Ndalama ndi zimenezo koma mzipatala mulibemo mankhwala shame. Bon kalindo Mulungu anasankha inuyo ngati ngelo wamulungu pakati pa dziko amalawi I silute you
Umboni tauwona kuno ku Zomba ma centre ena anatsegulidwa kwa 5 days ajambula kwa masiku awiri masiku enawo amati mafuta anawathera mu magenarators. Keep it up Kalindo we're proud of you.
Mbuli izi ndi kalindo wanuyo ine ndatulukamo mu DPP ndimaganiza anthu ake ndi a mzeru koma eeeeeeeee kuyambila atsogoleri ndi owatsatila omwe akuyendera magazi a ndale panopa akufesa ndalezo adzakololanso ndale zomwezo
Please a Law Society of Malawi ndi zipani za opposition zonse pitani Ku court mukane mfundo yoti opanda National Id asavote. Kuchokera pachiyambi timavota polembetsa mu voter register pogwilitsa ntchito passport, driver's licence,Kalata yochokera kwa mfumu etc . Every Malawian above the age of 18 is eligible to vote without National ID restrictions.
Mr kalindo ,mfundo imeneo ndiyoona a kufuna kubela ma vote njira yake imeneo .Ndie ndikofunika kti anthu asavotere through l D chifukwa xisokonexa xithuxi pls.
Wanthu azavota ngakhale alibe cha u nzika ngati bungwe lo imirira chisánkho achite zopusa Litha, Chakwera wapha Chilima.aliyense waziwa Ndipo Chakwera pa nyero pa mache
If only your family will vote you can talk that rubbish MCP it's not the way simple you think most MCP members they don't respond rubbish the don't talk nonsense they make sure keep quiet no fight with empty teen wait and see chakwera is not a small boy of Malawi so he is always showing the nation of Malawi that he is full grown up man always is away from the stupid people 2025 be careful
@@UTHMAN-WAYA police kapena MCP tell people the truth don't just talk cause you can talk what I need people must go to court tell them MCP is no longer MCP is a police but talking while you're sleeping by house it won't solve the problem
Izi ndizoonadi ku south kuno nrb palibe chikuchitika ife tikudabwa kuti a oppositions Ali kuti??? Nkhani ya ziphatso ikuyenda bwino only central region wat is this after all?? Nrb ikufunika kuyipangira ma demo akuzolowera tsopano kaya adya ndalama azisanza ndithu.
That's very wonderful massage it's true,tiyeni Malawi tisegule maso
Ndalama ndi zimenezo koma mzipatala mulibemo mankhwala shame. Bon kalindo Mulungu anasankha inuyo ngati ngelo wamulungu pakati pa dziko amalawi I silute you
Umboni tauwona kuno ku Zomba ma centre ena anatsegulidwa kwa 5 days ajambula kwa masiku awiri masiku enawo amati mafuta anawathera mu magenarators. Keep it up Kalindo we're proud of you.
Why translating it English ?
Ukhalise DC Ukutisegula maso
Big up DC
Mr DC timakunyadilani Cox mumatisegula maso and mumaima pachilungamo
Mumatiimila bro
Umakwana ase
The last man standing umakwana big man
Wake up call
❤
Yes tell him he think he is live president
Kom mcp kuwina tizavotaso cz axakhala kuti abela 99
Mbuli izi ndi kalindo wanuyo ine ndatulukamo mu DPP ndimaganiza anthu ake ndi a mzeru koma eeeeeeeee kuyambila atsogoleri ndi owatsatila omwe akuyendera magazi a ndale panopa akufesa ndalezo adzakololanso ndale zomwezo
Stupid 😢
Please a Law Society of Malawi ndi zipani za opposition zonse pitani Ku court mukane mfundo yoti opanda National Id asavote.
Kuchokera pachiyambi timavota polembetsa mu voter register pogwilitsa ntchito passport, driver's licence,Kalata yochokera kwa mfumu etc .
Every Malawian above the age of 18 is eligible to vote without National ID restrictions.
Mwana oopsa kwambiri the DC
Awa ndi big man amayankhura chilungamo ❤
Muthu openga ndiyekhayo angasapote mcp
I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi
Mr kalindo ,mfundo imeneo ndiyoona a kufuna kubela ma vote njira yake imeneo .Ndie ndikofunika kti anthu asavotere through l D chifukwa xisokonexa xithuxi pls.
Zonwe akunena Bon Kalindo zokhuza NRB ndivomelezane naye ndithu,kuno Kumangochi zachitika ndipo zikuchitikabe madela ena.Pano anthu ambiri asiyidwa mu masenta olembesela zaunzika kut alephele kukhala ndichipatso chaunzika ndicholinga kut anthu asazavote ambiri kuno kumwela ndipo Ineyo ndimboni ndithu kwa Born Kalindo.Pa anthu okwana 300 pamudzi uliwonse amene alembedwa zaunzika ndi anthu okwana 100 akha basi Kumangochi kuno,ambiri enafe tasiyidwa akuti nthawi yatha sapitiliza koma 2days yokha ndimene akhala akupanga process ya NRB mumasenta onse kumangochi kuno
Mose atamwalila mulungu anapeleka wina mtsolelli mpaka anakafika ku dziko lamalonjezano ndiye autm msabwelel ayi mulungu atipasa wina tisafooke tisapange mantha tipite chisogolo
Ayi ndithu tikuyenela kukavota opanda ID chifukwa zimenezi zitiphela maufulu athu,
A utm please stand up and be united. We love this party. We are behind you. We thank you Boni kalindo for saying the truth
Big Freedom fighter of Malawi
Yes,zoonadi tiyeni a Malawi tisagone tulo
Zawapengetsadi ndlam ndichifukwa akugula masuti ovala mwana opanda size ndipo olo chigawo chapakati sitikuwafuna achakwela ndi nduna zawo onse amenewo salowaso boma chaka cha 2025
Ndiyeno zikusonyeza kuti anthu amene akubwezedwao Sitidzavota? Chonde chinyengo chimenechi tayambatu kale kudandaula.
Wanthu azavota ngakhale alibe cha u nzika ngati bungwe lo imirira chisánkho achite zopusa Litha, Chakwera wapha Chilima.aliyense waziwa Ndipo Chakwera pa nyero pa mache
😂😂😂😂 a president ndeno mukuzikanda pasaya apo pakuyabwa mumanivesa kukoma inu aboni pangani chipani tizakuvotereni ife anthu osauka chonde
Muthu uyu wa dpp,osangobwerela ku dpp bwanji mbuzi yamuthu iwe😊
End of MCP ndanena ndanena /wetting zachitika ku Kenya basi!!!!
DCcc ndiwe katundu omanga ndi wire always proud of yu
If only your family will vote you can talk that rubbish MCP it's not the way simple you think most MCP members they don't respond rubbish the don't talk nonsense they make sure keep quiet no fight with empty teen wait and see chakwera is not a small boy of Malawi so he is always showing the nation of Malawi that he is full grown up man always is away from the stupid people 2025 be careful
@@JackMvura-ik2td🤣🤣🤣Inu MCP ikumanga anthu ndemuzit ili Quit aaa🤣🤣💔
@@JackMvura-ik2td uziwo ase kapena umadyanawo za chipanizo? Zako zimene asaah.....
@@UTHMAN-WAYA police kapena MCP tell people the truth don't just talk cause you can talk what I need people must go to court tell them MCP is no longer MCP is a police but talking while you're sleeping by house it won't solve the problem
Anzathu ku Kenya amuonetsa Ruto koma ifeyo a malawi Kaye tinabadwa bwanji?
Nkhani ya azanu nde simukamba ya avice pulesidenti takambani wez
Pangolini ululani tikavote asinthe zimenezo isagwilentchito.
UTM ingotuluka mwachangu isanafike thawi ya campaign
Iwedi ndikatundu....ine kudabwa kuti opposition mukudikila liti
Akalindo mulungu azikutsogolerani thawi zose❤
Zoona zake DC umakwanira iweyo tikavota bas ooanda cha uzika
Thanks kalindo for the good information.....keep it up am behind u
Neighbour waionera patali game ....this is true !
Ndipo ñdinu nokha otimenyera ufulu
🔥New clear BOM,Bonn Kalindo!
Tivote ndi ngati kale ma id tilibe
I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi
I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi
Openga kwambili ndiyemwe angabweleleso ku DPP mutu wake unayima fwetseke zanu ndi kalindo wanu yemweyo mwalandila ndalama kwa gogo wanu opanda mano mkamwayo ndinu zitsilu shupt
Lemekeza atateako ndi amako kut masiku amoyo wako apitilile
Pompano 😅Kenya Kenya game ndizikwanje
Chakwela awukhudzidwa za ifa ya saulo chilima
Timadalira inu bwana DC mumatiyimila amphawi
Muleken mwana wa eni alankhule za kumtima kwake.
Ulem wanu mnthu wamkulu kwambili
Ulem wanu mnthu wamkulu kwambili
Koma uyu Nde amatokotadi eish
Is our president thanks
For sure this is State Capture
Mbambande, keep it up
Tili pambuyo pano DC
Ichi chimandisangalatsa
Ulemu wanu big man,mumatiyimilila
Big up our own DC
Zoona big man kalindo
.... Kuswa kuswa....opha mnzake, naye aphedwe
Born kalindo nd Dolo
Mumakwana ulem wanu
Chakwera why are you evil 😈
Chakwera why are you wicked
God will punish you soon
Osamabisila
Pari galu wina mmenemu waremba masege yonyoza chilungamo cha DC mancgendeake ameneyo mot Malawi mmene akuvutikila ndipo ndikuuzen agalunonse zomwemwaba mukudyazo mukanyera mundende apa sitikusekerelan tatopananu iwenamachende chakwera segula zimakhutuzo uve nthawiyanu yatha
It's fact
It's true
Bg up Dc
DC 🥰
Ndalama za satanic, samalani. AMALAWI amzanga dziko ili laipa satanic yalowa mudziko lathu ili CHAKWERA atipereka kwa satana
Umakwana fadah
DC ❤
Dc
Chitsiru ichi
Ulemu wanu
kod bwana DC ukamapanga zimenezi umafuna chani kwenikweni ??? anthu andale awa amafuna kumatisokoneza anthu akumidzife mbolatu iyi
📌
❤❤❤
Izi ndizoonadi ku south kuno nrb palibe chikuchitika ife tikudabwa kuti a oppositions Ali kuti??? Nkhani ya ziphatso ikuyenda bwino only central region wat is this after all?? Nrb ikufunika kuyipangira ma demo akuzolowera tsopano kaya adya ndalama azisanza ndithu.
Campaign will be easier for opposition parties. A mcp apha chilima. 90% ya anthu mu Malawi akuziwa kuti mcp ndi amene apha chilima.
Chilombo chachilungamo koma bon kalindo mulungu akutetezele until nkhwandwe itachoka 'l think akufuna tipange ngat anthu akukenya.
Palibe munthu amene angavotere nkhope ya chakwera ndi mcp. Never
Tizavota zopanda ma ID apo ayi miyala izagwila ntchito kuphanakuphana basi
Bwana Dc mumakwanila hvy ndipo musasye kutimenyel ufulu
Born kalindo umatiyimilila,,,tili kumbali yako
Malawi cwa mun2 uyu
Umakwana mr DC tingopita pa nseu basi .mbuzi zimene zatitopesa kwambiri.
Big up born kalindo With powerful message 👍
ndimakukondani a born kalindo ❤❤❤
Osafooka go on
That's powerful message continue to show them the right way to catch this big fish mr nyo
I support the motion
Pamene anthu akuvota NRB izakhare pomwepo
Ndikungopanga scroll koma ndisanapeze pomwe amunenera zoyipa Bon kalindo more fire
Kkkkkkk akuti ndi president osauka ndiye inu ndi osauka moti daily amakupatsani chakudya
Aliyese akavota
kunali achina mtambo pano kuli ziiiii anadya chimbazi chafuleshi kkkkkkkk
Mulungu adalise Born kalindo ndi azake ose otimenyela ufulu
Mumatiyimilira Bwana BORNE KARINDO tilirimodzi osaopa
Ayaluka akubawo