Palibe Anganditume Ine Kuti Ndikasake Munthu - Mike Chitenje aka Bangwe One
Вставка
- Опубліковано 23 тра 2024
- On Nyasa VoiceBox, Businessman Mike Chitenje aka Bangwe One refutes claims that he is one of the alleged individuals sent by government to hunt down Owner and Manager of Bakili Muluzi TV.
Ku Nyasa Voicebox, bambo Mike Chitenje aka Bangwe One akutsutsa zoti ndi m'modzi mwa anthu omwe akuganiziridwa kuti anatumidwa ndi boma kukasaka Mwini komanso Manager wa Bakili Muluzi TV.
#malawi
ADPP anakhapidwa kulilongwe bwanji ngati muli madolo simukuwasaka mukulimbana ndi mfana wa bakili tv mknkuyu nkhani ya witika isakupweteke ukuziwapo kanthu
Thumbs up Mike for coming open and clear yourself and kuyankhula kwambiri,kuyipisilana mbiri baasi
Kuno ku South Africa bwerani koma sumuzabwerera bakili tv is our Chanel
MCP ngati mumapha anthu ndikale lomwe lija not now nthawi munapha achinagama aja.
MCP Ndichakwela emweyo pantumbo panu
Aaaaaa akunama sangampedze bakili muluzi
Amalawi Ali ku south Africa Ali ndi mifuti yambirimbiri Koma ndi zitsiru zosagwirizana akabwera ziombelani KOMKO
🔥🔥🔥🔥
Abwelele komwe anachoka💪💪💪
Good
Brother man Bangwe one ,mumatiyimila.
nyasi zanuzo kumalawi konko kuno mudzamenyedwa ndi azimayi
Koma ndizot south Africa angakudulekhos sangaziwike usayelekedze kusaka muthu abweleekha ofalitsa uthengayo
Wayakha bwino Brother amphawi awa asiyeni
Ma💯👍
Auze bro akanganya amvesese bho
Atha kupita ameneo asaname ameneo
Abwele ku south Africa kuno tiwaphela konkuno manyiwo azipanga ku Malawi komweko
Kunkuyu ndiwe opusa kwambli zoona uzikhara ulimbana ndi za pa social media
Nanga boma limasankha omgwilitsa ntchito? Mmesa amapereka chithumba?.. ndizowona ..komanso akati Ali ndi ndalama kale ,ndalama zimakwana..palibe akulimbana nanu atopwa...utsi sufuka popanda moto. Chilipo chomwe chachitika...
Komanso akamanena kuti akufuna awathandize kuti alowenso m'boma akuthandauza chani anatumidwadi garu ameneyu
Apite ku South Africa adzathela konko
Kuno ku SA zopusazo ayi ndale zaku malawi osabweletsa kuno anthu olephera. Musiyeni bakili muluzi TV limbanani ndi mbava kwanu konko anthu a MCP opanda chikondi ndi amalawi anzanu
Ngati mumapha nhthawi imeneyo si panopa ayi akukuyu abwele yekaha tsake yekha osamawatuma anthu kufuna kuphesa osalakwa..
Bwerani ku South Africa kuno tikuphulani osati masewera
Tikudziwa kuti ena ndi a Dpp pakhope pomwe mumtima ndiwa mcp
Ozatsaka Bakili Muluzi TV
Kuno ndimuphula
Bangwe 1 kukonda ndalama ku SA akaphwedwa za u Bangwe 1 kubangwe konko
Aise tangoti pasila voice yo tiinvele, mukuchulusa zoyakhula
Press fleedom. What does it mean. Please Malawians. These ministers. Democracy is what it means to be flee. If we copied this Democracy from the west. Do you follow how Americans behave. The land of flee in every aspect. Why does it pain you if one express his mind and opinion.
Kulavula chingamu chifukwa cha mtedza wolawa😅😅😅
Ndipo Ali busy kusaka bakili muluzi tv osasaka anthu akuba ndalama za boma koma kusaka za zii aPita ndi iyeyo ku ndende akusakila azawo ziwatsata
Mwati imeneyi ndi nduna kapena mbuzi?
Sayixiwa south africa abwere ndithu azamuonesa anyamata
Auzeni
Namachende ameneyo asabwele kuno athela mmanja zikutiwawa zomwe likuchita boma la agaru atonse bolo zawo
Moses bizy ndi za ziiiii osafufuza nkhani yophwedwa ka Alani witika,kumenyedwa kwa adpp kulilongwe bwanji,izi zaonesa kuti nde police basi malo moti muwasiyiile apolice ntchito manja mwawo
Kkkkkkkkkkkkkk km kumeneko malawi kokoma sizachoka sikuthawa ku malawi kuno kokoma ife ndi aphawi odya bwino
Galu ameneyo kwambili kukunyo
Moses agulu inu wakubaso ameneyo
Osusa akamusakeso ususa 😂😂 andiyankhulila bwino zikuchi kunveka kut munthudi wandalama
😂😂😂 kunkuyu mkazi uja akuti sumakoma unangoona kupha witika
Ubwino wake tamva kale kuti politics your doing at night but one day is one day
Chi kumkuu mbuzi,nthawi iyi ndi ufulu chidzete kumkuyu.
Ndalama zikugula anthu kut azigwira ntchito yausatana yosaka anthu osalakwa,sizikuyendera kut ali ndi ndalama kale.anthu ali ndi chuma chosefukira koma amafuna zambiriso.or ali a dpp atha kutumidwa ndi a mcp
Iwe galu kwabasi chendako
Iwe manyiiii
😂😂😂😂😂😂 umakwana chief kkkk
Ife timamva zowona kuchokela kutive imeneyi zopusa ayi
Uyu wa Bangwe waniyo,ndi mmodzinso amene ali mgulu lakupha the late Evison Matafale,now you want Bakili Muluzi tv,muphedwa ndi inu tsopano agalu inu
17 Billion ya Covid ija sitinaiwalebetu
Kkkkkkkkkk inu ndiye mumakumbukilatu
Muphedwa kuno si kwa masewera zimenezo komweko
Ba Malawi....kunyanda.
Sufuka popanda utsi sinanga munthu ukakhala okaikitsa🙆
Abwele takonzeka Malo moti timuphe chakwela tipha iyeyo tili lady
Inuyo mukufuna muzibisa zanuzo
Kulu wa yakhula zoveka bagwe 1
Napantumbo kunkuyu ukunama ndizosatheka zimenezo
Akukuyu pitani nokha koma simukabwera
Usaname galu iwe upita koma chot uziwe ndiyichi imeneyo ndi mcp mukapeleka bakili tv next ndiiweyo mcp imasinda mawamba isakutembenukila chisazo zadiki miya alikut anatotolatu pamoz ndi fayisi wake a mcp or kumalilo kwa zadiki miya sanapitu or moz zadiki miya kungopita ngat chizilu kumanda nde iwe usamale ndiganyu wako 🖕
Kunkuyu opusa ukufunika gahena iweyo galu iwe
Akusowa zochita awa
Wakukhalila baliiti khalamba ibwele ti yiske
Amutuma uyu tikuphulisa mutu ukabwera kuno demeti
Athu amisala inu
Chimanga chimalora opanda mano
Muphedwa kuno msete zanuzo muzipangila komko shit
Kunkuyu mboli yake
😂
😂😂😂😂 chilungamo
Kkkkk kuyankhulatu
Zovuta kobasi
Koma ziliko???????kkkkkkkk
Dpp boma 2025
Bangwe one asaname osakhulupilila munthu
Zimapanga hate iwe wekha osati enafe
It only hates 1% of Malawians .Sanena zabodza amene uja .Chifukwa chan a court akufuna kumufufuza the so falled minister of finance?
Kugulira mwana ma galimoto 20....So ukapanga hate ndani ...Musayerekeze kutuluka m'bomamo you will be arrested surely
Kd iye wabakili muluziyo alibe ufulu oyankhula chitukuko cha mcp ndikumanga anthu?
Koma ndiye munya kunkuyu ndi chakwera wakoyo simungampedze ameneyo
Ba Malawi....kunyanda.
Ba Malawi....kunyanda.