A Aisha Mambo Alandila 150 Million Kuti Asokoneze UDF - Evance Khaiya

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 4 жов 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Evance Khaiya claims that Honourable Aisha Mambo, chairperson of the UDF convention committee, has allegedly pocketed MWK 150 million from the MCP to sabotage the UDF's political ambitions.
    Pa Nyasa Voicebox, Evance Khaiya wati wapampando wa komiti ya chipani cha UDF a Olemekezeka Aisha Mambo ati apereka ndalama zokwana MWK 150 million kuchokera ku MCP pofuna kusokoneza zolinga za chipani cha UDF.
    #malawi

КОМЕНТАРІ • 82

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 8 днів тому +12

    Komanso UDF monga Chipani cha Opposition chikhalira limodzi ndi cholamula bwanji ? Pangani mgwirizano wo Koma MCP Will never rule again. God will save His people Mphamvu Zanu zingachuluke bwanji inu a MCP Koma simungagonjetse Namalenga. Lets wait and see.

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 8 днів тому +7

    Kodi opposition ikhala bwanji ubale ndi MCP?

    • @HaroonSaidi-jv3ek
      @HaroonSaidi-jv3ek 7 днів тому

      Ku Parliament kuja amatani Always kuzuzula ma mp a opposition

  • @binalidjeyshabahzombamalawi
    @binalidjeyshabahzombamalawi 8 днів тому +5

    Osaculusa kuyankhula muzingotipasa uthengawo

  • @Kabwilachikangawa
    @Kabwilachikangawa 7 днів тому +2

    AISHA MAMBO NDI GULU LAKO MUKATHERA KU CHIKANGAWA.BASOP!!!

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u 7 днів тому +2

    Vuto lake
    Umphawi sizinthu muyaluka nazo
    Inoyo ndi 2024 osati make zana 1965 kunalibe ma phone 🤳 Facebook

  • @PatrickMangochi
    @PatrickMangochi 7 днів тому

    Inu ndale simukudzidziwa,kodi mwaiwala kuti ndi Chair emweyo anasankha Honorable John Tembo kukhala Presidential Candidate wa Mcp/UDF alliance?musamanamize amalawi apa.

  • @MichaelMpeki
    @MichaelMpeki 7 днів тому

    Ife chipani cha udf timachikonda koma izi zokhalira limodzi ng'onazi aaaa ndanyasidwa kwambiri. Mcp zoona? Mai ameneyu waganiza bwanji?

  • @McfallenKayuni
    @McfallenKayuni 7 днів тому

    Kafufuka amene tapeza ndiwakuti UDF siyenda ndi chipani chimene sichili mboma

  • @adamujosaya-q8e
    @adamujosaya-q8e 8 днів тому +1

    Aisha mambo pamodzi ndi agaru omwe mwawayitanawo mudzagendedwa nawo limodzi komaso kwabwino kumango njamuka kusayana mkuwononga chipan sha UDF please Aisha mambo pamodzi ndi agaru omwe mukut abwere wo Koma a MCP ndat mukufuna mufike 2025 please don't come there this is oning??

  • @BilaalLalie
    @BilaalLalie 7 днів тому

    I AM UDF MEMBER...AISHA IS ASTUPID LADAY YOU MUST GO AWAY AND IWEYO SIUWINA NEVER UNTIL YOUR DEATH....YOU SEE ZITABU ZIGWIRA NTCHITO PAIWEYO UDZIWANSO.THIS IS YOUR LAST TIME TO BE AN MP

  • @IsaaczidanaZidana
    @IsaaczidanaZidana 7 днів тому

    Now muluzi ndi waufulu chifukwa cha mcp,a dpp amamuzunza chair,sukudziwa iweyo,opusa iwe

  • @DicksonYohane
    @DicksonYohane 7 днів тому

    Money is a devil

  • @NoohNowa
    @NoohNowa 8 днів тому

    Aisha Mambo ndiwadyela😢...amapanga zinthu Ngati sanatuluke kumatako Kwa anthu bwanji 😢😢😢

  • @McfallenKayuni
    @McfallenKayuni 7 днів тому

    Akutuma ndani?

  • @DysonTummiesSajiwa
    @DysonTummiesSajiwa 7 днів тому

    Ndachitsilu inu akayiya chifukwa chair ngakhale amati MCP sichipani chopanga nacho mgwilizano mwayiwala inu kut UDF idapangapo mgwilizano ndi MCP 2009

  • @RichwellKhauya
    @RichwellKhauya 6 днів тому

    Kodi ndale za kumalawi bwanji.Mwatitopetsa bwanji

  • @ChrissyKachina
    @ChrissyKachina 6 днів тому

    Koma zimayi ameneyo asatiyese inu a udf mikhala ngati
    Dzitsilu ayisha mambo siwa udf ndi wa msp mumuleke spite ngati azake

  • @HaroonSaidi-jv3ek
    @HaroonSaidi-jv3ek 7 днів тому

    Indedi uyu analandira mmamuona ku Parliament kuja mmene amachitira she came from opposition koma amayimira mcp ndipo izi ndi zoonadi uyu analowa kale mcp kale UDF wangovala nsalu yo

  • @IsaaczidanaZidana
    @IsaaczidanaZidana 7 днів тому

    Zimene amanena achair nthawi imeneyo MOTi akulu simukudziwa kuti ndiye ndala zakuno kumalawi?zoti nthawi ya achair ena anafa simukudziwa?matafale ndi ena anadwara nthenda yanji?iweyo ndiwe opusa asaye achipani apange zomwe akudziwa,osokoneza ndiweyo

  • @PatrickChirwa-cv5cd
    @PatrickChirwa-cv5cd 8 днів тому

    Inuyo akupatsani ndalama zingati a DPP? UDF anaipha ndi a DPP osati MCP kuti ikhale ndi ndi aphungu 7 okha out of 36 ku Eastern Region. UDF isaitane DPP ndi njoka.

  • @LeonardChinomba-r5e
    @LeonardChinomba-r5e 7 днів тому

    Man ulemu wanu ine ndili kuno ku south Africa koma ndakusatani mu VN yanuyi u spoke well Aish mambo is eival wangovala buyi buyi koma ndi mfiti sakumva chisoni ndi anthu mene akuvutikila son beich

  • @MoreenHussein
    @MoreenHussein 7 днів тому

    Ndipo asakapezekekoso,akasonezako

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 8 днів тому

    😮 mayi uyu ndi galu kwambasi pa nyini pakenso apite Ku mcp galu ameneyu

  • @AchiwaNikisya
    @AchiwaNikisya 8 днів тому

    Ndi zoona a kunena akhayiyazi ine zinandiwawa pitilizani comrade

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe 7 днів тому

    Mai oipa kwambiri ameneyu musamale naye

  • @StanelyPhiri-kg1ix
    @StanelyPhiri-kg1ix 8 днів тому

    Comrade you are not Worthy Freedom fighter

  • @TwalibiArafred
    @TwalibiArafred 8 днів тому

    Hule ameneyo ngt walandiladi ndalama ku mcp aziwe kut malawi sii yambuye akhe..ife tikuvutika mziko muno UDF ndichipani chathu.iyeyo ndi uhule wakheyo akachitile kunja kwa UDF

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 8 днів тому

    Komatu ngati UDF yathu ikutha chotchi ndichifukwa cha DPP not MCP

  • @IsaaczidanaZidana
    @IsaaczidanaZidana 7 днів тому

    Ngati si iwe wandale siya zolankhura zandale uzipanga zako

  • @McfallenKayuni
    @McfallenKayuni 7 днів тому

    There is no permanent enemy in politics

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 8 днів тому

    Mayi ameneyo ndi wa MCP ndi galu

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 7 днів тому

    Achotsedwe di adzipita Kung, ona ko okha, tengerani chitsanzo cha dpp anachotsa anthu wonse osokoneza

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 8 днів тому

    Zikudabwitsa ndizakuti anthu onse akukuwa kuwa apapa si a UDF onsewa ndi ADPP. Nonsense nonsenu sindinamve mukusapota UDF amene timamudziwa kuti ndi sapota wa UDF ndi ABDUL basi .Leave UDF alone. Mdani wa UDF ndi DPP si MCP AYI. For your I.nformation mbuli iwe a Tcheya anapangapo mgwirizano ndi John Tembo chifukwa Bingu anaipanga chipongwe UDF. Ndiye DPP ndi mdani number one wa UDF. Usachimvera Chikadeti cha Dpp chimenechi.

    • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
      @AbdulsharifulKalipinde-m6u 7 днів тому

      Is better DPP than MCP
      Anthu zimene akufuna kuti azidya katatu osati zonsezo
      Mukakamba za Bingu ndiye muyaluka
      Bingu anachita kugula chipani chija chifukwa vice president analipo ndiye palibetso kuyankhula za Bingu
      Acheyawo dyera kwambiri

  • @ChrisEnos-to5uv
    @ChrisEnos-to5uv 8 днів тому

    Muthu sungapange dzokozekera ndi m'dani wako kalipokalipo aishawo asatinamize

  • @AnnieNyirenda-d5t
    @AnnieNyirenda-d5t 7 днів тому

    A phweka chikangawa aliyese akufuna mahule onse akupita nkonko ku mcp

  • @Fanzo-h2l
    @Fanzo-h2l 8 днів тому

    A UDF akuyenera kusamala naye nzimaiyu musaiwala kuti ku dpp analiponso anthi amena amasokoneza dpp Anankhimwa atalandira ndalama ku mcp kuti awononge chipani cha dpp a mcp mukhalike komanso Aisha angotuluka achisiye chipanicho iye apite ki mcp ko 150 million ndi chiyani kuti agulitse anthi a UDF ku mcp

  • @Bashir-g1t
    @Bashir-g1t 8 днів тому

    Achoke zachibwa sitikufuna 😡

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 8 днів тому

    Aaaaa ndiwe wabodza amadziwadi iweyo ndamenesudziwa Kodi mesa

  • @AlickSylvester-ro3dd
    @AlickSylvester-ro3dd 7 днів тому

    Ma....activist azaka dzino osadziwa chomwe mukuchita hahaha

  • @UmariBashiri
    @UmariBashiri 8 днів тому

    Ayi MCP sitikuwamfuna

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 7 днів тому

    Ndalama ndi njoka yayikulu, inamuphadi yesu

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 8 днів тому

    MULUNGU walinyanyala dziko la malawi chifukwa cha mcp

  • @NolityKondowe
    @NolityKondowe 8 днів тому

    Koma 2009,Bakiri muluzi anapanga alliance ndi mcp.

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani 8 днів тому

      Ndye zinatha bwanji taswera limodzi tinachangamuka pano ovota ndi anthu osati azavota yekha uyo wankhope ngt mamunayo

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 8 днів тому

    Sanalakwe ai koma kuzolowera kutukwana

  • @MussaChilembwe
    @MussaChilembwe 7 днів тому

    Nkazi ameneyi walandira ndlama zamagazi basi wasatanic imeneyi achoke basi sakufunika ku udf

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 7 днів тому

    Aisha ndi chitsilu cha munthu

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 7 днів тому

    Chipani chamagazi achair anayankhula kale.then ndikuwaitana zowophyatu

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 8 днів тому

    Ndimaiopa MCP kwambri kupha Chilima ngongole tho fertilizer otchipa chimanga chotchipa eeee MCP mbambande

  • @ChikondiChauma-ib9pg
    @ChikondiChauma-ib9pg 8 днів тому

    Koma Dani lu watukwanika pang'ono koma mayiwa mpaka awakumbusa komwe anatulukira ayi zikomo

  • @Halima-i4x
    @Halima-i4x 7 днів тому

    Inde ayisha mambo achoke ku UDF ndi mayi oipa kwabas aaaa hijabu yabodza bas

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 8 днів тому

    2019 mesa anaphatikizana lero mukut bwa aaaa muzipaganawo

  • @AidantBwanali
    @AidantBwanali 8 днів тому

    Bambo ake analind udindo ku MCP

  • @ShaibuSmart
    @ShaibuSmart 8 днів тому

    Aishah Mambo Mai mulibe chison

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 8 днів тому

    Mcp ndiye kuti mukuiwopatu

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 8 днів тому

    Mukunama Kodi audf mesa adpp anathawa.kuudf

  • @SammyChakwana
    @SammyChakwana 8 днів тому

    Achindidwa kangati kuti agulise udf ku mcp pantumbo pako nzimayi iwe

  • @MauriceMukona
    @MauriceMukona 7 днів тому

    A Bakili Muluzi analipo ndi Tembo pa mgwirizano koma DPP idawagwetsa pano zichitikansi akalimbila mgwirizano uwu.ndipo tsopano udf iferatu

  • @AlexBanda-d5v
    @AlexBanda-d5v 8 днів тому

    Ee koma achakwera atha Azeru tsopano

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 7 днів тому

    Ase umawelenga bwino kwambiri

  • @NolityKondowe
    @NolityKondowe 8 днів тому

    Zalowa personal tsopano.Mwina anakukani chibwenzi

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc 7 днів тому

    Ai sha mukunena dzoona akufuna kuononga chipani cha u d f 'choti titsiwe m c p sichipani chabwino chakupa kuba ndi kumangana

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 8 днів тому

    Iwe mayi ndiwe chidebe cheni cheni chobooka

  • @PaisonUmali
    @PaisonUmali 8 днів тому

    aisha ndalamazo kadyereni ku mcp komweko tulukan mwaulemu

  • @TwalibiArafred
    @TwalibiArafred 8 днів тому

    amene akunenayo kut inu ndi a DPP ndichisilu komso galu pamozi ndi amakhe

  • @chesterkumwenda
    @chesterkumwenda 7 днів тому

    mcp yisapite kumene tikayigendako

  • @ChisomoBanda-jo4ix
    @ChisomoBanda-jo4ix 8 днів тому

    Nyini yake amenei Aisha ndi m c p yake

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 8 днів тому

    Tadziwa kut ndinu adpp zako

  • @jamesbanda8602
    @jamesbanda8602 8 днів тому

    Ufulu wakupanyo ulinawo iwe galu wamapolo panja

  • @bwenzilanga
    @bwenzilanga 8 днів тому

    Uchitsilu mayi inuyo

  • @JosephPhiri-z8b
    @JosephPhiri-z8b 7 днів тому

    Apange achokera limodzi

  • @LoyidKarebe
    @LoyidKarebe 7 днів тому

    Komaanthu atopa tsopano

  • @AngolanChinga
    @AngolanChinga 8 днів тому

    Aisha mambo inuyo panyini panu pamodzi ndi amuna anuo mapwala awo

  • @ishmaelsiffah9900
    @ishmaelsiffah9900 8 днів тому

    Ku constituency komwe amaimila Aisha ndikomwe kumachokera Abdul Lapken anaphedwa ndi MCP uja,zoona amai amenewa angamalimbe mtima kumaitana MCP kuzochitika za UDF zoona,anthu akudera lake azimuona ndidiso lotan maka maka akwachapola kwe Abdul Lapken amachokerako

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 8 днів тому

      Shame umunthu alibe ufiti koma eesh ndlama🙌🙌