Exactly!!!! Born kalindo atazakhala president zinthu zizasintha uyu kungoima tizamupatsa ma vote ,this guy is so special I’ve never seen courageous man in Malawi like Bon Kalindo (take care wherever you go coz maybe thy may plan to deal with you so please take care Bon kalindo we will stand wth you at least your giving hope?🙏🏼🙏🏼
And exactly mr born kalindo you're right, tonse alliance government is failed to ruling county of republic of malawi, you need to shout them powerful maybe they can change, malawi aonengeka I supporting you mr don't give up.
Kunena Chilungamo Bon Kalindo is the patriotic citizen. It may be true kuti mwna he is frustrated for not being given the minesterial position koma ngakhale akanakhala Nduna mkulu ameneyi akadalisusabe boma momwe lisakuyenda bwino. Kwa Maguys amene tikumu hater Bon Kalindo , let us think critically, nkuluyi if he was do it kt yekha apeze kenakake From Kuboma im telling you he would have been bribed by government as how other activists did. Mr Kalindo amaganizila anthu osauka kuposa mmene amaziganizilila okha. Mmene wakhala akumangidwila mkuluyi , he would have surrendered and began kumapanga ma business ake oti iye ndi banja lake kumasangalala koma iye amayesesa kuwayankhulila amalawi amene sangathe kuyankhula. BON KALINDO , kaya amapangira motive yanji koma Mulungu azikhala naye nkulu ameneyi
I hear you mr born kalinda your issues very sweet and truth go deeper, pakhani ya feteleza, passport, madzi,magesi and E.t.c zikolathu la malawi lalowa mbola akumuzi afanjala. I lke your speech winiko
Bon kalindo ur no 1 timenyereni khondo anthu comwe akucita sakucidziwa amaombera manja zosayennera koombera manja , anthu tikuvutika akumdzi soap,mafuta, mcere mmmm ili ndi boma lamwazi
Kkkkk koma inu dzikoli khaya ndichani amadya matembatu muchi njinga chija koma lelo sangakayendensotu ha ha ha kaya nyumba imeneyija khaya muli satana wanji khaya kkkkkkkkkkkkkkkkkk
Anthu wa amkafuna kukonza za mimba Yao aiwala za ovotafe so day ya ma demo yo please dziwitsen nili ni kagulu kanga kodzwa kuyatsa bwno matayala asatinyanye aguduwa malaw niyathu iyi
Ase ine panopa ndikukhala ku Singapore zinthu zakudula dziko lonse la pasi not ku Malawi kokha, anthu ambiri achotsedwa ntchito ma company ochuluka atsekedwa ndiye dziko lathu lodalila ma Donna's muti zinthu zitchipe munamanga ma factory muli ndi ma company?
@@clivendecha8554 I'm very proud kukhala wa MCP, iwe ndi cadet wa DPP, atsogoleli anu onse ku DPP munachokela ku Mozambique, Peter munthalika, Nankhumwa, Mwanavekha, Kabambe, Mchacha, Leston muli, nose munachokela ku Mozambique amalawi tatopa ndi kulamulidwa ndi ma Portuguese
@@robsontyg3928 thats right... you and me , we are not in Malawi so you can not say Mr kalindo asakunyase as if you are feeling the pain.... nothing wrong to support MCP but if there is wrong doing,akuyenela kuzuzulidwa . its right for everyone
@@robsontyg3928 i dont support dpp and i will support mcp either, not any political party..... i only support any govervement that run the country well..... people like you that is why malawi is poor..... mumangoimbila mmanja zilizonse
Exactly!!!! Born kalindo atazakhala president zinthu zizasintha uyu kungoima tizamupatsa ma vote ,this guy is so special I’ve never seen courageous man in Malawi like Bon Kalindo (take care wherever you go coz maybe thy may plan to deal with you so please take care Bon kalindo we will stand wth you at least your giving hope?🙏🏼🙏🏼
Zikho la malawi pazentenga thawi kuti lithukukhe Oze Andale Aku malawi ofuthikha ndiye akhalowa boma amafuna Kuti alemele pazentenga thawi Zaka Zaka Kuti malawi izayimire payekha .azepheseke president olikhonda zikho ngat johi makufuli
We need people like this to talk what is wrong in the country...no fear Mr ... tel them the truth
Apa ngati kuli anthu otukwana bon kalindo ndekuti munthu ameneyo ndiwontheratu zeru winiko wanyamula unthenga wabwino kwambili
And exactly mr born kalindo you're right, tonse alliance government is failed to ruling county of republic of malawi, you need to shout them powerful maybe they can change, malawi aonengeka I supporting you mr don't give up.
This is a true leader with people at heart not money may you keep on doing this good job Mr for the people of Malawi.Salute
Clap hand's for him ur my hero
Shaaàa
Mkuluyi koma akunena zoonatu
Tikanapezeka anthu angapo angati Kalindo dziko likadasintha pitiliza Bon tilipambuyo pako(Shadreck Matenje fromRSA)
Kunena Chilungamo Bon Kalindo is the patriotic citizen. It may be true kuti mwna he is frustrated for not being given the minesterial position koma ngakhale akanakhala Nduna mkulu ameneyi akadalisusabe boma momwe lisakuyenda bwino. Kwa Maguys amene tikumu hater Bon Kalindo , let us think critically, nkuluyi if he was do it kt yekha apeze kenakake From Kuboma im telling you he would have been bribed by government as how other activists did. Mr Kalindo amaganizila anthu osauka kuposa mmene amaziganizilila okha. Mmene wakhala akumangidwila mkuluyi , he would have surrendered and began kumapanga ma business ake oti iye ndi banja lake kumasangalala koma iye amayesesa kuwayankhulila amalawi amene sangathe kuyankhula. BON KALINDO , kaya amapangira motive yanji koma Mulungu azikhala naye nkulu ameneyi
I hear you mr born kalinda your issues very sweet and truth go deeper, pakhani ya feteleza, passport, madzi,magesi and E.t.c zikolathu la malawi lalowa mbola akumuzi afanjala. I lke your speech winiko
Mr born Kalindo Pa mfunso zanu zili bwino kwambili 😘 😘 ndiposo zikulimbikitsa kwambili Komaso zikupeleka tsogolo La bwino. Pano A 🇲🇼 ambili tikuvutika kamba koti tinkakhala busy kuvotel zolakwikwa
Am at the back to B kalindo 🔥🔥
Kkkkkkkkkk was waiting for this video upload! 🙏
Thanks for commenting we will keep on updating on what is happening in our country
@@tichezeamalawi9691 Yeah it had already gone viral even before uploading..
Moto kuti bhoooo winiko amayenda ndi machesi
Bon kalindo ur no 1 timenyereni khondo anthu comwe akucita sakucidziwa amaombera manja zosayennera koombera manja , anthu tikuvutika akumdzi soap,mafuta, mcere mmmm ili ndi boma lamwazi
Akamuna awa and my Uncle ipatseni moto basi
Moto Kuti buu chilungamo chikulakhulidwa APA
Tikufuna anthu olimba mtima ngati amenewa komanso oima pachilungamo.
Lets support him.
Kma pachilungamo kalindo ndilimbali yanu zomalemekeza asogoleli zikuwononga ziko
Boni kalindo ine naona ngati akusuta chamba kapena mkapime nzelu Kaye
Zinthu zadula mtengo ziko lonse lapansi
Iiwe ndi mbuzi yeni yeni
Winiko amandivesa kukoma ngati kumalawi kulimunthu amene akunena zoona palibeso oposa bon kalindo. MALEMA WAKUMALAWI
Akunama iyeso azachita zomwezo akunama uphawi amalawi wakuphetekani munthu wa zisunzo akhale president Winiko phawi ngati imeneyi
Amene akunyoza winiko Ndiye Kuti ameneyo akumabanawo ndalama
We are together Mr kalindo
Munthuyu ndiwazelu kwambiri mutagwila naye ntchito bwino dziko lamalawi lingasithe
God bless you
Very few can speak and stand on the truth
Iyeyu anali mp muja anapanga chiani?
Very strong en wise politician
Mwamasukatu akalindo koma nanu munali a mp Ku DPP mungatiuze chimene munapanga
Freedom of expression on the stearing..... Change must come...viva malawi
Wininko kodi ndi boma liti lina chitako bwino mutanena chifikwa izizi mulakhula panozi muziona kuchokela boma liri limodzi mpaka pano chomwe mukuwona kusitha ndichoti palibe chositha mungovutika kunali anthu alikuti tangokhalani bas
Kapena mwina mukufuna udindo chifukwa mwina achilima ada kunamizani zaudindo?
Ndikumamvelabe mpaka pano
Kalindo alibe matha
Truth should be taught.
Mukufuna udindo komano sizitheka remember mawu omwe udayankhula pa zodiak pa 08 may 2018 akulu akalindo ndinu opusa zedi
opusa ndi iweyo
@@clivendecha8554 Zimene akukamba Winiko mmalawi weniweni oganiza komanso kutengera ndi momwe ulili pa Malawi akukamba zoona Zokha Zokha ma business athu agwa Palibe chikuyenda
🙏🙏
Kkkkk koma inu dzikoli khaya ndichani amadya matembatu muchi njinga chija koma lelo sangakayendensotu ha ha ha kaya nyumba imeneyija khaya muli satana wanji khaya kkkkkkkkkkkkkkkkkk
Kalindo amwenyele nkhongo anthu akumudzi
Anthu wa amkafuna kukonza za mimba Yao aiwala za ovotafe so day ya ma demo yo please dziwitsen nili ni kagulu kanga kodzwa kuyatsa bwno matayala asatinyanye aguduwa malaw niyathu iyi
Akalindo kukwela kwazithu ndi dziko lililonse kusogolokuno ziyenda,vuto mwasauka mukulilila udindo takuonani kare,nde mwajijilika nazo
Iwe uzinva anayamba kuzuzula ali nboma la bpp osamango ombela nmanja zopusa
Fact💥💥💥
WINIKO AKANANKHALA NGATI NDI WADZIKO LA SOUTH AFRICA BWEZI ALI NDI SAPOTI YOWOPHA KWAMBILI
Achikulire adanena kuti mutipaty ndi nkhondo lero ndi izi,
dziko asamalitenge ngati munda wao a china tonse alliance wo, komaliza mkomweka next election sutuwafunanso
Winiko akunena zowona
Bon Kalindo tiri pa mbuyo panupo
People think you're acting
Muma nthiyimilila kalindo
Uchisilu fodya wankulu wakuzunguzani inu akalindo ugaru wanu
Zimakomatu poyankhula
Winiko ndakunyadila Kwambili chifukwa umatha
Ino sindawi ya kamuzu mukutengela kamuzu anthuluke akanika yaka ziko
Komaso ndalama sa kolona sikuteka mukunama kuti sakuyimisani kofiti bosa mutiononga mukupa ziko tiusani
Amatitenga Ngati zisilu one day wina azadulidwa machende
Ukunena ndani ?
Awuze tikuthawira mayiko ayeni chifukwa cha ulamuriro wa chakwera
Kuno kuthekerani mmmmmtikuvutika cipani cosintha zinthu cija
Utukwana chiyani ndinu sizilu akupasani ndalama machende ako pano sitiopa
Yes tell them bro there is another flooring man that his tonking zopanda mutu
Koma zotukwana on a public platform like this ndi usaveji, kusutsana ndi ufulu koma kutukwana ndi kusowa khalidwe.
Ngati mupita kusewu mugwilitse tchito malamulo chifukwa muka phonya mudzapeza vuto
Good one madala ndikubwela kuzakuthandizani
Alowe ndi anzelu uyu nde anakonza
Waboza abisala
Misala kupenga uchitsilu nguluwe fisi, mademo amenewo mudzipangila kwanu konko ku lilongwe kuno tikukhapani khapani
Monga Winiko akunama moyo uli pabwino pa Malawi pano? Zoti zinthu zikudula daily, ma business athu akugwa akunama? Let's love our country
Ase ine panopa ndikukhala ku Singapore zinthu zakudula dziko lonse la pasi not ku Malawi kokha, anthu ambiri achotsedwa ntchito ma company ochuluka atsekedwa ndiye dziko lathu lodalila ma Donna's muti zinthu zitchipe munamanga ma factory muli ndi ma company?
Ife sitikunena za Singapore, Tonse Alliance inalonjeza zambili zomwe amati aziona kuti ndizotheka, Lero mmalo mwake zinthu zikusintha from bad to worse, Zoti ku Singapore zinthu zikuvuta muzinamiza anthu ena pano maiko ambili akuchita recover after Covid-19 kuwasokoneza zinthu zikuyenda, Koma ku Malawi Palibe chikuyenda ma business athu agwa agwa, ndalama ikukwera daily, vuto uli kunja ubwere uzaone momwe zilili PA Malawi Lero, iweyo ukukamba zimenezo chifukwa uli kunja Kwa Malawi, munthu kugula galimoto 4 million kulipila duty 3 million, misonkho angokweza mosayang'ana economy yathu Toll gate kuchita kudula kuposa RSA dziko lolemera
@@tichezeamalawi9691 ase gwila ntchito kuti upeze zosowa zako usayembekezele kuti boma likupatsa zinthu zaulele wauponda
Sukudzowa zomwe ukuyankhula zinthu zikudula konse yes koma kumalawi it’s too much
Mr kalindo sakuyankhula izi kuti akufuna udindo limeneli ndi bodza, nkhani yayikulu ndiyoti tiwone zomwe akuyankhula bon kalindo kuti ndi zoona kapena ayi? yankho ndi loti akunena zoona chifukwa kalindo izizi adayamba kuyankhula motere ngakhale ali MP ndiye omwe mukuti sadampatse udindo mukulakwitsa
Iwe kalindo usatinyase wava
Mboli yako iwe kadet wa mcp
@@clivendecha8554 I'm very proud kukhala wa MCP, iwe ndi cadet wa DPP, atsogoleli anu onse ku DPP munachokela ku Mozambique, Peter munthalika, Nankhumwa, Mwanavekha, Kabambe, Mchacha, Leston muli, nose munachokela ku Mozambique amalawi tatopa ndi kulamulidwa ndi ma Portuguese
@@clivendecha8554 ine wa MCP panopa ndili ku Singapore ndumwa mkaka ndili phee
@@robsontyg3928 thats right... you and me , we are not in Malawi so you can not say Mr kalindo asakunyase as if you are feeling the pain.... nothing wrong to support MCP but if there is wrong doing,akuyenela kuzuzulidwa . its right for everyone
@@robsontyg3928 i dont support dpp and i will support mcp either, not any political party..... i only support any govervement that run the country well..... people like you that is why malawi is poor..... mumangoimbila mmanja zilizonse