ine ndamunatu chakwerayo akumwa magagada
@@MoosaTrouble-o7p broh wationjeza abusatu aja
Chipita ndi chitembo ??
Koma achakwelawo iwowo pamene akhala amangukhala ndidziwembubwanji osamasangalatsa amnthuawo akasakebonikalindo chifukwachiani bonikalindo safuna zopusa komaso iwowo adakamatopa ndikuganizakuti mdzikomuno amnthu adwachitedze ndipange bwanjikuti ndapulumutse kodi mesapaja adali abusapaja lelo mudziti mmatenda aaa kkkk kaya
Dzuro walengezamaliro lero ukulengeza matenda munthu yemweyemweyo? Iwe ulibe zogwirika ndiwekapekwabasi
Akasewerabwanji golf munthu oti mwamupha? Mbavainu mungofuna udanitsa anthu inu mukudya masupageti kunjakwanuko zipanganizanuka bonikalindo asamalachani alimwanaoopsya ngati adzafa ndinu anthuodanitsa munthu opemphera nchisaleyo ufuna adanenaye
Aaaaa mwachedwa nayo,
Che macdonald kachala ndi iwe wa mcp eti
Kunkuyu wachamba, panopa maiko usi akukozekela kunka ku state house, mkadakonda manganya akadantulitsa pasi udindo chimwendo kkkķkkk mimba njuu kulibe kusintha atsogoleleri kwa manu konko
Golf akamenyela kuti muthu wamwalira kkkk tiyeni only 2days
Machine
Ntanyiwa umangidwatu iwe ndi bodza lako misleading Malawian ndi za bodza,ngati ulibe zolankhura kumakharako chete pena,ngati momwe amachitirako a Bon Kalindo amazakharako chete pene osati kubwetuka
Aaa gofo sasewela nkono umoz
Esh osamafaritsi khani ya ifa Koma arimoyo esh zopusa bwanji
Musamunamizire ntanyiwa munthu wamulungu uyu
👍
Mumaitha a mtanyiwa
Iwe ndi galu kwabasi..izi sizoona lumikiza a Malawi kuti tigwirizane
Wabodza iwe wakhuta msima ya nyemba UDF woyeee
Kkk
Kulu uyu ngonama zulo watiuza zina apaso akutiuza izi mmmmmm
Ntanyiwa mabodza usiye
Azipita akapume
Munthu wakulu nthanyiwa
Pajatu boma ili silimanena chilungamo
Antanyiwaso u misleading ppo nanuso mumati watisiya now u changing
Abati Ali kuchipatala ku south Africa 😂😂
Now u want to mislead us😂😂😂😂 he never said wafa plzzzzzz he said he is sick and has been taken to SA kuchipatala osati zokufazoyi eeeeeeeeeh eeeeee😂
If you don't have news, you don't have it's not a crime, if you keep broadcasting false news, you will lose followers, that's my advice