Zomwe wayankhula Michael Usi Lero atangofika mu Mzinda wa Blantyre

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 25 сер 2024

КОМЕНТАРІ • 125

  • @benardisaac1986
    @benardisaac1986 Місяць тому +1

    Nyengo ndizosintha manvuto sankha moyo wose wamunthu koma Dr usi all the best

  • @user-zs6qc9dx8s
    @user-zs6qc9dx8s Місяць тому +5

    We all know kut anthu omwe avala makaka a UTM nd a MCP. Eni eni a UTM sitikupanga nawo zopusazo.

    • @JonesSiliya
      @JonesSiliya Місяць тому

      Zoona akufuna kupusitsa

    • @JonesSiliya
      @JonesSiliya Місяць тому

      Chilima nzake amane amakambilana naye ndi ndani nanga nthawi imene amakusekani pakamwa ndindani

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 Місяць тому +3

    Manganya ndi wa MCP kuchokera kalekale

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Місяць тому +1

    Michael usi is a matured intellectual who doesn't entertain nosense.

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 Місяць тому +4

    Wachepa nao u vice president.waiwala imfa ya skc.

    • @LukeKalima
      @LukeKalima Місяць тому

      @@paulnyondo7572 aaaaaaaaaaa imfa ya skc ndiyotani anthu samamwalira kodi kapena munamuphera dala kuti muzipangira ndale imfa yake, kodi maliro akwanzanutu amaphweka chomchi akadzakhala akwanu zidzakuwawa kuti anthu azidzaseweretsa dzina la malemuwo

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 Місяць тому +3

    Ndimaona ngati adziyankhula zogwira mtima

  • @moyowrobert3331
    @moyowrobert3331 Місяць тому

    zoti akumanga thumba ngati Mphaka sukuziwa

  • @hastingskalambo8502
    @hastingskalambo8502 Місяць тому +2

    Ndekuti zoti UTM yatuluka ku alliance iyeyo sakudziwa

  • @JacobKasalika
    @JacobKasalika Місяць тому

    UTM ndimaikonda komano tikudzibalalitsa yokhatu.Uyu ndinthu ndinyamata wa SCK

  • @LukeKalima
    @LukeKalima Місяць тому +1

    Wandisangalatsa usi sakupanga nawo za mtopola ena achita manyanzi kumeneko ndiye kulankhulatu ambuye akudalitseni dr usi

  • @sanddaniweck2703
    @sanddaniweck2703 Місяць тому +2

    Zangongole ife tilibenazo ntchito nkhani musise zinthu zakwela kwambili coz za Neef zo anthu ena akumamizi kwina salandila koma mukasisa zinthu anthu onse athandizika

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o Місяць тому

    Mbuz yamunthu iyi yudasi ife a Utm zopusazo ayi sitikupanga nawo

  • @LeviBlackson
    @LeviBlackson Місяць тому

    Anthu sakumudziwa Kodi ku Blantyre kapana amapanga sewero

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Місяць тому +3

    Ngongole imeneyi udzabweza ndiwe .
    Fataleza udula konseko

  • @Jane-qb5qf
    @Jane-qb5qf Місяць тому +1

    Amalawi look sharp amalawi tilindivuto akati uku komweko uku komweko lekani timapemphera kukhala ndi chiganizo chokhazikika zimandimvesa chisoni kwambiri tisinthe mindset plz plz tizagwa chagada ndikati ndione amazayesa zida kuti kuli bwanji uku aaaa kaya Malawi

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses Місяць тому +3

    Muli mbali iti kodi Fada

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Місяць тому +3

    Palibe azalande m'dalitso wamunthu, Dr usi ndiodalitsika muzonse komanso olimbika.

  • @joeldaniel-pc3ij
    @joeldaniel-pc3ij Місяць тому

    Mwapatsa anthu a MCP ma uniform a UTM kuti aziti chani?

  • @LeniaJosophat
    @LeniaJosophat Місяць тому

    Mukutipatsirazi ndizabwino zeedi koma you need to fix the sound kuti zizikomabe( this is the VP)

  • @user-vb1iq5un5p
    @user-vb1iq5un5p Місяць тому

    Kodi Usi ulimbali iti?. Koma umphawi luMalawi ukupepeletsa azibambo...

  • @VeronicaYohane
    @VeronicaYohane Місяць тому

    Mudyelen bambo wasikono akabwela osadziwa kuyankhula odvala madiresiyo

  • @JuniorKalipinde-gy7dx
    @JuniorKalipinde-gy7dx Місяць тому

    Usaone ngati ndi bugwe LA adla limenelo akupweteka

  • @johnbakali27
    @johnbakali27 Місяць тому

    Kodi iwe ukumenyera kampeni ya mco kapena UTM?

  • @user-hh4xg4hf2k
    @user-hh4xg4hf2k Місяць тому +2

    Enafe tisayankhire

  • @JonesSiliya
    @JonesSiliya Місяць тому

    Mwachedwa ndi chilima simunapange chifukwa chiyani

  • @FrankidEugenio
    @FrankidEugenio Місяць тому

    Ndale zayambika,Malawi ayiwale zambuyo.😂

  • @user-dv6rt6vb6e
    @user-dv6rt6vb6e Місяць тому

    Umbuli suzatha anthu munayambila kunamizidwa muja zilero changamukani

  • @constancemkandawire7378
    @constancemkandawire7378 Місяць тому

    You can't say that you love God if you don't love your nearby that's a total lie.You have failed to come together with your fellow utm members mukuti phala lomwe likudumpha mu mpoto lidumphe meaning you don't care ,ayi zikomo

  • @user-ni4nw1ee2f
    @user-ni4nw1ee2f Місяць тому

    Mwschedwa nayo ngongoleyo bwana kkkkkkk nyimbo ikhale ya mpaka malilo vinyo watha

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f Місяць тому +1

    Dziko la Malawi lafika pa uchitsiru weni weni

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Місяць тому

    Tasisani fertilizer zinthu zisike agalu inu muona muwina mosavuta

  • @RossanaMitha-tl9in
    @RossanaMitha-tl9in Місяць тому

    Kodi akuti kwabwela ndani ?😂😂😂😂

  • @lumbaninyirenda8223
    @lumbaninyirenda8223 Місяць тому

    tamangopitani muzikapanga ma drama,mfundo palibe apa

  • @ChrisjuZiyaya
    @ChrisjuZiyaya Місяць тому

    Chizindikiro choti Usi siwa utm onani zomwe zavalidwazo , zomwe Malemu Sks sadapangepo. Tikufuna m'tsogoleri wa serious not this gys.

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g Місяць тому

    Lelo akunamizila chilima lelo ndi mbuzi yamunthu

  • @genesismbewe
    @genesismbewe Місяць тому

    genius

  • @jedoforsure2842
    @jedoforsure2842 Місяць тому

    Umakwana us

  • @joekamphulusa4767
    @joekamphulusa4767 Місяць тому

    Chitsilu chenicheni ichi watenga athu a mcp kumati a utm 🚮🚮🚮

  • @footballhighlightsofficial7248
    @footballhighlightsofficial7248 Місяць тому

    Missing Chilima Already😢

  • @MlecheFatch
    @MlecheFatch Місяць тому

    A manganya mmmh

  • @enockharry8039
    @enockharry8039 Місяць тому

    koma izi wina aziona

  • @joma5327
    @joma5327 Місяць тому

    champhamvu kopasa kale kuthanthauza chani

  • @KondwaniNdobvie-f4v
    @KondwaniNdobvie-f4v Місяць тому

    Komatu adzake afanazo

  • @user-qu9ww1cd1y
    @user-qu9ww1cd1y Місяць тому

    Anamizana zokuti akope Southern Region

  • @ellahmvula
    @ellahmvula Місяць тому

    Hahaha awa a mcp achina Eliza avala za utm

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 Місяць тому

    Wakupha iwe manganya

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba Місяць тому

    Satan ndiyemwe ali kutsogolo kwakoyo

  • @RobertChisenga-ci2mq
    @RobertChisenga-ci2mq Місяць тому

    BT chitsilu2 paja

  • @MerySaid-uw3cm
    @MerySaid-uw3cm Місяць тому

    Tikufelanji

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Місяць тому

    Iweyo ukuti ukufuna ulongo sole, ndimaesa UTM yatuluka mungwirizano ukufuna kupusisanso Wanthu

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k Місяць тому

    Basi tizingokhalira ma handouts mpaka liti abale?

  • @NkosDysonNkosDyson
    @NkosDysonNkosDyson Місяць тому

    Tangotsitsani fertilizer muonanso mudzawina mosavuta ife amalawi sititichedwa kuiwala

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 Місяць тому

    Wosokoneza uyu

  • @macdonaldchaonekera834
    @macdonaldchaonekera834 Місяць тому

    Kodi akupanga sewero la tikuferanji et?

  • @frankwilliam9844
    @frankwilliam9844 Місяць тому

    There's contradictory in his mind,chomwe amalawi akufuna singongole,tsitsani zinthu,chepetsani kudalira ngongole za IMF...koma ndithu 60yrs independent Malawi yukanikabe kudalira payokha pa nkhani ya zachuma? so sad...Kodi maiko amzathuwa amatani Kodi ..adatukuka bwanji atalandila ufulu???

  • @NELSONMULIMAH-fv6ub
    @NELSONMULIMAH-fv6ub Місяць тому

    Zauchisilu zaziii

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p Місяць тому

    Aaaaaaaaaaaaaaaaaaa chitsiru mbuzi garu nyani mfiti iwe

  • @jeymulima9664
    @jeymulima9664 Місяць тому +2

    Zaziiiiii

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g Місяць тому

    Anthu 4 okha bs

  • @florenceharawa519
    @florenceharawa519 Місяць тому

    Uku wapita uku wapita punsi anagwa chada😂😂😂😂

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k Місяць тому

    Koma zimenezi zitithandiza izi????

  • @user-ep7gu2td6y
    @user-ep7gu2td6y Місяць тому

    Sakudziwa zomwe a makawi akukumana nazo ....,

  • @MuhammadNyambalo
    @MuhammadNyambalo Місяць тому

    😅😮😢😅😅😅😅😂 patumbo pako iwe nyo

  • @NathanMaunda-dz8gc
    @NathanMaunda-dz8gc Місяць тому

    Awa sakuyankhula zotigwira mtima kodi nd wa chipani chanji ameneyi

  • @LottiAffati
    @LottiAffati Місяць тому

    kod akuyankhula kut chan apa guys aaaaaa, komanso amalawi ngoputsadi ndithu

  • @MarthaChintolo
    @MarthaChintolo Місяць тому

    Aaaaaa chifukwa chani Chilima unalakwitsa ee

  • @AbdullCassim
    @AbdullCassim Місяць тому

    Iweso ndiye kayatu

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Місяць тому

    Ayakhura ali pat?

  • @chikondiyovita7210
    @chikondiyovita7210 Місяць тому

    My data hu!

  • @Vascomw
    @Vascomw Місяць тому

    Ïn̈ë n̈d̈ïm̈än̈g̈än̈ïz̈ä k̈üẗ äÿäk̈ḧür̈ä z̈äz̈ël̈üüü k̈m̈ ääää b̈ün̈d̈l̈ë ÿän̈g̈ä amayo

  • @momuumro
    @momuumro Місяць тому

    Situfuna kunva zimenezo Ife tufuna nkhani yotuluka mu tonse alliance

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651 Місяць тому

    Akufuna kugulitsa UTM KU MCP

  • @user-lu6nq9bs6w
    @user-lu6nq9bs6w Місяць тому

    Nde ku MCP' ko akuti chani kkkk 😂😂😂

  • @elizabethnkhata3438
    @elizabethnkhata3438 Місяць тому

    It's lik people are not happy

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh Місяць тому

    Ndimwana uyu alibe fundo

  • @QuotienieMw
    @QuotienieMw Місяць тому

    Tikufilanji episode 10

  • @user-ou4md5ud1u
    @user-ou4md5ud1u Місяць тому

    Sizikuveka ai komas sizikugwilizana ayi

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh Місяць тому

    Kupusa

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses Місяць тому

    Palibe kunyengelerana ndi ngongore nbuzi za anthu.

  • @ElizabethMwakamogho-x7j
    @ElizabethMwakamogho-x7j Місяць тому

    Sukuziwa make awo find alimbe

  • @user-zl1xz9kt5s
    @user-zl1xz9kt5s Місяць тому

    Amalawi mitu sigwiradi sure

  • @Vascomw
    @Vascomw Місяць тому

    Hhhhhhh

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p Місяць тому

    Palibe chanzeru waywnkhula

  • @FysonKaliba
    @FysonKaliba Місяць тому

    Kod ati Ali Mbali iti??????????

  • @SmithLikoswe
    @SmithLikoswe Місяць тому

    Zamasewelo bac

  • @jeymulima9664
    @jeymulima9664 Місяць тому

    Kkkkk ngabule moyo,thetsa,uthetsa suthetsa kkk yathayi kkk

  • @WindowSomanje
    @WindowSomanje Місяць тому

    Za ziii

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm Місяць тому

    Km malawi ndfe anthu opusa kwambiri tinakali kuvutika

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 Місяць тому +1

    Za ziii tu

  • @MECChiona
    @MECChiona Місяць тому

    wamisara uyu 😂😂

  • @NATASHAChimtolo
    @NATASHAChimtolo Місяць тому

    Opepela uyu malemu amavala makaka achipani chake

  • @RighteousMhone
    @RighteousMhone Місяць тому

    Shimeyi atukwane😂😂😂

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Місяць тому

    Emeneyi si dyera koma

  • @ChrisNkhoma-i8m
    @ChrisNkhoma-i8m Місяць тому

    Mcp BOMA labwino kwamunthu woganiza mwazelu tiwone komwe tachoka .

  • @user-uq4hn4rp2j
    @user-uq4hn4rp2j Місяць тому +2

    Nice

  • @thokofodya1583
    @thokofodya1583 Місяць тому

    😢

  • @user-hl3vl9nt1b
    @user-hl3vl9nt1b Місяць тому

    Aaaa zazi bas

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko Місяць тому

    Sanje bac amalawi eeee

  • @sonkieleymanni6312
    @sonkieleymanni6312 Місяць тому

    ndiopusatu awawa,,,,,,,,,,,,,,,palibepo chanzeru anena apa

    • @LukeKalima
      @LukeKalima Місяць тому

      😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu

    • @LukeKalima
      @LukeKalima Місяць тому

      😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu

  • @SiphiweTonnyChidumayo
    @SiphiweTonnyChidumayo Місяць тому

    Anthu sakusangalaratu😂😂

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 Місяць тому

      Ndizawo zimenezo komanso musawapangire Zochita anthuwo . ngati inuyo simukusangalala basi

    • @SiphiweTonnyChidumayo
      @SiphiweTonnyChidumayo Місяць тому

      @@ancientnkhata1137 eh eh iwe im commenting according ndimmene zuonekera nsiye ine