Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

Zomwe ayankhura Mai Joyce Banda zokhunza Tonse Alliance kucha kwa Lero

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 13 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 52

  • @PreciousKaliati-l6u
    @PreciousKaliati-l6u Місяць тому +3

    Your excellency,Dr banda, your charitable initiatives are reflection of your remarkable character and dedication to the betterment of society. Keep shining mama , kudana ndi inu ndi thembelero chabe.God bless you

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft Місяць тому +2

    Malawi leaders are always talk wisely when they are out of gavervent,give them charnceand see there performance

    • @mwale86
      @mwale86 Місяць тому

      This one performed kungoti amalawi mpandila u can't appreciate because she is a woman,when she came in kunalube fuel kunalibe Forex anthu kuchipatala kumwalila because of magetsi after generator zinalibe fuel magetsi akuzima mwanyasi but she did it in just 100 days I feel that's something we need to acknowledge that she did good.

    • @chelseajackson3200
      @chelseajackson3200 Місяць тому +1

      Performed where?? She is full of family politics. Look at her age kukakamila leadership in PP. I bet she was one of those voices calling for Chilima to join MCP! Fully knowing that she will get in through the backoffice.

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r Місяць тому

      @@mwale86why do you want to make women to look like they are the most hated beings for no reason?? Pali zinthu zina zake adachitadi bwino koma anapoilabe ndithu.

  • @chelseajackson3200
    @chelseajackson3200 Місяць тому +2

    Alipo women & girls oti anapindula ndi izi akamba awa?? Atchuleni. She could've mentored a girl or girls for presidency if she was sincere😢😢

  • @SanidaChirwa
    @SanidaChirwa Місяць тому +4

    Our excellent ngat mfuna mbiri yanu izakhale yabwino mkamwalira ,tulukani mu Tonse Alliance,mpakidwa magazi oyipa kwabas

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Місяць тому

    The best leader

  • @GilbetaMasamba-te8kp
    @GilbetaMasamba-te8kp Місяць тому +1

    God continue bless you your excellency ma, your such a blessing to malawi

  • @NatashaMakay-k5e
    @NatashaMakay-k5e Місяць тому +1

    Anthu omwe munapanga ngwilizano, mumafunika kutuluka kalekale. Mwaona zisankho zayandikila muzioneka ngati okonda anthu..antku munawatengela kumavuto.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Місяць тому +5

    Aaaa awa amayi adyela adzuzitsa malawi kutipatsa MCP yokupha komatsa yankhaza iiiiii tsitidzayiwala mayi banda anatipanga nkhadza dzedi chifukwa chofuna moyo wawo kukhale pabwino otsati amalawi akhala pabwini ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii mulape mulungu akhululukileni mwanatiyika pa dzuwa

    • @mkajikosya-uq5hs
      @mkajikosya-uq5hs Місяць тому

      Nanga malemu SKC apepesenso?

    • @FosterChakanga
      @FosterChakanga Місяць тому

      ​@@mkajikosya-uq5hskumakhala ndi umunthu sometimes

  • @chikondichanza9772
    @chikondichanza9772 Місяць тому +1

    Mayiwa is one of the creams ku Malawi Kuno. Awawa ndi machine enieni. Kudana ndi mayi awa ndikudana ndi chitukuko. aMalawi amzanga alot of known countries are recognizing her as very important trustworthy and helpful woman , why not us . Lord should have mercy on us , so that we can how potential this woman is. aMalawi tinazolowera kutamikira munthu akamwalira.what a shame

    • @juntoiman
      @juntoiman Місяць тому

      Mmmmm Iwe wachibwana Eti Ameney Mesa ndimunthu Modzi adapusisa malawi

  • @user-ry9ql9jv3y
    @user-ry9ql9jv3y Місяць тому +1

    This woman is our Gem. Very good and we love you

  • @MaryMlomba
    @MaryMlomba Місяць тому +1

    Repent before it is late

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe Місяць тому +2

    Kkkk Ndàlqma za cash gate zao sadzatenga kumanda.ayi..kumwamba sikufuna cuma..nkhale awawa a mr Sattargate wa a mcp wa ndi zinduna zaozi.kwa Yehovah kuchiweruzo sadzatenga Sattargate chuma chaocho amenYoù honoüable Robbers of our nation just be awaiting to be thrown in ĥll fire by Jesus Cĥrist.for crime of Stealing or Robbing malawi nation.all the same .be blessed as you walk towards jesus christ to be judged

  • @mkajikosya-uq5hs
    @mkajikosya-uq5hs Місяць тому

    God bless her excellence Dr Joyce Banda

  • @dianachabs
    @dianachabs Місяць тому +2

    Ambuye adzikudalitsani masten ntchito zachifundo ndiye mukuzichita

  • @AlexBand-f4p
    @AlexBand-f4p Місяць тому +1

    Mwaganiza bwino kwambirimbiri tulukakoni kumeneko mwaganiza bwino kwambiri mayi zikomo zikomo

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому +1

    Chipanda Dr Joyce Banda sitikanadziwa kuti mu Boma mukunedwa ndalama

    • @mwale86
      @mwale86 Місяць тому

      Ndipo zowona no president has allowed an audit while in office it's only HE Dr Joyce Banda mayi awawa ndikatundu

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Місяць тому

    Unakasiya Chilima mkamwa mwa Ng'ona.

  • @BenardPhili-wp5jt
    @BenardPhili-wp5jt Місяць тому +1

    Amayi anthu timakukondani komanso Inu Mai mumatikonda amalawi munawamangira yumba anthu osauka ambirimbiri kuno kunkhamenya, anthu atavutika ndi ngozi za madzi munawathandiza powamangiranso nyumba kumwera

  • @FosterChakanga
    @FosterChakanga Місяць тому +1

    Tulukakoni masten,,asakupakeni nawo manyiwa pliz.Inu ndi mbambande

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 Місяць тому +6

    Makhuluku akumalawi

    • @vitujames53
      @vitujames53 Місяць тому

      Ukhuluku wakuti anasintha dzikoli with 100 days ukhuluku anapangila kuti

  • @PreciousJames-fh1xs
    @PreciousJames-fh1xs Місяць тому +1

    Amai mumakwanila palipose zitukuko muno mudziko lamalawi mwapanga m, boma ririrose
    Tikanena zothandiza osowa nde ndikudya kwanu ndipo simuona khope kana mtundu
    Amai Banda Mulungu azikudaritsan thawi zonseeee eee

  • @DevisonHala
    @DevisonHala Місяць тому

    Inu mayi chilima mumanena kuti ndi mwana wanu ndiye munachilandila bwanji chipongwe chimenechi

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому

    Anamanga nyumba Kameme , Chisenga in Chitipa District..
    Chilumba and Khwawa in Karonga
    Chintheche, Bandawe, Vizara, Chisala in Nkhata Bay
    Mzimba Boma, Njuyu, Thunduwike, Nkhamenya in Mzimba
    Lula and Ng'onga in Rumphi list endless under Mudzi Transformation

  • @BlessingsBanda-nh7ur
    @BlessingsBanda-nh7ur Місяць тому

    Zilibwino koma zomayika background music instrumental ndizopoyila pama serious massages

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 Місяць тому

    Lankhurani chabe chichewa

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому

    Anthu amalandila nkhuku kumaweta mabanja kumapeza ndalama ndikumadya bwino panyumba pawo..
    Mbuzi, N'gombe

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut Місяць тому +1

    hule wachabe chabe

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому

    Nthawi yawo mankhwala mzipatala samasowa..kunalibe basi kaguleni ku pharmacy

    • @mwale86
      @mwale86 Місяць тому

      Ndipo zowona

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Місяць тому

    Mmmmmm m'mai otapa tapa uyu uliboh mudzapita ndindalama amzathu

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому

    Nzeru zawo ndizopititsa patsogolo dziko maka maka anthu ovutika ammamidzi

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому

    Ambuye azikudalitsani ndikukupatsani moyo wautali

  • @rightlombe380
    @rightlombe380 Місяць тому +2

    Which youths do you assist?

    • @mwale86
      @mwale86 Місяць тому

      Ambilimbili through her community Development initiative project people mainly youths benefitted kupeza chakudya in kasungu isn't that helping youths??

    • @mkajikosya-uq5hs
      @mkajikosya-uq5hs Місяць тому +1

      Ambiri anapindula anagawa njinga zamoto pano akulipilira ana ma school fees through Joyce Banda foundation

    • @mwale86
      @mwale86 Місяць тому

      Ndipo zowona zake even she feeds over 15,000 children through her Joyce Banda foundation pajatu Amati mmela poyamba hence ana akakula bwino azakhala ma youth othandiza dziko lawo​@@mkajikosya-uq5hs

    • @vitujames53
      @vitujames53 Місяць тому

      Kodi kabaza ku Malawi kuno anabwera ndindani

    • @vitujames53
      @vitujames53 Місяць тому

      Tapitani ku ma secondary a Boma mdziko muno atsikana akupelekedwa ma fees..

  • @vitujames53
    @vitujames53 Місяць тому

    Mzimayi wachikondi uyu

  • @JusticeMpondaphili
    @JusticeMpondaphili Місяць тому +1

    Awa ndi mai amzelu sangakakamile ku mcp acokako

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p Місяць тому

      Nzeru sabwelekana inuyo muganiza zanu

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p Місяць тому

      Inuyo mukati achokako ku mcp inu mudakhalapo wa mcp?

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p Місяць тому

      Sitikufunaso makadeti muno mmmalawi