Kodi comrade ntanyiwa nkhamiyi wayinva pena amabakera atupere ndi Achair nanga apa akuti bwanji ?uyuyu wasambamo mmanjatu akuti achair ndi atupere akuziwa bhobho za kuyitanidwa kwa MCP shame on you people for UDF.we will not trust you anymore chifukwa penapache ndinu ang'oma yaganda iya
UDF TU NKHANIYI SIIKULIMBIKIRA. NKHANIYITU YACHOKERA KU DPP NDI AMENE AKUYANKHULA PA SOCIAL MEDIA.DPP NDIYE MDANI WANKULU WA MCP CHIFUKWA ANAPITIKITSA MBOMA ASANAMALIZE KUBA.
Iwe aisha iwe ndichitsilu kwambiri iwe garu kwambiri wadya ndalama ya mcl wekha ndiye iwe ukumutenga mmalawi kukhala chitsilu chaiwe hule wachabe chabe zonse zimene ukupanga ukuyesa anthu sakuziwa samala ufa posachedwa garu iwe ukuyankhula chiyao bwanji chipanichi ndi cha nthundu wina uli onse samala phwanga ndakuchenjeza chaka chino ndi chomaliza kukhala kupaliyamenti kukakhals pakhomo kapena kumanda be careful
Zikungoonetsa kt chomwe mukuchita smukuchidziwa tonse ndi ife amalawi nde chooyankhulila mu chiyawo ndichan zikungotanthauza kt Oro mutawina upere ndekuti zonse muzazipanga kudzela nchiyawo ,,,,,,,zosankhanazo ndizomwe tikuukanazo ,
Momwe mwatelemu ndiye kuti chipani Cha UDF chatha ndipo muyembekezele kuluza or ma Mp ambili sumawapeza anthu a UDF tiyeni tiyendele limodzi tipite mu zipani Zina monga DPP afford ndi UTM bs zinazo zitayeni ndi achina UDF awowo
Komabe tiwalangize asanapange zopusazi
Naweso Ayisha mambomo bwanji ukuyankhula mchiyao mwakomo ukufuna ife sitinve nawo kelekete kelekete chiyao chakocho kumapete ukumalizira chichiwe koma naweso😂😂😂😂
Eti ine palibe chimene ndamvapo 🤷🤷🤷🤷🤷
Pena zikundidabwitsa kuti bwanji atupele ndi bambo ake ali duuuuu osalakhula chilichonse since ngozi ija chichitikireni
Bakili muluzi sangayankhule kanthu chifukwa paja amuchotsera mulandu uja ndiye wadya banzi akakhala Atupele anatha amene uja akuwaseweretsa amalawi
Azimwale andalama awa cholakhulira chiyao ngat chipanicho chayao bwanji
Eti eti ma savage kupusa
Aisha.., wagulitsa . ndi. Lilian. Patelo.... asakupusitseni..... akulu akulu.... tidzaliratu. Patsogolo
panjanso atupere ndimchewa ndichifukwa akufuna kupanga alayasi ndi mchewa mzacheyo tizaona 2025
Amuluzi dpp yawazuza mokwana komaso inawachita chipongwe moti Atupele chonde ganizani mofasa dpp imafunafuna kuti ikuthesereni chipani
Zopusazokhazokhabas zikuineselatu kut mulimbaliya mcp kaliwen muzazivotela nokha
Nambo achakulungwa manyilile the invitations ungwi nambo yawogoya ,Aisha Mambo sampano tupikene nsampano tupochele uthengawo wanuwo ,😅😊 nsampano tindende ULI Aisha ??
Tiye nazo kuchenjera kumeneko kutha aise Malawi anadzuka pano 150million udzalira mchiyawo uone nonsense
Kodi comrade ntanyiwa nkhamiyi wayinva pena amabakera atupere ndi Achair nanga apa akuti bwanji ?uyuyu wasambamo mmanjatu akuti achair ndi atupere akuziwa bhobho za kuyitanidwa kwa MCP shame on you people for UDF.we will not trust you anymore chifukwa penapache ndinu ang'oma yaganda iya
ndakuvetsa zachiziwikire anthu amenewo adapha nawo Shani, ndakuva sister, anthu oti adawaphera akuziwa kathu tidangoyiwala that guy is evil remember matafale
Chokan makadeti mukufuna kumagwilitsa tchito athu ngat audf chosecho makadeti
Ife ngati masapota a UDF dzamanyi ayi ngati wadjandalama ndidzako ife tikhodza kukugendani
UDF TU NKHANIYI SIIKULIMBIKIRA. NKHANIYITU YACHOKERA KU DPP NDI AMENE AKUYANKHULA PA SOCIAL MEDIA.DPP NDIYE MDANI WANKULU WA MCP CHIFUKWA ANAPITIKITSA MBOMA ASANAMALIZE KUBA.
Km zowatenga anthu ngt opusa sidxabwino udziwe sudzavota wekha ovota ndi anthu ndye mukanakhal kuti mumaona mavuto aanthu sibwezi mukupanga zopusa zanuzo mai
Iwe aisha iwe ndichitsilu kwambiri iwe garu kwambiri wadya ndalama ya mcl wekha ndiye iwe ukumutenga mmalawi kukhala chitsilu chaiwe hule wachabe chabe zonse zimene ukupanga ukuyesa anthu sakuziwa samala ufa posachedwa garu iwe ukuyankhula chiyao bwanji chipanichi ndi cha nthundu wina uli onse samala phwanga ndakuchenjeza chaka chino ndi chomaliza kukhala kupaliyamenti kukakhals pakhomo kapena kumanda be careful
Ndi chisiru kumene iweyo ngt sukudziwa udziwe lerol ndwe opepera wamva osanena zoona kwauza anthu
Atcheya and his so called son ndi athu osakhala bwino ma betrayer,atupele si mtsogoleri ndanena ndanena period
kod simungamayankhule chichewa kupangila enafa?
Ifeno timva chani simungayankhule chichewa aaaa
AISHA MAMBO NDIWE KANYIMBI KUNYASA KUCHIKAMWA KONUNKHAKO
Vito lanu mukukonda ndalama mudya Za satanic
A tupere nd mamuyesa ngat nd oganiza bho
Inu athu akutulukan ndivuto zainu akumipando
Ndiyeno pangani cas asabwere mcp bas
Ndiye potenafe sitivachiyawo
Kagendeni amene wa MCP aliyense.
Mulibe zeru achina kholokolo
lwe aisha ndiwe ngalu nditu
Nde ife tikumva zimenezi aaa
Salani ndi udf yanuyo
Ndiwe galu kwabas
Mwapanga zibwanatu
Tulan pans udindo
Kwavuta UDF yatha
UDF yatha basi
More 🔥 Aisha Mambo
Uyu si Aisha Mambo ayiii bozairi
Hule iwe
Nde uthengau ukupita kwa ayao basi?
Ayi si ayao wokha ayakhulanso chichewa athathauzila
Ndiye kuti bakili anapanga nawo chiwembu chopha shanil ndipo zinamisangalatsa kwambiri