A Timothy Mtambo Akufuna U President - Country Man & Uncle
Вставка
- Опубліковано 30 вер 2024
- On Nyasa VoiceBox, loyal DPP supporters Country Man and Uncle says that the U-turn Honourouble Timothy Mtambo, Former Minister of National Unity has taken on President Chakwera simply means he wants a crack at the presidency himself.
Mtambo u president hahahaha....kape ameneyi kapeeeee. Mwina anthu arelo sadziwa kuti kape ndichani??? Cosefera mowa wa masese ..
Dzina lake ndi kape...ndiye mtabo galu wa Munthu...wobwera
Mtambo u president? Mtambo adasewera game yovuta kwambiri pa Malawi pano so paibe angamufune. Thumba lomwe adalandira ku MCP latha pano akufunaso ife a Malawi kut atipusitseso? Uchitsiru sagawana so usilu wakowo khala nawo wekha😂😂😂
Vuto ndi ife amalawi kuchemelrla zilizonse monga a nanenela achakwela timangoyamikila olo tikuziwa kuti akutipusisa muona ena akwela ya amtamboyo
Mtambo what is that? Alibe nzelu ndipo aziwe kut choipa chisata mwini coz watizunzisa aMalawi mfiti
Mtambo angakhale President, asah! Adaika anthu mu mavuto , akagwele uko chitsilu cha munthu.
Hahahaha 🤣😂🤣 Mtambo sitidzamukhululukira anatigulitsa ife a Malawi m'manja mwa satana relo tikuzunzika kamba kazibwana zake.
Zopanda mutu, sanali Mtambo yekha odana ndi dpp koma a Malawi. Ndiye musatinamizepo apa
Ndiye zakupindulirani Chan
Akhale presented ku family kwawo angomvotere ndani ngalu wamuthu akanyere uko
Koma ndie akanyeredi iyaaa😂
Ndinkhani yomveka ntambo tachuluka omudandaulo chifukwa ndi amene ankalimbikisa uchiganga 😂😂😂
Koma ndiye kulakalaka kkkkkk!
Kkk akuti ndi chigawenga