THE COURT (Malawi)

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 7 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 87

  • @KestonNGUBO
    @KestonNGUBO 24 дні тому +4

    Ndere imwe

  • @user-qe9pd4qr4m
    @user-qe9pd4qr4m 21 день тому +3

    Koma abambowa ndi omweoso ankati banja lithe chifukwa cha ma ARV , lero ndimboni yaboma🤣🤣🤣

  • @SaudaKennedy
    @SaudaKennedy 16 днів тому +1

    Kkkkk koma zinazi kusowa zochita kumalawi nkhona anthu akungonkhalila maboza zaziiiiiiii

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Місяць тому +4

    Muziika nkhani za nduna apa osati anthu opanda kathu,zachipongwe basi 😢😢😢

  • @SuccesMaliro
    @SuccesMaliro Місяць тому +2

    Kd bwanji simuyankhula Chichewa pakuti nose ndi aMalawi
    Ku South Africa tikalakwa timadikila Loyer kumalawiso ndiye kwanthu ndikuti zanchamba zimenezo

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Місяць тому +9

    Nkhani zooona zenizeni mukuzisiyaa.
    Chikangawa akusowatu

  • @BhekiLithuli
    @BhekiLithuli Місяць тому +7

    Bvuto ndi boma lipereke chochita
    Kwawanthu

  • @CharlesChilemba
    @CharlesChilemba 3 дні тому

    Koma adha awa 😂😂😂 asiya zawo lero ndi mboni ayi tathokoza, koma amayi musamamange koma apatseni ndalama akayambe bussness kuti azisamalira ana awowo

  • @SlyviaPhiri-bd9uu
    @SlyviaPhiri-bd9uu Місяць тому +2

    Koma zovesa chisoni kwambiri azimayi ena alibe zeru kwambiri zoonadi kutuma Mwana kukamphempha 🙆🙆🙆💔💔💔

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 Місяць тому +2

    Abambowa ndie ndikabwelebweletu ku court 😂

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Місяць тому +1

    Vuto kumalawi kuno uphawi wachuluka olo atati azigulitsa masambao panopa palibe chikuyenda ndiy olo kholo langofika poti mutu sukugwila ndichifukwa athu akungozimangilila kusowa kuti apanga bwanji koma mulungu atikomele m,tima ndithu

  • @user-dn3gp6yi4y
    @user-dn3gp6yi4y Місяць тому +1

    Ada awa ndi woipa mtima kwambili iyeyo atawona kuti amaiwa akutelo bwanji osatengapo mbali bwanji komaso Ada awa amayiwa amafuna

  • @PatrickLuis-g2c
    @PatrickLuis-g2c Місяць тому +1

    Neba wamaboza

  • @CharityGondwe-bw9gs
    @CharityGondwe-bw9gs Місяць тому +1

    Talowesani khani yakuchikangawa menemo osati zimenezo. Zaziiiiii

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly Місяць тому +2

    Paja ku court ndi kwa mphawi zopusa basi

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Місяць тому +2

    Aboma inu ndinu zisilu

  • @BrownBanda-q3t
    @BrownBanda-q3t 10 днів тому

    Mmmmm malamulo enawa aziyenda ndithandizo nanga akanatani mayiwo??

  • @AulivinChaula
    @AulivinChaula 19 днів тому

    Abambowa ndaboza mesa ndiomwe anabweras ndi yawo kt anthetse banja iiiiyaaa nkhan za bonza

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Місяць тому +1

    M, tendele ose wadziko la Malawi uli m, manja mwa chikangawa ndi nduna zake basi

  • @michealchilemba3149
    @michealchilemba3149 28 днів тому +1

    Onse a Malawi choyankhulira English ndi chiani ngati muli Azumgu ku Court ko

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Місяць тому +1

    Vuto lokwatiwa ndicholinga choti mamuna azikudyetsani ndilimelo. Kuntumiza mwana ku umasikini malo momutumiza kusukulu.
    Pezani chochita, mamuna akamakukwatirani mukupanga ka geni kangachepe. Ndi izi amuna kukuthawani basi inu simudya. Olo ntchito yochapa malainimu simungagwire? Olo business ya masamba simungapange? Mwanayo tsogolo lake mukuliganizira? Mwangokhala amai opusa, opepela, ndipo ankhanza. Pitani mukailawe ndende mai.

    • @AnnieKazembe-ic5vp
      @AnnieKazembe-ic5vp Місяць тому

      Ndiudindo waketu umenewo zimangotengera ndimamuna amene wakumana naye kuti kodi mapezedwe ake ndiotani akazifetu ndichongothandizirq osati tingatenge udindo onse wazibambo ayi

  • @user-tn2qg1vs9j
    @user-tn2qg1vs9j Місяць тому +1

    Neba neba neba mutu sukungwira ❤😂😂😂

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Місяць тому +1

    Km iyi nd nkhan yen yen kapn sewelo pot abambowa ngt Tinawaonas week yatha pa nkhan yinas yokhuzanas za banja

  • @anastasiakalipalire6260
    @anastasiakalipalire6260 23 дні тому

    Kd abambo awa mesa last WK anali ndimulandu wawo,,,tchito yawo ndiyokharira Court,,,

  • @PaulNdala-kw3ob
    @PaulNdala-kw3ob Місяць тому

    🎉 please next time finish the store komamso osamangoti tanvan sikukwanira kukhala title s

  • @HalimuChisaka-o1t
    @HalimuChisaka-o1t 5 днів тому

    Kod simungapase chisamariro

  • @CathreenKadwala
    @CathreenKadwala Місяць тому

    Zaziii osabweresa poyera aja apezeka ndindalama kubwalo landege ku Zambia aja

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t Місяць тому

    Neva iwe chimene ukadachita ukadapeza njira zoti mayiyu athandizidwe pazimene akusowa pakhomo ndiye APA mwamanga mayiyu mwanayo pakhomopo azikhalapo ndindani munasowa nzeru pachiyambi neba

  • @MerryWayson
    @MerryWayson Місяць тому

    Program iyitu ndaikonda, tamphunzila kwambiri kuziwa udindo Wa Mwana komaso Mai pakhomo kkkkkk komano Mai mzangayu ndichisilu chamunthu Mai wanzelu kutumiza Mwana ndithu komapemphesa ngat wamisala zowona aàa Alandile chilango

  • @jameskamanga628
    @jameskamanga628 29 днів тому

    Koma ziliko 🙌😋

  • @creativecassim4831
    @creativecassim4831 27 днів тому

    I have seen a guy with different names in two episodes

  • @mphatsomaluwa
    @mphatsomaluwa 24 дні тому

    Tiziyakhulanapo chichewa apa

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Місяць тому

    Iwe neba uzafera zayeni ugowona mene akukuoneramo iiiii zilikotu 😅😅

  • @CHAPITASINGINI
    @CHAPITASINGINI 23 дні тому

    Ugalu basi ndiye kupepha ndi kuba chabwino ndichani mukusiya milandu ikuluikulu kumakamba zithu zaziiii uchitsilu et dikilani ndimuwuze JB akutukwaneni mapwala

  • @Esther-r8c
    @Esther-r8c Місяць тому

    Neba uyu mesa ndi uja anamangitsa nkazi wake kuti wamupasira matenda

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 Місяць тому

    Akuvutik kulankhul chichewayo ndi mchew oimbidwa mland mchew kom ndikumufun munthu win mchewanso kut azimasulir pal nzer yanj tsono kungonong nthawi

  • @edgarmsofi589
    @edgarmsofi589 Місяць тому

    Judgement: suspended sentence. A tengerepu phunziro basi.

  • @Esther-r8c
    @Esther-r8c Місяць тому

    Mmm iwe sunawathandize bwanji

  • @AnnieKazembe-ic5vp
    @AnnieKazembe-ic5vp Місяць тому

    Boma limanga bwanji maiyu pomwe ana ake amavutika nawo okha opanda otengako mbali even bomalo siliwathandiza ,ine nde anaanga munthu wina sangandiuze zochitatu pokhapokha ngati amandithandiza atha kutengapo mbali

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON Місяць тому

    Nde ndimene lilidzikoli lathu li china chili chonse ndichovuta kupeza nde mumafuna kuti atani mmene dziko lilimu mfunso langa ndilakuti chomunjaJila mulandu Chifukwa chani

  • @FireKajambe
    @FireKajambe Місяць тому

    Court's Powerful are from dark kingdom

  • @user-zl9eq8jw1q
    @user-zl9eq8jw1q 24 дні тому

    Tufuna za chifunga ife osati izizi ayi

  • @creativecassim4831
    @creativecassim4831 27 днів тому

    Kodi ilili ndi sewero chan?

  • @AndileyaMkandawire-x8r
    @AndileyaMkandawire-x8r Місяць тому

    Aneba mukanapanga njila kuti muzimayiyu azipezela chakudya chifukwa akamangidya anao avutikabe ndiye asambuka oyendanyendao chifukwa aziwa kuti njila yomwe amamuuza mayio ndiyolondola kom siyorondola tiyeni tizipasana zelu zokhwima khani isana fike poyipa, naweso mayi ukanauvomela mulandoo pachithu choona sitimakana akanakuthandizani zelu yopezela chakudwacho eeee zovesa chisoni chifukwa mbali zose sizinali bwino bamafunika oyimilila waphavu kuthesa votolo

  • @LinasMunthali-gb1md
    @LinasMunthali-gb1md 24 дні тому

    Nde tidziwa bwanji kuti chigamulo chinali bwanji?

  • @user-tg3ju1mw9t
    @user-tg3ju1mw9t Місяць тому +1

    Kodi nkhani izi bwanji zumakhala za anthu amodzi modzi? Ndi drama mwina? Onsewa aliapawa amabwela ndi nkhani zosiyana siyana

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 Місяць тому

    Kodi ana amasiye woynaglidwa ndi a ma bungwe,amafunika kuti azigwira ntchito yolima minda??? Kuno ku mudzikwarhu kuno tikuwona ana amasiye akulima Munda,zikumandimvesta chisoni

  • @gladysmanthimba7851
    @gladysmanthimba7851 Місяць тому

    Bambo a mwana amangidwe

  • @user-ym6xu3xt2i
    @user-ym6xu3xt2i Місяць тому

    Ku nzunza mwana kumpatsa udido pamene suli wake

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Місяць тому

    Vuto ndi njala MCP ndiyomwe ikubwelesa mavuto amenewa maboma apita mbuyomu kunalibe zimenezi

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Місяць тому

    ❤❤❤

  • @jahmanmakwinja-ef7zn
    @jahmanmakwinja-ef7zn Місяць тому

    Ndye akusamalidwa nindan panopa mutamumanga mzimayiyu?

  • @MalackPatrick-jt4hk
    @MalackPatrick-jt4hk Місяць тому

    Koma maniwa atava anachitapo chani ndiompenga ameneyi

  • @aurorethomas5814
    @aurorethomas5814 Місяць тому

    Muzimalizitsa tinve chigamulocho

  • @AUFIMADENGU
    @AUFIMADENGU Місяць тому

    KHANI YAVEKA KOMA VUTO NDIMAVUTO BOMA LIKUYENERA KUKHARA NDI NDONDOMEKO YO PHUZISA MIZI KUTI KUTERO KULAKWILA MALAMURO IZI ZAPANGIKA CHIFUKWA CHOSAZIWA ZIKOMO

  • @AtupeleChitenje
    @AtupeleChitenje Місяць тому

    Ma number ama athu oona zakhaza zanawo tipaseko 😢

  • @HalimuChisaka-o1t
    @HalimuChisaka-o1t 5 днів тому

    😂

  • @jahmanmakwinja-ef7zn
    @jahmanmakwinja-ef7zn Місяць тому

    Neba oipa iwee

  • @ForsterThawan
    @ForsterThawan Місяць тому

    Ada awaso ndiopa ntima kwambili

  • @joma5327
    @joma5327 Місяць тому

    Stupid program bwanji simumaonetsa the conclusion of the case chigamuro

  • @CliveChikaphonya
    @CliveChikaphonya 29 днів тому

    Kd mboniyi ikupezeka bwanj pa nkhan zambir

  • @egreymkumba-tj5ji
    @egreymkumba-tj5ji Місяць тому

    Anthu ake angokhala omwewo kodi ndi drama eti

  • @wezzieneba9238
    @wezzieneba9238 Місяць тому

    She is so innocent, please, forgive her and tell her what is supposed to be done. She has said that she didn’t know. Even God will punish us on what we know. She doesn’t know what it means, the so called constitution. She is there to be forgiven and tell her what to doing. What she did or she was doing is just the consequence of poverty and neglect from her husband. Yes, it wasn’t right, but she needs to be guided and not penalized. My food for thought. Thank you.

  • @amaliphiri1846
    @amaliphiri1846 Місяць тому

    😂

  • @EusébioLucianoGaiondo
    @EusébioLucianoGaiondo 21 день тому

    Aaaa

  • @HarryChikandira
    @HarryChikandira Місяць тому

    Ndi program yodziwitsa anthu za malamulo okhudza ana Komanso chilango chomwe chimaperekedwa Kwa olakwa.Program imatenga nkhani zenizeni zomwe zimachitika mmalo momwe tikukhalamu bwana wanga ndithu ACC mene munafunsa kuti ndi drama kodi nanga bwanji anthu ake as mangokhala Omwe omweomwewo.

    • @AnnieKazembe-ic5vp
      @AnnieKazembe-ic5vp Місяць тому

      Aziwisa bwanji Ngati amatengako udindo okithandizira

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 Місяць тому

    Mwano mulibe podaliraa

  • @IkhenaCalvin
    @IkhenaCalvin 21 день тому

    Kwambili owe unatumiza nkhaniyi plus just check out for this woman maybe we can help her

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Місяць тому

    Vuto ndi MCP fertilize ndi wodura china chilichose chakwera ndiye amuna akuthawa banja chifukwa akusowa mtengo wogwira

  • @chiletsokazembe-ri4ic
    @chiletsokazembe-ri4ic Місяць тому

    Neba munakangopita ndithumba lachimanga basi kut maiwa achite manyazi

  • @BhekiLithuli
    @BhekiLithuli Місяць тому +2

    Can you send me that number for she's number kuti tiwathandize
    Tiwapatse ndalama kuti ayambe business pepani pa izi plz

    • @g_deonm5793
      @g_deonm5793 Місяць тому

      Chokani apa...mungofuna muwapange ujeni........