Interview ndi Norman Chisale

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лис 2023

КОМЕНТАРІ • 361

  • @RuthNankumba-ux3sw
    @RuthNankumba-ux3sw 7 місяців тому +14

    Big up Norman Chisale ,I love your courage 🔥 Ambuye apitilize kukumenyeran nkhondo ,,,I'm one of your supporters

    • @NzeruDesign-ut1go
      @NzeruDesign-ut1go 4 місяці тому +1

      Ndpo nthawvyamayankho ikubwela big tipanga zobwezera ntoporao

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 Місяць тому +2

    Komano pa point ya human rights Peter Muthalika he really respects

  • @mengokumwenda3832
    @mengokumwenda3832 7 місяців тому +19

    The lady was carefully selected to handle this interview am impressed with how she has handled this heavy interview. Professional indeed

  • @JamesKamanja
    @JamesKamanja 9 годин тому

    God bless Mr chisale komano mokupemphani ndithu pepani uyu akufuna kut mumukhululukileyu imvani kulila kwake kut ukulu wayehova ukhalebe pa inuyo yesu anat muwakhululukile chifukwa sakuziwa chimene akuchita
    Musaiwale kut munthu payekha alibe vuto koma satana akamulowa amapangisa munthu kuchita zimene choipa chili mwa iyeyo chikufuna please ndikuziwa ndithu ululu ndi ochuluka kwambili koma khululukani ambuye apitilize kukupasani moyo wamphanvu madaliso avumbebe kut wamasiye apeze popumila

  • @user-pn7cj9hb3t
    @user-pn7cj9hb3t 3 дні тому

    Am watching this interview kachikenaso Norman Chisale yu ndi #1 kwa amene alipa chilungamo akudziwa kuti big wa ndi real man osangoti mwakati poti umadana naye.

  • @paulgodfrey3361
    @paulgodfrey3361 7 місяців тому +9

    Leah you the best journalist...well done to Me Chisale

  • @user-gz9iy7sd7j
    @user-gz9iy7sd7j 3 місяці тому +1

    Mr Chisale isn't my relative but ndawamvesa he is a real soldier, BRAVO CHISALE. BULL Sheet kayun.

  • @Catherinesmart-xk4zx
    @Catherinesmart-xk4zx 7 місяців тому +2

    Chisale ndimunthu wabwino kwambiri wamanga ma church wachita zambiri Ambuye akudalitsen achisale long live

  • @user-zg7iw8kq4r
    @user-zg7iw8kq4r 3 місяці тому +1

    Bravoooo big man chisale i salute you

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 7 місяців тому +8

    Chisale akumva zowawa chifukwa cha anthu ansanje but Chisale is the best Man in Malawi he spend his money to help the orphans and community, God bless you always and protect you Mr Chisale.

    • @user-or8cw6md7t
      @user-or8cw6md7t 7 місяців тому

      Zoonad ol evn Ines zimandiwaw, km Amalawi if nsanje😢

    • @homeremedys3748
      @homeremedys3748 7 місяців тому

      @@user-or8cw6md7t amalawi amamukonda munthu akafa, that's why dzikoli lili lobwerera mbuyo,

  • @hectortambuli605
    @hectortambuli605 7 місяців тому +3

    Great man Norman Chisale. Oceans of luv to you and your family.

  • @mijerimasiye7310
    @mijerimasiye7310 4 місяці тому +3

    Azodiak tamakhalani ndi ma bottle amadzi mukamapanga interview ndi anthu please

  • @maskinmsungeni8763
    @maskinmsungeni8763 7 місяців тому

    Kkkkkkkkkk Norman Chisale !!!!! Ur a big Man. Wandiwaza kwambiri Msungeni all the way from Zambia.

  • @user-nn5ug7ul4d
    @user-nn5ug7ul4d 7 місяців тому +1

    Msilikari adzakhare msilikari mpaka kare. Big up bro N. Chisare❤❤

  • @thomluciouss7360
    @thomluciouss7360 7 місяців тому +11

    The one who talk the truth doesn't fear and it's really true that the truth pains big up Mr Chisale

  • @LetsSeePlaces43
    @LetsSeePlaces43 7 місяців тому +11

    Interviewing a well trained professional soldier should be different with interviewing a well trained professional economist💪🏾💪🏾Bravo snipper Norman Paulosi Chisale🤣🎉🎉💥💥

  • @user-nr2th9wu6i
    @user-nr2th9wu6i 7 місяців тому +3

    Chisale your number 1 well trained soldier

  • @user-sx1gr6fz1s
    @user-sx1gr6fz1s 7 місяців тому +4

    Akuzuzika ngati yesu chisare ndi Good Samaritan athu abwino amazuzika

  • @matembanevermind-po3me
    @matembanevermind-po3me 7 місяців тому

    Gud interview love you questioner and Mr interviewer Norman

  • @user-ro7rb9hj8k
    @user-ro7rb9hj8k 7 місяців тому

    😂😂😂 so in love with his courage 🤦🥰

  • @NodiceChakwala-tz5gg
    @NodiceChakwala-tz5gg 7 місяців тому +1

    great mtolankhani , kip the fire burning girl

  • @winniekelvin7135
    @winniekelvin7135 6 місяців тому +2

    Steven kauni samalani komwe muliko chisale ndiokwiya

  • @jumazabula2908
    @jumazabula2908 7 місяців тому +1

    Definition of having readership, fire 🔥 chisale

  • @ndalamaandrew
    @ndalamaandrew 7 місяців тому +2

    Koma Chisale uyuyu eeeeeeh 🙌🙌🔥🔥🔥

  • @Liam-ky5cu
    @Liam-ky5cu 7 місяців тому +1

    Bravo Bravo 👏 😁 Soldier...

  • @chifunirosaka9077
    @chifunirosaka9077 7 місяців тому +11

    Soldier never die chisale more 🔥

  • @MisheckChangata
    @MisheckChangata 20 годин тому

    Great man ,i like u

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 7 місяців тому +1

    Well trained,,, the bodyguard from bejin

  • @williammaseko8542
    @williammaseko8542 7 місяців тому +3

    He is very emotional and trying to run away from facing justice. No one accepts to be guilty in public and whatever is doing here is normal for suspects. 42years doesn't match with the way he looks unless he tells us kuti amasamba Nyanga.

  • @chimwemwenkosi-nl4zj
    @chimwemwenkosi-nl4zj 7 місяців тому

    True leadership timakunyadilani mr

  • @falayichitsotso5371
    @falayichitsotso5371 7 місяців тому

    Mr Chisale I hear ur story it's very bad and am very happy with u ustand with God dnt give up mukuyakhula kwako mulungu akumva ndipo mulungu amalora Kuti ana Ake andutse mmavuto ndicholinga Choti ukulu wake ukaonekere God will be with u mwaiwe muli usogoleri

  • @vitumbikocobysinyiza-5116
    @vitumbikocobysinyiza-5116 7 місяців тому +1

    Big up Mr chisale

  • @lonjiekaselera9651
    @lonjiekaselera9651 7 місяців тому

    The real legend khaaa wauuza ngamo

  • @user-xb2dz8vo5z
    @user-xb2dz8vo5z 7 місяців тому +2

    Tikukuvesesani mr chisale.

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 7 місяців тому +10

    I like the energy tht u hv Mr chisale as a soldier...big up❤

  • @Chief-Phungwako
    @Chief-Phungwako 7 місяців тому +1

    This was nice chisale seems a good one though ndindale

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 7 місяців тому +1

    Chisale usatiuze kuti akhale wo opa mulungu suyo chakwera wo opa mulungu akutizunza

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 2 дні тому

    Norman your statement is clear and comprehensive but what about Chthyola, Chimwendo Banda, Kunkuyu etc ??

  • @patrickjoda2165
    @patrickjoda2165 7 місяців тому +2

    Mulungu akhale patsogolo basi Mr chisale Angoni

  • @chawagondwe6404
    @chawagondwe6404 7 місяців тому +1

    Those who are saying bravo chisale you need special prayers..this guy stole our money tax payers money....he accumulated wealth within a short period of time....hotels cars houses etc he is backing himself apa he can't admit it.....and you are busy kumunyadira 😮Malawi ndife ogona too much.....he is lucky he is outside otherwise he belongs inside

  • @user-qy6nj9ii6n
    @user-qy6nj9ii6n 7 місяців тому

    This lady 🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-xl6jq1zw5d
    @user-xl6jq1zw5d 7 місяців тому +4

    This guy is some how mad

  • @user-yh4qx6xq7u
    @user-yh4qx6xq7u 7 місяців тому +1

    Komatu chisale ndye akumulakwla

  • @user-pl5pg8fp8s
    @user-pl5pg8fp8s 7 місяців тому +1

    Watching from zambia

  • @paulmakaula4937
    @paulmakaula4937 7 місяців тому +6

    Political prosecution has ever been in existence since our independence....please follow the rule of the law always! Clear conscious is the medicine...God is watching and will judge everyone right..

  • @paulgodfrey3361
    @paulgodfrey3361 7 місяців тому +1

    Your the best Leah

  • @blessedmichael5124
    @blessedmichael5124 7 місяців тому

    I like sir Norman Chisale he's been good in speech osamaopa pa chilungamo

  • @sainetjackson6183
    @sainetjackson6183 7 місяців тому +2

    Chisale ndikatumdu🤗

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 14 днів тому

    Mr Chisale i understand your pain please please firgive him isbus for your own good, you saud you are Christian our master jesus taught us to forgive those who do us wrong before we ask to be forgiven

  • @user-pr6fm8dp1e
    @user-pr6fm8dp1e 7 місяців тому +4

    Mr chisale attitude in this interview shows kuti bambowa ndionama..😂

    • @magdalenachipeta2394
      @magdalenachipeta2394 7 місяців тому

      Ndipo sukunama uku ndiwabodza auze mtundu wa a Malawi kuti ma billions a chuma anawapaeza bwanji osamangobwebweta zopanda phindu, kufuna anthu akumvele chisoni.

    • @user-pn7cj9hb3t
      @user-pn7cj9hb3t 3 дні тому

      Ndinu mabulutu guys

  • @user-nj4ob8jw6y
    @user-nj4ob8jw6y 7 місяців тому +1

    Akunama uyu, wakupha komanso wakuba, chitsiru chimangidwa chisiyeni, sakudziwa kuti apita kundende.

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i 7 місяців тому +2

    Mbavaizi aaaaaa awonongachumachamalawikwambili

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 7 місяців тому +1

    Chisale🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-zg7iw8kq4r
    @user-zg7iw8kq4r 3 місяці тому

    One thing i like this guy he talk straight

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 7 місяців тому +1

    Kkkkkk ayayaya malawi tingogulisa tigawane dollar zo

  • @yamikanichakuluntha651
    @yamikanichakuluntha651 7 місяців тому +2

    Kulavula Moto munthu wamkulu, Lord have mercy on him

  • @magdalenachipeta2394
    @magdalenachipeta2394 7 місяців тому +1

    1986 he was already working as a soldier but he is saying is 42 years old eeeeeish!!! 😂😂😂komatu munthuyu akuoneka ndiokakala mtima mayankhulidwewa atha kupanga zoophsya. He is saying kuti ndiopemphela koma akuti sangakhululukile aSteven Kayuni 😭😭 chonsecho amayenda ndi bible , mawu a Mulungu mwamunthuyu mulibemo.

  • @ibrahimjackson-cg6tc
    @ibrahimjackson-cg6tc 7 місяців тому +2

    Soldier sakugawa kamba

  • @user-rz9cr2nu1d
    @user-rz9cr2nu1d 7 місяців тому

    Big up boss

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g 7 місяців тому +1

    True leadership

  • @oscarkachale9234
    @oscarkachale9234 5 місяців тому

    Aaaaaa mbalame iyi

  • @chrisscapper-zw5rk
    @chrisscapper-zw5rk 6 місяців тому

    Bravo Mr Chisale

  • @samaxodala7587
    @samaxodala7587 7 місяців тому +1

    Chisale💪💪💪🇲🇼🇲🇼

  • @InnocentMsiska-sr8pe
    @InnocentMsiska-sr8pe 3 місяці тому

    Norman is right,the fact that aperson is working in the government does not bar aperson from being rich . Malawians justify poverty as being honest and truth

  • @hendrinagama5325
    @hendrinagama5325 7 місяців тому +1

    Uyu mafunika brain Banda osati ana awa

  • @Johnybegood260
    @Johnybegood260 7 місяців тому +9

    This woman is brave

  • @ChifundoKadaleka
    @ChifundoKadaleka 7 місяців тому

    Fire 🔥

  • @thokojona9686
    @thokojona9686 7 місяців тому

    Fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @Discar_mw
    @Discar_mw 7 місяців тому +2

    This was a hot 🔥 one lol 😂

  • @lukainnocent5380
    @lukainnocent5380 7 місяців тому +1

    mbuzi chisale ukuona ngati bambowakowo sangawine ameneyo wapha albino wakwa na

  • @user-to4or4jw9g
    @user-to4or4jw9g 7 місяців тому +2

    MCP ikazachoka m'boma idzazunzika kwambiri

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk 7 місяців тому +6

    Powerful talking and intelligent, proud of you @Norman Chisale

    • @henryhenry6632
      @henryhenry6632 7 місяців тому

      Intelligent ya ku machende amalawi mapanga support zingawenga bwanji, kupusa

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 7 місяців тому

      Mukuyamikila chisale man? After all what he did now you're embracing his work.... don't you know people lost trust in DPP and one of the biggest reason ndi iyeyu

    • @LetsSeePlaces43
      @LetsSeePlaces43 6 місяців тому +1

      People never lost trust with DPP...anthu tinanamizidwa kuti tizaona zabwino...pano misozi yatha mmaso yayamba kutuluka ndi misozi ya magazi chifukwa Cha bodza la CHAKWERA ndi chilima.

  • @peterbyson6269
    @peterbyson6269 2 місяці тому

    respect to you both you building Malawi in this interview ..

  • @user-wc4er3lc3l
    @user-wc4er3lc3l 7 місяців тому +2

    Courage muli nayo...komano kusa kululukako kuchita kuoneseratu kuti muli ndi mtima wakupa

    • @happyzumatembo2174
      @happyzumatembo2174 4 місяці тому

      😢 or uli iweyo kut munthu akunamizele mulandu wa murder. Uthakumukhululukira?

    • @user-pn7cj9hb3t
      @user-pn7cj9hb3t 3 дні тому

      Sukudziwa chomwe ukunena, sukuona kuti Chisale amuzuza popanda zifukwa?

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 7 місяців тому +2

    Ndamva chisoni pokumva nkhani yanu bambo Chisale 😢 koma chilungamo chilipo ndipo momwe mwadutsa inumo enanso adutsamo ili ndidziko. Abale whyyy a police athu mmatero, olo ndiliineyo ndingaophwezetu ndipo ndikanamizilidwa ndimakwiya kuposanso achisalewo 😂😂

  • @shupikayintuwaluwa-5899
    @shupikayintuwaluwa-5899 7 місяців тому

    Kkkkkkk aaa zoona. Msilikali kiching, amba chilungamo n how he's feeling with de way they r treating him

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 7 місяців тому

    Yeah azayakha zomwe amamangila Norman chisale

  • @quintonmutume82
    @quintonmutume82 5 місяців тому

    Dpp yangoyenera kubweler 💓💓🙌🙌

  • @user-fj3pw4gk5r
    @user-fj3pw4gk5r 7 місяців тому +1

    Lea ndi makina respect

  • @JosephMussa-gz9co
    @JosephMussa-gz9co 7 місяців тому

    Nice interview

  • @user-cy1vf5vz8y
    @user-cy1vf5vz8y 7 місяців тому +1

    🔥🔥🔥🔥

  • @yilinase2905
    @yilinase2905 7 місяців тому

    Wow!!

  • @frazerbstaffwell5083
    @frazerbstaffwell5083 7 місяців тому +3

    Wabodza iwe umakhala kukawale pa rent bingu akulamula unalibe kanthu unaba chuma bingu atamwalira ku state house

    • @user-rr3il1vg7f
      @user-rr3il1vg7f 6 днів тому

      Eeeeeeeeee ai zikomo kwambili koma Mulungu arimbariyakhe

  • @user-lx8ow6ek6k
    @user-lx8ow6ek6k 7 місяців тому +2

    I love you Mr noman❤

  • @PetrosKachingwe
    @PetrosKachingwe 6 місяців тому +1

    Once a soldier always a soldier

  • @V_Diesel
    @V_Diesel 5 місяців тому

    42 years old? Did I hear that well? 🤔 Interesting.

  • @esthermasamba7423
    @esthermasamba7423 7 місяців тому

    Ambuye Awakhululukiredi😢😢

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 6 місяців тому

    Muluzi wa agalu ndiumozi, Chisale i fill your pain

  • @Innocentkhalani
    @Innocentkhalani Місяць тому

    Chisale katundu omanga ndi mawaya

  • @user-sf4yy6so9m
    @user-sf4yy6so9m 7 місяців тому +2

    Aaaa😮zaka 42 ndeine ndili 15 years 😂😂awa ngabodza

  • @Oscarchizula
    @Oscarchizula 7 місяців тому +3

    Chisale nd galu ndthu

  • @AlexBanda-sl7pn
    @AlexBanda-sl7pn 6 місяців тому

    Uyu ndi nsamariya wathu ku Ntcheu

  • @Resterzambasa
    @Resterzambasa 7 місяців тому +2

    😂😂😂😂😂😂😂moto kuti buuuuu L malekano umatimilila koma bwinotu akubandula mbakela bwana ameneyo 😂😂😂😂😂

  • @user-nj4ob8jw6y
    @user-nj4ob8jw6y 7 місяців тому +2

    The most evil person during Peter Mutharika regime is this bastard called Norman Chisale, very evil creature from Ntcheu. Akufanana ndi malemu a Fokus Martin Gwede omayenda ndi ma warrant of arrest m'thumba. Oyipa uyu, mbuzi, mphaka, kanyimbi.

  • @user-eg9tz6jk8n
    @user-eg9tz6jk8n 5 місяців тому

    Leah , bravo 💪

  • @user-pn7ek7wb7n
    @user-pn7ek7wb7n 7 місяців тому +2

    Takhulupirira ndiwe wachabechabe mbava

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 7 місяців тому +1

    ❤❤❤❤❤❤

  • @user-wi9hz8fk8i
    @user-wi9hz8fk8i 4 місяці тому

    Mbava chisale

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Chisale mbava yayikulu mumalawi

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8d 7 місяців тому +4

    Once a soldier always a soldier❤❤❤